Shehe uyuso wagagada ulariki wake mopanda mantha kusiya anthu akungoombera mmanja

Пікірлер: 156

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b5 күн бұрын

    Tayesedwa ndi president wakhaza chakwera ndie timupempha Allah kuti atichosele chakwelayo ameen

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo5 күн бұрын

    Sheikhe ulaliki wanu siukugwilizana ndi ma aya omwe mumatulutsa pakamwa panu, uku ndikugulitsa mawu amulungu, ambuye akumvelen chison Ameen

  • @omardyman8083

    @omardyman8083

    5 күн бұрын

    Analandila ndalama nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto zachamba

  • @rasulmaulidi2224

    @rasulmaulidi2224

    3 күн бұрын

    zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu

  • @abdulhameed7808
    @abdulhameed78085 күн бұрын

    Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.

  • @NenehMasanje
    @NenehMasanje5 күн бұрын

    Sheikh mwadya now ndrama

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv5 күн бұрын

    7:53 7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizanu Mayeselo aifa muyesa ife sitimaziwaaa, Nde imfazake zochita kumugwira munthu pakhosi mwadaladala , kumuombela mfuti mkamwa munthu ,kodi yinu mulankhulabwanj muli ndiwumunthuyinu ,aaa muzichotsela ulemu nokhatuyinu mwangotengana nonse odya ndalama zamagazibasi , Afitiwo alimwetuuuu ati zikuyenda malawi wake utiyo amene mungamunamize lelo , Azibusa muzichotsera ulemu nokha mwamva

  • @SulaimanaJames-b9v
    @SulaimanaJames-b9v3 күн бұрын

    Maa Shaa Allah May Allah bless this message and make it beneficial

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Wadya nawo ndalama zamagazi iwee, usatinamize asilamufe pamodzi ndi amalawife, ifenso ndife asilamutu, mayesero ukunena apawa simayesero ochokeraxkwa ALLAH, awa ndimayesero ochokera kwa satana kudzela kwa chizukulu tudzi chake chotchedwa chakwela ndi boma less lake 😂😂😂😂😂

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya5 күн бұрын

    Odya ndalama zamagazi ngati akumasowa zoyankhula zawo? Allah mukunenayo akuyendereni Sheik😢

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam5 күн бұрын

    Ameen sheikh Allah ahead u. From Cape Town centre

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Chemoto alipomwepo anapha ALLAN WITIKA, anapha chilima kuchikangawa 😂😂😂😂

  • @SteveriaZimba-qs1id
    @SteveriaZimba-qs1id5 күн бұрын

    Amen and amen uthenga wamphavu ambuye alemekezeke ndipo akhululukire zochimwa zathu

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali5 күн бұрын

    Naam sheikh ma shaa Allah ulaliki wabwino ndithu ❤❤❤❤

  • @BrownMatonyola-xi3lb
    @BrownMatonyola-xi3lb3 күн бұрын

    Mwadya zingati Aliyese wanyambita ndalama zoti azizilise za imfa yachilima ndikupepha Yehovah Mulungu wathu amuonetse kiyama akumane ndi mavuto

  • @FebbieMaulidi
    @FebbieMaulidi5 күн бұрын

    God bless you sheik for unity message ❤

  • @SayidiIshmael
    @SayidiIshmael3 күн бұрын

    ❤Allah give you more life and imaan to defending this deen

  • @IshaaakKango
    @IshaaakKango2 күн бұрын

    Maashallah sheikh

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv16 сағат бұрын

    Aaaa sizomwezija Izi inu asheikh opanda manyazi , Panja peni peni wadya ndalama Za Chikangawa uyu, Sali pachilungamo uyu

  • @muhmmadsarwer9527
    @muhmmadsarwer95274 күн бұрын

    Ameen thuma ameen Allah tichotseleni President ameneyu..ndipo tipatseni mtsogoleri wabwino mdziko mwathu muno

