Limpopo FM yomweyo galu iwe Ntanyiwa kufotokoza za anthu 7 omwe anakamaliza a Chilima ndi anzawo
Жүктеу.....
Пікірлер: 134
@giftwankhama991410 күн бұрын
Stay safe comrade. May the God in heaven keep u safe my brother.u the only source of true information to us.
@peterlowole784110 күн бұрын
We are great to have you comrades
@jacquelinecunningham36310 күн бұрын
Limpopo 🎉🎉❤❤🔥🔥🔥🔥🔥💯
@eliasnyilongo48659 күн бұрын
My redio in malawi
@user-ph3zy9ox7d9 күн бұрын
From South Africa all i have is a protecton prayer for you my brother ,, may God protect you from these anacondas for not swallowing you Amen
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Tikuziwa zisisi zambiritu mmm
@user-kr4wb2th9i10 күн бұрын
❤❤❤❤more fire 🔥🔥🔥 ndipo titemana serious muno oky mungoti pheee anthu amenewa asazayerekeze kubwera kumangochi serious azaona ngati akufuna kuti azalembe book la history lomkuzana anthu akumangochi 2024 yelekezani kubwera kuno , zimunezo kulilongwe komweko kwa anthu aganiza mwauchitsiluwo try to come here in Mangochi try
@Hudhayf
10 күн бұрын
😂😂😂😂 Mangochi m'bomamo
@user-rg4du4vu9r10 күн бұрын
Kunena zowona paziko rapansi pano paribe chinsinsi sure nyimbo ikhare ya grace chinga ndizaurura tchimo rimazunza orichita sure 🥱🙆
@augustMag10 күн бұрын
Tili pano kudikira Chilungamo chioneke ndi Limpopo FM radio 🔥♥️
2025 they will be no votes. Dziko lonse lapansi kukhala Climate Lockdown(NWO) mufufuze zimenezi
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Kkk
@Musa1828-l5d8 күн бұрын
Viva Limpopo FM ❤❤🔥🔥🔥🔥🔥
@TryceMagombo-sh7kb2 күн бұрын
Big up big more and more imfo
@emmanuelalbertbotolo9 күн бұрын
More fire Mr muthanyiwa
@user-mh5xw5xu9w7 күн бұрын
Number one Limpopo FM more 🔥
@AliceGeorge-il6ig9 күн бұрын
Bravo bravo achimwene,be safe plz
@samchibenene44589 күн бұрын
Mo fire Limpopo FM
@user-wg8tp8in1v10 күн бұрын
Koma mathelo a nkhani izi ndi Otani?
@WilliamKapungu10 күн бұрын
Amfumu akabudula 😂😂😂😂 muziti Chan? 😂😂😂😂
@RichardMphopheya9 күн бұрын
more fire limpopo
@user-qg4it7my9n10 күн бұрын
kkkkkkk ooooh ndodo itulukedi basi
@KeltonKapanda2 күн бұрын
May God keep you safe comred
@jonas-xh4hz10 күн бұрын
mumakwanira a mtanyiwa
@ZelipaMalanda9 күн бұрын
Munthu akuyankhula za achewayu wangoonetseratu umbuli waku wonse kuti za democracy sazidziwa. Democracy imabwera ndi ma condition ake. Boma lingapereke ku ma company angati ndi ufulu wa pa malonda omwe ulipowu? Muli ma company angati m'Malawi muno kuti boma lingakwanitse kuperekako ndalama? Taganizirani za fetereza wotsika mtengo momwe zikuyendera, akupindula ndi amphawi kapena anthu andalama? Zomwe zikuchitika ndi fetereza ndi zomwe zikhoza kuchitikanso ndi sopo kaya ndi sugar kaya ndi mafuta ophikira. Omwe ali ndi ndalama zambiri akhoza kumakangozikokololako zonse nkumagulitsa ku amphawiwo modulabe.
