JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1

Пікірлер: 229

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko8 ай бұрын

    Malawi needs such people to develop!!!

  • @charlesmuwanya7845
    @charlesmuwanya78458 ай бұрын

    Mr John Kapito has given a true account of the real situation in Malawi. He is a senior soothsayer. He is always for the whole truth. He doesn't mince words & his desire is to set things right.

  • @user-ym9eg6qg6t

    @user-ym9eg6qg6t

    8 ай бұрын

    Jst straight to the point

  • @JafaliAkimu-ll1bf

    @JafaliAkimu-ll1bf

    19 күн бұрын

    chakwera ndi chitsiru cha munthu mdziko muno mbava

  • @user-bq9rj2mi4h

    @user-bq9rj2mi4h

    6 күн бұрын

    koma maiko anzathu zimachitika ngati zimachitika kwathu kunozi kapena nkhani ndiyathu kunjaku....malawi wafika penipeni pomvesa chisoni mmmmm Mulungu atithandize

  • @user-ez4ru5sk2l

    @user-ez4ru5sk2l

    5 күн бұрын

    Mr Kapito we are very happy with your insight....Malawi ... needs a Servant not a leader....All our former presidents have travelled and most of them been overseas....but they are failing to bring our country to the international standards....I live in South Africa my passport expired last year...I renewed from the consulate....I paid in Blantyre....but up to now Nothing..I am working here no passport..... Immigration is in full corruption..... and disfunctional ...and it's a revenue govt department..Now if they are failing it means that they are bringing the country down.....suck all corrupt officials....we can't be suffering outside the country cause of these rotten officials...... and where is the minister of homeland security.....where is the president.....shame on you guys.....

  • @PatrickTembo-lm1ih
    @PatrickTembo-lm1ih6 күн бұрын

    Koma apapa mwayankhula chilungamo ngakhale msogoleli alindimaganizo amenewa likhoza kukhala boma mkhoza kuyendesa boma bwino ❤❤❤❤

  • @AllanMwakalenga-wn5ib
    @AllanMwakalenga-wn5ib8 ай бұрын

    Kapito umakwana... If possible mungoyima pa u president.. we will vote for you

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk8 ай бұрын

    Big up Bwana Kapito, you are indeed a great man, I have really enjoyed your explanations 🔥🔥🔥🔥

  • @user-fg8zw2bf4m
    @user-fg8zw2bf4m8 ай бұрын

    Very clear message Mr Kapito may God bless you and your family and God bless Malawi country

  • @user-vt5cf3dw1l
    @user-vt5cf3dw1l10 күн бұрын

    Good explanation without taking politics but only justice ⚖ landilani ulemu Mr John Kapito😊😊😊

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz6 күн бұрын

    thank you sir kapito for your explanation

  • @simionkonyane368
    @simionkonyane3684 күн бұрын

    God bless you Mr Kapito wayankhula mfundo zenizeni❤

  • @mkhulukinyata5198
    @mkhulukinyata51988 ай бұрын

    Well spoken Mr Kapito..Indeed Malawi tikufuna anthu wolankhula dzokupsa ngati momwe alankhulira Mr KAPITO apamu

  • @user-iy8vi7nn8r
    @user-iy8vi7nn8r8 ай бұрын

    Good explanation sounds like izeck somewhere (kukagwirana ndi azungu 😅😅😅 nice one Mr kapito

  • @user-hu7qs5be4j
    @user-hu7qs5be4j20 күн бұрын

    Mr kapita you're true leader

  • @williamskondowe8795
    @williamskondowe87958 ай бұрын

    Respect Mr kapito otsaopa ,otsapweketsa we're all malawian don't fear lf there's justice

  • @user-id9df1kn1i
    @user-id9df1kn1i8 ай бұрын

    Kapito your e a big man ayi pano ndiye ku Malawi sikulibwno ayi.

  • @user-xi2vo4gc4u
    @user-xi2vo4gc4u9 күн бұрын

    Mr Kapito a man himself he doesn't fear nothing .He is so intelligent

  • @alicekalupsya7149
    @alicekalupsya71497 күн бұрын

    Ur a man full of wisdom.

