Dont provoke DPP, we hate them earlier, and chose to change, DPP remain silents for us to taste and enjoy our choice.
@Dakamacdonald-sl4rk13 күн бұрын
True son of malawi kapito
@petermasenti20848 ай бұрын
Mr kapito inuyo ndi a bodza nthawi ya dpp mumapanga ma demo Koma pano zinthu zikulakwikwa mwangokhala chete chifukwa Mukudya nawo ndalama, chotsani kaye chisoso chili diso lanu musanayambwe mwawona chili mwa zanu
@MarkGonda-qr4vm7 күн бұрын
Nthawi imeneyi dpp imalamula otsutsa amatsutsa zimene iwowo akhoza kukonza zinthu koma zinthu sizinasithe ndiye lero kuti dpp azitsutsa a mcp akhoza kumati munali m'boma momwemu mumatani ndiye izi ndi zandale zozuta kumalawi bas
@winstonpchilonga67128 ай бұрын
I saw the whole interview, Walakhula zilungamo zenizeni
@achithoko19818 ай бұрын
Nyau yalira mokweza pk kutukwana😅😅
@user-zj2dr2rp1e8 ай бұрын
Chikhulupililo chatha Brian pa boma la Chakwera, eish! Kaya tilowere kuti a Malawi. 😢
Kodi Mr kapito mukulakhula bwino kwambiri ngat big man bingu anakusilani zeru asanamwalire or bwanji
@user-kp1zc6su3k8 ай бұрын
Our president chakwera , He was thinking to rules world is easy 😂😂😂
@JossumPhiri-qx9jx8 ай бұрын
See the real malawian citizen 💯
@Syakinongwa21 күн бұрын
CS wachisawawa ngati ameneyu
@fysonbilly41237 ай бұрын
You Said Chakwera doesn't have experience simply mean he cannot run the government,,,
@MaxwellMustafa-ec8fc8 ай бұрын
Maso phenya yanga ine mr simbi phiri koma apo biii malawi never come alright never
@SheenahMwalabu-iz3pr
8 ай бұрын
Ndipo zoona zake ❤
@user-mc8gk4xv3f8 ай бұрын
Komadi a kapito ndiinu ofonikira mutakhala president wa dziko
@rachelbanda21318 ай бұрын
😂😂😂it's sizibwera pa manja koma wakaaaaa😂😂😂zalowa ku account
@louismlanga22308 ай бұрын
Komandekulakhula mosaopa eeeehe
@frankkasenda92528 ай бұрын
Malawi lawi la moto
@user-jk8sh7fh2d8 ай бұрын
Eeeh ok hp u r saying the fact , kma ndie zosaenda , apa nkhani yakula anthu azindilambila pa chifukwa choti ine ndi wankulu than enawa zavuta. Vuto ndi lomweri nsogoleri wadyela osakonda ziko lake
@kejescompany-zi1ft7 ай бұрын
Zaziiiiii Mesa malawi ankauzidwa kuti MCP dizinthu Koma okha Amafuna dala nde mukufuna DPP izitani? Asiyeni a DPP azipuma... Mesa mumati asogoleri aDPP samatha kulankhula nde mukufuna chani?,,, mpando wa u president anausiya mopanda kukangana ndi munthu kuutengaso azatenga mosakangana ndi munthu.... Zomwe mukukamba zikunveka zanzeru Koma musalimbane ndi DPP, am not a politician but,, vuto si DPP or MCP Koma tokha amalawi timafuna kusintha now kusintha takuona.. Then next choice we shall make it with real sense.