We are very angry we want to given us good information,we are not joking, Chakwera,Chakwera, Becareful., you will flee and Leave Malawi One Day,zida wagula zija ndi zathu tizazi tenga zonse tiku ziwa Chakwera Ufa ngati Nazombe Malawi uyu ndiwa sopano Siwa Kale munapha uja Chirima ndiye Anali bwana wanu,siku limodzi ma ofesi a MCP aza pshya tsiku ndi limodzi Osati Ndi chipani,Gulu la anyamata liku konzeka wenatu Alípo secret soldiers Malawi an there's is outside, Asirikari mukama gwiri sidwa ntchito Ndi MCP zizakuvutani yang'anirani Amalawi,Os militar não tenho partido, tem dereito para defender população ouviu Malawiano Malawiano não pode deixar Chakwera para vingar cidadão malawiano quidado Chakwera
@partmaulidiPatrick10 күн бұрын
Adahinuyo makwana
@user-pj9rs6vj8x10 күн бұрын
Iwe osatulutsa lako lowonalo bwanji?hahaha mabodza awa
Bwanji ya nzungu wamathanyula sunafune kuti tiyikepo maganidzo
@IssacMateyo
10 күн бұрын
Sangave samadikila kuti amuuzeko ena kkkk
@Musa1828-l5d
8 күн бұрын
Ife tupanga kaye za ifa ya Malawi nzathu, akanakhala Chakwera wafa ifa yotere ifeso sitikanakhala chete tikanafuna chilungamo chioneke
@LazaroSinerioSineiro8 күн бұрын
Mcp omse ndi amagazi manja agalu Eni Eni mbuzi za wanthu
@AhmedKjuma10 күн бұрын
❤❤😂😂😂 Koma kuthawadi
@PililanilikomwaLuwesi7 күн бұрын
😢😢😢😢ok Malawi
@CathyYassimin9 күн бұрын
Kumatu muli phwete achimwene
@rashidadan25339 күн бұрын
Kagwedwe ka ndege tilibenazo ntchito , kubedwa kwa black box yamu ndege izo tilibenazo ntchito , Mufunilanji umboni wina chonsecho tikudziwa kuti chakwela ndi nduna zake ndizomwe zinapanga plani yogwetsa ndege yomwe inapha anthu 9 kuphatikizamo V'P Claus chilima .
@user-dk6yc8pl2m9 күн бұрын
Limpopo number one
@gremarmbewe99066 күн бұрын
Following
@paulinekayuni16217 күн бұрын
Vuto ndiloti report yanuyi sikhala official zomwe zikuoneka zabodzazo ndizomwe zizamveke makutu a anthu ambiri. Koma tingopemphera ngati zanuzi zili chilungamo zizakhale official and anapanga azazengedwe mlandu
@ChristopherNikola10 күн бұрын
Zilengwalengwadi eee
@OwamThoko10 күн бұрын
Zero ya bwino pofuna kukamiza chakwera kuti asiye anthu onse Malawi asiye lupita muzintchito dzeko lonse mabungwe ,aboma,amwenye asilikali,apolisi,mabusi,matekesi,mbc,wina aliyese,magurd ,capita muzintchito,palibee kanthu muvutike koma mawa muzasangala,dzeko lonse liyime paka achoke.mukuina bwanji amalawi
Wokhulupirira mabodza a Limpopo mutu wake sugwira. Ndani adatuma anyamata achipani kukafufuza za ndege? Muzichita manyazi ndi propaganda yanu makape inu.
@user-vh9uk1jy7w9 күн бұрын
Kkkkkkk achewa koma nyawu basi mukhaula munya
@user-lg2ws2ki3d9 күн бұрын
Koma mbuli iyi aaaa
@BlessingsTembenu10 күн бұрын
🔥🔥🔥🔥 Limpopo umakwana
@oathbilliot
10 күн бұрын
❤❤❤❤Limpopo
@user-mz8nw6nx6p8 күн бұрын
Vutoso la inu ndi la propaganda,,, Zikanakhala kuti mumangotiuza nkhani kuti tinve tidziwe mmene zinthu zikuyendela Koma mumapangaso campaign kuti anthu anvotele yemwe inu mukumufuna this is no sense
@user-pj9rs6vj8x10 күн бұрын
Hahaha wailesi yabodza iyi dzulo imatiuza bodza kuti vice president ndi chidanti malunga lero alengeza kuti ndi manganya hahaha ndinkana social media sindimaikhulupirira
Пікірлер: 134
Stay safe comrade. May the God in heaven keep u safe my brother.u the only source of true information to us.
