Asilikali 62 a Rwanda alowa mdziko la Malawi motsogozedwa ndi General wamkulu kwambiri.

Пікірлер: 226

  • @obimonegev5579
    @obimonegev5579 Жыл бұрын

    Anthu ngat iweyo ndiyamene akufunika kumakhala dziko muno, receive your flowers 🎉

  • @francistonysanena5349

    @francistonysanena5349

    Жыл бұрын

    I don't think that the government has to review everything to the public

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk Жыл бұрын

    Mmm MCP itipweteketsa ndithu, go deeper our own informant, love you, proud of you always 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @TONYJUSTIN-cx7yt
    @TONYJUSTIN-cx7yt Жыл бұрын

    Iweyo ase the best of the best history in malawi 🇲🇼 👌

  • @onester4946
    @onester4946 Жыл бұрын

    This journalist is genius. Umafufuza aise. Big up. I like how you use deep knowledge to research news. Chakwera is killing refugees.

  • @bernadakim6544

    @bernadakim6544

    Жыл бұрын

    Kod ndinu muli ndi ka KZread Channel kanu kopepela mumakatcha bakili muluzi 🤣🤣🤣, zot kutali pass out week yatha ya ma cadet simumaziwa? Zot kunafika ma general from different countries like Zambia, Rwanda, eswantin, Mozambique,Kenya, Tanzania pamwambowo chifukwa ena mwa omwewa amapanga pass out are from those countries simukuziwa iyayi? Page iyiyi yazaza NDI ma bulutu.. very foolish, stupid and ignorant.. ka school kaja pena pake kamathandiza

  • @devlinebhema2729

    @devlinebhema2729

    Жыл бұрын

    @@bernadakim6544 bulutu nd iwe aise palibe akukukukamamiza kut uzinvela

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Жыл бұрын

    This journalist is very great.

  • @honourablemcgregorysc97tv
    @honourablemcgregorysc97tv Жыл бұрын

    One of the best Channel🔥🔥🔥🙏🙏😍

  • @successngoma
    @successngoma Жыл бұрын

    Malawi 🇲🇼 God help us

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 Жыл бұрын

    Ohoho thanks very much bg mn respect ndawi zonse

  • @thomassimbaya197
    @thomassimbaya197 Жыл бұрын

    Watching from Zambia muchinga province God bless you,you are the best,

  • @EmmanuelThom2-xf6ij
    @EmmanuelThom2-xf6ij Жыл бұрын

    More thanx bro 4 keeping us updated

  • @yasinkamwendo-jf7sc
    @yasinkamwendo-jf7sc Жыл бұрын

    Big up brother King 🤴 of history ❤❤❤

  • @matamandonkhoma8163
    @matamandonkhoma8163 Жыл бұрын

    You stand for Us Boss

  • @wilsonsawasawa3794
    @wilsonsawasawa3794 Жыл бұрын

    You are the best! Big up

  • @rashidstamburi2705
    @rashidstamburi2705 Жыл бұрын

    Big up 💪🏻

  • @mathiasmajamanda5797
    @mathiasmajamanda5797 Жыл бұрын

    This is great and well explained

  • @davenchimadzi6529
    @davenchimadzi6529 Жыл бұрын

    Asazakunamizeni chakwela sanali m'busa wa mulungu. Awawa ndmaplan omwe akupanga kukhomzekela zisankho gyz tisamale kufa anthu kuno😭😭😭😭

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Yaaaaah oooooh!! Point iyi zedi thanks brother Wanga 😢😢

  • @chitimbethegreat-pc1bp
    @chitimbethegreat-pc1bp Жыл бұрын

    Chakwera ndi mzake chilima have change Malawi to den of robbers

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 Жыл бұрын

    Koma ase iweyu u can rule Malawi coz u know history alot

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Ndipo zedi brother ndidolo uyu zed

  • @user-tp7ze7qy3s
    @user-tp7ze7qy3s9 ай бұрын

    Inuyo munadalitsika boss much respect, izizi nde zikufunikila mu dziko lathu lino

  • @mateyudyton4739
    @mateyudyton4739 Жыл бұрын

    Good work brother keep on informing us

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 Жыл бұрын

    Asilikali a Malawi ndiye kuti ntchito Samatha??? Mpaka kuwabweletsela asilikali adziko lina aaaaaa shame

  • @drbanda6105
    @drbanda610511 ай бұрын

    Bbe up♥️♥️♥️

  • @andersonmaster8055
    @andersonmaster8055 Жыл бұрын

    Best chanel than ever

  • @misianguisheraufi4803
    @misianguisheraufi4803 Жыл бұрын

    This is nice narration, evidence based journalist

  • @farookousmane715
    @farookousmane715 Жыл бұрын

    King of history!

