Man banja losagwirizira ili nawenso ndiwachibwezi basi zatherana Malo ndi awana
@chippiephiri4505 Жыл бұрын
Mamunayi ndiwopoyila
@grantmachira9668 Жыл бұрын
Mayiyo ndiwosalakwa amadzilimbikira ekha abambowa angothetsa banja basi but it seems mkaziyo ndi bread winner mkazi malo anagula yekha
@Xtar_deadlol126 күн бұрын
Za ziii kusowa zotola nkhani Chan
@lamackbanda6869 Жыл бұрын
Olakwitsa ndi mamunayi zinthu zonsezo zimachitikazo opanda action kuonesa. Nkhani yamalilo inaliso yayikulu olo sanayithambasule. Komaso zimayiyu sanatenge ndalama ku bank koma zimuna akewo ndi amene amamanga nyumbayo. Naye mamunayo ofafusa kuti ndalama akuzithenga kuti zomangila nyumba kumangoyang'ana zimamutsangalasa
@zakeyophiri4308 Жыл бұрын
Pls inuyo nkhani zina muziysa Kubisa nkhope kapena azalankhula atayang.ana kumbali chitsazo nkhani ya mnyamata akuti anapeleka mimba kwa mtsikana kapena mtsikana uja amene chifukwa media imapita patali tidzalephela kumufusila kapena kukwatiwa adzati ena anampatsa kale mimba
@chicco2294 Жыл бұрын
Mainawa akuti bwanji?? I didnt know ku mosco mumalankhula Chichewa choncho
@user-ez7th2rv7g6 ай бұрын
Thanks for the update
@westonnsulupi4056 Жыл бұрын
From Malawi
@ernestbwanalisauteni3483 Жыл бұрын
Kkkkkkkkkk zosokonezeka kkkk
@victorsmbewe4816 Жыл бұрын
Emotional damage 🤕🥴😜
@DelcidioDiogoPedro-ir9ni Жыл бұрын
Nkazio ntanbuali
@chembachilemba7623 Жыл бұрын
Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi
@ndazionaanastasiaannaphiri4843 Жыл бұрын
Palibe chabwino zonse zolakwika mkazi yo nde worsen
@josuahkachali1489 Жыл бұрын
From Malawi but am stay in Kuwait
@jamesselemani1003
Жыл бұрын
Oky
@joebrown1158 Жыл бұрын
In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
of cause
@chifundoalfred14
Жыл бұрын
Mozambique
@peterbanda7003 Жыл бұрын
Osamusiya bwanji
@lamackbanda6869 Жыл бұрын
Ntchito yapamwamba guys mumayitha♨♨♨♨
@ngendahayososthene1398 Жыл бұрын
bambo inu ndi inu opoyira zedi.
@floramtiwa211 Жыл бұрын
Koma ma statement akusiyana mwamunayu akuyankhula mosiyana ndiazimayi aja
@smithelectro-plumb2994 Жыл бұрын
Kodi akulankhula chilankhulo chanji guys
@chancyutekakayala2445 Жыл бұрын
May someone assist me Kodi zikuchitika ku dziko lanji izii komanso nchiyankhulo chanji
@Envanceabwinobamusieli-sf9tt
11 ай бұрын
It's chichewa in Mozambique 🙄
@zaithwachiwaya8885 Жыл бұрын
Kom nkhaniyo mamunai zikuoneka kut malo sanagule nao.Komaso zimaiyo ndi uhule lothelatu zochitisa manyanzi zed
@zaithwachiwaya8885
Жыл бұрын
Kom saname nkhaniyi kadakonda mukanamuonesa mzimai wa chigololo yo timuone kkkkkkk
@simangodickson1794
Жыл бұрын
Mahule , Mabanja oyambila mvitsamba
@promise3693 Жыл бұрын
Kulakwa🤔
@bosconthandala9905
Жыл бұрын
👀 from malawi
@zecamariosandifolo8535
Жыл бұрын
Malowo ngakhale atakhala kuti nyumbayo anagula ndi iwowo komabe ali pa banja nyumbayo ndiyawose basi
@paulmgombebanda-mr19sate Жыл бұрын
Zovuta izi
@luciajames604 Жыл бұрын
It's Mozambique
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
Yes
@tadalaimwa394 Жыл бұрын
Ndemwati ndinu amalawi? I really wish to visit and learn more about this place
So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?
@joegibsonzulu2599
Жыл бұрын
It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.
Пікірлер: 64
Koma atolakhan ku Mozambique mukugwira ntchito yotamandika mpaka kutiwonesa stadium 😂😂😂😂
Two bad, watching from malawi
Vuto ndi mamunayo........ Anyway watching from Maputo (koma ndine mmalawi ndithu)
@helderdias5523
Жыл бұрын
Me too
Akacheza amamwa eti kkkkk
Language is clear komano zudabwisa mainawo koma mwat ndiku malawi uku?
