Akufuna kupha mafumu a ku Ntcheu; Umboni wa mfuti 400 tili nawo
Жүктеу.....
Пікірлер: 824
@GraceMaida14 күн бұрын
Muyalukatu agalu inu chaka chake ndichino keep it up my comrade
@user-uc1pd1tc2x
13 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤Mbambande Gra ayalukadi
@paulpaseli631014 күн бұрын
Machine bakili muludzi
@user-ne7rn4ki3c14 күн бұрын
Without Bakili Muluzi TV and the great journalist we are nothing why this is the only TV channel that reveals the hidden story. I❤ the guy coz he exposes the secret of the useless government under Chakwela to let us know. May Allah the almighty protect him as he did with Moses pamene falao amkafuna kumupha.kunkuyu avule dzina la Moses coz Moses amene tikumudziwa ife adali ooa Yehova ndibwino atamatchedwa Yudas ndikupha kwakeko
Iweyo ndi number 1 umatha kafukufuku Bakili Tv mulandire ulemu wanu bro, pitilizani kutisegula maso may God protect everywhere you are
@ulongwearomakawanga231814 күн бұрын
Best and reliable TV in malawi
@user-mw8dq4is6k13 күн бұрын
Our best TV Bakili muluzi Inu ndi big man pazofufuza kulibeso Malawi yonse🔥🔥🔥
@JafaliAkimu-ll1bf14 күн бұрын
mkulu wa police nkhope ngati chiswa bumbu zigawenga chakwera pantumbo pa make
@user-hm9nc7lz6e
14 күн бұрын
Kkkkkk
@ChrispinTaombe
13 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
@thomasyohane98714 күн бұрын
Eeeeh, Kodi mwaziziwa kuti ngakhale kumamiziku anthu asiya kumvera ma radio angomvera Bakili Muluzi Tv ??
@peterchikwakwa8476
14 күн бұрын
I can be true
@user-hm9nc7lz6e
14 күн бұрын
Zoona zake
@actuarialscience2283
14 күн бұрын
Zoona anthu akumaika nkhani zake pa loud speaker. Let's do that midzi yonse ya ku Lilongwe , Ntcheu, etc. Anthu asafe ndi MCPigs.
@user-be5fc3ed1i
14 күн бұрын
Anthu anasiya kalekale kuvera chiwayalesi Cha radio1 ndizinanzi sopano anthu angoveza Bakili muluzi tv bon kalindo ndi Limpopo FM mosogozedwa ndi mtanyiwa 😂😂😂
Bambo, Bambo; haaa!! "Ndaitenga ku Statehouse kumene kumakhala Chakwera". Inu basi ndinu patali. God shield you
@SiphoZungu-tt9iu
13 күн бұрын
Koma amawapeza bwanji ma information amenewa eish bakili muluzi ndi 1
@RichardJere-oz7tu
12 күн бұрын
Pamenepo 😂@@SiphoZungu-tt9iu
@AngellMoyo
11 күн бұрын
Ine to say the fact I don't understand him kkkkk u know uyu akuvesa chimbenene ruling party kkkk
@user-nd9cm3yl7e13 күн бұрын
Boma la mcp kuyambila kale silipanga chitukuko km kusaka athu tiyeni tipephe mwini moyo atilanditse kuzoopswazi but God is not human body atimenyela khondo yawe bless yours and you me love getting blessed with God amen
@joyahmedjoma461514 күн бұрын
Allahu akbar may Allah protect you brother all the time your the best tv ❤❤❤❤
@ApocheC.
13 күн бұрын
😂😂😂😂 🙌
@IbraheemclassickmahmoodIbrahee14 күн бұрын
Our best brother man mmatiphuzisa mokwanira timakunyadilani
Once a wise man said,, Malawi OSAOPA , OSATOPA, OSAFOOKA📌✊ VIVA MA NYASA, VIVA BAKULI MULUZI TV VIVA✊✊✊✊
@AbuOsman-ts6ef14 күн бұрын
🎉❤❤Bakili muludzi oyeeee osawopa osa
@JafaliAkimu-ll1bf14 күн бұрын
kunkuyu adapha witika chakwera adapha chilima boma la zigawenga zokha zokha ili zitsiru mbava
@AiameAdamo-su1nt14 күн бұрын
Great freedom fighter we salute you!
