Ndiye Tsangano Imeneyo, Zikomo kwambili tikudziwa zithu zakumudzi mwasanga kudzela kwa inu Balanço Semanal. From Maputo
Zikomo tikuziwa nawo mmene moyo wa abale athu okuyendera madera ena pa dziko pano one love from malawi
Keep up the good work proud of you guys,mmatidziwitsa zambiri watching you here from South Africa Durban.
Koma dela ili mumachitika ma story ambiri. Koma good job guys. Love here in MALAWI
thanks
Zokumva zimapweteketsa mutu , program iyi ili boh, tikumanva ndikuona mmene zikukhalira , here Durban love you guys pitilizani
Koma mayi amenewo saanabe malo ena ake ?komanso kumeneko kwa angonia nkutheka kuti aanthu aufiti akupanga izi pofuna kutchuka komaso kuyesa matsenga kuti aone kuti zikutheka.Nkhani Ina aanthu akumeneko bwanji sakutchuka ndi ulaliki? nkuti aanthu akumeneko sakonda kupemphera chifukwa izi zikuchulukira kwambiri.May almighty God show powerful below this
This Chanel is working .thanks
A sing’anga Amati amachokera ku Mozambique aja mwati samachokera ku dera limeneli?
Zochitika mmasiku otsiriza, love this channel
Keep it up good work I like this channel
Keep it up guys.... watching from Durban
Very very sad news Mmmm dzikoli ndithu langotsala pakaphindi chabe mwini wake akubwela atenge ake oyera m'tima
Keep up the good work guys informing us what's going on there
iiii mulungu amusungolele nsikanai 🙏Kuno ku guruwe Zambézia ine dakumudwa Izi zamasiku osiliza 🙏chomfunika tilimbike kumpepera usiku ndiusana🙏
Ineso poganiza pa ine ndikuona ngati ndi mkazi nzakeyo olo amacheza ndi pamaso zamumtima ndi za wenkha eyetu
Zovetsa chisoni . Koma akuyenera apite ku chipatala kuti akawapange check . I love your Chanel. From 🇲🇼
OMG 😳 what plz anthun mudziweni yesu komazoona nkumuika nzanu chinthu Ngati in cho mmimba .Koma Choti mudziwe mfiti yozafaso
Mmm mulungu sizoti wangokhala chete ayi
Life yaku Mudzi ndiyovuta eeesh
Kwa Angonia ni koipa , kuli nfiti olo atafuna ukussandutsa Ka mbalame ni mpompo , hmmmmm
Eeee😱 koma dziko abale anthu saopa kumwamba hmm ayi Ambuye aweruzepo ndithu.
Eshiiiii but govati u're trying the best really appreciate u
Ine Friday kuno ku South Africa a Malawi chepesan uthakati schupit
zomvetsa chisoni mutengeleni ku chpatala please..komanso upeze wako mamuna mitala ndi umfiti...
Mmmmhhh pitani naye kuchipatala please before is too late Mmhhh koma zoopsya
malodza nkhani yovetsa chison ambuye alowerelepo kuti zoyipazi zisamachitike
Muzimayiyo wataya mwana kapena analibe mimba amanama
Is this moshiko?, mumakwana guys
Kulakwirana uku 😭😭 munthu kutenga mimba nukachira mtengo Mmmh shame
Very sad
Pepani mai wanga mulungu akudziwa zonse imani Pamanso ake komanso ndimayamika kwa inu amene mumatipatsira nkhani zonse ambuye azikudalitsani nthawi zonse
zikomo
Koma kuli anthu omudziwa mulungu ukuuuu kumango chitika zinthu zopanda umunthu ukuuuuu
Dziko lafikapo ambuye bweraniiii
Keep it up
& tikuthokoza channel iy ikumatiziwisa zambri
pepani
Koma ndiye
Munthuyu anachira bwinobwino koma mwanayo amafunika kukangaroo coz of kuchepa weight koma poti mkumudzi asowetsa mwanayo nkulenga nkhani yoti wachira mtengo nde poti mumakhulupirira changu mwavomereza mukafufuza mkhaniyo muzingonva kuti aliyense ananva
Ayi ndithu zoopsya kwambiri.Malodza saposa apa.
Mmm kom zoopsa apite kuchipatala kma mmm
Sim boca ,essas mulheres
Mmm this is very sad eish
Nkuthekaso kuti mwina zikuchokera pakhomo pompo komaso mwina ndinkazi nzakeyo amangomukonda pamaso koma muntima sasangala naye awo anali maganizo anga chabe
zoona
Mmm koma abale kkkkkkk koma zoopsya
Very sad.matsiku osiliza
Zosakhala bwino
Zosakhala bo
Kulakwatu uku
Maloza awa eish
Apite kuchipatala akamuone mmimbamo
😂😂😂
Zoona zake ufiti ulipo
Mmmm soo sad.
mmm zovuta zoopsya
Eeeeeeeeish koma anthu mmmm
Nde mwati mtsikana osati mzimayi
Dzaka 17
Eish 🤔
Komatu anthu amuziwe yesu Mmmm ayenjeza
Kusatira mwachete chete
Mmmm zoopsa ndithu koma apite kuchipatala akamuone mzimayi ameneyi
Uuuuuuhhhh very sad may God bless her life in the name of Jesus Christ.
zilibwino malume
Ufiti
No good
Thawizina mitalayiso siyabhoo.
zoona zeni zeni
Koma !!!
zochttsa matha
Angónia assusta hiii
Mm zosakhala bwino mmmm
Mmmmmm km ufiti uliko mmmmm
yaaa
Пікірлер: 80
Ndiye Tsangano Imeneyo, Zikomo kwambili tikudziwa zithu zakumudzi mwasanga kudzela kwa inu Balanço Semanal. From Maputo
Zikomo tikuziwa nawo mmene moyo wa abale athu okuyendera madera ena pa dziko pano one love from malawi
Keep up the good work proud of you guys,mmatidziwitsa zambiri watching you here from South Africa Durban.