  • @user-eu1qs1eu5q
    @user-eu1qs1eu5q8 ай бұрын

    Mr kapito ukunena zoona koma nkhani yimozi yonkha ndiyankhepo. Chilima sangayendese boma ndimunthu wonama kwambiri. Ndiye ngati mutsogoleri ali ndiboza sangatumikire anthu. Chilima ndi chakwera ndichimozimozi. Chilima ngati akanankhala kuti akufunila zabwino amalawi bwezi atatuluka mu MCP chifukwa akanamuwuza chakwera kuti zimene tinauza anthu kuti tiwachitira sizikuchitika naye ali mphee Choyamba kuyendesa ziko ukhale wa zeru and kuzichepesa kwa amene anakukweza. Kuopa Mulungu.

  • @user-bq9rj2mi4h

    @user-bq9rj2mi4h

    6 күн бұрын

    mfundo ndipo ndizoona

  • @JUMAHSabiti
    @JUMAHSabiti11 күн бұрын

    Good explanation posatengela ndale ❤ koma chilungamo chokhachokha

  • @user-ur2pf9ts2p
    @user-ur2pf9ts2p7 ай бұрын

    Thank you Mr kapito mwanena zothandiza ziko la malawi Kodi achakwera mkuva please pasto mrungu akuyang,oneni

  • @MikeMadeya-xm4uy
    @MikeMadeya-xm4uy8 ай бұрын

    Mr kapito please 2025 please stand for people

  • @lame8
    @lame88 ай бұрын

    Zimangovuta koma chaka China tizapeza wabwinoyo❤ msogoleli wabwinoyo is our hope tizabowoleza tili ndi anthu azelu kumalawi ambiri

  • @blandinabonaventure

    @blandinabonaventure

    8 ай бұрын

    Yes

  • @macdonaldphiri4826

    @macdonaldphiri4826

    8 ай бұрын

    Anangokhala ndi nsanje kumuchosa peter pampando

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y8 ай бұрын

    Good explanation uncle. The Country need people like you not Chakwera,He must go back to his church not rule the country. The citizens are suffering alot because of him.

  • @petertukula1649
    @petertukula16498 ай бұрын

    Mr Kapita Bravo.... awa ndi mau

  • @Yasinta-mh3cb
    @Yasinta-mh3cb4 күн бұрын

    Ineyo I don't say much kuopa wat am saying is may the good Lord in heaven protect U in his wings be safe my father it's my prayer eeeesh real man for Ur own parents who is U exactly heeee God save my father his real

  • @stevenchidathas4477
    @stevenchidathas44778 ай бұрын

    I like this Man, Mr Kapito keep on😊

  • @douglasturner2992
    @douglasturner29927 ай бұрын

    You deserve to be a leader...

  • @MuhammadSamson-yz1kl
    @MuhammadSamson-yz1kl8 ай бұрын

    Respect kapito osaopa achakwera ndi nyani

  • @LovelyAzaleaFlower-uc8vr
    @LovelyAzaleaFlower-uc8vrАй бұрын

    Well explanation, Malawi needs such people

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w8 ай бұрын

    We're together mr Kapito

  • @user-qg6su9rx2k

    @user-qg6su9rx2k

    7 ай бұрын

    Kodi akapito amagwira ntchito yanji kodi abale

  • @user-qg6su9rx2k

    @user-qg6su9rx2k

    7 ай бұрын

    A brian banda mulibenso nzeru ndiyesa ndi mankhwala oyeretsa thupiwo mwina ,kodi ndege ku malawi zinasowa liti?

  • @EliahLetulo
    @EliahLetulo7 ай бұрын

    Kma mr kapita you are the great man ❤😂

  • @jaydee1236
    @jaydee12368 ай бұрын

    Brilliant ❤ Mr John kapito

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr19 күн бұрын

    True Malawian, Mr Kapito. Okumbira mnzake dzenje, adzagweramo yekha. Lero anadzikumbira okha dzenje ku IMF.