  • @martinkhozombah
    @martinkhozombah Жыл бұрын

    Keep up the good work boss

  • @nickmagola278
    @nickmagola278 Жыл бұрын

    You are a machine in history

  • @johnchavula3282
    @johnchavula3282 Жыл бұрын

    Thanks but please do Hosni Mubarak

  • @argentchilanga3246
    @argentchilanga3246 Жыл бұрын

    Zikachitika timvera Kwa inu big man give us more zomwe zikuchitika mziko lathu from South Africa

  • @isaactembo6164
    @isaactembo6164 Жыл бұрын

    Tikhale ndi airport ya asilikali payokha iyo ndi public airport, sikofikila asilikali.

  • @dhaoudhiabedinegomaseko2363

    @dhaoudhiabedinegomaseko2363

    Жыл бұрын

    Ndipo kwambiri zoona ada koma MCP ayi zikomo

  • @titomethiwa4213
    @titomethiwa4213 Жыл бұрын

    Ndimakunyadilani big man koma ndimafuna ndifunse zikuwoneka kuti kangame ndimuthu oipa kwambiri koma sangakusakeni inuyo chifukwa ndimuthu oipa

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Amakhala Kuti iyeyonso Ali well safeguarded by his people boss

  • @alfredbanda886
    @alfredbanda886 Жыл бұрын

    Chakwela alionetsa Zinthu Dziko Lamalawi

  • @josuahkachali1489
    @josuahkachali1489 Жыл бұрын

    Keep it up Mr

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Жыл бұрын

    Chakwera khala serious osaononge dziko la Malawi ndi nkhondo, ona ku DRC nkhondo yemwe amalimbikitsa ndi Kagame yemweyonso,kulira kulowetsa zigawenga m'dziko zoona, watitopetsa ndiwe munthu osaganiza.

  • @wensleyshumba8205
    @wensleyshumba8205 Жыл бұрын

    Chakwela ndichitsiru kwambili angalole bwanji asilikale alowe mu mziko ngat muli khondo , Nundwe naye angokhala ngat alibe mutu zautsilu kwabwas nkondo yili ku ukraine not ku malawi

  • @promisemakawa1556
    @promisemakawa1556 Жыл бұрын

    Atsogoleri aku Malawi ndi zitsiru

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Жыл бұрын

    BIG 👍

  • @Razarusmbavachakwera
    @Razarusmbavachakwera Жыл бұрын

    As malawian citizens I will never allowed this nonsense to happen m"boma liyenela kuwasiya anthuwa tizikhalanawo mwantendele ngatimene timakhaliramu osamati kumazuka ndikumasawusa mitima yaanthu osalakwa

  • @NeversonGonthi-fg3zm
    @NeversonGonthi-fg3zm Жыл бұрын

    Chitetezo cha Malawi chalowa mbola,aganiza bwanji abusa?

  • @idrissaeliassa
    @idrissaeliassa Жыл бұрын

    Politicians ndi anthu onyasa zochitika zawo

  • @khamaneizarif4491
    @khamaneizarif4491 Жыл бұрын

    Good job

  • @user-pt1fy3qg4u
    @user-pt1fy3qg4u Жыл бұрын

    Never give up

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Жыл бұрын

    Chiopsezo chiliso kwaife pamenepo dziko lilibe security ili😣😣

  • @user-bc4zy7cv2y

    @user-bc4zy7cv2y

    Жыл бұрын

    😢😢

  • @irenechirwa9710
    @irenechirwa9710 Жыл бұрын

    Brother bwanji mungopanga zoti muzapikjsane nawo pa chisankho cha upule tizakuvotelani ife pls.

