BAKILI MULUZI TV 21 JUNE 2024 IYI NDI MBIRI YA MANGANYA

Ойын-сауық

Пікірлер: 130

  • @user-gr2vr6yw8b
    @user-gr2vr6yw8b8 күн бұрын

    Izi zilibe ntchito musiyeni nzanu pano ndi VP wa dziko lathu la malawi ❤❤❤❤

  • @ThomsonMusowa
    @ThomsonMusowa8 күн бұрын

    Akuluakulu izi sizabodza zinachitikadi ndithu izi sizalelo zinaulusidwa kalekale

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l8 күн бұрын

    Mwalowa kolakwika, ndiwe galu mbuzi chitsiru.... Kape manganya ndi munthu wabwino kwambiri ngati nfikusintha, asintha pano koma we have hope kuti he will continue with chilima vision

  • @alicksonmakata7544
    @alicksonmakata75447 күн бұрын

    Inu muyenera kudziwa kuti M U ndi vice president wa Malawi China Mulungu ali mbali yake mbili yake mukhoza kukamba ife tilibe nayo ntchito ife tingokupemphani kuti mudzipempherera kuti Mulungu apitilize kutidalitsa ndi kutiteteza tilifunire dziko lathu zabwino osati zaumphawi zosauka chifukwa ndi ziwanda.

  • @MemoryMbalat

    @MemoryMbalat

    7 күн бұрын

    Ndiponso

  • @EdythGloryNamponya
    @EdythGloryNamponya8 күн бұрын

    Komatu mungoona kumutsutsa uyu...manganya ndi birimankhwe ohoooo

  • @TaitasMakombe-ql4rr
    @TaitasMakombe-ql4rr8 күн бұрын

    Umafuna asankhe iweyo mbuli ngati iwe kumangoipitsa azanu bas

  • @AlinafePililani
    @AlinafePililani8 күн бұрын

    Zanzi Mwayamba nsanjetu tikutulukani..

  • @JustinLipipa

    @JustinLipipa

    8 күн бұрын

    Ndiyakale angoibweleza😂😂😂😂😂

  • @harrispheleni2205
    @harrispheleni22057 күн бұрын

    Ineyo l always say akuluwa amatenga ndalama Kwa APM and target yake ndi campaign ya DPP check all his videos palibe chomwe anakambako Cha DPP choipa as if a DPP ndima saints. Pakatipa wanyoza chilima atamwalira kuyamba kuyamikira, lero waipa manganya. Za ndalama anagawana a DPP za COVID sakamba, za chisale sakamba, mombera university sakamba uona akujama ya nankhumwa hater uyu mxiew😮

  • @AlufeyoBanda-cv2we
    @AlufeyoBanda-cv2we7 күн бұрын

    Kkkk koma ma reporter ena kubwera ati mbiri koma kuli kudzayalutsana kkk

  • @user-ol1hf7ru1v
    @user-ol1hf7ru1v7 күн бұрын

    Nkhaniyi ndi ntchito wapatsidwa munthuyu sizikugwilizana ata pan'ono kulakwa kumeneko aaa kale simumanena bwanji

  • @kingzack8999

    @kingzack8999

    4 күн бұрын

    Nkhani ndi yale iyi

  • @FelixKazembe-wi5zb
    @FelixKazembe-wi5zb7 күн бұрын

    Komaso iwe usamakhale ndisanje pola moto wava wawonjezano ndale zako ".. zinthu zina muziyamikilako eeee mwatani bambo inu ayi chitani manyazi😂😂😂