@KwapataLovemorejun14 күн бұрын
Watching live from Denmark, bakili muluzi tv l respect you
@shayrafernandeslatif955614 күн бұрын
Ndipoo mawu mawuu ine ndimaImvela chisoni ife Malawi,😢tawonane azanthu ku kenya,
@gregorychristian380514 күн бұрын
The best ever TV love you king 👑
@Thewarrior709314 күн бұрын
Agalu amenewa ayaluka ndithu . Amva kuwawa sanati akhaula . Ife tili pambuyo pa bakili muluzi TV nganganga ur the best
@KunyengaMoyo14 күн бұрын
Angotipha tonse amalawi atsale okha agalu amenewa
@milajimussa412014 күн бұрын
Best tv in Malawi
@GeoffreyDoctor-p5n14 күн бұрын
Siber security minister! Kuying'alula to the maximum 💃. Tell dem straight 🇱🇾
@Moses5114 күн бұрын
Best TV in Malawi keep up update 💪💪💪🇲🇼🇲🇼🇲🇼 kalikose tikaziwa social media is best because we know true
@innocentchirombo207314 күн бұрын
Ipondeni fadah ❤❤❤
@dalitson355814 күн бұрын
Sitingavotele zigawenga za mcp
@user-xd2uz1bh3l14 күн бұрын
The best tv in the world
@user-Grant26014 күн бұрын
Much respect elder ❤❤❤
@JonathanMunthali-n3c13 күн бұрын
Inu ndiamuna recturer, professor akazawina peter azakupaseni reward
@HappyAbyssinianCat-xt2bm14 күн бұрын
Ndpo Mai yolamuyo ndi onyasa kwambiri akuoneka ndi chinkhope yakeyo
@mikemakamo736014 күн бұрын
Fire 🔥 instudio keep going our comrade atambasule aziwe kuti no secret under the sun
@IbnTaymiahIbrahim14 күн бұрын
Best tv 🎤🥰💞
@rashidsaid223214 күн бұрын
That's why we love our only bakili muluzi channel TV every explation it's their own witnesses no matter how u hate it mr promise president with ur ministers mcp evil government of Malawi
@munashemoyo419014 күн бұрын
Mai wapolice kuchita kunyasa nkhope chochi tiyeni nawoni osawasiya ai ayaluke bas tatopa ife
@alickziba675614 күн бұрын
Opposition parties, this is the time to invest a lot in security services. Every opposition party has to have heavy security
@Sleemsteri12 күн бұрын
Chakwera akungoyalukabe uku eeish so sad kkkkk angoni mwayamba kulimbana nawowa muwakwanitsa koma? These are born warriors tu ohoo
This guy is number one,,,and he is not alone 😂😂😂muli finger mkatimu,alipo akumuuza zinsisi from state house, chakwera galu iwe uyaluka,,,pantumbo pako pamozi ndi gulu lako
@EliasApofu14 күн бұрын
Ulemu wanu wa bakili muluzi tv ❤
@RAJABSTYLESTYLE-yi1el13 күн бұрын
bakili muluzi tv iweyo ndi number one ndipo iweyo ndi womphuzila kuposa achakwela enafe mwatitsakula maso ndi chilungamo chanu ndipo musasiye ayii ndipo mulungu ayenjezele mzeru zina
@ElonBlack199913 күн бұрын
This is why I liked DPP not MCP
@ibrahimalfred653913 күн бұрын
You always talk the truth bakili maluzi TV
@user-uc1pd1tc2x13 күн бұрын
Koma guys tiyeni tigwirizane Bakili Muluzi Tv tiipatse award eeeeeee imatha ndi akatundu zedi❤❤❤❤❤
@Dinalamakanjira14 күн бұрын