We are great to have you comrades
Limpopo 🎉🎉❤❤🔥🔥🔥🔥🔥💯
My redio in malawi
From South Africa all i have is a protecton prayer for you my brother ,, may God protect you from these anacondas for not swallowing you Amen
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Tikuziwa zisisi zambiritu mmm
❤❤❤❤more fire 🔥🔥🔥 ndipo titemana serious muno oky mungoti pheee anthu amenewa asazayerekeze kubwera kumangochi serious azaona ngati akufuna kuti azalembe book la history lomkuzana anthu akumangochi 2024 yelekezani kubwera kuno , zimunezo kulilongwe komweko kwa anthu aganiza mwauchitsiluwo try to come here in Mangochi try
@Hudhayf
10 күн бұрын
😂😂😂😂 Mangochi m'bomamo
Kunena zowona paziko rapansi pano paribe chinsinsi sure nyimbo ikhare ya grace chinga ndizaurura tchimo rimazunza orichita sure 🥱🙆
Tili pano kudikira Chilungamo chioneke ndi Limpopo FM radio 🔥♥️
Viva Limpopo FM
❤❤❤❤ More fire comrade ntanyiwa
Tili pa mbuyo panu
watching from cape town limpopo no: 1
Mulungu salakwitsa kalikose adziwa yekha chochita nximu wanu uuse mumtendere bwana chilima
Chakwerao osangomuombera bwanji watikwana kwambiliaaa
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Ndipo inu mmm
Thanks alot comrade, May God protect u so that a Malawi tipitilize kuziwa zoona zenizeni
Comrade mtanyiwa! Chamzelutu apa kunali kungotulusa zinthuso coz mukat mwatulusa olo report mudikilalo sangatuluseso n mukhoza kumacedwa conco then kaya nditsokaso akusowetsan sibas zizakhala kut mwatidikilisa pachabe umbon muli nawowoso mwapita nawo! Tulusan chabe zomwe muli nazozo mukucedwa mukucedwa
@user-pj9rs6vj8x
10 күн бұрын
Umboni alibe awa chomwe akukanikira kutulutsa ndi chani?monse muja
@user-mq7ou5xp5m
8 күн бұрын
Chabodza ichi
Following.... Limpopo 🔥 🔥 🔥
Mbuzi zawanrhu zukanika kulamulira dzko
Umunthu alibe mphamvu ya satana basi,ngati opemphera koma Satana weniweni ineso ndi mchewa koma awaso aonjeza
More fire
Magalimoto adutsa ku Lunzu?
Chidanti Malunga wako uja amusankhadi kukhala VP monga umanenera dzulo lija
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Anaisintha game
Limpopo ❤🔥🔥🔥
Keep on inform us good work
This is true station
Magalimoto amene mukunenawo mungovutika amene aja ndi alendo ongudusa amachoka ku nacala port adusa ku Moçambique mpaka zimbabwe
Watching from limpopo province in lephalale town
Emusipi Chipani Cha Nkhanza komanso chakupha
Wina aziphe kumene agalu amenewa sangatiphele adzibale athu motelo
More fire comrade kusatira ndi chidwi
Ipanse Moto tiziwe zoona zen zen
2025 they will be no votes. Dziko lonse lapansi kukhala Climate Lockdown(NWO) mufufuze zimenezi
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Kkk
Viva Limpopo FM ❤❤🔥🔥🔥🔥🔥
Big up big more and more imfo
More fire Mr muthanyiwa
Number one Limpopo FM more 🔥
Bravo bravo achimwene,be safe plz
Mo fire Limpopo FM
Koma mathelo a nkhani izi ndi Otani?
Amfumu akabudula 😂😂😂😂 muziti Chan? 😂😂😂😂
more fire limpopo
kkkkkkk ooooh ndodo itulukedi basi
May God keep you safe comred
mumakwanira a mtanyiwa
Munthu akuyankhula za achewayu wangoonetseratu umbuli waku wonse kuti za democracy sazidziwa. Democracy imabwera ndi ma condition ake. Boma lingapereke ku ma company angati ndi ufulu wa pa malonda omwe ulipowu? Muli ma company angati m'Malawi muno kuti boma lingakwanitse kuperekako ndalama? Taganizirani za fetereza wotsika mtengo momwe zikuyendera, akupindula ndi amphawi kapena anthu andalama? Zomwe zikuchitika ndi fetereza ndi zomwe zikhoza kuchitikanso ndi sopo kaya ndi sugar kaya ndi mafuta ophikira. Omwe ali ndi ndalama zambiri akhoza kumakangozikokololako zonse nkumagulitsa ku amphawiwo modulabe.