  • @user-mz4tk1pw3f
    @user-mz4tk1pw3f Жыл бұрын

    Mumakwana big ❤

  • @wensleyshumba8205
    @wensleyshumba8205 Жыл бұрын

    Munthu wogwila kuchipiku angalamulire dziko anazolowela kunyamula mathumba akamba bas mbuz yeniyeni

  • @emmanuelkhosa-ze6fl
    @emmanuelkhosa-ze6fl Жыл бұрын

    Please tell us about the story of the people leaving in moon

  • @pastonmoda-pk4uj
    @pastonmoda-pk4uj Жыл бұрын

    Koma mulungu akuwaona sangasanglale muthu akuvutika chocho

  • @levisondaka6392
    @levisondaka6392 Жыл бұрын

    This is true story I remember well my friend from Rwanda who were taken to that country they were killed by this guy's truly you can feel bad what I Saw that time please work up Malawi

  • @kamwendoderek6567
    @kamwendoderek6567 Жыл бұрын

    TRUE GOD IS GOING TO FIGHT FOR THIS ARMY,

  • @rosseshaibu1576
    @rosseshaibu1576 Жыл бұрын

    ❤❤❤

  • @nelsonmacken7662
    @nelsonmacken7662 Жыл бұрын

    Koma bwanji Mr president Alola zimenezi

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Жыл бұрын

    ndakugomelani..ndipo umantha...abusa sadapange bwino ndipo asilikali amenewa anyamuke

  • @kuziririzaisabatosiitegeko7088
    @kuziririzaisabatosiitegeko7088 Жыл бұрын

    Kagame anayambitsa nkondo mu drc,njira zimene anazera mukulowa drc ndizimene ukuzera kuyambitsa nkondo ku Malawi!

  • @josephychisoni8628
    @josephychisoni8628 Жыл бұрын

    Ndiye mvuto ndichani mesa akutenga akwawo Ngati akutenga a Malawi 🤷🤷

  • @ibrahimatibu8784
    @ibrahimatibu8784 Жыл бұрын

    Malawi kwathu bass ndi mbili yakale palibe chabwino misonzi yokha kumangotuluka

  • @bayview4554
    @bayview4554 Жыл бұрын

    Koma chakwerayu ndi buzi yamunthu akulolawesa zigawenga ziko zoo a

  • @user-ib5fc1jf7o
    @user-ib5fc1jf7o Жыл бұрын

    Crying for my mother Malawi

  • @jermahkell8538
    @jermahkell8538 Жыл бұрын

    Zomvetsa chisoni, ku mchinji anachita kubwera asilijali nkumamatchola ma shop nkumauza anthu kut azitulutsa katundu, God over everything

  • @eunicemoyo6024

    @eunicemoyo6024

    Жыл бұрын

    Shaaaaa kom zomvesatu chisoni mpakana kwatengela zinthu mushop pali uzimu apa

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Mmmmmmmm zachitika litiro zimenezi?😢😢😢😢😢 Koma Chakwera guys ai zikomo 😭😭😭😭

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    ​@@eunicemoyo6024Ndagwetsa nsonzi inee😭

  • @marthankhoma1063
    @marthankhoma1063 Жыл бұрын

    Akuyanjana ndi anthu oipa kufuna kusokoneza bziko la Malawi

  • @maxgulani1391
    @maxgulani1391 Жыл бұрын

    Chakwera ndi Mbuzi yamunthu ameneyi angobwerera Ku church basi

  • @georgechikafutwa1334
    @georgechikafutwa1334 Жыл бұрын

  • @khulienakabwere7720
    @khulienakabwere7720 Жыл бұрын

    Also tell us about the genocide committed by the Hutus against the Tutsis. Is that not what led the Hutus to flee their country in the first place? Fear of retribution. After the Hutu government genocidal army was defeated, they left the country and hid amongst civilian refugees. The hutus civilians have been allowed back into their country and one has to wonder why some of them refuse to go back, unless they were part of the genocidal army and militias.

