TULANI PANSI UDINDO

Yathu Music Official

Пікірлер: 114

  • @user-dn5sf3md5t
    @user-dn5sf3md5t2 ай бұрын

    KOMATU WABAYA MWANA WELL DONE APSE NTIMA ZENIZENI GALU KWABASI CHAKWERA ANLONJEZAYEKHA ATULEPANSI UDINDO EYAAAAAAA GALU KWABASI NDI BWEREZASO CHAKWERA NDI GALU MBUZI YA MANU PANSI

  • @marryphili5419
    @marryphili54192 ай бұрын

    More 🔥🔥 ndimomwemo basi ananenadi

  • @CalistoZidanna-kj2st
    @CalistoZidanna-kj2st10 ай бұрын

    Yes !!!this is good music and iyeyo akuyenela ayivere b4 3 hours

  • @ibrahimatibu8784
    @ibrahimatibu8784 Жыл бұрын

    Akulu wakulu aku malawi koma kuba katundu wa anthu ovutikanso chakwera ndi mwana sakuziwa kathu bola Peter mutharika uja kusiyana ndi izi mbuzizi

  • @JohnThomas-fo8jb
    @JohnThomas-fo8jb Жыл бұрын

    Koma munthu waimba bwino uyu, kip it up, osamaopa pa chilungamo

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io10 күн бұрын

    Yomweyo kuyipatsa Moto Chakwerayo abowoke mmimba sazawinaso galu wakupha Mpheketsela zake Zamuwonongela Mbili

  • @josephncekane4567
    @josephncekane4567 Жыл бұрын

    He sang the best ever song with sense n strong messege. I'm sorry to say this but this government they all Mbuzi I repeat they all Mbuzi, they have not even single feeling of willing to save the people of Malawi

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d3 ай бұрын

    Koma angatule panopa sakugona kufu funa njila yoti adzabele ma voti koma Muthu mmm ayi ndithu m,busa wa satana

  • @stevinmuhone877
    @stevinmuhone877 Жыл бұрын

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💃💃💃💃 vuto lake anthu awa sizikuwakhunza or tingayankhure motani mmmmmmmmm

  • @IshmaelKamwana-sv6bo
    @IshmaelKamwana-sv6bo8 ай бұрын

    This is nice songs agalu amenewa tatopha nawo

  • @user-qe2lz7mx7u
    @user-qe2lz7mx7u3 ай бұрын

    Man muyimbenso lilikuti ziko yalucias bandana kapena life

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel25419 ай бұрын

    Nyimboyi ili bwino kwambiri 100% ndipo a Malawi pakufunikanso osaopa, osagona tulo ndikuzunzika chifukwa cha magulu ena a wanthu azinyengo, akuba, ozikonda ndi akupha

  • @user-td5yb3cw7u
    @user-td5yb3cw7u Жыл бұрын

    Lulululu malawi wanga akumbuse ndithu amati azasiya udindo

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282Күн бұрын

    Nice song 👍

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 Жыл бұрын

    Tiope ndaninso!!!!Chilima ananenakale #OSAOPA.

  • @lamulatusaiti7581
    @lamulatusaiti7581 Жыл бұрын

    Waimba nyimbo imeneyi mulungu amusogolele ndipo aimbeso nyimbo ina yoposa pamenepa ... Mbuzi zonsezi zimve zenizeni zeni

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi6 күн бұрын

    I'm feeling sorry for people who are in Malawi things are not good on the ground tingotchona mu Capetown

  • @user-qm1qb2jp4s
    @user-qm1qb2jp4s3 ай бұрын

    Chakwera and his mcp dictatorship tonse alliance must go

  • @ayandajack6019
    @ayandajack6019 Жыл бұрын

    Mmmmmmm muli uthenga munyimbomu I respect u bro .

