KULONDOLOZA ZA IMFA YA AGNESS KATENGEZA...@MibawaStudios

Пікірлер: 49

  • @ChristianChimwaye-yg9ti
    @ChristianChimwaye-yg9ti6 ай бұрын

    Koma MALAWI 🇲🇼 POLICE MWAYIGWIRA NTCHITO. ❤❤❤❤❤❤

  • @ChisomoMsiska-oi2vg
    @ChisomoMsiska-oi2vg6 ай бұрын

    Uyu nayeso aphedwe chimunthu chopanda nzeru zoona kupha mubale wako yemwe amakudyesa😢

  • @user-hs5xv6bk2f
    @user-hs5xv6bk2f6 ай бұрын

    Mapazianu apolisi mukulephela kumanga anthu amene akuphesa amalawi ambiri Pano zakubuchala zilipati zakufamase zilipati zawitika zilipati lelo mwabwela poyela chifukwa Choti ndimphawi uyu mukunena Kuti simumauzidwa inu apolisi zonse zakufamase kubuchala Moti simukuziwapo khanthu site ana tsiku likubwela muzanena nokha tisanakufunseni mafunso

  • @raytavares2256
    @raytavares22566 ай бұрын

    Why Are police exposing the details now while the other group is not arrested? You are still investigating the matter and revealing updates just gives a chance to the other criminals Amos committed all the crimes with. You have given the chance for other robbers and nurderes to escape justice.

  • @SinoliaEfelemu
    @SinoliaEfelemu6 ай бұрын

    Good job keep it up

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g6 ай бұрын

    Uyuso aphedwe bas palibe kuchitila mwina ai ⚔️🗡️⚒️🧷🔪🐯🐆🐅🪱🦂

  • @user-is9fk8uz9i
    @user-is9fk8uz9i6 ай бұрын

    Good job

  • @MercyMwale-wc4lr
    @MercyMwale-wc4lr6 ай бұрын

    Mmmh koma abale...your own blood

  • @user-tz5jo3dd9t
    @user-tz5jo3dd9t3 ай бұрын

    Mmmm koma anaganiza bwanji uyu

  • @raytavares2256
    @raytavares22566 ай бұрын

    This boy Amos Is dangerous, having a sister and living with his sister for free food and secured free

  • @johnman4619
    @johnman46196 ай бұрын

    Apolice athu simumachedwa kumpeza munthu aka thawa .koma mulibe chilungamo mumamtayanso after mutadya mabanzi

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft6 ай бұрын

    Nkuthekanso kuti mwina waulura kale Amosiyo Koma mwina ndiodziwika Akulephera kumubweretsa poyera

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo29726 ай бұрын

    Police you have been fast to talk to the public before arresting the others...you have made them run now.

  • @grayjames904

    @grayjames904

    6 ай бұрын

    Zaboza inu ogwidwa agwidwabe though ayankhulapo and they’re not going in deep details zoyakhula zinalipo lkale how come they catch the dude? Mufuna Muzise ntchito a police 😅😅

  • @matheromichellenkhalamba

    @matheromichellenkhalamba

    6 ай бұрын

    They know their job, if they have managed to find the lead they have already cracked the case.

  • @noshallsnesu9174

    @noshallsnesu9174

    5 ай бұрын

    4:36

  • @user-fg5iw1qy1k
    @user-fg5iw1qy1k6 ай бұрын

    Kuthamangatu kumuonesa koma akapezeka wagulu la apolice azanu mubisa agalu inu mmmm

  • @ibrahimbamusi109
    @ibrahimbamusi1096 ай бұрын

    Allan witika ndiye zili pat

  • @masulasanudi7286
    @masulasanudi72866 ай бұрын

    Kod mulandu wa Witika uli pat? Pot uyo sali m'boma ndy kuthamangatu kumuyalutsa eee koma apolice mmmm chinyengo