  • @Mfwanayo
    @MfwanayoАй бұрын

    This Mr Kapito why he's true and direct like this.......shaaaa ndipo ndamkonda bwanj.....in Malawi we also have brilliant and straight people this like

  • @user-zj2dr2rp1e
    @user-zj2dr2rp1e8 ай бұрын

    Brian ndi bambo kapito, boma ili ndi masanje eni eni, ndipo ukunena zoona bambo kapito, Chakwera sankhadziwa kuti angalamule dziko, mu mutu muli gwa! Sadziwa chilichose.

  • @charlesmuwanya7845

    @charlesmuwanya7845

    8 ай бұрын

    The real situation. Mr kapito is a soothsayer. He doesn't mince words. He calls a spade by its name.

  • @natashayohane

    @natashayohane

    7 ай бұрын

    Zowona m bomamu muli nyasi

  • @user-ej5mc5cj8f
    @user-ej5mc5cj8f8 ай бұрын

    Big up boss man... you're a great man

  • @DoreenAllan-tg1dz
    @DoreenAllan-tg1dz8 ай бұрын

    Mr Kapito muyakhura chilungamo

  • @allanbanda4388
    @allanbanda43888 ай бұрын

    100% Mr man matiimilila ifeyo anthu amene tilibe kuthekela kofikitsa nkhawa zathu koyenela kupititsa nkhawa coz anthu tilinazo zolankhula zodzadza mitima komaso chilungamo dziko lamalawi lofunika fix kugwedeza kukhutchumula nyansi tikhale ndiatsogoleli osadzikonda moonjeza amene amalimbikitsa timbamva ma offence ndicholinga chofuna kukhututsa mimbazawo kumamupsinja munthu angakhale olimbikila paiye yekha km Mmmm oky god bless you Mr kapito please musakakhale pansi mubweleso kumalankhula osaopa please thanks

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox28658 ай бұрын

    Bravo kapito!...respect

  • @user-vf9oz7jq6r
    @user-vf9oz7jq6r8 күн бұрын

    Bwana kapito kuzang"alula khokhooo

  • @ChomeNgondolo-uh5mu
    @ChomeNgondolo-uh5mu8 ай бұрын

    😂😂kugwilana zanja ndi mzungu mkumatinamiza ife kuti zinthu ziyenda 😂😂😂

  • @greymasha838
    @greymasha8388 ай бұрын

    God bless you and keep it up and this is well said

  • @MaxwellMustafa-ec8fc
    @MaxwellMustafa-ec8fc8 ай бұрын

    God bless you sir Mr kapito

  • @FanscioDancun
    @FanscioDancun17 күн бұрын

    This man is speaks the truth

  • @ChimwemweMarkBanda-yj7yk
    @ChimwemweMarkBanda-yj7yk8 ай бұрын

    Pempho Mr Brian Banda. Would you please visit anthu anchimidzi kuti muone how pple are suffering and see how they are surviving with every days life. Anthu amene adavota akufatu😢

  • @innocentkapachika6591

    @innocentkapachika6591

    8 ай бұрын

    Take this comment very seriously. Take a chance and visit voters in the the remote areas. For example, come and visit Dedza South Constituency the most Least Developed Constituency in Malawi

  • @user-zz3lf9qd5m

    @user-zz3lf9qd5m

    8 ай бұрын

    Eish ndipo very pain full vote lako lomwe kumagona osadya😢

  • @alexdausi5167

    @alexdausi5167

    8 ай бұрын

    ​@@user-zz3lf9qd5mkoma Mesa amati tizidya katatuh everydey

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata693319 күн бұрын

    I like Mr kapito's explanation

  • @georgesmart3791
    @georgesmart37918 ай бұрын

    More fire mr Kapito🔥 🔥 🔥

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward9478 ай бұрын

    Boma lavuta ili pangolini amanena zoona respect the DC

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox28658 ай бұрын

    50 years plus depend on foreign aid....i wish bingu was alive

  • @MikaNamwada
    @MikaNamwada19 күн бұрын

    Well said kapito🔥🔥🔥🔥🔥

  • @chikaonekarh
    @chikaonekarhАй бұрын

    Our own KAPITO mumatiyimilira koma kunsanva a President,ndakusokosela mkulinga utava! Zayekha adaviyika nsima madzi musiyeni timuona 2025 Chakwera