  • @IbrahimDailes
    @IbrahimDailes9 ай бұрын

    Yaar nice musice osamuda zinthu Mene zilili

  • @PatriciaMbewe-xn7ke
    @PatriciaMbewe-xn7ke11 күн бұрын

    Ndaimvera mobwerezabwereza😂

  • @MourinhoJabur
    @MourinhoJabur8 күн бұрын

    💥💥💥💥💥 chilungamo

  • @fridaygonela
    @fridaygonela9 күн бұрын

    IZI ndizoona waimba zoona titsatile sadick Mia ndi achilima

  • @hamidaakimu4188
    @hamidaakimu4188 Жыл бұрын

    Zomvesa chisoni momwe anthu akuvutikira ndi njala, ambuye chitanipo kathu zithu sizili bwino

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y7 күн бұрын

    Good Messnge Chakwela you mast go

  • @enerstntakhala4679
    @enerstntakhala4679 Жыл бұрын

    Ndithyole dance koma oimba uyu anaganiza

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw6 күн бұрын

    Anatule udindowo simuli gondolosi mumpandomo

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q28 күн бұрын

    Kkkkkkk iwe wayimba bwino wava ndipo usaope ayi pitiriza man

  • @rasulmaulidi2224
    @rasulmaulidi22244 ай бұрын

    well done boys..

  • @preciouseInussah-lh6oz
    @preciouseInussah-lh6oz9 ай бұрын

    Ipatse moto

  • @ShukuranAMadu
    @ShukuranAMadu3 күн бұрын

    Zachabe kwabasi pa Malawi ndi president chakwera

  • @phillipkapata3790
    @phillipkapata3790 Жыл бұрын

    Kkkkk ndipo ikuvinika guys🤣🤣🤣🤣

  • @user-oc8xu5co8y
    @user-oc8xu5co8y6 ай бұрын

    mwatiimirira kumuuza m,busa onyengayo komaameneyo amaziwakuti azamwarira

  • @angellasamuel8186
    @angellasamuel8186 Жыл бұрын

    Koma guys alusonu tamati fikisilani mauthengo ndipo musamaope akufuna azitiopseza akapolowa mphenvu dyera Ku nthiko

  • @gizzykondwani865
    @gizzykondwani86510 күн бұрын

    Mwaphatu sound makani

  • @chimwemwe2
    @chimwemwe2 Жыл бұрын

    They should not be intimidating you because its the people that gave them power and thy are now abusing the power by mistreating the same people that gave them power. Keep speaking for the voiceless brother 🙏🙏🙏🙏🙏 I love it❤️

  • @Rose-tr6pn
    @Rose-tr6pn3 ай бұрын

    Ukuyimba bwino kom upange chako tune, ukuba luso la Billy ndiy akusaka mpakana akuthila dzigwe before aweek

  • @IsakyIsak
    @IsakyIsakАй бұрын

    Nyimbo yayimbiwda bwino zedi

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk Жыл бұрын

    Powerful!!!! Very nice Song

  • @VeronicaMarten
    @VeronicaMarten9 ай бұрын

    Muiponye palipose averebe

  • @AnusaNkhoma
    @AnusaNkhoma11 сағат бұрын

    100% boy

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 Жыл бұрын

    Ngakhale akukusaka big koma unaimba boo yes

  • @lamulatusaiti7581
    @lamulatusaiti7581 Жыл бұрын

    Tinasukusula pano amalawife. Makapewa akuona ngati dziko la Malawi ndi la agogo awo kapena la makolo awo, totopa nazo izi

  • @HelenMachanya-ip7zv
    @HelenMachanya-ip7zv9 ай бұрын

    Nyimboyi si ya Billy kaya anayimba ndindan.....akusiyana mawu

  • @imuranmkwanda9669
    @imuranmkwanda9669 Жыл бұрын

    Very nice song and it has come at a right place and right time this time around not in 2002🔥🔥🔥🔥