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani49215 күн бұрын

    Mukufuna mutamike. M'nungu tam'nyekule ngulumbira une

  • @mosewallace9717
    @mosewallace97173 күн бұрын

    mweye che kuntamba 🔥🔥

  • @kekeaufi9834
    @kekeaufi98345 күн бұрын

    *WA ALYKUM SSALAAM WARAHAMATULLAHI WABARAKATUHU,,,,Inna lillah wa Inna ilayh rajoon*

  • @TWAIBAKBANIES
    @TWAIBAKBANIES4 күн бұрын

    Ma vesi ali apa zili kutali tali . Aaaaaaa koma akulu akulu sheikh mudziima pachilungamo komanso ma ves osamawakhitetsa ai

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson5 күн бұрын

    Kkkkkkkkkkk wabodza ndiwe ma inovolopu yakutseka pakamwa ya chakwela, zikhale ndi kunkuyu 😂😂😂 waukape ndani sakudziwa.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv5 күн бұрын

    Sheikh awa salibwino akugulitsa mawu aMulungu ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa mutsiku lomaliza

  • @AndersonTsoyo
    @AndersonTsoyo23 сағат бұрын

    100% shehe uthenga omanganga dziko

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f2 күн бұрын

    Ili ndiye gulu loyitana chakwela ku Eid atawapasa mbia makwacha mashehe adyera ichoooo!

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Usatiipisile Islam yathu iwe wamva , bwanji sukuwalesa makafiir omwe ulinawo pomwepowo kuti azikha okonda anzawo?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv5 күн бұрын

    Mwapatsidwa ndalama

  • @Macsaidi
    @Macsaidi5 күн бұрын

    Komabe sitinganame pa chilungamo. Saulos Chilima anaphedwa ndi ndege ya boma la mcp

  • @omardyman8083
    @omardyman80835 күн бұрын

    Ndine msilamunso koma sheikh uyu wapochelaapo nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto akatero anali ku state house

  • @MollenMponya
    @MollenMponya2 күн бұрын

    Awa ndye mau ochokwera kwa Mulungu osati Za Anja amaziyesa Okha opambana

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io5 күн бұрын

    Alhamudulillla sheih my Allah bless you all the time what's a sweet Message like 💋💗 this Marshall ( port Erizabeth SA missionvale

  • @johnarushamasese108
    @johnarushamasese1085 күн бұрын

    Ana usawi chemwalimu apochele silingwa

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    4 күн бұрын

    Soni jamanja

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati31665 күн бұрын

    God bless you Sheik all the time ❤❤❤❤❤

  • @juntoiman
    @juntoiman4 күн бұрын

    Mmmmm sheikh zoona malo molankhula chilungamo pamaso pa anthu muli busy kubisa choona.Pamenepotu padali anzanu koma lero alikyt

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr5 күн бұрын

    Nyasi zenizeni pamaso pamulungu chilungamo mukuchidziwa Shehe iwe. Wadya ndalama

  • @MafumuBanda
    @MafumuBanda5 күн бұрын

    Sheikh ilim yanu ndiyochepa mupite mukaphunzirenso, ngati mukuzitenga zinthu za Allah maso mmwamba eeeeee chilango chaukali chkupezani pompo mulipo asakutameni awowo andalewo ndizotsala , ifenso tinaphunzira kwambiri kuposa iweyo xxx

  • @AbouzaidahSayeed
    @AbouzaidahSayeed5 күн бұрын

    Kkkkkk sheikh wasanjatu uyu 😅

  • @NuradinaAbrahima-rt9ip
    @NuradinaAbrahima-rt9ip4 күн бұрын

    No i was interested ndi ulaliki wanu Sheikh koma kumapetoko mwandionongela data yanga😭😭😭😭

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Ine ndine Msilamu, uyu ndi sheikh wa chishiya uyu kafiir weniweni uyu,

  • @HusseinAdamLidezo

    @HusseinAdamLidezo

    5 күн бұрын

    Sheikhe wamanyi uyu mbuz

  • @harrisbanda5891

    @harrisbanda5891

    5 күн бұрын

    @@HusseinAdamLidezo zoona angamasinthanise chisilamu ndi ndalama?, bwanji sakulesa asatana anzakewa kuzunza ndikupha anthu mdziko muno ?

