Limpopo FM yomweyo galu iwe Ntanyiwa kufotokoza za anthu 7 omwe anakamaliza a Chilima ndi anzawo

Пікірлер: 134

  • @giftwankhama9914
    @giftwankhama991410 күн бұрын

    Stay safe comrade. May the God in heaven keep u safe my brother.u the only source of true information to us.

  • @peterlowole7841
    @peterlowole784110 күн бұрын

    We are great to have you comrades

  • @jacquelinecunningham363
    @jacquelinecunningham36310 күн бұрын

    Limpopo 🎉🎉❤❤🔥🔥🔥🔥🔥💯

  • @eliasnyilongo4865
    @eliasnyilongo48659 күн бұрын

    My redio in malawi

  • @user-ph3zy9ox7d
    @user-ph3zy9ox7d9 күн бұрын

    From South Africa all i have is a protecton prayer for you my brother ,, may God protect you from these anacondas for not swallowing you Amen

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Tikuziwa zisisi zambiritu mmm

  • @user-kr4wb2th9i
    @user-kr4wb2th9i10 күн бұрын

    ❤❤❤❤more fire 🔥🔥🔥 ndipo titemana serious muno oky mungoti pheee anthu amenewa asazayerekeze kubwera kumangochi serious azaona ngati akufuna kuti azalembe book la history lomkuzana anthu akumangochi 2024 yelekezani kubwera kuno , zimunezo kulilongwe komweko kwa anthu aganiza mwauchitsiluwo try to come here in Mangochi try

  • @Hudhayf

    @Hudhayf

    10 күн бұрын

    😂😂😂😂 Mangochi m'bomamo

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r10 күн бұрын

    Kunena zowona paziko rapansi pano paribe chinsinsi sure nyimbo ikhare ya grace chinga ndizaurura tchimo rimazunza orichita sure 🥱🙆

  • @augustMag
    @augustMag10 күн бұрын

    Tili pano kudikira Chilungamo chioneke ndi Limpopo FM radio 🔥♥️

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em10 күн бұрын

    Viva Limpopo FM

  • @WilliamKapungu
    @WilliamKapungu10 күн бұрын

    ❤❤❤❤ More fire comrade ntanyiwa

  • @MustapherDavie-su3nk
    @MustapherDavie-su3nk10 күн бұрын

    Tili pa mbuyo panu

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9n10 күн бұрын

    watching from cape town limpopo no: 1

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka10 күн бұрын

    Mulungu salakwitsa kalikose adziwa yekha chochita nximu wanu uuse mumtendere bwana chilima

  • @PetroMatias
    @PetroMatias10 күн бұрын

    Chakwerao osangomuombera bwanji watikwana kwambiliaaa

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Ndipo inu mmm

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili13627 күн бұрын

    Thanks alot comrade, May God protect u so that a Malawi tipitilize kuziwa zoona zenizeni

  • @JamesKakhome
    @JamesKakhome10 күн бұрын

    Comrade mtanyiwa! Chamzelutu apa kunali kungotulusa zinthuso coz mukat mwatulusa olo report mudikilalo sangatuluseso n mukhoza kumacedwa conco then kaya nditsokaso akusowetsan sibas zizakhala kut mwatidikilisa pachabe umbon muli nawowoso mwapita nawo! Tulusan chabe zomwe muli nazozo mukucedwa mukucedwa

  • @user-pj9rs6vj8x

    @user-pj9rs6vj8x

    10 күн бұрын

    Umboni alibe awa chomwe akukanikira kutulutsa ndi chani?monse muja

  • @user-mq7ou5xp5m

    @user-mq7ou5xp5m

    8 күн бұрын

    Chabodza ichi

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti10 күн бұрын

    Following.... Limpopo 🔥 🔥 🔥

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika678410 күн бұрын

    Mbuzi zawanrhu zukanika kulamulira dzko

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo10 күн бұрын

    Umunthu alibe mphamvu ya satana basi,ngati opemphera koma Satana weniweni ineso ndi mchewa koma awaso aonjeza

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w10 күн бұрын

    More fire

  • @yassinn5634
    @yassinn563410 күн бұрын

    Magalimoto adutsa ku Lunzu?

