May God protect you Comrade Ntanyiwa, tili komweko pa 10
@daimajames8714Сағат бұрын
Pepani ndithu, may his soul R. I. P💔
@MaggieManganiСағат бұрын
Kalindo
@MariamJohn-dg4emСағат бұрын
Osaopa osatopa osafooka, that words Chilima he left for us
@joneswillymakaniko-dg8ubСағат бұрын
Chilungamo sichiphedwa Bwana stand on your feet
@SaidiMbawa-st6bjСағат бұрын
Mtanyiwa ben longwe bon kalindo Malata Mangochi palibeso ena apa anthu awa akusokoneza amalawi kwambiri bwanji mutakumana mumenyane osati kumatisokonezapo apa
@cynthiakananji1608Сағат бұрын
Mzimu WA chilima usagone mpaka chilungamo chidziwike
@GidionLufani2 сағат бұрын
Mcp yapha athu ofunikila ambili kumalawi
@frankkamwendo49502 сағат бұрын
I like the ending..."iweyoo?" 😂😂😂
@user-pc3jg6pd1h2 сағат бұрын
😢😢😢
@MisheckAselo2 сағат бұрын
Anthu awa ndioipa kwambiri chifukwa iwowa ananena kuti 21 days, tsopano apa 21 days yantha wat a shame on you kumkuyu ndimazidala opanda nzeru ngati ameneo mulungu azikuonani agalu😹
@KingashinaRambo2 сағат бұрын
The DC umàkwana iweyo mr president wa anthu osauka 😂😂😂 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 Osaopa osatopa
@MarcFelson2 сағат бұрын
Kodi uyu former pastor wa Assembles Of God sangamvomereze Kut walephera kutsogolera dziko Monga analepherera kugwira ntchito ya Mlungu sangatule udindo pansi Kut ena apitilize kulamulira dziko?? Mmmm ai tatopa nawe iwe Chakwera ngakhale sitili Ku mlw Koma tiri ndi ana komanso makolo kumudziko
Пікірлер
Chikuwalephelesa ndi mulungu cifukwa mulungu sangalore kut anthu amene akulankhura chilungamo chakwera athane nawo ndpo sizizatheka kut azathana nawo mulungu ndi mulungu
May God protect you Comrade Ntanyiwa, tili komweko pa 10
Pepani ndithu, may his soul R. I. P💔
Kalindo
Osaopa osatopa osafooka, that words Chilima he left for us
Chilungamo sichiphedwa Bwana stand on your feet
Mtanyiwa ben longwe bon kalindo Malata Mangochi palibeso ena apa anthu awa akusokoneza amalawi kwambiri bwanji mutakumana mumenyane osati kumatisokonezapo apa
Mzimu WA chilima usagone mpaka chilungamo chidziwike
Mcp yapha athu ofunikila ambili kumalawi
I like the ending..."iweyoo?" 😂😂😂
😢😢😢
Anthu awa ndioipa kwambiri chifukwa iwowa ananena kuti 21 days, tsopano apa 21 days yantha wat a shame on you kumkuyu ndimazidala opanda nzeru ngati ameneo mulungu azikuonani agalu😹
The DC umàkwana iweyo mr president wa anthu osauka 😂😂😂 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 Osaopa osatopa
Kodi uyu former pastor wa Assembles Of God sangamvomereze Kut walephera kutsogolera dziko Monga analepherera kugwira ntchito ya Mlungu sangatule udindo pansi Kut ena apitilize kulamulira dziko?? Mmmm ai tatopa nawe iwe Chakwera ngakhale sitili Ku mlw Koma tiri ndi ana komanso makolo kumudziko
Mulungu akuyang'anileni Comrade. Ife timati alunta continuea abasha chkonyoka.
Abwana chonde mupite ku immigration anthu akuvutika kwambiri
Dzoooona osamalimbana nawo inu pangani ubwedzi ndmlungu osati munthu odzuza thupi ndyesu yekha oteteza lnuyo antanyiwa❤❤❤❤
❤ we love you man of vision
Za ziiiii Takalandilenkoni mdulidwe galuwe, MCP ndi chani? 🐐
Dc ndimakunyadirani❤❤❤
Ifetilinganga ndi ntanyiwa pa limpompo FM
tikalira mn pa 10
limpopo fm ft bakili muluzi tv 🔥🔥🔥🔥
Voice ikusonyeza kuti munali mu ndegedi
DC
Rip😢😢😢😢😢
Bill yawoyo idutsa ndi imfa ina osati ya A Chilimaaa😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭mpaka tsiku la lero tulo likukanika
Iwe ndiwe chisili kwambili, wadyadi chibamsi choka apa, ndimau amenewo anthu Atha kukuonongatu iwe
Iwe lyton mangani
God bless you and make you stronger
Mumatilimbikisa kwambili tili pa mbuyo panu
I love you sir this true leader who shows the way and follow the way 💪💪💪💪
Olo ndi ana omwe akudziwa chilichonse za ifa imeneyo
Kungofuna kutchuka etiiii
Family yose apa mboro mboro b wak mose
Osaopa,osafooka,tizafera mbendera yathu anatero Chilimaaaaaaa😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Rip tikusowani
Mboro Yako nyin yakazi Ako galu mavi inu bwan
Mavi ako family yose mboro yako
Osaopa osafooka
Rest in peace L Banda
Ambuye apitilidze kukutetedzani
Wawa antanyiwa
Zomvetsa chisoni kwanthu ku bakaka kwachoka kumbari ya maimbidwe
Mzimu wawo ukause mtendere amen
Kumbuyo kwanu😭😭😭😭😭😭
R I P
Thanks born karindo
Ndinamutuluka atangolowa mcp
Kodi chifukwa chiyani dpp yimapha azathu achilibino iwe wajoyina kupha malibino
Bon kalindo ndi dpp awapeza ndi mafupa achilibino