  • @DannieChimenya
    @DannieChimenya19 күн бұрын

    Mr kapito God bless you sir

  • @user-fk3vw7ck3z
    @user-fk3vw7ck3z7 ай бұрын

    Us Malawians we need to have readers from over seaze

  • @George-zd5le
    @George-zd5le8 ай бұрын

    Sir Kapiti ndinu munthu wanseru. Genius man

  • @FernandosLuciano-bb9or
    @FernandosLuciano-bb9or8 ай бұрын

    Uwuwu ndi kantho kapena chilango cha mulungu pochosa msogoleli wabwino peter ndijuika mbava ngothi ndizisilu zones zili mu tonse palibe chomwe chisinthe mpaka 2030

  • @ChristinaNyirenda-zb1if
    @ChristinaNyirenda-zb1if9 күн бұрын

    Good Mr kapito

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv2 ай бұрын

    Great ones Mr kapito

  • @user-hu8vp4wt7j
    @user-hu8vp4wt7j8 ай бұрын

    Mr kapito i respect you 🙏

  • @natashayohane
    @natashayohane7 ай бұрын

    Zovetsa chisoni mmene yatulukila maina oti apindule ndi zipangizo zotsika mtengo pa fumu dzina limodzi

  • @Goliath461
    @Goliath4618 ай бұрын

    Paja nyau yonunkha manyi ija amati zinalake chani?la chakwera tachosa koma la nyau yonkha ija😂😂😂

  • @bigmount563
    @bigmount56319 күн бұрын

    I am sorry for my self I missed this program, but I koma Mr kapito Mulungu azikudalisani ngati chakwer a sakumva ixi afe ndithu

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf22 күн бұрын

    Bambo Kapito now you are Talking. Keep it up

  • @user-ez4ru5sk2l
    @user-ez4ru5sk2l5 күн бұрын

    Mr kapito well said as far as you not talking on behalf of someone....

  • @user-gv3rt3in9l

    @user-gv3rt3in9l

    5 күн бұрын

    Then don't comment if you don't trust him

  • @CeciliaKamanga-mx9dc
    @CeciliaKamanga-mx9dc6 күн бұрын

    Bravo kapito 100% agree 👍

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr8 ай бұрын

    M'manja mwa akapito pwa pwa pwa

  • @user-ez4ru5sk2l
    @user-ez4ru5sk2l5 күн бұрын

    Malawi needs the young leadership with vision...all old people please sit down....u have not done our country any good

  • @user-dr7ct2zt8n
    @user-dr7ct2zt8n18 күн бұрын

    Mr John kapito keep on trying to assist the blind

  • @khalifacalvinajass9998
    @khalifacalvinajass99988 ай бұрын

    Akulu awa ndagwilizan nawo kwambir

  • @AgnessKavalo
    @AgnessKavalo2 күн бұрын

    Kkkk koma ndaseka mokweza atagwilana ndi nzungu 😅😅😅😂😂😂

  • @MahmoudZebron
    @MahmoudZebron11 күн бұрын

    Ndilibe mau mbili bwana kapito you're good man you're a m'dala 😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @mussamapira801
    @mussamapira8018 ай бұрын

    A chakwera Ali ngati chipilala 2angokhala mu office ndiye zinduna zano zimangobwela zainani apa chakwera ku zaina palibe chomwe akuziwa dzikoli akuyendeza ndi zinduna pamodzi ndi banja lawo

  • @user-tn2qg1vs9j
    @user-tn2qg1vs9j8 ай бұрын

    Appreciate bwana kapito

  • @alexvwalika2242
    @alexvwalika22427 ай бұрын

    Mr kapito inutu inutu mukukamba dzeni dzeni

  • @phillimonzgambo1663
    @phillimonzgambo16638 ай бұрын

    Good speech kapito

  • @madalitsokalulu2720
    @madalitsokalulu272018 күн бұрын

    Mr Kapito katswiri

  • @HanishaissahKagansa
    @HanishaissahKagansa8 ай бұрын

    Ndizoonadi alowa m,boma alibe Maso mphenye then nsamadziwa kuti kuyendetsa dziko ndichinthu chomvuta

  • @raytavares2256
    @raytavares22568 ай бұрын

    How can you say Chilima has not been tested and yet he was arrested for thieving yet still working getting payed on Malawian tax payers? Was he not suspended?