  • @ShyreenMbwana
    @ShyreenMbwana10 күн бұрын

    Chidanti Malunga wako uja amusankhadi kukhala VP monga umanenera dzulo lija

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Anaisintha game

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce210 күн бұрын

    Limpopo ❤🔥🔥🔥

  • @LuciousKotamu-dh5uq
    @LuciousKotamu-dh5uq6 күн бұрын

    Keep on inform us good work

  • @user-pf5hu2pd2b
    @user-pf5hu2pd2b10 күн бұрын

    This is true station

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias99729 күн бұрын

    Magalimoto amene mukunenawo mungovutika amene aja ndi alendo ongudusa amachoka ku nacala port adusa ku Moçambique mpaka zimbabwe

  • @user-qv4ko6ps4j
    @user-qv4ko6ps4j9 күн бұрын

    Watching from limpopo province in lephalale town

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r10 күн бұрын

    Emusipi Chipani Cha Nkhanza komanso chakupha

  • @ChawingaMwaseteza
    @ChawingaMwaseteza10 күн бұрын

    Wina aziphe kumene agalu amenewa sangatiphele adzibale athu motelo

  • @ModesterMkawa
    @ModesterMkawa8 күн бұрын

    More fire comrade kusatira ndi chidwi

  • @BarnettWitness
    @BarnettWitness10 күн бұрын

    Ipanse Moto tiziwe zoona zen zen

  • @YatoRoy-kt4lh
    @YatoRoy-kt4lh10 күн бұрын

    2025 they will be no votes. Dziko lonse lapansi kukhala Climate Lockdown(NWO) mufufuze zimenezi

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Kkk

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d8 күн бұрын

    Viva Limpopo FM ❤❤🔥🔥🔥🔥🔥

  • @TryceMagombo-sh7kb
    @TryceMagombo-sh7kb2 күн бұрын

    Big up big more and more imfo

  • @emmanuelalbertbotolo
    @emmanuelalbertbotolo9 күн бұрын

    More fire Mr muthanyiwa

  • @user-mh5xw5xu9w
    @user-mh5xw5xu9w7 күн бұрын

    Number one Limpopo FM more 🔥

  • @AliceGeorge-il6ig
    @AliceGeorge-il6ig9 күн бұрын

    Bravo bravo achimwene,be safe plz

  • @samchibenene4458
    @samchibenene44589 күн бұрын

    Mo fire Limpopo FM

  • @user-wg8tp8in1v
    @user-wg8tp8in1v10 күн бұрын

    Koma mathelo a nkhani izi ndi Otani?

  • @WilliamKapungu
    @WilliamKapungu10 күн бұрын

    Amfumu akabudula 😂😂😂😂 muziti Chan? 😂😂😂😂

  • @RichardMphopheya
    @RichardMphopheya9 күн бұрын

    more fire limpopo

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9n10 күн бұрын

    kkkkkkk ooooh ndodo itulukedi basi

  • @KeltonKapanda
    @KeltonKapanda2 күн бұрын

    May God keep you safe comred

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz10 күн бұрын

    mumakwanira a mtanyiwa

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda9 күн бұрын

    Munthu akuyankhula za achewayu wangoonetseratu umbuli waku wonse kuti za democracy sazidziwa. Democracy imabwera ndi ma condition ake. Boma lingapereke ku ma company angati ndi ufulu wa pa malonda omwe ulipowu? Muli ma company angati m'Malawi muno kuti boma lingakwanitse kuperekako ndalama? Taganizirani za fetereza wotsika mtengo momwe zikuyendera, akupindula ndi amphawi kapena anthu andalama? Zomwe zikuchitika ndi fetereza ndi zomwe zikhoza kuchitikanso ndi sopo kaya ndi sugar kaya ndi mafuta ophikira. Omwe ali ndi ndalama zambiri akhoza kumakangozikokololako zonse nkumagulitsa ku amphawiwo modulabe.

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda9 күн бұрын

    Katundu akudula chifukwa cha kugwa kwa Kwacha yathu. Kwacha yathu ikugwa pafupipafupi chifukwa chosowa forex, forex ikusowa chifukwa chochepa kwa export; amalawi tachulutsa ma import osati export. Amalawi tiyeni tilimbikire kugwira ntchito zomwe zitha kutibweretsera katundu yemwe titha kutumiza mayiko akunja kuti forex ilowemo yambiri muno.