@preciousdyton9108 ай бұрын
Akapito ali ndi nzeru 😮munthu wanzeru amaoneka polankhula
@user-fr3ge2hf6s8 ай бұрын
Mr kapito zikomo tikuziwa zambiri koma amalawi tikuvutika 😱
@namberalovemore20568 ай бұрын
😂😂😂 Koma mkulu uyu sapsatira
@user-qp8kh2hj9o22 күн бұрын
Koma mwamumva wanena tu kuti a DPP ndi anthu ozikonda a kunama? 😂😂😂😂😂😂😂
@stephancommercial5807 ай бұрын
Where were you⁉️ here to go
@richardbanda9997
21 күн бұрын
A Kapito izi mukanakhala Kuti munayamba chonchi poyamba atakupatsani udindo Ku Cama, bwenzi nditakupangani salute Koma Ai udindo wanu ,mumangodya osaganizira the poor Malawian as poor consumers. SHAME, mukufuna udindo winanso? People have been criticizing you for not assisting them as per your responsibility to Malawians.
@user-yk1dt1vj2x8 ай бұрын
Iwe ndi fisi bakha mbalame Kodi si inu nomwe dpp ikakonza zinthu mumawononga inu nomwe munati achoke osatenga iwe bwanji bomalo ukhale wanzeru kuliratu uku ukumufuma peter kuti abwelere unali kuti anthu amaphwanya sukulu misewu yomangamanga takhalapo bwino nthawi ya Bingu tikukumbukila sizoyenela iwe kutiuza unali kuti iweyo
@user-fl5im4us7x8 ай бұрын
Chiyembekezo pa chakwela tinasosa
@samdiverson97337 ай бұрын
vuto ndi nankhumwa he is sleeping sakulankhula kanthu😴
@AustinChiyembekezo-cx4mz8 ай бұрын
And it's very true why Dpp annoying,ana
@rodrickphiri
8 ай бұрын
DPP will never bounce back is dead and the country is moving without opposition this is pathetic
@patriciap.bandah33858 күн бұрын
Panopa ndawamvesa a DPP chimene amakhalira chete President uyu ndi wamagazi ifeyo tikuziwonela kunja koma anzathuwa akuziwonela pafupi President uyu si munthu wabwino a DPP akhalebe chete mpaka campaign iyambe
@samdiverson97337 ай бұрын
ngwabodzadi president yu
@AkimuKalinde-kx4cn8 ай бұрын
chakwera sinikumuonera kukondwa ta mins watipha
@user-my5jj5we5j3 ай бұрын
Voti yaimwe yilipo
@ChamboChange-pq1hd8 ай бұрын
Chakwela ndi galu kwabansi tsiku transport moyenda
Пікірлер: 97
I love your speech Kapito keep on telling them the fact we have suffered for so long and this is too much now
This man has leadership qualities right away from secondary school days at Mulanje Secondary school . Malawi needs leaders of Kapitos cariber.
Mr kapito God bless to open eyes all Malawian I never seen a man like you to openly talking nicely
koma boma ndi ndale zinayandikana kwambir mpake dziko silitukuka ku malawi. thanks mr kapita❤❤❤❤
Truth and powerful talking, proud of you Bwana Kapito, inu ndi mtondo, I salute you, ulemu wanu Bwana 🔥🔥🔥🔥
Tapangani chipani Chanu inu akapito muwina inu muli kuganiza Kwa u utsogoleri 100% ❤❤❤❤
Mr Kapito ?? Thanks very much for your experience & knowledge Apatu mukulilira dziko lathu deep from your heart ❤ Mulungu..The heaven creator must
Koma Kapito ndi 🔥🔥😝😝🙏🙏❣❣
More power Mr kapita may God bless you you're a true reader mr
Properly articulated. God bless and good day
Powerful message mr kapoto
One of eye open master... Mr you know what you're saying, God bless you... MCP ibwelere ku opposition kumene Kujadi ndi mbali yawo
what u r saying Mr kapito it's real true we are suffering in many occasions so we need a patriotic leader
Great and true saying Mr kapito
You are a true man of God, Mr Kapito. May the Good Lord, Jesus Christ, bless you and your family
Mr Kapito tikupempheni mubwere ku UTM muzatiyimilire u president ine ndimafuna munthu wosatila zama Reform ngati inu bwana
Mr kapito we thank God in everythings ❤
Thanks Mr kapito telling trueth
Mfiti yayikazi ikulamulira dziko la Malawi ndiye walodza aliyense kudwala manthong'o😢 mu ndale za nyasalande.