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w6 ай бұрын

    Mukamaliza mlandu umenewu mumtengenso Soulosi Chilima wa ku maulanso naye

  • @EdythGloryNamponya
    @EdythGloryNamponya6 ай бұрын

    Kenako tidzamva zoti wafera mu cell

  • @daniellchinjati2557

    @daniellchinjati2557

    6 ай бұрын

    Ampanga xinthu kubisa zinaxi

  • @user-vp5mg5qz9e
    @user-vp5mg5qz9e5 ай бұрын

    Congratulation Lilongwe police

  • @davidzgambo
    @davidzgambo5 ай бұрын

    tikufuna detailed report ya Witika

  • @user-mu2qw6br2f
    @user-mu2qw6br2f6 ай бұрын

    Mtolakhani usamangoti "mlongo wawo" use also brother wa omwalirayo chichewa Cha mlongo wawo sichigwiritsidwa ntchito dziko lonse

  • @azunguauskay4903
    @azunguauskay49036 ай бұрын

    Mnyamata oyipa

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w6 ай бұрын

    Ndipo tikudikila kuti timve watching from Lesotho

  • @user-qh3nb4vx9j
    @user-qh3nb4vx9j6 ай бұрын

    We need cctv

  • @user-in3sh8ru7o
    @user-in3sh8ru7o5 ай бұрын

    Sikusinja uyu amphedwe

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri85176 ай бұрын

    Eeeeeeee 🙆🙆🙆🙆

  • @user-uu3wy8vl1y
    @user-uu3wy8vl1y6 ай бұрын

    Kodi za Njaunju zinathela pati?

  • @Martha1436

    @Martha1436

    6 ай бұрын

    Ndipo Inenso ndikadakonda nditadziwa.

  • @ChristianChimwaye-yg9ti
    @ChristianChimwaye-yg9ti6 ай бұрын

    Palibeso zoti uyuyu ndi mlongo wawo ayi afunika akaphedwe

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri85176 ай бұрын

    Iiiii chimunthu chikulukulucho kumasungidwa mmmmm ndekutidi chinali chigawega kwao anachilemphera mchobvuta iiiiii koma mpaka kupha mlongo wake eeeeee

  • @user-qj7ze8vh4l
    @user-qj7ze8vh4l6 ай бұрын

    Eeeee

  • @user-zy8uy3fw5x
    @user-zy8uy3fw5x6 ай бұрын

    Inu anatumidwa ndi andale ameneyo

  • @austinvincent773
    @austinvincent7736 ай бұрын

    Anamuphelanji

  • @BeautyKunje
    @BeautyKunje6 ай бұрын

    Mu2 oipa kwambri olo umunthu osampeza

  • @user-to4or4jw9g
    @user-to4or4jw9g6 ай бұрын

    Koma ngakhale amupeza Amos'yo amufunse bwino bwino chifukwa nkutheka alipo anamutuma

  • @daniellchinjati2557

    @daniellchinjati2557

    6 ай бұрын

    Andale anazela mwa iye

  • @tshepangmatebele7822

    @tshepangmatebele7822

    6 ай бұрын

    Ndipo mukunena zoona

  • @raziejaymw4205
    @raziejaymw42056 ай бұрын

    sad news😡

  • @user-rv2sr2gr5f
    @user-rv2sr2gr5f6 ай бұрын

    Km galu iwe kupha mulongo wako food for free

  • @user-ic1xl1tu3m
    @user-ic1xl1tu3m6 ай бұрын

    Khondo ndanasi amakupha ndi wako

  • @EstherZintambira-sq3yy

    @EstherZintambira-sq3yy

    6 ай бұрын

    Ndipo iih chibale chinaopsya

  • @ChrissyKazinga-jd8dx

    @ChrissyKazinga-jd8dx

    6 ай бұрын

    Km zoti ndichibale ai ndithu muthu oipa uyu

  • @user-zr9uw5hd5f
    @user-zr9uw5hd5f6 ай бұрын

    Good job