BON KALINDO 11 JULY 2024 KUNG’ALURA PA THURSDAY

Пікірлер: 223

  • @VungaQueen
    @VungaQueen19 күн бұрын

    Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥

  • @FRAVIOKUNSANJA

    @FRAVIOKUNSANJA

    19 күн бұрын

    Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk19 күн бұрын

    Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana19 күн бұрын

    Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg

    @INNOCENTMOFOLO-io8tg

    19 күн бұрын

    😂😂😂😂😂 DC ndiyakatundu zoona

  • @user-hk3hg1to4e
    @user-hk3hg1to4e19 күн бұрын

    Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢

  • @FisherAction
    @FisherAction19 күн бұрын

    Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt18 күн бұрын

    God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np19 күн бұрын

    This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note

  • @GoodsonDiwadiwa
    @GoodsonDiwadiwa18 күн бұрын

    The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi

  • @StevieChikaonda
    @StevieChikaonda18 күн бұрын

    Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya19 күн бұрын

    Koma Mulungu ngati kunali kufuna kwanu kuti munthu uyu awulawe u president ayi pafikapa ife anthu anu timveni kulira kwathu 😢, Ife anthu akumuzi kuti tigule sopo timadalira kuvuwula mchenga omwewo kuti tichape, onani pomwe zinthu zafikapa Yehova, ingobwerani muzaweruzepo dziko lanuli Ambuye

  • @EmmanuelMpalagule
    @EmmanuelMpalagule19 күн бұрын

    Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,

  • @vitumbikokamanga5869
    @vitumbikokamanga586919 күн бұрын

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤

  • @raytavares2256
    @raytavares225619 күн бұрын

    Mr president the DC we love you and greetings from North London UK

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope19 күн бұрын

    Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you

  • @GamaGama-z8p
    @GamaGama-z8p19 күн бұрын

    Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN19 күн бұрын

    Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉 ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas

  • @RidwanAdam-nq6lz
    @RidwanAdam-nq6lz19 күн бұрын

    Booooon kalindooooo 🔥🔥

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo950218 күн бұрын

    Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂

  • @user-or7ng3fj8f
    @user-or7ng3fj8f19 күн бұрын

    Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC

  • @limbanimtitima9170
    @limbanimtitima917019 күн бұрын

    Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon18 күн бұрын

    Born kalindo more 🔥

  • @pacharokoloviko1694
    @pacharokoloviko169414 күн бұрын

    😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC

  • @kelvinmphande3754
    @kelvinmphande375419 күн бұрын

    It's the sikusinja Gwenembe song for me

  • @user-wu4tl2yn9e
    @user-wu4tl2yn9e18 күн бұрын

    Khaaaaaa wafika the DC

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju19 күн бұрын

    Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t19 күн бұрын

    The dc our poor president in Malawi

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi19 күн бұрын

    The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _

  • @chimwemwemasamba2880
    @chimwemwemasamba288018 күн бұрын

    Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu

  • @user-ko1lk3br4r
    @user-ko1lk3br4r19 күн бұрын

    Mafuta ayamba kuchoka ku Mozambique kukafika ku area 50 ku Lilongwe kudzela pa njanje ai zikomo

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge19 күн бұрын

    ULEMU WANU MR, THE DC..... BON KALINDO 💪✊✊✊📡🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @PempheroKasimongwa
    @PempheroKasimongwa18 күн бұрын

    Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤

  • @JabesAlfaiate-t4v
    @JabesAlfaiate-t4v19 күн бұрын

    A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.

  • @AudettaYohanie-fl3oc
    @AudettaYohanie-fl3oc19 күн бұрын

    Aaaah koma izizi ndiye chakwera wationjedza zedi ,koma chifukwa chani kweni kweni?

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w18 күн бұрын

    Our president more fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌

  • @KnowledgecGodwin-xo4pw
    @KnowledgecGodwin-xo4pw19 күн бұрын

    Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.

  • @MouriceChimkondo

    @MouriceChimkondo

    18 күн бұрын

    Kkkkkk

  • @LovelyJapaneseMaples-xc2bc
    @LovelyJapaneseMaples-xc2bc18 күн бұрын

    Kuswakuswa big osaopa😊

  • @RafickRaj
    @RafickRaj18 күн бұрын

    Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb18 күн бұрын

    MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa

  • @OmegaNjati
    @OmegaNjati18 күн бұрын

    Ambuye nditengeni

  • @mbewemisoyaanenenji1908
    @mbewemisoyaanenenji190818 күн бұрын

    Boooon Kalindo , Pangolin mwana womvuta kwambiri

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb18 күн бұрын

    Uchitsilu ndiye umeneo Sizidachitikepo

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi18 күн бұрын

    Kkkk Boma amalawi kutifinya tiwona zinthu shop chaine chasala ndi maepute katoni okhaokha ndatawira kunnjenga ndiyemukulesa mukufuna kundipha chani mukandiphera kuzenje komweko 😮😮😮😮