@TichezeChitukula-zn5xh
8 ай бұрын
😂😂😂. Mfiti yayikazi ndiyowoopsaa kwambiri
That's talking mr kapito, tell them n open the eyes for Malawians ❤
You deserve my credit.
Awa ndiakatudu 🎉🎉🎉🎉
Thank you very much bro chakwera alibe zeru ndi BULUTU wachabechabe ndi Chilima wakeyo
You have a big word Mr Man....I really wish we have dozen like you.... Malawi can change so far
True what you're saying Mr kapito
Keep it up to mr kapito ❤
iam agree with you big kapito you are talking truely but dpp was tried than this
Proud of you Mr kapito
Well said kapito 🔥🔥🔥🔥
Kapito thank you for opening our minds
kapito ndimunthu oziwa zasogolo komaso ndimuthu waluntha kwambili
@ArnoldBinali
19 күн бұрын
Ndipo kwambili
Mr kapito mwakambatu za nzeru kwambiri
Dont provoke DPP, we hate them earlier, and chose to change, DPP remain silents for us to taste and enjoy our choice.
True son of malawi kapito
Mr kapito inuyo ndi a bodza nthawi ya dpp mumapanga ma demo Koma pano zinthu zikulakwikwa mwangokhala chete chifukwa Mukudya nawo ndalama, chotsani kaye chisoso chili diso lanu musanayambwe mwawona chili mwa zanu
Nthawi imeneyi dpp imalamula otsutsa amatsutsa zimene iwowo akhoza kukonza zinthu koma zinthu sizinasithe ndiye lero kuti dpp azitsutsa a mcp akhoza kumati munali m'boma momwemu mumatani ndiye izi ndi zandale zozuta kumalawi bas
I saw the whole interview, Walakhula zilungamo zenizeni
Nyau yalira mokweza pk kutukwana😅😅
Chikhulupililo chatha Brian pa boma la Chakwera, eish! Kaya tilowere kuti a Malawi. 😢
Mmakwana inuo mulibho
Akapito mukuyakulazoozake muntuamenesamafunakulagizidwaamaonogeka achakwela akupezamavutochifukwachosavela mulungu awatadize kwabili
Malawi watelekedwa pamoto pano ,kwende nayo tilikumastand kuno tione zomwe Mulungu atichitile amphawife
Dpp ikudwala adverse reaction yotchedwa covid 2024🎉❤🎉😮
Kodi Mr kapito mukulakhula bwino kwambiri ngat big man bingu anakusilani zeru asanamwalire or bwanji
Our president chakwera , He was thinking to rules world is easy 😂😂😂
See the real malawian citizen 💯
CS wachisawawa ngati ameneyu
You Said Chakwera doesn't have experience simply mean he cannot run the government,,,
Maso phenya yanga ine mr simbi phiri koma apo biii malawi never come alright never
@SheenahMwalabu-iz3pr
8 ай бұрын
Ndipo zoona zake ❤
Komadi a kapito ndiinu ofonikira mutakhala president wa dziko
😂😂😂it's sizibwera pa manja koma wakaaaaa😂😂😂zalowa ku account
Komandekulakhula mosaopa eeeehe
Malawi lawi la moto
Eeeh ok hp u r saying the fact , kma ndie zosaenda , apa nkhani yakula anthu azindilambila pa chifukwa choti ine ndi wankulu than enawa zavuta. Vuto ndi lomweri nsogoleri wadyela osakonda ziko lake
Zaziiiiii Mesa malawi ankauzidwa kuti MCP dizinthu Koma okha Amafuna dala nde mukufuna DPP izitani? Asiyeni a DPP azipuma... Mesa mumati asogoleri aDPP samatha kulankhula nde mukufuna chani?,,, mpando wa u president anausiya mopanda kukangana ndi munthu kuutengaso azatenga mosakangana ndi munthu.... Zomwe mukukamba zikunveka zanzeru Koma musalimbane ndi DPP, am not a politician but,, vuto si DPP or MCP Koma tokha amalawi timafuna kusintha now kusintha takuona.. Then next choice we shall make it with real sense.