  • @babranzima8120
    @babranzima812010 күн бұрын

    Ndizisiru chakwera watha basi South Africa

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe395810 күн бұрын

    We are very angry we want to given us good information,we are not joking, Chakwera,Chakwera, Becareful., you will flee and Leave Malawi One Day,zida wagula zija ndi zathu tizazi tenga zonse tiku ziwa Chakwera Ufa ngati Nazombe Malawi uyu ndiwa sopano Siwa Kale munapha uja Chirima ndiye Anali bwana wanu,siku limodzi ma ofesi a MCP aza pshya tsiku ndi limodzi Osati Ndi chipani,Gulu la anyamata liku konzeka wenatu Alípo secret soldiers Malawi an there's is outside, Asirikari mukama gwiri sidwa ntchito Ndi MCP zizakuvutani yang'anirani Amalawi,Os militar não tenho partido, tem dereito para defender população ouviu Malawiano Malawiano não pode deixar Chakwera para vingar cidadão malawiano quidado Chakwera

  • @partmaulidiPatrick
    @partmaulidiPatrick10 күн бұрын

    Adahinuyo makwana

  • @user-pj9rs6vj8x
    @user-pj9rs6vj8x10 күн бұрын

    Iwe osatulutsa lako lowonalo bwanji?hahaha mabodza awa

  • @CheMass-05
    @CheMass-0510 күн бұрын

    🔥🔥🔥🔥

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip9 күн бұрын

    Am watching you from Lusaka zambia

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of10 күн бұрын

    awa ndachisilu sanena zobveka amakonda bodza uzanamiza alomwe azako

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg10 күн бұрын

    Bwanji ya nzungu wamathanyula sunafune kuti tiyikepo maganidzo

  • @IssacMateyo

    @IssacMateyo

    10 күн бұрын

    Sangave samadikila kuti amuuzeko ena kkkk

  • @Musa1828-l5d

    @Musa1828-l5d

    8 күн бұрын

    Ife tupanga kaye za ifa ya Malawi nzathu, akanakhala Chakwera wafa ifa yotere ifeso sitikanakhala chete tikanafuna chilungamo chioneke

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro8 күн бұрын

    Mcp omse ndi amagazi manja agalu Eni Eni mbuzi za wanthu

  • @AhmedKjuma
    @AhmedKjuma10 күн бұрын

    ❤❤😂😂😂 Koma kuthawadi

  • @PililanilikomwaLuwesi
    @PililanilikomwaLuwesi7 күн бұрын

    😢😢😢😢ok Malawi

  • @CathyYassimin
    @CathyYassimin9 күн бұрын

    Kumatu muli phwete achimwene

  • @rashidadan2533
    @rashidadan25339 күн бұрын

    Kagwedwe ka ndege tilibenazo ntchito , kubedwa kwa black box yamu ndege izo tilibenazo ntchito , Mufunilanji umboni wina chonsecho tikudziwa kuti chakwela ndi nduna zake ndizomwe zinapanga plani yogwetsa ndege yomwe inapha anthu 9 kuphatikizamo V'P Claus chilima .

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m9 күн бұрын

    Limpopo number one

  • @gremarmbewe9906
    @gremarmbewe99066 күн бұрын

    Following

  • @paulinekayuni1621
    @paulinekayuni16217 күн бұрын

    Vuto ndiloti report yanuyi sikhala official zomwe zikuoneka zabodzazo ndizomwe zizamveke makutu a anthu ambiri. Koma tingopemphera ngati zanuzi zili chilungamo zizakhale official and anapanga azazengedwe mlandu

  • @ChristopherNikola
    @ChristopherNikola10 күн бұрын

    Zilengwalengwadi eee

  • @OwamThoko
    @OwamThoko10 күн бұрын

    Zero ya bwino pofuna kukamiza chakwera kuti asiye anthu onse Malawi asiye lupita muzintchito dzeko lonse mabungwe ,aboma,amwenye asilikali,apolisi,mabusi,matekesi,mbc,wina aliyese,magurd ,capita muzintchito,palibee kanthu muvutike koma mawa muzasangala,dzeko lonse liyime paka achoke.mukuina bwanji amalawi