@kairaruphan2639
Жыл бұрын
Akuti Mozambique osati malawiyi
Mayi uyo ndiwolakwa bola akanathesa banja za uhule wake akanapangila pa nkhomo pa makolo ake fro malawi
Komatu. Kulakwa chommenyera mwamuna wako nchiyani nzimayi oipa ukupha mwana waeni 😭😭😭
Nkaziyo ndihule aphesa amuna
Man banja losagwirizira ili nawenso ndiwachibwezi basi zatherana Malo ndi awana
Mamunayi ndiwopoyila
Mayiyo ndiwosalakwa amadzilimbikira ekha abambowa angothetsa banja basi but it seems mkaziyo ndi bread winner mkazi malo anagula yekha
Za ziii kusowa zotola nkhani Chan
Olakwitsa ndi mamunayi zinthu zonsezo zimachitikazo opanda action kuonesa. Nkhani yamalilo inaliso yayikulu olo sanayithambasule. Komaso zimayiyu sanatenge ndalama ku bank koma zimuna akewo ndi amene amamanga nyumbayo. Naye mamunayo ofafusa kuti ndalama akuzithenga kuti zomangila nyumba kumangoyang'ana zimamutsangalasa
Pls inuyo nkhani zina muziysa Kubisa nkhope kapena azalankhula atayang.ana kumbali chitsazo nkhani ya mnyamata akuti anapeleka mimba kwa mtsikana kapena mtsikana uja amene chifukwa media imapita patali tidzalephela kumufusila kapena kukwatiwa adzati ena anampatsa kale mimba
Mainawa akuti bwanji?? I didnt know ku mosco mumalankhula Chichewa choncho
Thanks for the update
From Malawi
Kkkkkkkkkk zosokonezeka kkkk
Emotional damage 🤕🥴😜
Nkazio ntanbuali
Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi
Palibe chabwino zonse zolakwika mkazi yo nde worsen
From Malawi but am stay in Kuwait
@jamesselemani1003
Жыл бұрын
Oky
In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
of cause
@chifundoalfred14
Жыл бұрын
Mozambique
Osamusiya bwanji
Ntchito yapamwamba guys mumayitha♨♨♨♨
bambo inu ndi inu opoyira zedi.
Koma ma statement akusiyana mwamunayu akuyankhula mosiyana ndiazimayi aja
Kodi akulankhula chilankhulo chanji guys
May someone assist me Kodi zikuchitika ku dziko lanji izii komanso nchiyankhulo chanji
@Envanceabwinobamusieli-sf9tt
11 ай бұрын
It's chichewa in Mozambique 🙄
Kom nkhaniyo mamunai zikuoneka kut malo sanagule nao.Komaso zimaiyo ndi uhule lothelatu zochitisa manyanzi zed
@zaithwachiwaya8885
Жыл бұрын
Kom saname nkhaniyi kadakonda mukanamuonesa mzimai wa chigololo yo timuone kkkkkkk
@simangodickson1794
Жыл бұрын
Mahule , Mabanja oyambila mvitsamba
Kulakwa🤔
@bosconthandala9905
Жыл бұрын
👀 from malawi
@zecamariosandifolo8535
Жыл бұрын
Malowo ngakhale atakhala kuti nyumbayo anagula ndi iwowo komabe ali pa banja nyumbayo ndiyawose basi
Zovuta izi
It's Mozambique
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
Yes
Ndemwati ndinu amalawi? I really wish to visit and learn more about this place
@zexndaomba3011
3 ай бұрын
Samalawi this is angonia
Zosankhala bwino ayi
@nemamoleni3041
Жыл бұрын
Ati agulitse malo ndalama agawane?? Zosakhala bho
Where exactly is this sad news happened
@mtimbasonjojailos5106
Жыл бұрын
Mozambique iyi
Koma ndi ku Malawi kapena Mozambique?
@kalimawandale7161
Жыл бұрын
Mozambique
Mabanja akenso ndendi achi'chainatu
@eliasfaunteni6849
Жыл бұрын
Mchifukwa chake timanena kuti akaziwa tikawamphunzitsa amachuluca mzelu zovetsa chisoni kwambiri
So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?
@joegibsonzulu2599
Жыл бұрын
It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.
Kodi mayina akuchulidawa ndi ku malawi ?
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
ayi, koma kalipentalayo
@chifundoalfred14
Жыл бұрын
Mozambique
@chifundoalfred14
Жыл бұрын
Mozambique
Penço nr d BS de Whatsapp
@balancosemanalckgovate8464
6 ай бұрын
865112269