kunoku moyo wake ndi osiphina omwewu basi. Malawi zikuoneka kut m'manja mwa atsamunda sitinachokemo ayi
@user-py4nr7yz4x8 ай бұрын
Mukutiyimirira kumred go go go km ndikufuna nyimboyi yoti chakwera watipweteka anayimba ND ndan
@user-du9qs4tb6u20 күн бұрын
Live from south Africa Muyaluka chaka chake ndi chino
@MarthaJafali
8 күн бұрын
Auzeni
@MagretMvula8 ай бұрын
Tikuthokozeni ntciito ndi yayikulu mukugwila more fire mulungu aikepo zanja tione mphumulo mumalawi
@user-kw7hv5kg7z8 ай бұрын
More fire no fear comrade go go go!!!!!!
@AnishaMoosa-ej7yr6 ай бұрын
Online from Pretoria
@GanizaniKamvazaana10 күн бұрын
Koma ambuye kumwambako musatipitirire ku Malawi 😢😢😢
@user-xt2gu9yt9q3 ай бұрын
Kulonjedza nde analonjeza ndikalephela kusitha dzithu kwa dzaka wilili ndizatula pasi udndo Kodi pana pano sanavomeleza kuti alephela kukweza Malawi pano Malawi alipamoto kuposa alamulilo wa muthalika
@peterphir22508 ай бұрын
Atsogoleri tikuyamikireni koma nkhani zanu simukumaliza mukaziyamba ngati mukunena kuti ntchito zomwe akugwira anthuwa ndi malipiro pa zomwe achita powotcha wa police ku Nsanje kutanthauza kuti anatumidwa ndi abomawo, ndiye a bomawo akuuzani chilungamo chotani? Inu mukadaulula zifukwa zomwe adamuwotchera wa police kuti womutumawo adziwe kuti abisala mmbatata musamangochulukisa kuseka ndi kamangoyimba nyimbo ayi, ifeyo timamvetsera ndi chidwi kuti nkhanga zaonanji tidziwe koma mumango nena molumpha lumpha ngati kuti zomwe mukuwulusa ndi zongopeka so please help us we love you
@SheenahMwalabu-iz3pr
8 ай бұрын
Ndipo message yomwe imasowa muno ndeiyiyi kkk kumatambasula bobo ngati muja apangila DC Kalindo, otherwise zikumavuta kuzitsatatu. Love you ❤❤
@user-oj5ye6bj9q
4 ай бұрын
That's true muzimalizisa nkhanizo kut tiziziwa zoona zenizeni wr real love you mr Comrade
@ChrifordBiziel7 күн бұрын
Opusa iwee ukusochelesa amalawi koma amalawi anapenya zidya drama za muthalikazo ife tikupitax chisogolo ndi mcp bas
Пікірлер: 88
Mwaswela bwanji nonse amene mumamvela pa nkhanga zaona.ngati mulibwino dzikomo
More fire kt Buuuuuuu!!!
Ndipo musasiye mukutisegula maso❤
Yomweyo galu iwe Nankhumwa😅😅😅😂😂😂😂😂😅😅😅😅😅
Antanyiwa ndakusowani
Zana amayi asanka chifanti malunga ngati vice koma pano ndi opposite ndi zambiri zomwe amalankhula za boza
Osafoka osatopa osawopa
timakunyadilila big man .mtiuzilekoso wa bakili Muluzi tv tawasowa mau ake😢😢😢 guys timakunyadilan
😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅kwagwanji bambo
Mwaswela bwanji abale anga pa nkhanga zaona,ineyo kuno ndilibwino
Keep giving us updates
Limpopo fm moto buuuuuu
Osaopa mulipa bill yanga 😂😂😂
Tiyenazoni ,ife tilipambuyopa tidziwe
Limpopo FM more fire
Mundifunsilenso chipatala chakumangochi chimawotchedwa chakandichaka zikukhalabwanji?
Limpopo moto kuti buuu
Timanyadila Limpopo fm
More fire broo osaopaaaa kunena chilungamo.
Koma nyimbo zachuluka
Mbambande nkhanga zaona❤️🔥
kunoku moyo wake ndi osiphina omwewu basi. Malawi zikuoneka kut m'manja mwa atsamunda sitinachokemo ayi
Mukutiyimirira kumred go go go km ndikufuna nyimboyi yoti chakwera watipweteka anayimba ND ndan
Live from south Africa Muyaluka chaka chake ndi chino
@MarthaJafali
8 күн бұрын
Auzeni
Tikuthokozeni ntciito ndi yayikulu mukugwila more fire mulungu aikepo zanja tione mphumulo mumalawi
More fire no fear comrade go go go!!!!!!