  • @trickermussa472
    @trickermussa4724 күн бұрын

    Kukangotinyasisila deen yathu mbuzi ya shaikh

  • @marvelousmadzimure1811
    @marvelousmadzimure18113 күн бұрын

    Masha Allah ❤❤❤

  • @Sasha-g3z
    @Sasha-g3z4 күн бұрын

    Bas allah awadalotse ndi ulaliki wawow

  • @yassinn5634
    @yassinn56344 күн бұрын

    Msilamu wolakira zau Mulungu osati enewa .Akuti ngati munthu wa mulungu walalika osanyoza president akuti ndiye sadziwa kulalikira. Shame

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember5 күн бұрын

    Soka kwaiye akupindisa chilungamo popeza akuziyandikisa matako ake kumoto

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Zikhale ng'oma akuwombelanso mmanja pamfundoless zomwe wanena, kodi unamulesa kuti asamaphe ma ruandaniz and Burundians komanso amalawi?.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv16 сағат бұрын

    Inu nde muletsa zoipazooo suyu muyamikira mfiti ,wakuba, musatinyase

  • @Musa-cz1nm
    @Musa-cz1nm5 күн бұрын

    Ma shaallah ma shaallah ma shaallah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Izo mzoona zoti tiziphunzisana zabwino ndikulesana zoyipa, funso kwa iweyo shehe ndiloti; Kodi zoipa zomwe akuchita chakwelayo wamulesa? Kupha kumene akupha aboma anthu kumalawi kuno wawalesa aboma ako awusiluwo ?,

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xoКүн бұрын

    Thanks shelk potipatsa ulaliki wabwnowu

  • @KasundaAbbasi
    @KasundaAbbasi5 күн бұрын

    Ngakhale mawu akewo akupepuka zoyakhula zakeso kumalemelera abusa aja

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani49215 күн бұрын

    Mzimu wa Chilima ukunyetseni nonse amene mukugawa ma yellow band ndi inu amene mukudya ma bans

  • @AminahMussah
    @AminahMussah5 күн бұрын

    sheikh zamanyazitu iziii kufuna kuoneka wabwino pamanso pa pule mwadya zingat

  • @JUSTINChigamba

    @JUSTINChigamba

    4 күн бұрын

    Ndipo inu zosayenda

  • @amoschataika7440
    @amoschataika74405 күн бұрын

    Chemoto akhale Kunkuyu😅😅😅😅

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv5 күн бұрын

    Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya , Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva

  • @FarhaazbashaMdoka
    @FarhaazbashaMdoka3 күн бұрын

    Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏

  • @FarhaazbashaMdoka

    @FarhaazbashaMdoka

    3 күн бұрын

    Koma ndalamazi guyz tisamale nazo

  • @udkconsultancy5567
    @udkconsultancy55675 күн бұрын

    POWERFUL

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon5 күн бұрын

    SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI

  • @Ishmael376
    @Ishmael3765 күн бұрын

    Komati choti muziwe kulankhula boA pamaso pamulungu pomwe chilungamo mukuziwa muziwe kuti akakuwochani

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z5 күн бұрын

    Chakwela akusapoter Israel shehe wa mabi

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael5 күн бұрын

    Naam ena akwiya chifukwa mwayakhula zosephana ndizomwe Iwo akufuna

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy17495 күн бұрын

    Awaso nawo aaaaaa zaziiii mazidyani wosatipusitsa

  • @emilynthite6545
    @emilynthite65455 күн бұрын

    Apasidwa ndarama alaliki adyela

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja5 күн бұрын

    Akutuma Kodi sheikh wachinyengo iwe nde akupasa zingati ?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv5 күн бұрын

    7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizaunu

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o5 күн бұрын

    Sheikh apatu nanu mwanama kwambiri 😂😂😂😂😂😂

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn5 күн бұрын

    Mashala

  • @ChristianMtambalika
    @ChristianMtambalika5 күн бұрын

    Anthu muzinena chirungamo osamabisala mukaona omunenayo kuti alipopo mamizimu anthu akuvutika pqmene iweyo ukufunq kukomesera president umenewo moyo oyipa ngati uli sogoleri wapingo ndiwe waboza liuze chirungamo dziko

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi5 күн бұрын

    Walykum ssalam wakahmatul llah wabaraktu

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od5 күн бұрын

    Kmatu musamapange zindu kut akutamen shehe Allah wanji angasangalale ulaliki zimayi sisi kunja osamvala pango 😢😢😢 dini ulindo bas inarilah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Moses kumkuyu akukuwombela mmanja pamfundoless zakozo, kodi unamulesa kuti asamaphe anthu ngati mmene anaphela ALLAN WITIKA uja?

