Munthuyu kumutengera ndiekut wasatira Misara yake palimbepo chazelu akuuza amalawi
@user-bn8ci6vx5c
6 күн бұрын
Wamisala ndi iweyo ife tiri pa mbuyo pa DC.
@ChrifordBiziel
6 күн бұрын
Ife palibepo tikuchiwona chovuta inumukudya ndrama zaku opposition ndinu mukunjoya
@ChrifordBiziel
6 күн бұрын
@@user-bn8ci6vx5c DC waboma lanji'?
@SameKaposa
6 күн бұрын
Osati ife uziti iwe
@user-gx8or3yz9u
6 күн бұрын
uli mgulu lofuna kuononga malawi nde unyatu Born kalindo akunyeletsani mukalaka kulowa pansi
@berthamigodi65296 күн бұрын
Vuto takutulukilan kut siinu omenyera ufulu koma cadet wa dpp kkkk vote ndmutima ukunama iwe
@user-jd3zg3ly8o
6 күн бұрын
Kwambiri kwake iyee ndiwandale chabe uyoo
@ChrifordBiziel7 күн бұрын
Azathuwa akupangatu business mwina simukudziwa munthuyu akudya ndrama za opposition mwina simudziwa mukupanga ma moment azanu zikulowa Inu mulichete ndinakholowa kumudz
Пікірлер: 21
Zoona kalindo awuuze mbuzi za chakwera ife ahlomwe sianthu opusa tu uziona.
We're behind you the DC
The DC mwana owoopsa kwambiri,we are behind you
Zokha tikuchita dziko lamalawi mulungu alekelera'zoon lelo UDF lelo yakhalaso yazelu lelo DPP lelo yakhalaso yazelu chomwe tikufuna amalawi ndichan mfziko mwathu momo ndiuzen
Zinthu zake dziko muno nsaname zafika poti munthu ukumazifusa kuti koma anthu opanda ma lawyer fe tili ndikoti tikasume????
Koma amalawi, munapanga ma demo nkhani zazing’ono, mademo mukulephera pano zinthu zitayipiratu. Mwagonanso amalawi, mademo akufunika
Chinthu chikafa ndieno chizikhara chazelu kapena boma likatuluka ndipomwe lizikhara lazelu
When This Chakwela is out of power him and his whole cabinet minister they must be arrested and all state money they stolen they must pay back
Booon kalindo usasochelese amalawi
@PempheroMoleni
6 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkkk inuyo mukuti Malawi Ali bwino et ????
Iweyo udzafera anako osati amalawi aliyense pano wadziwa kt iweyo ukupanga business pabuyo pamalawi uzisochelesa machota omwewa
@DennisDonework
6 күн бұрын
Iweulindi boza
Munthuyu kumutengera ndiekut wasatira Misara yake palimbepo chazelu akuuza amalawi
@user-bn8ci6vx5c
6 күн бұрын
Wamisala ndi iweyo ife tiri pa mbuyo pa DC.
@ChrifordBiziel
6 күн бұрын
Ife palibepo tikuchiwona chovuta inumukudya ndrama zaku opposition ndinu mukunjoya
@ChrifordBiziel
6 күн бұрын
@@user-bn8ci6vx5c DC waboma lanji'?
@SameKaposa
6 күн бұрын
Osati ife uziti iwe
@user-gx8or3yz9u
6 күн бұрын
uli mgulu lofuna kuononga malawi nde unyatu Born kalindo akunyeletsani mukalaka kulowa pansi
Vuto takutulukilan kut siinu omenyera ufulu koma cadet wa dpp kkkk vote ndmutima ukunama iwe
@user-jd3zg3ly8o
6 күн бұрын
Kwambiri kwake iyee ndiwandale chabe uyoo
Azathuwa akupangatu business mwina simukudziwa munthuyu akudya ndrama za opposition mwina simudziwa mukupanga ma moment azanu zikulowa Inu mulichete ndinakholowa kumudz