Akapito ali ndi nzeru 😮munthu wanzeru amaoneka polankhula
Mr kapito zikomo tikuziwa zambiri koma amalawi tikuvutika 😱
😂😂😂 Koma mkulu uyu sapsatira
Koma mwamumva wanena tu kuti a DPP ndi anthu ozikonda a kunama? 😂😂😂😂😂😂😂
Where were you⁉️ here to go
@richardbanda9997
21 күн бұрын
A Kapito izi mukanakhala Kuti munayamba chonchi poyamba atakupatsani udindo Ku Cama, bwenzi nditakupangani salute Koma Ai udindo wanu ,mumangodya osaganizira the poor Malawian as poor consumers. SHAME, mukufuna udindo winanso? People have been criticizing you for not assisting them as per your responsibility to Malawians.
Iwe ndi fisi bakha mbalame Kodi si inu nomwe dpp ikakonza zinthu mumawononga inu nomwe munati achoke osatenga iwe bwanji bomalo ukhale wanzeru kuliratu uku ukumufuma peter kuti abwelere unali kuti anthu amaphwanya sukulu misewu yomangamanga takhalapo bwino nthawi ya Bingu tikukumbukila sizoyenela iwe kutiuza unali kuti iweyo
Chiyembekezo pa chakwela tinasosa
vuto ndi nankhumwa he is sleeping sakulankhula kanthu😴
And it's very true why Dpp annoying,ana
@rodrickphiri
8 ай бұрын
DPP will never bounce back is dead and the country is moving without opposition this is pathetic
Panopa ndawamvesa a DPP chimene amakhalira chete President uyu ndi wamagazi ifeyo tikuziwonela kunja koma anzathuwa akuziwonela pafupi President uyu si munthu wabwino a DPP akhalebe chete mpaka campaign iyambe
ngwabodzadi president yu
chakwera sinikumuonera kukondwa ta mins watipha
Voti yaimwe yilipo
Chakwela ndi galu kwabansi tsiku transport moyenda
Dpp ikamatsutsa zinthu zopusa tikumati kusagwilizana kwakuchipani kwanuko musabweletse kuno
President wathu akulamulila dziko lonse lapansi osati Malawi yokha 😂😂😂 ndipo ndege ndiye siyikwatopetsa 😂 tsiku ndi tsiku asilikali akuvina pelete ku airport😂😂😂😂
@paulpaseli6310
8 ай бұрын
😂😂😂
@SheenahMwalabu-iz3pr
8 ай бұрын
😂😂😂😅😅😅
Koma kapito ndi akatundu
So that the best solution he must step down........pa 11 ma demo alipo omuuza kt atule pansi udindo
No direction. No hope
Machende ako kapito , panga chipan chako mbuzi ya munthu
@omarajibu860
8 ай бұрын
Ukumtukwana Kapito chifukwa chani? Are you a beneficiary of this rubbish happening now?
@omarajibu860
8 ай бұрын
Ngati dziko lisakuyenda bwino it's because of people like you, arrogant.
@henryhenry6632
8 ай бұрын
@@omarajibu860 achawa machende anu
@amisichiphiri8227
8 ай бұрын
Munthu opanda mzeru ongutukwana anthu osalakwa
@MuhammadTennes-tx5ti
8 ай бұрын
Anthu osafuna kudzudzulidwa aja ndi amenewa ,nkhani kutukwana basi,why kumtukwana Kapito? Mfundoyo yamubaya kkkk