  • @user-zf7xk8fk5s
    @user-zf7xk8fk5s5 күн бұрын

    Km Inu sheikh ndinu opanda nzeru apurezident akunyoza chisilam kms amakokomezera nkhondo ku Palestine kut adziwapha asilam zoon Inu kumaim pagulu kwacemera

  • @user-zf7xk8fk5s

    @user-zf7xk8fk5s

    5 күн бұрын

    Ndipo panop asilam akumalaw akuchititsa manyaz chisilam chifukwa chokonda ndalam mmmm zomvetsa chison

  • @HalisonSolomon

    @HalisonSolomon

    5 күн бұрын

    Ndipo sheih uyu watinamizapo wadya nao ndalama za pule malawi sadzathekayi

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv

    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv

    5 күн бұрын

    Alibenzeru uyu

  • @user-fm7yg5yc2c
    @user-fm7yg5yc2c5 күн бұрын

    Walaikum salaam warahmatullah wabarakatuh... Innalillah wainna illaih rajiun

  • @AliSinoya
    @AliSinoya4 күн бұрын

    Sheikh uyu manyakwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg5 күн бұрын

    Shehee wadya chamba chanji chakwera Mutu Ngati gwafa😂

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg3 күн бұрын

    Mashallah

  • @user-qs7xw4ph7z
    @user-qs7xw4ph7z4 күн бұрын

    Amen

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi5 күн бұрын

    Chakwera anapha chilima😊

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh5 күн бұрын

    Live from Gaza city

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv5 күн бұрын

    Palibe amene angakutameni yinu bodza zidyani ndalamazo msilamu weni weni akuonani Kuti mwanama akulu ndinu adyela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg5 күн бұрын

    Achina chimoto ndi a MCP ndiwe shehe😂

  • @moosakananji1879
    @moosakananji18795 күн бұрын

    Sheikh awa Malo ngt awa kumafunika Sheikh ayyub azipita kumeneku not awa

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv68965 күн бұрын

    Ndiye ulaliki otaninso uwu, mukulalikila ngati simukumva kuwawa bwanji, odya banzi sasowa.

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y5 күн бұрын

    Ndalama Za mcp zikuyakhula

  • @bisweckchimphamba8497
    @bisweckchimphamba84975 күн бұрын

    Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope

  • @abbasdamsonamini4888
    @abbasdamsonamini48884 күн бұрын

    Naam Ameen thumma Ameen

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p5 күн бұрын

    Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl5 күн бұрын

    Ameen

  • @shadrackdrums3536
    @shadrackdrums35365 күн бұрын

    Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t4 күн бұрын

    Chemoto ndinu mwandila ma unforp

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja5 күн бұрын

    Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja5 күн бұрын

    Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58915 күн бұрын

    Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir

  • @JumaMboneka
    @JumaMboneka4 күн бұрын

    Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi5 күн бұрын

    Awapasa ndalama 😮 awa

  • @NchocitoTuaibo
    @NchocitoTuaibo5 күн бұрын

    Naam sheh

  • @JamesRoben-dy7bx
    @JamesRoben-dy7bx5 күн бұрын

    Uyu anadya kale ndalama uyu komaso ndi wa mcp uyu

  • @abdulllahanubieimran06comanubi
    @abdulllahanubieimran06comanubi5 күн бұрын

    Jazackah alla

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f2 күн бұрын

    Shehe my foot 😅😅😅

  • @EmanuelPaul-io2hk
    @EmanuelPaul-io2hk3 күн бұрын

    Shehe akufuna chuma chamagazichi eti?