  • @OwamThoko

    @OwamThoko

    10 күн бұрын

    Yah mzeru yabwino,achoke basi ameneyu,

  • @SolomonAmon-bu5qc
    @SolomonAmon-bu5qc9 күн бұрын

    Koma yaah

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata40239 күн бұрын

    Limpopo iweyo umakwanila ndipo mulungu azikudalisani ndikupasani moyo wautali

  • @christopherchikankhen
    @christopherchikankhen10 күн бұрын

    Limpopo Yayamba Kunamiza Anthu, Munatiuza Kuti A Chidanti Malunga Ndiomwe Adasankhidwa Ukhala Wachiwiri.

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    10 күн бұрын

    Kkkk

  • @KennethChagunda-gn8kg

    @KennethChagunda-gn8kg

    9 күн бұрын

    Uyuyu ndiwa bodzadi akulu

  • @PatriciaIron
    @PatriciaIron10 күн бұрын

    Sanati amusankha chidanti koma amati ndizomwe akukambirana ndye nzosadabwitsa kuti ayitembenuza pamenepo

  • @user-pj9rs6vj8x

    @user-pj9rs6vj8x

    10 күн бұрын

    Mmmm anati amusakha osabakira mveraninso mwina simunamve bwino

  • @KennethChagunda-gn8kg

    @KennethChagunda-gn8kg

    9 күн бұрын

    Ndykt iyeyu amatiuza zopanda umbon

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Anaisintha game

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    ​@@KennethChagunda-gn8kgkoma zimaphelezera akulu sikuti amanama ayi

  • @JulietKamanga-t5n
    @JulietKamanga-t5n2 күн бұрын

    Ndipo ndimsona Ngati fm'yi ndiyakujonitu🤣🤣🤣🤣pa Malawi ayi ndithu

  • @AllanKasalu
    @AllanKasalu9 күн бұрын

    comrade Ntanyiwa woyeeeeeeeeeeeeeee

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of10 күн бұрын

    Lelo akuluwa zolakhula khalangati zasowa

  • @KennethChagunda-gn8kg

    @KennethChagunda-gn8kg

    9 күн бұрын

    Ndiwa bodza inu munthu uyu. Kd iyeyu akudziwa bwanji zonsezi munthu ali ku SA??

  • @lloydmushali-dw2td
    @lloydmushali-dw2td9 күн бұрын

    Limpopo FM❤❤

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias99729 күн бұрын

    Its better kumakamba zinthu ndi umboni coz pamawa uzayankha brother

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    La 40likwana one day is one day

  • @JoyceChimphwika
    @JoyceChimphwika8 күн бұрын

    Ulosi wa grace chinga umandikumbusa kwambili chipani chamwadzi ichi mulungu achite nawo ndithu

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Ndipo kwambiri tu mmm

  • @DanielErnest-ez1qw
    @DanielErnest-ez1qw3 күн бұрын

    No comment

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko9 күн бұрын

    Inu ndabodza,anthu akumayakhula bwanji sakuwamanga?

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda9 күн бұрын

    Alimi afodya asangalala chaka chino musanamizepo anthu pamenepo inu a Limpopo FM. Ifenso alimi achimanga tikusangalala panopa chafika kale 750 per kg osati za 150 zija tinkaona mmbuyo zija ali, zomathandiza alesi osalima, olima nkumangolira. Kazingokhalani kumeneko anthu osowa zochita inu.

  • @priscillamangata4023

    @priscillamangata4023

    9 күн бұрын

    150 mukuinenayo and imagula feteleza 18000 matumba awili zingafanane ndipano 200000 matumba awili

  • @LucianoKapepuza-sy9wx

    @LucianoKapepuza-sy9wx

    4 күн бұрын

    Are u a member if MCP or are u from central region u show your evil and dirty mind here better no comment if u not interested with him

  • @LucianoKapepuza-sy9wx

    @LucianoKapepuza-sy9wx

    4 күн бұрын

    Its not home of debates

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal9 күн бұрын

    Ndiye akugwesa kwachayo ndindani mesa ndichisilu chanucho

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh10 күн бұрын

    Mesa mumati asankha a chidati malunga inu mungodziwa kunamiza a malawi basi

  • @asayileernestsapao
    @asayileernestsapao10 күн бұрын

    Ndayamba kukukayikilani

  • @KennethChagunda-gn8kg

    @KennethChagunda-gn8kg

    9 күн бұрын

    Uyuyu atisokoneza mitu aaaaa

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko9 күн бұрын

    Asilikali aku Malawi amasunga mwambo,uyu ndiwabodza simsilikali!