  • @markoviskyhernandez9706

    @markoviskyhernandez9706

    Жыл бұрын

    Don't you know what the rwandan government does daily in the country? They take by force goods and lands of people without giving them any compensation. Do you know what they did to the people of Kangondo I, Kangondo II, Kibiraro I, Kibiraro II, ....?? Do your research please!! They kill people every day in Rwanda. Dusabemungu Syldio was killed by the government, Anselme Mutuyimana was killed by who? Policemen came and pick him in car station, the following day, his body was found in Gishwati forest. What about Dr Gasakure? Personal doctor of the president shot when he was handcuffed and the government pretended that he was shot while he was fighting against policemen whom he wanted to grab guns from them by force. You understand this? The list is too long including ordinary people. People are got missing too many time. People like Boniface Twagirimana, Illuminée Iragena, Bahati Innocent, Nyimugabo Gérard, ....!! Can you tell us where they are? People are jailed for no reason. Example: Niyonsenga Dieudonné (journalist), Nsengiyumva Théoneste (journalist), Karasira Aimable (Human right activist), Idamange Yvonne (human right activist), Hakuzimana Abdul Rachid (politician), ....!! With this atrocities, people should not flee the country? Rwandans flee every day. We have too many millions in Uganda, too many thausands in SADC and all over the world. You say that people who flee the country are only hutus. Really!!??🤔🤔!! Cassien Ntamuhanga, Theogene Rudasingwa, Jean Paul Ntagara, Jean Paul Tirayishimye, ....are they hutus!! Pure liar!! You say that hutus are genocidors and this is why they are refusing to go back home. Really!??🤔🤔!! It has been 29 years since 1994. Go and have a look on these refugees. How old are they!?? With the atrocities of rwandan government, every one can flee the country. And the rwandan government knows that. That is why they supervise highly the borders of Rwanda and they always shoot people who try to cross the borders illegally because too many Rwandans want to escape. You are accusing them to be genocidors but you forgot that on the list that the government of Rwanda gave interpol, there remain only two people who are still hiding themselves. The one who was caught recently in South Africa was the third, Kabuga Félicien who was caught before was the 4 th!! What is surprising is to see how you accuse others but what you are doing in DRC with your M23 is right? In Kishishe recently, you killed more than 280 people mostly children and women. You ignore what tutsi soldiers of Paul Kagame did during the genocide when they were killing tutsis?? You have to hear the testimony of Tito Rutaremara. What people like Caporal Kiyago, Sergent Serwanda, Caporal Ntukayajemo, ....were doing in interahamwe militia. These are examples of some tutsis soldiers of Kagame who were in interahamwe killing tutsis. Do you forget that interahamwe (militia that is accused to kill tutsis) was leaded by a tutsi. Yes, Robert Kajuga was a tutsi. Do you know the relationship between him and the first family!?? Do your research and stop killing congolese people. They did nothing wrong to you!!

  • @johngashayija5664

    @johngashayija5664

    Жыл бұрын

    Any action of killing was done by regime of pkagame, if you hear very well Tito rutarema speach

  • @jaykar-issa706

    @jaykar-issa706

    Жыл бұрын

    I'm not sure if you a Malawian or a Pro Kagame rwandan but before you say anything, you should at least know that justice sasunga mbali!! Anthuwa amene aki ndi udindo ku Rwandapo ndi anthu oopsa zedi, ndi oipa kwabasi, anapanga ndi kuchita genocide ndi iwowo.... Ma hutu ndi ma tutsi ankakala limodzi mwa mtendere awa asanayambitse nkhondo ku dziko la mtendere. Ever since Oct 1, 1990 anthu awa anayambitsa nkhondo kwa nzika za ku rwanda, kuwapa ngati mbuzi ku butchery koma mpaka na pano... palibe wazengedwa mlandu!! They just decided to put all their deeds on innocent hutu population. It is not fair! It is very troubling to hear a leader of a nation saying that even those hutu generations born after genocide should apologize in behalf of their parents!!! How could reconciliation process will be possible with such leader?? 😢😢😢

  • @markoviskyhernandez9706

    @markoviskyhernandez9706

    Жыл бұрын

    All these you are repeating is the narrative of conquerors. Anglo-Saxons helped Kagame and Museveni to invade Rwanda in order to use it as the bridge leading them to the Democratic Republic of Congo. Their narrative is consisting to whitewash themselves and put all the committed atrocities on the defeated government's shoulders and silence all members of the ancient government or other voice which is saying anything different from their narrative because they know that they fed the whole world pure lies!! The court of Arusha had the task of judging both sides and promoting the reconciliation. Instead of promoting reconciliation, they dismissed from the court the General Prosecutor who wanted to judge also the side of Kagame. They instead promoted the division among Rwandans and even at this second, Rwandans are fleeing the country. Don't put the genocide on refugees because the majority of them are below 40 years old and they are of all ethnies!!