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo950218 күн бұрын

    Koma mpaka chenga mmmm mawonjeza

  • @user-lp8wj3vq4x
    @user-lp8wj3vq4x18 күн бұрын

    Ife dzuro timadikira mademo, agalu amenewa atitopesa

  • @HawardStainly
    @HawardStainly18 күн бұрын

    Akubwila fodya wamagogo wakuzino uja,(maganga).

  • @user-hb1ll8lj3v
    @user-hb1ll8lj3v18 күн бұрын

    Gwenembe ND sikisinje yemweyo 😂😂😂😂

  • @OsmanBakali-s5x
    @OsmanBakali-s5x19 күн бұрын

    Where are we going to make our hustle now😭😭😭 mpakana nchenga omweu tkatenge chilolezo? 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MarkinaJohn
    @MarkinaJohn19 күн бұрын

    Kkkkkkk koma DC kkkkk gwenembe

  • @babranzima8120
    @babranzima812018 күн бұрын

    Ndizisilu zaathu zathu ananyerapo chenga iyewo chakwera

  • @MouriceChimkondo
    @MouriceChimkondo18 күн бұрын

    Following boss

  • @loycemmadi9303
    @loycemmadi930318 күн бұрын

    And it's the song for me😂😂😂😂Winiko Ayi ndithu

  • @texonkautera
    @texonkautera18 күн бұрын

    Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula

  • @LamseyChimah
    @LamseyChimah18 күн бұрын

  • @LoveBanda-sw1nu
    @LoveBanda-sw1nu19 күн бұрын

    😅😅😅😅kumalawi mkokoma ndithu bwanawa akutiposa zochita

  • @user-gd6zb2bv8f
    @user-gd6zb2bv8f18 күн бұрын

    Koma funso nkumati kuti, Kodi Chakwela ndi Zikhale wacheyo, samachita manyazi konse akamamva izi? kapena umunthu wanu unatha?? The DC tell them shit

  • @happychimwemwe-1805
    @happychimwemwe-180519 күн бұрын

    Umakwana booooon kalindo

  • @mlimolubanda6348
    @mlimolubanda634818 күн бұрын

    The DC .....

  • @TutuAlfred-y2l
    @TutuAlfred-y2l18 күн бұрын

    😂😂😂😂😂. Zosatheka sizidzatheka nanga chenga ndichani uyo wasala pang'no kt amfe ameneyo chisilu chamunthuyo muuze ambere Ku muloza border kuno aone kt angatile ife kuvuula chenga.

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh627619 күн бұрын

    Uyu ndi nyoooo kwa nyooo ulemu wanu aaaa mchenga athu anayambira kale za mchenga athu amadyera momo abale eishh sambi

  • @BatsonKadzuwa-tl3rp
    @BatsonKadzuwa-tl3rp18 күн бұрын

    Zoonadi mboni ndineyo nditachita ngoz ku Queens ndinalipira kut andithandize

  • @SteveKanongwa
    @SteveKanongwa19 күн бұрын

    A born kalindo mukadikira opposition kuti itisogolere tichedwa inuo tayambisani ife tili mbuyomo

  • @JaxyKumwenda
    @JaxyKumwenda18 күн бұрын

    Tikufuna mademo bwana osamunyengerera Chakwera

  • @InnocentBanda-g6i
    @InnocentBanda-g6i18 күн бұрын

    ❤❤

  • @Vascomw
    @Vascomw18 күн бұрын

    Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza

  • @Sugerman-tw4do
    @Sugerman-tw4do17 күн бұрын

    Big Bos DC mumakwa

  • @IvieMwabile
    @IvieMwabile18 күн бұрын

    Akufuna kutimpha agalu amenewa.go deeper

  • @loycemmadi9303
    @loycemmadi930318 күн бұрын

    Mr kalindo munafika aaaah kukanapezeka ambiri ngati inu bwezi dzikoli titaona zina aaaah

  • @dinahmunthali5324
    @dinahmunthali532418 күн бұрын

    Ine nyimbo ndi zomwe zimandi waza koophya ati Sikusinja ndi Gwenembe amkaimba agogo awake DC popita ku Mzuzu akudutsa mu chikangawa 😂😂😂😂😂 DC makina 😂😂