Ulemu wanu big brother
@user-oc9vl9xz8e14 күн бұрын
Anthu samakhulupilila nkhani ngati izi koma amakhulupilila chinachake chitachitila guys tigwilane manja kuchosa MCP kulibwanji ikazawinanso 2025 azapha mitundu yonse azasale a Chewa okha Mmalawimuno
@JohnRasheed13 күн бұрын
I remember wht my grandfather used to tell me about mcp zikungofanana nzomwe chakwela akupanga
@user-zr7wk4oq2x14 күн бұрын
Koma akulu awawa eeeh🙌🤣😂 Akuti ndaitenga konko ku state house 😂 Ulemu wanu captain
@zelliachamboto5744
14 күн бұрын
Hahahaha ndipo ndi moto buuu
@user-du9qs4tb6u12 күн бұрын
Bakili muluzi your are the one we trust sitiopa sitifooka osachita matha
@johnmiselo223014 күн бұрын
They will not kill you And am happy to see that you got that receipt 🧾 from state house where chakwera stays
@IssaBwanali-v6r14 күн бұрын
Go ahead big brother
@user-eh1mg3ww6d14 күн бұрын
Mai yolamu mwaipa khope Ndi m tima omwe ite mulungu akuoneni
@Lunnah-b1t10 күн бұрын
God please keep him safe ,u really love Ur country
@tisuhmakhwah708513 күн бұрын
MCP trying to be strong in a democratic nation nzosatheka izi.
@BenissoneErnesto-eh6zs14 күн бұрын
Inu ndinkhani zina brother watching from Mozambique never give up BG brother tili pano kukusatiran 🎉🎉🎉
@ShadyShariefAlieck14 күн бұрын
Indeed bro keep it up a good job brother
@JohnstonNyirenda-zw6jd13 күн бұрын
Kalikose tikamva , our SKC is still with us
@saidichirwa545613 күн бұрын
Mkulu iwe mulungu awonjezele masiku amoyo wako ndithu.Ulindiukadaulo osati wamasewela ayi.Malawi yense pano anakukhulupililadi ndithu.Moyo wanga ndadziwa ma history ambiri kuposa kusukulu kamba ka chanel imeneyi❤
@davidcainoiss276214 күн бұрын
Viva ..best tv ever connected from London
@isaaczuze14 күн бұрын
Chakwera ndi munthu woyipa kwambili ndi amalawi sitinayembekezele zimenezi
@yohanekanjana492513 күн бұрын
Best of the best journalist, eyes of the country, we know kuti chakwela ndi gulu lake la zigawenga spent sleepless night planning to silence you. But you're in our prayers, God is gonna fight for you.
@user-ul1fb4yn5o11 күн бұрын
I love bakili muluzi tv timakunyadiran, Comrade
@user-mz4tk1pw3f14 күн бұрын
Ulemu wanu big ❤❤❤❤ ndimakunyadilani kwambiri
@user-xx5dc5wl7g13 күн бұрын
If there's a journalist who knows tracking government Pvt things ndiye Bakili TV believe u Will never attack this giy
@user-be5fc3ed1i14 күн бұрын
That's why l like this chanel chifukwa Akayankhula amationesa umboni kp it up Bakili muluzi tv.mbuzizi zayamba kuyaluka ndipo ziyalukadi sazayiona voti yathu agalu awa tinawabitera kamba ka manifesto achilima za MCP tinazitaya kalekale iya
@LionPhiri11 күн бұрын
You got my endless respect brother... awululeni ayaluke kumene dziko laMalawi likuyenera kudziwa chilungamo.