  • @mathewsmwale20
    @mathewsmwale20 Жыл бұрын

    Lazarus chakwera is not fair why can he allow such people to enter his country maybe he knows something and they offered him some money

  • @user-ks3uw3pq7d
    @user-ks3uw3pq7d Жыл бұрын

    Pena ndkaikhala ndi kumawona ngati kamuzu anasiya buku lina rake kuchipani cha m.c.p lophuzitsa dza ulamurilo wawo 😢😢

  • @andrewkapanga-jo2cj

    @andrewkapanga-jo2cj

    Жыл бұрын

    Exactly the way i think.

  • @user-ks3uw3pq7d

    @user-ks3uw3pq7d

    Жыл бұрын

    Sirius

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Fact brother

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 Жыл бұрын

    Malawi lero Ali pa mpeni vuto ili Matsatatsata Amalawi lero ndi izi Ntchito Qne million zija ma Mega farm aja Kudya katatu kuja ndikumeneku amalawi kususuka lero ndi nkhondo iyo

  • @frankmajawa528
    @frankmajawa528 Жыл бұрын

    Km iziz sizabwino these ppo came here bcoz they wanted peace and they hav sweat alot fo them to get wat ever they hav now penapake ndbwino kumaganiza kut ndtakhala ine ndkupangidwa zimenezo ndnganve bwanj, God must be the only helper

  • @user-bm8kh9rw6u
    @user-bm8kh9rw6u9 ай бұрын

    But the question is How many richest people are leaving in out of the country? Chakwela please treat well the pples

  • @nyararaishumba9288
    @nyararaishumba9288 Жыл бұрын

    Chakwera walandilapo ndalama pamenepo afuna aphese Anthu bas

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Kwambiri zedi iye wadyapo miyoyo yathu ikupululuka😢

  • @justicenyirenda2049
    @justicenyirenda2049 Жыл бұрын

    Timva zinthu🙌

  • @AlexKaunda-ir6rz
    @AlexKaunda-ir6rz Жыл бұрын

    Zikhare ng'oma mbuzi yamunthu mulizelu m'menemo Mutu unangokula 😂😂😂❤

  • @aishaayatu8653
    @aishaayatu8653 Жыл бұрын

    Koma tiona zindunthu muulamuliro wa chakwera Sono anthu ameneyo akayamba kuwaombera abale awowo ife amalawi tiziti kuli chani

  • @anafieintuka8090
    @anafieintuka809011 ай бұрын

    Inu ndiye mozi kwa history

  • @user-zh1th3uc9f
    @user-zh1th3uc9f Жыл бұрын

    Abusa sakuchitadi bwino Dr chakweka

  • @professorsafuta3936
    @professorsafuta3936 Жыл бұрын

    Mmmm koma ndiye zosakhala bwino ndithu, eeish

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 Жыл бұрын

    Chakwera ndichitsilu mbolo yamake wakupha!! Guys we vote for wrong person , chosadzi nafenso!! Big up my brother for your good research!!

  • @ManuelMalunga-fl3vq

    @ManuelMalunga-fl3vq

    Жыл бұрын

    Very bad my Malawi😢😢😢😢😢

  • @JeanMarieNsengiyumva-qu9vm
    @JeanMarieNsengiyumva-qu9vm Жыл бұрын

    😭😭😭😭😭yoooooohhh Mulungu Tetezelani ana akoo

  • @alannyirenda588
    @alannyirenda588 Жыл бұрын

    Very shameful

  • @AlexKaunda-ir6rz
    @AlexKaunda-ir6rz Жыл бұрын

    Chakwera mbolo yako sure Ngati dziko lakurephela zisiye panyapako😂😂😂❤

  • @sumanmedson6068

    @sumanmedson6068

    Жыл бұрын

    Koma adaha😄😁😁😆😅🤣😂😂

  • @nashoniclifford172
    @nashoniclifford172 Жыл бұрын

    Wait Malawi idzazindikira bwino patsogolo

  • @jaykar-issa706
    @jaykar-issa706 Жыл бұрын

    Gen Nyakarundi Vincent is Army chief for intelligence, Imachedwa Department Military Intelligence ( DMI)... ndi anthu oopsa zedi! 😢😢😢

  • @daviemafunga
    @daviemafunga Жыл бұрын

    Munabadwa masiku okwanira brother mumakwana heavy

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b3 ай бұрын

    Chonde Mulungu lowereraniponi amenyereni nkhondo ma refugees amene akukhala dziko la Malawi mizimu ya anthu osalakwa ikuzunzika

  • @emmanuellemson2683
    @emmanuellemson2683 Жыл бұрын

    Mamvuto osewa akudza kamba ka gulu lomenyera ma ufulu nd omwe anakankhira dziko la malawi ku gahena pofuna kuti chakwera ankhale mtsogoleri wadziko la malawi.