Katundu akudula chifukwa cha kugwa kwa Kwacha yathu. Kwacha yathu ikugwa pafupipafupi chifukwa chosowa forex, forex ikusowa chifukwa chochepa kwa export; amalawi tachulutsa ma import osati export. Amalawi tiyeni tilimbikire kugwira ntchito zomwe zitha kutibweretsera katundu yemwe titha kutumiza mayiko akunja kuti forex ilowemo yambiri muno.
Ndizisiru chakwera watha basi South Africa
We are very angry we want to given us good information,we are not joking, Chakwera,Chakwera, Becareful., you will flee and Leave Malawi One Day,zida wagula zija ndi zathu tizazi tenga zonse tiku ziwa Chakwera Ufa ngati Nazombe Malawi uyu ndiwa sopano Siwa Kale munapha uja Chirima ndiye Anali bwana wanu,siku limodzi ma ofesi a MCP aza pshya tsiku ndi limodzi Osati Ndi chipani,Gulu la anyamata liku konzeka wenatu Alípo secret soldiers Malawi an there's is outside, Asirikari mukama gwiri sidwa ntchito Ndi MCP zizakuvutani yang'anirani Amalawi,Os militar não tenho partido, tem dereito para defender população ouviu Malawiano Malawiano não pode deixar Chakwera para vingar cidadão malawiano quidado Chakwera
Adahinuyo makwana
Iwe osatulutsa lako lowonalo bwanji?hahaha mabodza awa
🔥🔥🔥🔥
Am watching you from Lusaka zambia
awa ndachisilu sanena zobveka amakonda bodza uzanamiza alomwe azako
Bwanji ya nzungu wamathanyula sunafune kuti tiyikepo maganidzo
@IssacMateyo
10 күн бұрын
Sangave samadikila kuti amuuzeko ena kkkk
@Musa1828-l5d
8 күн бұрын
Ife tupanga kaye za ifa ya Malawi nzathu, akanakhala Chakwera wafa ifa yotere ifeso sitikanakhala chete tikanafuna chilungamo chioneke
Mcp omse ndi amagazi manja agalu Eni Eni mbuzi za wanthu
❤❤😂😂😂 Koma kuthawadi
😢😢😢😢ok Malawi
Kumatu muli phwete achimwene
Kagwedwe ka ndege tilibenazo ntchito , kubedwa kwa black box yamu ndege izo tilibenazo ntchito , Mufunilanji umboni wina chonsecho tikudziwa kuti chakwela ndi nduna zake ndizomwe zinapanga plani yogwetsa ndege yomwe inapha anthu 9 kuphatikizamo V'P Claus chilima .
Limpopo number one
Following
Vuto ndiloti report yanuyi sikhala official zomwe zikuoneka zabodzazo ndizomwe zizamveke makutu a anthu ambiri. Koma tingopemphera ngati zanuzi zili chilungamo zizakhale official and anapanga azazengedwe mlandu
Zilengwalengwadi eee
Zero ya bwino pofuna kukamiza chakwera kuti asiye anthu onse Malawi asiye lupita muzintchito dzeko lonse mabungwe ,aboma,amwenye asilikali,apolisi,mabusi,matekesi,mbc,wina aliyese,magurd ,capita muzintchito,palibee kanthu muvutike koma mawa muzasangala,dzeko lonse liyime paka achoke.mukuina bwanji amalawi
@OwamThoko
10 күн бұрын
Yah mzeru yabwino,achoke basi ameneyu,
Koma yaah
Limpopo iweyo umakwanila ndipo mulungu azikudalisani ndikupasani moyo wautali
Limpopo Yayamba Kunamiza Anthu, Munatiuza Kuti A Chidanti Malunga Ndiomwe Adasankhidwa Ukhala Wachiwiri.
@inessmsiyambiri8517
10 күн бұрын
Kkkk
@KennethChagunda-gn8kg
9 күн бұрын
Uyuyu ndiwa bodzadi akulu
Sanati amusankha chidanti koma amati ndizomwe akukambirana ndye nzosadabwitsa kuti ayitembenuza pamenepo
@user-pj9rs6vj8x
10 күн бұрын
Mmmm anati amusakha osabakira mveraninso mwina simunamve bwino
@KennethChagunda-gn8kg
9 күн бұрын
Ndykt iyeyu amatiuza zopanda umbon
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Anaisintha game
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
@@KennethChagunda-gn8kgkoma zimaphelezera akulu sikuti amanama ayi
Ndipo ndimsona Ngati fm'yi ndiyakujonitu🤣🤣🤣🤣pa Malawi ayi ndithu
comrade Ntanyiwa woyeeeeeeeeeeeeeee
Lelo akuluwa zolakhula khalangati zasowa
@KennethChagunda-gn8kg
9 күн бұрын
Ndiwa bodza inu munthu uyu. Kd iyeyu akudziwa bwanji zonsezi munthu ali ku SA??