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata40239 күн бұрын

    Prophet mbeweyo Ndie ayiso aaaaaaaa athu opephela siawa akutiliza apawa

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda9 күн бұрын

    Mabodza anuwo akutsalirani makape inu. Mwakonzekeratu zodzatsutsa lipoti powanamiza amalawi. Muchite manyazi.

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon8 күн бұрын

    Ndichifukwa chiyani osangomuchoseratu pompano chakwerayo? Apatu zikuonesakuti before 2025 kukhala kutafa anthu ambiri chakwera salibwinoyi

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Ndipo kwambiri tu mmm

  • @AbbeyJere
    @AbbeyJere7 күн бұрын

    26:58

  • @KennethChagunda-gn8kg
    @KennethChagunda-gn8kg9 күн бұрын

    Koma kodi iweyo ngati ukudziwa chulungamo bwanji osangonena?komanso ngt unkadziwa chomwe chinkachitika udatan iweyo kukawapulumutsa?? Komanso apa unanena kt Vp asankha Chidathi Malungo now is Usi ndy anthu tikukhulupilira bwanj kt umanena zoona??

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc9 күн бұрын

    Chakwera evil 😈

  • @Emmanuelisraelsimbi
    @Emmanuelisraelsimbi10 күн бұрын

    Why unati kut chidanti ndi amene akhale vice president lero tu ndi Usi

  • @KennethChagunda-gn8kg

    @KennethChagunda-gn8kg

    9 күн бұрын

    Uyuyu ndiwa bodza akulu akungofuna kumatipatsa uthenga wabodza

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 күн бұрын

    Anaisintha game kkk

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWO9 күн бұрын

    🔥🔥🔥🔥🇲🇼🇲🇼🇲🇼💕✔️

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro8 күн бұрын

    Usiyo chiwembu chomwe anafera chilima uja akuchiziwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg10 күн бұрын

    Nzunguyo amafunika kuti akadzike nayo chakwera 😂😂😂 wakupha

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda9 күн бұрын

    Wokhulupirira mabodza a Limpopo mutu wake sugwira. Ndani adatuma anyamata achipani kukafufuza za ndege? Muzichita manyazi ndi propaganda yanu makape inu.

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w9 күн бұрын

    Kkkkkkk achewa koma nyawu basi mukhaula munya

  • @user-lg2ws2ki3d
    @user-lg2ws2ki3d9 күн бұрын

    Koma mbuli iyi aaaa

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu10 күн бұрын

    🔥🔥🔥🔥 Limpopo umakwana

  • @oathbilliot

    @oathbilliot

    10 күн бұрын

    ❤❤❤❤Limpopo

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p8 күн бұрын

    Vutoso la inu ndi la propaganda,,, Zikanakhala kuti mumangotiuza nkhani kuti tinve tidziwe mmene zinthu zikuyendela Koma mumapangaso campaign kuti anthu anvotele yemwe inu mukumufuna this is no sense

  • @user-pj9rs6vj8x
    @user-pj9rs6vj8x10 күн бұрын

    Hahaha wailesi yabodza iyi dzulo imatiuza bodza kuti vice president ndi chidanti malunga lero alengeza kuti ndi manganya hahaha ndinkana social media sindimaikhulupirira

  • @user-bz4dw6vy7w
    @user-bz4dw6vy7w4 күн бұрын

    Maloza ndithu

  • @CvgGgbnb
    @CvgGgbnb9 күн бұрын

    Wabodza uyu bwanji osamuchula munthu ndimozi yemwe

  • @francismlilima
    @francismlilima8 күн бұрын

    Koma mukuchulikitsa gagadiwa...go straight to the points

Келесі