@MisheckAselo14 күн бұрын
😮Boma ili litipweteka ndiana omwe kupanda kusamala tikutha ndi ana omwe 😭😭
@ChikumbutsoJohn-rs4tt14 күн бұрын
The best tv but MCP must know A TIME IS SELFISH, MULUNGU AMAKONDA MALAWI, CHAKWERA MUST GO enough is enough
@AbuMussah-wi7gb14 күн бұрын
The best tv and speech i ❤
@macbestermtonga301514 күн бұрын
😂😂😂 Kama jacket
@MUSTAPHERMALIDEN13 күн бұрын
Koma anyaniwa tikazawachotsa m'boma chaka cha mmawachi dziko likuna likuziwen big man not now because we know anthu akukusakan but next year amalaw tikufuna tizakuziwen akulu 💪
@AlbertDuke-of9nn14 күн бұрын
inu ndi one big,mzelu Ngati king Solomon
@Penior2659 күн бұрын
I think this guy is not mad there is something behind guys lets focus
@arafatMtyala-bo8ev14 күн бұрын
Mumaitha big broh, iloweleni ndi mkabulula momwe anthu amenewa akuwonjeza kosakhala bwino
@martintivalenji32014 күн бұрын
Thanks for the update best TV ever
@dontreybanda27813 күн бұрын
More fire big boss, akanganya amenewa alira.
@fyopokappata97384 сағат бұрын
Nthawi ya Peter mumapqnga zomwezi pano ndia Achakwera mukupangaso chimodzi modzi . Mwalowa ndinu ndinuyo big ... Inuyo loaning m'boma tione ngati mungayendetse aaa .
@user-et5vn3yh4j13 күн бұрын
Inuyo mumanena chilungamo god bless you my brother ❤
@princedetbozsmallboy174913 күн бұрын
Chakwera sanakhalepo mbusa ndichigawenga kuyambila pachiyambi pamozi ndi nkazi wake zigawenga koma satitha. Akulu ndinu patali tisaname mukuvesa kukoma ndithu
@user-qq1uj7ct6n13 күн бұрын
You are No 1 bro.. Chiyembekezo chathu chili mwa inu sir. God keep you safe. Amene amaikira kumbuyo MCP Mmmmm ndi athakat anthuwa sure
@user-cy9zp4fb2m14 күн бұрын
God shud keep on protecting you our brave journalist
@PrinceThom-pe6ie13 күн бұрын
May the Lord protect you with the protection from heaven
@EphraimNaveya-hz1du3 күн бұрын
Timakunyadirani bg for true information,Kodi mbuzi imeneyi chakwerayo ndi mbuzi zinzakezo apha anthu angati,iyenso adziwe kt sazakhala wamuyaya
@HsienSawez-hr5xq14 күн бұрын
Great bakili
@YONA-v5o14 күн бұрын
Bwana ndimakunyadilani I wish you all the bey💯❤
@alicegama813814 күн бұрын
Kama jacket 😂😂😂😂😂
@user-bw2cv9sd7x14 күн бұрын
ing'alule fada ayaluke agaluu amenewa ur the one who bring truth to us
Пікірлер: 824
Muyalukatu agalu inu chaka chake ndichino keep it up my comrade
@user-uc1pd1tc2x
13 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤Mbambande Gra ayalukadi
Machine bakili muludzi
Without Bakili Muluzi TV and the great journalist we are nothing why this is the only TV channel that reveals the hidden story. I❤ the guy coz he exposes the secret of the useless government under Chakwela to let us know. May Allah the almighty protect him as he did with Moses pamene falao amkafuna kumupha.kunkuyu avule dzina la Moses coz Moses amene tikumudziwa ife adali ooa Yehova ndibwino atamatchedwa Yudas ndikupha kwakeko
@kotking-xg7pp
13 күн бұрын
slaute inenso ndimawalemekeza awa amadziwa kufufuza nkhani mulungu akhale nanu.
