#malawi #trending #news
😢😢😢😢pepani kwambili
Akaidi awa ..amankhala anthu akundende ..ma prisioners ..
Ndiye paliso ena pa social Amati ndi azising'añga ine ndiye andibera mokwana okwana 7
Olo ine ndabeledwa ku besa R2000 kenako kuyamba kusowa ndiwo iiiii ayi
Kkkkkkkkkkk kufuna ndalama yosavutikila et mudziona
Basi kulimbikila kugwila tchito ndi njila yokhayo basi pangako ganyu kapena ayi kabisinesi kangachepe
iiii alipo ambiri. akubawo ineso umboni ndili nawo ndikukupaseni ma nbr ndibupasani
Ndi ayawo akumapanga zimenezo
Adzapezeka ndi mneneri wabodza
Babo asapesa ndi zoonadi ineso zinadichitiki ndili ndi umbone ose moti ndinabesa ndalama
Chonde abale anga, chinsinsi choti ukhale ndi moyo ochita bwino ndi chimondzi chokha "KUCHIRIMIKA, KAPENA KUTI, KUGWIRA NTCHITO NDI MPHANVU ZAKO".
akuba avutatu mmmm
😢😢😢😢😢😢
Mmmm kma abale mulungu alowelelepo
Amankhala anthu akundende awa ma prisoners ...akaidi
😢😢
Mavuto 😢😢😢😢😢
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Kuchita kudziwikilatu kuti wakuba uyu mmmm zokamba zake mmmm Mulungu akuyendereni muyaluke komwe muliko
amalawi kupusa anthu ali kundende kale milako ichoka kuti ali ku chichili phulizoni
Mulungu amukatha munthu ameneyo ndithu mmmm😢😢😢😢
Mauwo ngati nyapala, koma kumalawi eeeee mbola zokhazokha.
Ndi emweyo😅😅😅
@@emiliaumali8360 kkkkk koma iwe usanditseketse.
Пікірлер: 24
😢😢😢😢pepani kwambili
Akaidi awa ..amankhala anthu akundende ..ma prisioners ..
Ndiye paliso ena pa social Amati ndi azising'añga ine ndiye andibera mokwana okwana 7
Olo ine ndabeledwa ku besa R2000 kenako kuyamba kusowa ndiwo iiiii ayi
Kkkkkkkkkkk kufuna ndalama yosavutikila et mudziona
Basi kulimbikila kugwila tchito ndi njila yokhayo basi pangako ganyu kapena ayi kabisinesi kangachepe
iiii alipo ambiri. akubawo ineso umboni ndili nawo ndikukupaseni ma nbr ndibupasani
Ndi ayawo akumapanga zimenezo
Adzapezeka ndi mneneri wabodza
Babo asapesa ndi zoonadi ineso zinadichitiki ndili ndi umbone ose moti ndinabesa ndalama
Chonde abale anga, chinsinsi choti ukhale ndi moyo ochita bwino ndi chimondzi chokha "KUCHIRIMIKA, KAPENA KUTI, KUGWIRA NTCHITO NDI MPHANVU ZAKO".
akuba avutatu mmmm
😢😢😢😢😢😢
Mmmm kma abale mulungu alowelelepo
@MuhaShaibu
Ай бұрын
Amankhala anthu akundende awa ma prisoners ...akaidi
😢😢
Mavuto 😢😢😢😢😢
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Kuchita kudziwikilatu kuti wakuba uyu mmmm zokamba zake mmmm Mulungu akuyendereni muyaluke komwe muliko
amalawi kupusa anthu ali kundende kale milako ichoka kuti ali ku chichili phulizoni
Mulungu amukatha munthu ameneyo ndithu mmmm😢😢😢😢
Mauwo ngati nyapala, koma kumalawi eeeee mbola zokhazokha.
@emiliaumali8360
Ай бұрын
Ndi emweyo😅😅😅
@unarinematshomo2841
Ай бұрын
@@emiliaumali8360 kkkkk koma iwe usanditseketse.