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet3 күн бұрын

    Apo wayiska sum iyo

  • @tingoalex6478
    @tingoalex6478 Жыл бұрын

    Very nice song keep up asakuopseze ai

  • @moyo77777
    @moyo77777 Жыл бұрын

    Nice music brother aziva

  • @user-qm1qb2jp4s
    @user-qm1qb2jp4s3 ай бұрын

    Good music with full of msg tonse did nothing but taking malawi to bagamoyo😢

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Жыл бұрын

    Odi ndivine ine💃💃💃💃💃💃

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 Жыл бұрын

    WaaaaaaaaaWoooooooooo zuka malawi atule pansi udindo

  • @kennethkaunda3636
    @kennethkaunda3636 Жыл бұрын

    Msembe Yanga izakhala apule Kwa Yahweh

  • @lamulatusaiti7581
    @lamulatusaiti7581 Жыл бұрын

    Mbuzi zenizeni zogona kunja ........ Mabongwe

  • @martinjames5639
    @martinjames5639 Жыл бұрын

    Sadalakwitse kuimba nyimbo iyi Zili bho

  • @user-yo6ql5co1f
    @user-yo6ql5co1f4 ай бұрын

    Ipase moto bgy

  • @luciascharles4345
    @luciascharles4345 Жыл бұрын

    Nice one big up

  • @user-ic4qi7yy5l
    @user-ic4qi7yy5l11 ай бұрын

    Koma zongo paikana izi kuti aziti nyimbo iyi waimba ndi Billy kaunda pomwe wina wangotenga instrument ya billy yagalatiya koma voice yaleka naso Billy akaimba mau amaveka ngat alindichifine koma awa ati ayesere zawakanikaso!!

  • @davidlinerevelation3427
    @davidlinerevelation342711 ай бұрын

    I cried after listening to the song

  • @NankafumbweJames-cw7vu
    @NankafumbweJames-cw7vu10 ай бұрын

    Nyimbo ya mphavu ngati iyi imachedwa pati

  • @user-ye8tt9tu4t
    @user-ye8tt9tu4t Жыл бұрын

    Nyimboiyi sanayimbendibilekaunda komasosanayimbebwino

  • @kaisimaidankota9023
    @kaisimaidankota9023 Жыл бұрын

    Anakwera bwino kkkkk azaona zotsatira

  • @mphatsoyakobe1557
    @mphatsoyakobe1557 Жыл бұрын

    Ili Mwala eeeeee km ndiye wabayatu iweyo ukufunika kukupasa inayake bas

  • @grantmphamba6772
    @grantmphamba6772 Жыл бұрын

    Mr hanifa Nanu wosangoyamikira bwanji tikunven nyimboyi ili boh komanso ndizachidziwikile Kuti si Billy Kaunda yi

  • @lamulatusaiti7581
    @lamulatusaiti7581 Жыл бұрын

    He is best musician in Malawi

  • @hassanmussa5205
    @hassanmussa5205 Жыл бұрын

    Amayichotsa pa chanel pawo aja amaona ngat alinayo okha, nice hit

  • @neemahkapatamoyo9563

    @neemahkapatamoyo9563

    Жыл бұрын

    Kkkkkk Koma ndimposooo agwa nayo

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole3 ай бұрын

    Bravo❤❤❤

  • @bizwickmbwindinga9751
    @bizwickmbwindinga9751 Жыл бұрын

    Yomweo waitha kuwakumbusa agaluwa ailtikwana kwambili

  • @user-el8to1te3l
    @user-el8to1te3l3 ай бұрын

    Mumantha inuyo

  • @bilalikamwendo1629
    @bilalikamwendo1629 Жыл бұрын

    Odiiiiii ndijaze ine 💃💃💃💃💃💃💃💕💓💓💓💓 Chakwela atule pasi udindo waulephela komaso akadulidwe m.jando kut adziganiza dzabwino🤐

  • @user-bh7ns3rq1v
    @user-bh7ns3rq1v3 ай бұрын

    Zilli boh atule basi zamuvuta!

