Zomwe Wakamba Lero Bon Kalindo | Nzeru Zilimo Umu

#malawi #trending #viral

Пікірлер: 21

  • @LekkttarKhembo-or1tx
    @LekkttarKhembo-or1tx7 күн бұрын

    Zoona kalindo awuuze mbuzi za chakwera ife ahlomwe sianthu opusa tu uziona.

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute38397 күн бұрын

    We're behind you the DC

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa62676 күн бұрын

    The DC mwana owoopsa kwambiri,we are behind you

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel7 күн бұрын

    Zokha tikuchita dziko lamalawi mulungu alekelera'zoon lelo UDF lelo yakhalaso yazelu lelo DPP lelo yakhalaso yazelu chomwe tikufuna amalawi ndichan mfziko mwathu momo ndiuzen

  • @MorganBanda-oc2jx
    @MorganBanda-oc2jx7 күн бұрын

    Zinthu zake dziko muno nsaname zafika poti munthu ukumazifusa kuti koma anthu opanda ma lawyer fe tili ndikoti tikasume????

  • @shotsfired588
    @shotsfired5886 күн бұрын

    Koma amalawi, munapanga ma demo nkhani zazing’ono, mademo mukulephera pano zinthu zitayipiratu. Mwagonanso amalawi, mademo akufunika

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel7 күн бұрын

    Chinthu chikafa ndieno chizikhara chazelu kapena boma likatuluka ndipomwe lizikhara lazelu

  • @user-mf5ce9wj4m
    @user-mf5ce9wj4m6 күн бұрын

    When This Chakwela is out of power him and his whole cabinet minister they must be arrested and all state money they stolen they must pay back

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel7 күн бұрын

    Booon kalindo usasochelese amalawi

  • @PempheroMoleni

    @PempheroMoleni

    6 күн бұрын

    Kkkkkkkkkkkkk inuyo mukuti Malawi Ali bwino et ????

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel7 күн бұрын

    Iweyo udzafera anako osati amalawi aliyense pano wadziwa kt iweyo ukupanga business pabuyo pamalawi uzisochelesa machota omwewa

  • @DennisDonework

    @DennisDonework

    6 күн бұрын

    Iweulindi boza

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel7 күн бұрын

    Munthuyu kumutengera ndiekut wasatira Misara yake palimbepo chazelu akuuza amalawi

  • @user-bn8ci6vx5c

    @user-bn8ci6vx5c

    6 күн бұрын

    Wamisala ndi iweyo ife tiri pa mbuyo pa DC.

  • @ChrifordBiziel

    @ChrifordBiziel

    6 күн бұрын

    Ife palibepo tikuchiwona chovuta inumukudya ndrama zaku opposition ndinu mukunjoya

  • @ChrifordBiziel

    @ChrifordBiziel

    6 күн бұрын

    @@user-bn8ci6vx5c DC waboma lanji'?

  • @SameKaposa

    @SameKaposa

    6 күн бұрын

    Osati ife uziti iwe

  • @user-gx8or3yz9u

    @user-gx8or3yz9u

    6 күн бұрын

    uli mgulu lofuna kuononga malawi nde unyatu Born kalindo akunyeletsani mukalaka kulowa pansi

  • @berthamigodi6529
    @berthamigodi65296 күн бұрын

    Vuto takutulukilan kut siinu omenyera ufulu koma cadet wa dpp kkkk vote ndmutima ukunama iwe

  • @user-jd3zg3ly8o

    @user-jd3zg3ly8o

    6 күн бұрын

    Kwambiri kwake iyee ndiwandale chabe uyoo

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel7 күн бұрын

    Azathuwa akupangatu business mwina simukudziwa munthuyu akudya ndrama za opposition mwina simudziwa mukupanga ma moment azanu zikulowa Inu mulichete ndinakholowa kumudz