Waying'alula koma adha awa anabwela kuzakhala❤❤❤ I will appreciate boss
Malawians let’s gather here en fight for our nation ,like this guy
@StanleyChirwa-d6b
13 күн бұрын
Ndpo tiima pamseu asakaike
@user-uc1pd1tc2x
13 күн бұрын
❤❤❤❤
It is my strong prayer that you will never be attacked by any evil will
@AudettaYohanie-fl3oc
14 күн бұрын
Amen
Chigawenga chopanda masophenya Chakwera ameneyu aphedwe bas mbuz yamunthu...kukamwako Ngat basen losambila akazake iyaaa 💪💪💪💪💪
Apapa ifeyo tipange plan ngati opposition... APM apange machawi kuremba achinyamata ngati private security
@Dysonkhofi
14 күн бұрын
A papa nkhondo yayamba
@kenmasta
14 күн бұрын
Tilowa mthengo nafenso mcp isatinyanseso
@thomphalavi5027
13 күн бұрын
🎉
A brave man himself,ulemu wako,
Koma inuyo ndi one 💪💪💪💪
History is the best teacher long live BMTV ♥️
Iweyo ndi number 1 umatha kafukufuku Bakili Tv mulandire ulemu wanu bro, pitilizani kutisegula maso may God protect everywhere you are
Best and reliable TV in malawi
Our best TV Bakili muluzi Inu ndi big man pazofufuza kulibeso Malawi yonse🔥🔥🔥
mkulu wa police nkhope ngati chiswa bumbu zigawenga chakwera pantumbo pa make
@user-hm9nc7lz6e
14 күн бұрын
Kkkkkk
@ChrispinTaombe
13 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
Eeeeh, Kodi mwaziziwa kuti ngakhale kumamiziku anthu asiya kumvera ma radio angomvera Bakili Muluzi Tv ??
@peterchikwakwa8476
14 күн бұрын
I can be true
@user-hm9nc7lz6e
14 күн бұрын
Zoona zake
@actuarialscience2283
14 күн бұрын
Zoona anthu akumaika nkhani zake pa loud speaker. Let's do that midzi yonse ya ku Lilongwe , Ntcheu, etc. Anthu asafe ndi MCPigs.
@user-be5fc3ed1i
14 күн бұрын
Anthu anasiya kalekale kuvera chiwayalesi Cha radio1 ndizinanzi sopano anthu angoveza Bakili muluzi tv bon kalindo ndi Limpopo FM mosogozedwa ndi mtanyiwa 😂😂😂
@inessmsiyambiri8517
14 күн бұрын
Eeeee zoona nnamvapo ndikudutsa ku lirangwe kumva anthu akumvera bon kalindo
Bambo, Bambo; haaa!! "Ndaitenga ku Statehouse kumene kumakhala Chakwera". Inu basi ndinu patali. God shield you
@SiphoZungu-tt9iu
13 күн бұрын
Koma amawapeza bwanji ma information amenewa eish bakili muluzi ndi 1
@RichardJere-oz7tu
12 күн бұрын
Pamenepo 😂@@SiphoZungu-tt9iu
@AngellMoyo
11 күн бұрын
Ine to say the fact I don't understand him kkkkk u know uyu akuvesa chimbenene ruling party kkkk
Boma la mcp kuyambila kale silipanga chitukuko km kusaka athu tiyeni tipephe mwini moyo atilanditse kuzoopswazi but God is not human body atimenyela khondo yawe bless yours and you me love getting blessed with God amen
Allahu akbar may Allah protect you brother all the time your the best tv ❤❤❤❤
@ApocheC.
13 күн бұрын
😂😂😂😂 🙌
Our best brother man mmatiphuzisa mokwanira timakunyadilani
@philemontitusnkhoma7740
13 күн бұрын
Kukuphinzitsani chani. Akukuonani kupusa kani. APM ndamene akupanga izi zamaboza kufuna mavoti. Iwe Bakili, samala. Ugwidwa posachedwapa.
@Hassanianusa-go9wv
13 күн бұрын
@@philemontitusnkhoma7740kape iwe
@Eric-gb9ms
13 күн бұрын
@@philemontitusnkhoma7740panyapako usamale ndiweyo sali yekha
@HappyBirchForest-zy8nq
13 күн бұрын
Choka iwe wakupha iwe ndichipani chako cha mcp mukhaulapotu muziona mukanthidwa ndi mulungu posachedwapa muone
@blessingsphiri-ev6xi
12 күн бұрын
Apm akupanga motani pereka umbon@@philemontitusnkhoma7740
Talk munthu wamkulu mitima inafa kale amanyereni nkhondo Ana akubwera kumboyoku
Best Bakili muluzi TV
The true Zodiac station is Bakili Muluzi TV. You are the revealer
Abale chkwera why why ukupanga zimenez ukufuna uchose miyoyo yanthu 😭😭😭😭 wanthu osalakwa
@user-ko1lk3br4r
13 күн бұрын
Akupusitsani uyu ndipo muthawa opanga okuthamangitsani
Once a wise man said,, Malawi OSAOPA , OSATOPA, OSAFOOKA📌✊ VIVA MA NYASA, VIVA BAKULI MULUZI TV VIVA✊✊✊✊
🎉❤❤Bakili muludzi oyeeee osawopa osa
kunkuyu adapha witika chakwera adapha chilima boma la zigawenga zokha zokha ili zitsiru mbava
Great freedom fighter we salute you!