Online from Pretoria
Koma ambuye kumwambako musatipitirire ku Malawi 😢😢😢
Kulonjedza nde analonjeza ndikalephela kusitha dzithu kwa dzaka wilili ndizatula pasi udndo Kodi pana pano sanavomeleza kuti alephela kukweza Malawi pano Malawi alipamoto kuposa alamulilo wa muthalika
Atsogoleri tikuyamikireni koma nkhani zanu simukumaliza mukaziyamba ngati mukunena kuti ntchito zomwe akugwira anthuwa ndi malipiro pa zomwe achita powotcha wa police ku Nsanje kutanthauza kuti anatumidwa ndi abomawo, ndiye a bomawo akuuzani chilungamo chotani? Inu mukadaulula zifukwa zomwe adamuwotchera wa police kuti womutumawo adziwe kuti abisala mmbatata musamangochulukisa kuseka ndi kamangoyimba nyimbo ayi, ifeyo timamvetsera ndi chidwi kuti nkhanga zaonanji tidziwe koma mumango nena molumpha lumpha ngati kuti zomwe mukuwulusa ndi zongopeka so please help us we love you
@SheenahMwalabu-iz3pr
8 ай бұрын
Ndipo message yomwe imasowa muno ndeiyiyi kkk kumatambasula bobo ngati muja apangila DC Kalindo, otherwise zikumavuta kuzitsatatu. Love you ❤❤
@user-oj5ye6bj9q
4 ай бұрын
That's true muzimalizisa nkhanizo kut tiziziwa zoona zenizeni wr real love you mr Comrade
Opusa iwee ukusochelesa amalawi koma amalawi anapenya zidya drama za muthalikazo ife tikupitax chisogolo ndi mcp bas
Akut anapengapo Misara kkkkkk amawona ngt amalawi angagwrinse ntchito Misara yakeyo
Uyu ngwa maboza saziwa kufufuza nkhani zoona
@robenallie6985
8 күн бұрын
Ndizzkho zimenezo ife tikumudalira anatiuza kuti onse amu ndege amwalira zinali zoona
Koma comrede indipha ndi phwete😂😂😂😂😂😂😂
dyimboyi iilibwinowo😂😂😂😂😂
More fire Limpopo
Lipopo fm Palibeso ai
Bola bon kalindo ndi bakili mukuzi tv amafufuza mokuya kwambiri
Wanunkha malawi
Awa ndaboza awa
Mumakwana bwana
Zomaotchazi zisiyike chifukwa tsiku lina mudzagwidwa ndiye tidzaona
❤ big up brother
Mwadza bwanji
Osapa todze ndi amalawi fredom c_to_
Auzeni apite kumangochi aone
Zoona big man
Osafooka osatopa osagonja
Yah tamudziwa.....uja ali ndi bukula azibambo
Kkkkkk koma nkhani zimankhala apa🤣🤣
Timakudyadirani our comrade!!
Tilinawe limodzi limpopo Fm mumatiimilila
Kkkkk koma eeeee
Never give up
fire fire
Lipopo mo faya
Achimwene mumanikwana
Eisj where are you brah Malawi first we're confused ryt niw so brah plz tell us the truth
😂😂😂😂😂😂
😂😂 amangonyera mplastic
😂😂😂😂😂 Limpopo fm
Auze ngozi
Zikachitika timvera kwainu
Kkkkkkkkkkkk Sevethday
Morefire
avomele zavuta ayimikemaja
Mulipo angt,
Koma Patricia unaziyamba wenkha kkkkk
😊
Limpopo fm ndimainyadila kwambli simabisa zigawenge 😂😂😂 more fire nkhanga zaona ife nde malawi olilawo
@HOMEOFTECHNOLOGY
8 ай бұрын
Mumakwana Limpopo mumatiimirira Ife a malawi potidziwitsa zonunkha za afisi a nkhaza awa tikudziwanao zambiri 😂😂😂
@GanieAlidih
8 ай бұрын
Kwan
Kkkkkkkk 😂😂😂😂😂
Zamphanvu
Zifukule zose zidziwike❤
😂😂😂
😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Go deeper comrade, proud of you always 🔥🔥🔥🔥
Lovely song🎉🎉🎉
Network problem ashh
Limpopo fm moto buuuuuu
Limpopo fm moto buuuuuu
Limpopo fm moto buuuuuu