Koma dela ili mumachitika ma story ambiri. Koma good job guys. Love here in MALAWI
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
thanks
Zokumva zimapweteketsa mutu , program iyi ili boh, tikumanva ndikuona mmene zikukhalira , here Durban love you guys pitilizani
Koma mayi amenewo saanabe malo ena ake ?komanso kumeneko kwa angonia nkutheka kuti aanthu aufiti akupanga izi pofuna kutchuka komaso kuyesa matsenga kuti aone kuti zikutheka.Nkhani Ina aanthu akumeneko bwanji sakutchuka ndi ulaliki? nkuti aanthu akumeneko sakonda kupemphera chifukwa izi zikuchulukira kwambiri.May almighty God show powerful below this
This Chanel is working .thanks
A sing’anga Amati amachokera ku Mozambique aja mwati samachokera ku dera limeneli?
Zochitika mmasiku otsiriza, love this channel
Keep it up good work I like this channel
Keep it up guys.... watching from Durban
Very very sad news Mmmm dzikoli ndithu langotsala pakaphindi chabe mwini wake akubwela atenge ake oyera m'tima
Keep up the good work guys informing us what's going on there
iiii mulungu amusungolele nsikanai 🙏Kuno ku guruwe Zambézia ine dakumudwa Izi zamasiku osiliza 🙏chomfunika tilimbike kumpepera usiku ndiusana🙏
Ineso poganiza pa ine ndikuona ngati ndi mkazi nzakeyo olo amacheza ndi pamaso zamumtima ndi za wenkha eyetu
Zovetsa chisoni . Koma akuyenera apite ku chipatala kuti akawapange check . I love your Chanel. From 🇲🇼
OMG 😳 what plz anthun mudziweni yesu komazoona nkumuika nzanu chinthu Ngati in cho mmimba .Koma Choti mudziwe mfiti yozafaso
Mmm mulungu sizoti wangokhala chete ayi
Life yaku Mudzi ndiyovuta eeesh
Kwa Angonia ni koipa , kuli nfiti olo atafuna ukussandutsa Ka mbalame ni mpompo , hmmmmm
Eeee😱 koma dziko abale anthu saopa kumwamba hmm ayi Ambuye aweruzepo ndithu.
Eshiiiii but govati u're trying the best really appreciate u
Ine Friday kuno ku South Africa a Malawi chepesan uthakati schupit
zomvetsa chisoni mutengeleni ku chpatala please..komanso upeze wako mamuna mitala ndi umfiti...
Mmmmhhh pitani naye kuchipatala please before is too late Mmhhh koma zoopsya
malodza nkhani yovetsa chison ambuye alowerelepo kuti zoyipazi zisamachitike
Muzimayiyo wataya mwana kapena analibe mimba amanama
Is this moshiko?, mumakwana guys
Kulakwirana uku 😭😭 munthu kutenga mimba nukachira mtengo Mmmh shame
Very sad
Pepani mai wanga mulungu akudziwa zonse imani Pamanso ake komanso ndimayamika kwa inu amene mumatipatsira nkhani zonse ambuye azikudalitsani nthawi zonse
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
zikomo
Koma kuli anthu omudziwa mulungu ukuuuu kumango chitika zinthu zopanda umunthu ukuuuuu
Dziko lafikapo ambuye bweraniiii
Keep it up
& tikuthokoza channel iy ikumatiziwisa zambri
pepani
Koma ndiye
Munthuyu anachira bwinobwino koma mwanayo amafunika kukangaroo coz of kuchepa weight koma poti mkumudzi asowetsa mwanayo nkulenga nkhani yoti wachira mtengo nde poti mumakhulupirira changu mwavomereza mukafufuza mkhaniyo muzingonva kuti aliyense ananva
Ayi ndithu zoopsya kwambiri.Malodza saposa apa.
Mmm kom zoopsa apite kuchipatala kma mmm
Sim boca ,essas mulheres
Mmm this is very sad eish
Nkuthekaso kuti mwina zikuchokera pakhomo pompo komaso mwina ndinkazi nzakeyo amangomukonda pamaso koma muntima sasangala naye awo anali maganizo anga chabe
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
zoona
Mmm koma abale kkkkkkk koma zoopsya
Very sad.matsiku osiliza
Zosakhala bwino
@shammimmhangoh
Жыл бұрын
Zosakhala bo
Kulakwatu uku
Maloza awa eish
Apite kuchipatala akamuone mmimbamo
😂😂😂
Zoona zake ufiti ulipo
Mmmm soo sad.
mmm zovuta zoopsya
Eeeeeeeeish koma anthu mmmm
Nde mwati mtsikana osati mzimayi
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
Dzaka 17
Eish 🤔
Komatu anthu amuziwe yesu Mmmm ayenjeza
Kusatira mwachete chete
Mmmm zoopsa ndithu koma apite kuchipatala akamuone mzimayi ameneyi
Uuuuuuhhhh very sad may God bless her life in the name of Jesus Christ.
zilibwino malume
Ufiti
No good
Thawizina mitalayiso siyabhoo.
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
zoona zeni zeni
Koma !!!
zochttsa matha
Angónia assusta hiii
@shammimmhangoh
Жыл бұрын
Mm zosakhala bwino mmmm
Mmmmmm km ufiti uliko mmmmm
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
yaaa
A sing’anga Amati amachokera ku Mozambique aja mwati samachokera ku dera limeneli?
Zosakhala bwino
Very sad