Watching live from Denmark, bakili muluzi tv l respect you
Ndipoo mawu mawuu ine ndimaImvela chisoni ife Malawi,😢tawonane azanthu ku kenya,
The best ever TV love you king 👑
Agalu amenewa ayaluka ndithu . Amva kuwawa sanati akhaula . Ife tili pambuyo pa bakili muluzi TV nganganga ur the best
Angotipha tonse amalawi atsale okha agalu amenewa
Best tv in Malawi
Siber security minister! Kuying'alula to the maximum 💃. Tell dem straight 🇱🇾
Best TV in Malawi keep up update 💪💪💪🇲🇼🇲🇼🇲🇼 kalikose tikaziwa social media is best because we know true
Ipondeni fadah ❤❤❤
Sitingavotele zigawenga za mcp
The best tv in the world
Much respect elder ❤❤❤
Inu ndiamuna recturer, professor akazawina peter azakupaseni reward
Ndpo Mai yolamuyo ndi onyasa kwambiri akuoneka ndi chinkhope yakeyo
Fire 🔥 instudio keep going our comrade atambasule aziwe kuti no secret under the sun
Best tv 🎤🥰💞
That's why we love our only bakili muluzi channel TV every explation it's their own witnesses no matter how u hate it mr promise president with ur ministers mcp evil government of Malawi
Mai wapolice kuchita kunyasa nkhope chochi tiyeni nawoni osawasiya ai ayaluke bas tatopa ife
Opposition parties, this is the time to invest a lot in security services. Every opposition party has to have heavy security
Chakwera akungoyalukabe uku eeish so sad kkkkk angoni mwayamba kulimbana nawowa muwakwanitsa koma? These are born warriors tu ohoo
Komadi guys zinthu zikamachitika choncho zimapyesadi mtima atsogoleliwa umunthu alibe 😢😢😢😢
Akuti ndaitenga komweko inuyo ndi big
Koma bvuto ndichani abale Mafumu mmayesa kunali kulira? Mmayesa munanena nokha kuti wolira Maliro sasekedwa pakamwa? Km boma limeneli ngt tikulimbvetsa zomwe likufuna
This guy is number one,,,and he is not alone 😂😂😂muli finger mkatimu,alipo akumuuza zinsisi from state house, chakwera galu iwe uyaluka,,,pantumbo pako pamozi ndi gulu lako
Ulemu wanu wa bakili muluzi tv ❤
bakili muluzi tv iweyo ndi number one ndipo iweyo ndi womphuzila kuposa achakwela enafe mwatitsakula maso ndi chilungamo chanu ndipo musasiye ayii ndipo mulungu ayenjezele mzeru zina
This is why I liked DPP not MCP
You always talk the truth bakili maluzi TV
Koma guys tiyeni tigwirizane Bakili Muluzi Tv tiipatse award eeeeeee imatha ndi akatundu zedi❤❤❤❤❤
Ulemu wanu big brother
Anthu samakhulupilila nkhani ngati izi koma amakhulupilila chinachake chitachitila guys tigwilane manja kuchosa MCP kulibwanji ikazawinanso 2025 azapha mitundu yonse azasale a Chewa okha Mmalawimuno
I remember wht my grandfather used to tell me about mcp zikungofanana nzomwe chakwela akupanga
Koma akulu awawa eeeh🙌🤣😂 Akuti ndaitenga konko ku state house 😂 Ulemu wanu captain
@zelliachamboto5744
14 күн бұрын
Hahahaha ndipo ndi moto buuu
Bakili muluzi your are the one we trust sitiopa sitifooka osachita matha
They will not kill you And am happy to see that you got that receipt 🧾 from state house where chakwera stays
Go ahead big brother
Mai yolamu mwaipa khope Ndi m tima omwe ite mulungu akuoneni
God please keep him safe ,u really love Ur country
MCP trying to be strong in a democratic nation nzosatheka izi.