  • @ChikumbutsoTsalangu
    @ChikumbutsoTsalangu19 күн бұрын

    Ati pedza madzi mu tikuvula chenga tikhapanamo

  • @MarthaJafali

    @MarthaJafali

    19 күн бұрын

    Sure

  • @jameskamanga628
    @jameskamanga62817 күн бұрын

    Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk

  • @densonchiwaya8439
    @densonchiwaya843918 күн бұрын

    Mau awaa sikalindoo

  • @duncainjimmy
    @duncainjimmy18 күн бұрын

    Mulungu adalenda dothi osati Chakwera ai

  • @user-kw7wr4kq9w
    @user-kw7wr4kq9w18 күн бұрын

    We only need solutions not only kulalika

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q19 күн бұрын

    Mafumu aku ntcheu mtima wawo ukuwawa alibe dyera ndi mafumu odziwa kulira moyo wa munthu sizocheza

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo18 күн бұрын

    Ng'alula DC

  • @HannockMesiwni
    @HannockMesiwni18 күн бұрын

    Njira ya ld pokavota sitikavota nkhondo ichitike ichitike

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa834519 күн бұрын

    Kodi a Pule alibe olo foni ya mmanja kuti azitha kuona zomwe anthu akukamba online incase samadziwa zomwe nduna zake zikugwilira ntchito.What kind of leadership is this.

  • @ChondezVick
    @ChondezVick19 күн бұрын

    The DC himself 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @azunguauskay4903
    @azunguauskay490318 күн бұрын

    😂😂 Akalindo nyimboyo ndayikonda

  • @MartinsKhumalo
    @MartinsKhumalo19 күн бұрын

    ❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏

  • @ErnestAllex
    @ErnestAllex19 күн бұрын

    Ku opposition kuli mbuzi zokhazokha ,munthu anali yemwe uja atiphela uja bas😢😢

  • @LinoMatchado
    @LinoMatchado19 күн бұрын

    Iyayi na ya mchenga yokhayo boma likunena zoona chifukwa mchenga is in the group of minerals and any mineral is a government property which is minored through the government permission. Everywhere in the world illegal mining is prohibited citizens are allowed to collect sand ndi wilibala basi not with a thipa truck then you have to go face the law which is in the constitution every country.

  • @JamesKambale-s2c
    @JamesKambale-s2c18 күн бұрын

    Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t19 күн бұрын

    Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo

  • @user-qc7qg4cy6k
    @user-qc7qg4cy6k19 күн бұрын

    Totally agree the dc

  • @user-sv5yi9gt4u
    @user-sv5yi9gt4u19 күн бұрын

    Zoona Born Kalindo auzeni ife tikuvutika kwambirii pa msewu kuno ku Kasungu chamama

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo18 күн бұрын

    Ndiye zaonjedzatu mpaka kuletsa mchenga????

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin19 күн бұрын

    Osakhala presdent bwanji abon kalindo Tayambitsani chipani cha amphawi

  • @PatronChanza
    @PatronChanza19 күн бұрын

    The DC 😂😂😂 😂😂😂

  • @jamesgama5489
    @jamesgama548918 күн бұрын

    Koma inuu!! Ayi zikomo.

  • @christophermukaka7403
    @christophermukaka740319 күн бұрын

    Kalindo ndisaname mukuwatsegula anthu koma bvuto opposition ili weak

  • @KnowledgecGodwin-xo4pw
    @KnowledgecGodwin-xo4pw19 күн бұрын

    Mumatimilira mr president

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn19 күн бұрын

    We are in a Failed State and Chakwera uyuu achoke

  • @IsraelMtawali
    @IsraelMtawali18 күн бұрын

    Chakwera is apus must go

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali19 күн бұрын

    The DC boooooon kalindoooooooo

  • @ZainuluNsalule
    @ZainuluNsalule18 күн бұрын

    Good

  • @chipilirokalison1334
    @chipilirokalison133419 күн бұрын

    Denkha Born mulungu azikudalisani koma opposition yadekha ndicholinga usadande iwe mulungu azikudalisa

  • @KnowledgecGodwin-xo4pw
    @KnowledgecGodwin-xo4pw19 күн бұрын

    Mulungu wanthu ndiwamoyo Sagona ndipo saodzela Ndithu chakwela alandila mphoto yake monga mwa ntchito zake zokupha wanthu osalakwa.

  • @stanfordnsona
    @stanfordnsona18 күн бұрын

    Kalindo umatitsekula maso

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q19 күн бұрын

    Ndipo zoonadi chonsecho sanapangile anthuwo chochita