  • @lukeshawa-mv6ed
    @lukeshawa-mv6ed8 ай бұрын

    Yea man of confidence

  • @ammaarahkhota7939
    @ammaarahkhota79398 ай бұрын

    ACHAKWERA AKUFUNA KULEMERA SINANGA AKUDZIWA SAKHALANSO PA MPANDO. PALOWANSO ENA .NDIYE OSAMADABWA RATE YAKUNJAILI KUTI .UTSOGOLERI SASITHA NGATI MALAYA .MAPETO AKE ALIYENSE AZINGOLOWA CHOLINGA CHOTI NDILEMELELETU SINANGA CHAKA CHAMMAWA AKULOWA ENA. AWA NDI MAVUTO AWAYAMBA DALA. VUTO NDI IEFE OKHALA KUMUDZI.

  • @user-qm1qb2jp4s
    @user-qm1qb2jp4s7 ай бұрын

    Bravo kapito chakwera and his government they have failed to read 🇲🇼

  • @user-re5of7tl2o
    @user-re5of7tl2o8 ай бұрын

    Palibe angamutsutse mkuluyu

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera72718 ай бұрын

    That's true chakwera has failed eeeich Malawi 😢 need good leaders

  • @user-oi8ol1tx8h
    @user-oi8ol1tx8h3 күн бұрын

    Stay safe Mr Kapito

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward9478 ай бұрын

    Respect Mr kapito

  • @user-oh6qd3xx4i
    @user-oh6qd3xx4i7 ай бұрын

    Bravo Mr kapito

  • @joicemartin-ji5zu
    @joicemartin-ji5zu8 ай бұрын

    Cakwera ndi wasatanic sAngamve china chiri conse sangaone Kuti anthu akuvutika akufuna anthu afe ndi njala kumidimakupite magazi ambiri

  • @mariezorgen7735
    @mariezorgen77358 ай бұрын

    Thanks alote

  • @JonahTBrighton
    @JonahTBrighton3 күн бұрын

    Reality is needed to make something right

  • @gkay-striker
    @gkay-striker7 ай бұрын

    Chakwera Ndi Galu Kwambili We Are Tired Of Him

  • @blessingsphiri878
    @blessingsphiri8787 ай бұрын

    True about fac leadership

  • @YohaneChimkango
    @YohaneChimkango11 күн бұрын

    Mr kapito mumakwana mukunena zoona

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc8 ай бұрын

    Kunena zoona, mmalawi muli anthu amitu yoganiza kwambili.2025 achoke basi.

  • @mkhokholasamuzonda5094
    @mkhokholasamuzonda50948 ай бұрын

    iwe chakwera ndi chilima mboleizamanu anthu anga akubvutika kwambiri mwanva...

  • @RaphickBanda-hz4gx
    @RaphickBanda-hz4gx8 ай бұрын

    Part 2 please

  • @solomongondwe8610

    @solomongondwe8610

    8 ай бұрын

    26:58 27:00

  • @user-yx9qz2lp5h
    @user-yx9qz2lp5h18 күн бұрын

    Carry.on.bwana.kapito

  • @alomuddin8801
    @alomuddin88017 ай бұрын

    Mr kapito mukunena zoona, tilakhulireni ife tilibe mwayi olakhula zakhosi

  • @Johnfrank-gi5uc
    @Johnfrank-gi5uc8 ай бұрын

    That's true Mr kapito awunikileni Mr president kut asagwe kupompho

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e19 күн бұрын

    Izizo ndi zoona,Koma ku malawi sikudzatheka muika bwanji munthu osaphuzila Kukhala president,inu mmaona ngati m'busa ndiwomukhulupilira kwambili,munatilakwila kwambili ndipo mulungu azikukhulukilani anthu inu

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so8 ай бұрын

    Big up mr kapita malawi need people like you.

  • @ibrahimdini2148
    @ibrahimdini21487 ай бұрын

    Kapito is genius

  • @mphatsocaseywilson9113
    @mphatsocaseywilson911318 күн бұрын

    Big up