Limpopo FM❤❤
Its better kumakamba zinthu ndi umboni coz pamawa uzayankha brother
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
La 40likwana one day is one day
Ulosi wa grace chinga umandikumbusa kwambili chipani chamwadzi ichi mulungu achite nawo ndithu
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
No comment
Inu ndabodza,anthu akumayakhula bwanji sakuwamanga?
Alimi afodya asangalala chaka chino musanamizepo anthu pamenepo inu a Limpopo FM. Ifenso alimi achimanga tikusangalala panopa chafika kale 750 per kg osati za 150 zija tinkaona mmbuyo zija ali, zomathandiza alesi osalima, olima nkumangolira. Kazingokhalani kumeneko anthu osowa zochita inu.
@priscillamangata4023
9 күн бұрын
150 mukuinenayo and imagula feteleza 18000 matumba awili zingafanane ndipano 200000 matumba awili
@LucianoKapepuza-sy9wx
4 күн бұрын
Are u a member if MCP or are u from central region u show your evil and dirty mind here better no comment if u not interested with him
@LucianoKapepuza-sy9wx
4 күн бұрын
Its not home of debates
Ndiye akugwesa kwachayo ndindani mesa ndichisilu chanucho
Mesa mumati asankha a chidati malunga inu mungodziwa kunamiza a malawi basi
Ndayamba kukukayikilani
@KennethChagunda-gn8kg
9 күн бұрын
Uyuyu atisokoneza mitu aaaaa
Asilikali aku Malawi amasunga mwambo,uyu ndiwabodza simsilikali!
Prophet mbeweyo Ndie ayiso aaaaaaaa athu opephela siawa akutiliza apawa
Mabodza anuwo akutsalirani makape inu. Mwakonzekeratu zodzatsutsa lipoti powanamiza amalawi. Muchite manyazi.
Ndichifukwa chiyani osangomuchoseratu pompano chakwerayo? Apatu zikuonesakuti before 2025 kukhala kutafa anthu ambiri chakwera salibwinoyi
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
26:58
Koma kodi iweyo ngati ukudziwa chulungamo bwanji osangonena?komanso ngt unkadziwa chomwe chinkachitika udatan iweyo kukawapulumutsa?? Komanso apa unanena kt Vp asankha Chidathi Malungo now is Usi ndy anthu tikukhulupilira bwanj kt umanena zoona??
Chakwera evil 😈
Why unati kut chidanti ndi amene akhale vice president lero tu ndi Usi
@KennethChagunda-gn8kg
9 күн бұрын
Uyuyu ndiwa bodza akulu akungofuna kumatipatsa uthenga wabodza
@user-ky4ce9gb6j
5 күн бұрын
Anaisintha game kkk
🔥🔥🔥🔥🇲🇼🇲🇼🇲🇼💕✔️
Usiyo chiwembu chomwe anafera chilima uja akuchiziwa
Nzunguyo amafunika kuti akadzike nayo chakwera 😂😂😂 wakupha
Wokhulupirira mabodza a Limpopo mutu wake sugwira. Ndani adatuma anyamata achipani kukafufuza za ndege? Muzichita manyazi ndi propaganda yanu makape inu.
Kkkkkkk achewa koma nyawu basi mukhaula munya
Koma mbuli iyi aaaa
🔥🔥🔥🔥 Limpopo umakwana
@oathbilliot
10 күн бұрын
❤❤❤❤Limpopo
Vutoso la inu ndi la propaganda,,, Zikanakhala kuti mumangotiuza nkhani kuti tinve tidziwe mmene zinthu zikuyendela Koma mumapangaso campaign kuti anthu anvotele yemwe inu mukumufuna this is no sense
Hahaha wailesi yabodza iyi dzulo imatiuza bodza kuti vice president ndi chidanti malunga lero alengeza kuti ndi manganya hahaha ndinkana social media sindimaikhulupirira
Maloza ndithu
Wabodza uyu bwanji osamuchula munthu ndimozi yemwe
Koma mukuchulikitsa gagadiwa...go straight to the points