Inu ndinkhani zina brother watching from Mozambique never give up BG brother tili pano kukusatiran 🎉🎉🎉
Indeed bro keep it up a good job brother
Kalikose tikamva , our SKC is still with us
Mkulu iwe mulungu awonjezele masiku amoyo wako ndithu.Ulindiukadaulo osati wamasewela ayi.Malawi yense pano anakukhulupililadi ndithu.Moyo wanga ndadziwa ma history ambiri kuposa kusukulu kamba ka chanel imeneyi❤
Viva ..best tv ever connected from London
Chakwera ndi munthu woyipa kwambili ndi amalawi sitinayembekezele zimenezi
Best of the best journalist, eyes of the country, we know kuti chakwela ndi gulu lake la zigawenga spent sleepless night planning to silence you. But you're in our prayers, God is gonna fight for you.
I love bakili muluzi tv timakunyadiran, Comrade
Ulemu wanu big ❤❤❤❤ ndimakunyadilani kwambiri
If there's a journalist who knows tracking government Pvt things ndiye Bakili TV believe u Will never attack this giy
That's why l like this chanel chifukwa Akayankhula amationesa umboni kp it up Bakili muluzi tv.mbuzizi zayamba kuyaluka ndipo ziyalukadi sazayiona voti yathu agalu awa tinawabitera kamba ka manifesto achilima za MCP tinazitaya kalekale iya
You got my endless respect brother... awululeni ayaluke kumene dziko laMalawi likuyenera kudziwa chilungamo.
😮Boma ili litipweteka ndiana omwe kupanda kusamala tikutha ndi ana omwe 😭😭
The best tv but MCP must know A TIME IS SELFISH, MULUNGU AMAKONDA MALAWI, CHAKWERA MUST GO enough is enough
The best tv and speech i ❤
😂😂😂 Kama jacket
Koma anyaniwa tikazawachotsa m'boma chaka cha mmawachi dziko likuna likuziwen big man not now because we know anthu akukusakan but next year amalaw tikufuna tizakuziwen akulu 💪
inu ndi one big,mzelu Ngati king Solomon
I think this guy is not mad there is something behind guys lets focus
Mumaitha big broh, iloweleni ndi mkabulula momwe anthu amenewa akuwonjeza kosakhala bwino
Thanks for the update best TV ever
More fire big boss, akanganya amenewa alira.
Nthawi ya Peter mumapqnga zomwezi pano ndia Achakwera mukupangaso chimodzi modzi . Mwalowa ndinu ndinuyo big ... Inuyo loaning m'boma tione ngati mungayendetse aaa .
Inuyo mumanena chilungamo god bless you my brother ❤
Chakwera sanakhalepo mbusa ndichigawenga kuyambila pachiyambi pamozi ndi nkazi wake zigawenga koma satitha. Akulu ndinu patali tisaname mukuvesa kukoma ndithu
You are No 1 bro.. Chiyembekezo chathu chili mwa inu sir. God keep you safe. Amene amaikira kumbuyo MCP Mmmmm ndi athakat anthuwa sure
God shud keep on protecting you our brave journalist
May the Lord protect you with the protection from heaven
Timakunyadirani bg for true information,Kodi mbuzi imeneyi chakwerayo ndi mbuzi zinzakezo apha anthu angati,iyenso adziwe kt sazakhala wamuyaya
Great bakili
Bwana ndimakunyadilani I wish you all the bey💯❤
Kama jacket 😂😂😂😂😂
ing'alule fada ayaluke agaluu amenewa ur the one who bring truth to us