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumani11 күн бұрын

    apano mutuala udindo

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Жыл бұрын

    The original song is massive

  • @robertnkhoma5776
    @robertnkhoma5776 Жыл бұрын

    Dandaulo limveke😭😭

  • @lamulatusaiti7581
    @lamulatusaiti7581 Жыл бұрын

    Ndikupezekaso kuti fertiliser kundulisaso mbuzi zimenezi sukufuna ziphe mtundu wa amalawi

  • @happycow1227
    @happycow1227 Жыл бұрын

    KUSWA KUSWA

  • @shadrecknamvula4381
    @shadrecknamvula4381 Жыл бұрын

    Much respect guys

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 Жыл бұрын

    Umatha ayise ndikanakuziwa ndika naku pangira order pa Mukuru 1000 rands

  • @user-ye8tt9tu4t
    @user-ye8tt9tu4t Жыл бұрын

    Waipitsambili yabilekaunda

  • @user-ye8tt9tu4t
    @user-ye8tt9tu4t Жыл бұрын

    Waipitsambili yabilekaunda 6:39

  • @user-bs5fk5rd2n
    @user-bs5fk5rd2n10 ай бұрын

    Nice song 5:48

  • @noahtsamdoka1172
    @noahtsamdoka1172 Жыл бұрын

    Bola amva basi chakukhosi chatiphwa ife ndipo nyimbo ikumveka mwauzimuzimu kuli kulira Kwa amphawi 🤐🤐🤐🤐🤐🤐

  • @lamulatusaiti7581
    @lamulatusaiti7581 Жыл бұрын

    Inu zoona chimanga kugula anthu pa mpaka k 25 000 thumba limodz chimanga chomwe chimagudwa k 4000 kapena k 5000

  • @mzaminphili8550
    @mzaminphili8550 Жыл бұрын

    Unaitha udzi bwela bwela.

  • @adini2919
    @adini2919 Жыл бұрын

    Very nice song 🌟

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus11 күн бұрын

    Bola akanalonjeza kut tidzamudule mutu akakana kupanga resign Km mutuwo tikanadula ? 😅😅😅😅 MCP WOYEEE😅

  • @africulturetv6498
    @africulturetv6498 Жыл бұрын

    True cry

  • @gifomusik8241
    @gifomusik8241 Жыл бұрын

    This voice must be junior k

  • @ibrahimatibu8784
    @ibrahimatibu8784 Жыл бұрын

    I like the song

  • @alihibrahim
    @alihibrahim Жыл бұрын

    Obviously

  • @StainGondwe-bq1cg
    @StainGondwe-bq1cg Жыл бұрын

    Nice

  • @bilalikamwendo1629
    @bilalikamwendo1629 Жыл бұрын

    Iiiiiii muthuyu waimba bwino kwambili Bola asamusake namabwalayu kut amphe pajatu chipqni ichi chilibe chison ndikupha athu Ndikusavinidwa kwachakwela pamenepo amusaka

  • @mlezanyirenda2815
    @mlezanyirenda2815 Жыл бұрын

    Good song

  • @user-nd4gh1fi5q
    @user-nd4gh1fi5q4 ай бұрын

    🎉🎉🎉🎉

  • @stewartgodfrey2336
    @stewartgodfrey2336 Жыл бұрын

    mbudzi idzi

  • @thomasshabalala7999
    @thomasshabalala7999 Жыл бұрын

    Is true

  • @omarcharlie5247

    @omarcharlie5247

    Жыл бұрын

    Zoona atule basi mwayitha man mix yanu

  • @jagudanicolas5436
    @jagudanicolas5436 Жыл бұрын

    Or chakwerayo wa ikondaxo atule pansi basi

  • @user-zv1so2pd7u
    @user-zv1so2pd7u11 ай бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂💯

  • @patsalama1028
    @patsalama1028 Жыл бұрын

    God hv mercy

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 Жыл бұрын

    Kod uchitsiluwamtunduwanji munthu ukulephelakulamulilabwino dziko ndikumangipitiliza kuwonongadziko ? Kapena kusavinidwa chakwela

  • @susanmbewe5109

    @susanmbewe5109

    Жыл бұрын

    zilibwino heavy atule ndithu chindele chomene

  • @idahmbungo4223

    @idahmbungo4223

    Жыл бұрын

    Nice song keep it up 👌👌👌

  • @lameckchiwaya2976
    @lameckchiwaya2976 Жыл бұрын

    Cosoma ikupeza aise (copyright)