  • @evancenasoro922
    @evancenasoro922 Жыл бұрын

    Mwatisuka mmaso apa boss 🎉😊

  • @user-yk9lx7xd1i
    @user-yk9lx7xd1i Жыл бұрын

    Marefugees sakhala pakati padziko ayi uyu amalandila ndalama kuti azitchuka ndi zinthu zopweteka amalawi azake mtayeni

  • @kamwendoderek6567
    @kamwendoderek6567 Жыл бұрын

    MAY TRUE GOD SAVES THE LIFE OF INNOCENT PEOPLE LIFES,,, MAY THOSE REFUGES DEPEND REFUGE IN GOD ALMIGHTY GOD AND JESUS CHRIST, THE OWNER OF LIFE

  • @user-bg5sl3xk6n
    @user-bg5sl3xk6n Жыл бұрын

    😢Yo

  • @jacquesnsabiyaremye3166
    @jacquesnsabiyaremye3166 Жыл бұрын

    Apapa zayambika, Chakwela akusewela ndi team((Rwandan Solders) imene sakiyidziwa. Anthuwa amalora kupeleka ndalama iliyonse cholinga aketse mwazi(Blood) basi. Mukaitsatila bwino nkhani mupeza kuti boma la Malawi lalandira ndalama za nkhani nkhani cholinga Ma Refugees asowe mtendele basi. Si izi Zayayambika ku Chileka ndi madela ena ndi ena.

  • @alfredbanda886
    @alfredbanda886 Жыл бұрын

    Bulutu chakwela mbuziiiii meeeeeeee chitsiru chamunthu

  • @NgaboJeanvier-iw4yu
    @NgaboJeanvier-iw4yu Жыл бұрын

    Great documentary from intelligent man... true story of best killer in our continent..big up man

  • @AlickNyirongo-cp1dn
    @AlickNyirongo-cp1dn Жыл бұрын

    chakwela sure bt niphala la munthu angalowese asilikali a ku ruward sure

  • @georgechikafutwa1334
    @georgechikafutwa1334 Жыл бұрын

    Funso nkumati kodi ma Hutuh kwao ndikuti ngati akukhala mothawathawa dziko laku Rwanda?

  • @yampanyamulenda9377
    @yampanyamulenda9377 Жыл бұрын

    Whaooww 😲😲 I can't believe that in Malawi you have such brilliant journalist 🤔🤔 Tell them, teach them 😂😂😂 Many people don't know exactly what we be the consequences of the presence of this rwandeses on the Malawi land

  • @adsonphiri6497
    @adsonphiri6497 Жыл бұрын

    Kagame waona KT ma masters ake a NATO mphamvu zayamba kutha ndichifukwa chake akufuna kupha,ma Hutu onse kuopa kuzalandidwa boma,munthu oyipa kwambiri

  • @user-yk9lx7xd1i
    @user-yk9lx7xd1i Жыл бұрын

    Osaopseza a malawi chifukwa chofuna kutchuka ayi malawi sikuyenera kusunga marefugees pakati pa DZIKO ndichibwana away azipita akulepherana olha kudziko lakwawo kukambilana atisiye amalawi tizipanga azathu achoke pakati padziko

  • @ChrispinMachemba-zt6rm
    @ChrispinMachemba-zt6rm Жыл бұрын

    Aboma angosatila chomwe auzidwa alibe direction yoyendesela dziko

  • @oscarkachale9234
    @oscarkachale9234 Жыл бұрын

    Live them

  • @Rafiki-pk7hw
    @Rafiki-pk7hw Жыл бұрын

    Chakwala ndikamukonsa koma mmmm ndaona kuti ndi manyi amuthu

  • @jimmyzgambo9928
    @jimmyzgambo9928 Жыл бұрын

    We don't want war here in Malawi