  • @amosnyongo6565
    @amosnyongo65658 күн бұрын

    Best TV ever

  • @yosefemichael7588
    @yosefemichael75887 күн бұрын

    Zabodza zimenezo Zinali kuti kale lonse zaziii

  • @CalistoLinoSobrinhoSobrinho
    @CalistoLinoSobrinhoSobrinho8 күн бұрын

    Wazidziwa lero tinaonaona kale 3 years ago

  • @user-oy1yk3hg9k
    @user-oy1yk3hg9k8 күн бұрын

    Kma ndy atigazazira ma sisterz athutu kkkk

  • @josejoaolamissone4195
    @josejoaolamissone41958 күн бұрын

    Video iyi ndi yakale zediii ndipo tinayiwalanso zoti kunali video imeneyi

  • @BlessingsBanda-hk3hp
    @BlessingsBanda-hk3hp17 сағат бұрын

    Ada awawa amatha continue bro kkkkkkk

  • @SakinaModi-pf9co
    @SakinaModi-pf9co7 күн бұрын

    Maphuzilowo sanakwane

  • @christophergibson72
    @christophergibson726 күн бұрын

    Chitsiru garu usamatisokoneze wava

  • @khaleedsaidi6232
    @khaleedsaidi62328 күн бұрын

    Koma iweyo ndi katundu bale ❤😂

  • @Jermah51kennias
    @Jermah51kennias8 күн бұрын

    Aaaaah iwe uzipanga zako wamva ife tonse tima mpanga follow

  • @MemoryMbalat
    @MemoryMbalat7 күн бұрын

    Tingoti kudziko lapansi kulibe wagwilo aliyense alindidzake

  • @DINAHMCHUNU
    @DINAHMCHUNU6 күн бұрын

    Ife timakukondan uncle,,🎉🎉🎉

  • @MasterJailos-kv5sd
    @MasterJailos-kv5sd7 күн бұрын

    Nkhani anayangura asanasangidwe ndiye inu chikukupweteka chani

  • @YusiraFaheem
    @YusiraFaheem8 күн бұрын

    Izi tinazivela kale kale boss

  • @ThandieMushali-gi7js
    @ThandieMushali-gi7jsКүн бұрын

    Ing'alule😂😅

  • @DANGOman-ev4fs
    @DANGOman-ev4fs7 күн бұрын

    Akut aone ngat kometa bwino😂😂😂

  • @maggiekuyere6401
    @maggiekuyere64017 күн бұрын

    Mukapsa

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl8 күн бұрын

    Guy's tizimuopa mulungu

  • @deanmossiwa1415
    @deanmossiwa14152 күн бұрын

    Iyiyi mbiri ya manganya kapna mulandu wa manganya?😅... Ndimayembekeza kumva nkhan zilongosokatu kuti ndimudziwe kut ndindan iyeyu

  • @Donnexbatumeo
    @Donnexbatumeo6 күн бұрын

    Komatu ya Gladys Phiri yi ndi yoona, koma poti enanu munali ana, basi ziletsani.

  • @albertkwizombe988
    @albertkwizombe9887 күн бұрын

    Lero ndi vice president

  • @user-di8hq3dl9o
    @user-di8hq3dl9o8 күн бұрын

    Zakalekale mzanu wapita zilibe ntchito zimenezo ngati ndi umphawi zakuvutani bambo

  • @nkhwaziaeros1845
    @nkhwaziaeros18457 күн бұрын

    Manganya uja waipa lero??? Lol umbuli basi a malawi. Nkona amalawi ali osauka. Why didn’t you bring all this bs when he was appointed by Chilima to be his vice president?? Education/civic education is very important.

  • @FrankKadangwe
    @FrankKadangwe7 күн бұрын

    This voice ikundikaikitsa

  • @user-hc9hc3dk5o
    @user-hc9hc3dk5oКүн бұрын

    Koma guys kung'alula kwa bwanji uku😂

  • @PatriciaemilyMpokwe
    @PatriciaemilyMpokwe8 күн бұрын

    Ndipo izi mukuti titani nazo mmm wasowa chonena iwe

  • @user-dx4zu1wv4q
    @user-dx4zu1wv4q8 күн бұрын

    Timakunyadila man kwambiri

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire7 күн бұрын

    Mmmmmh mmmmh!🤔🤣🤣🤣🤣🤣oyamwidwa chokodzera ooo akhare president lero 🤣🤣🤣🤣☠️😷

  • @user-xi7bo8jx8h
    @user-xi7bo8jx8h8 күн бұрын

    Best TV

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga17818 күн бұрын

    Greatest liar I have ever seen is Bakili Muluzi tv .

  • @AmulatDenis
    @AmulatDenis6 күн бұрын

    Enanu ndi alendo pa Chanel chimenechi ndiye u uth wanuwo musatinyase ife timapanga follow

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn8 күн бұрын

    Lero ndie mapolopangada osusa bakili tv ndie achulukatu lero iiiii,tv iyi simanamatu samatumiza nkhani zopanda umboni uyu

  • @EstherKamphale-yq8dm
    @EstherKamphale-yq8dm8 күн бұрын

    Za ziiii kuti zimveke bwanji. Still ndi vice president wa dziko LA Malawi basi. Muchira koma mochedwa

  • @RodwellLayford

    @RodwellLayford

    7 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂

  • @ChisomoNyimbo
    @ChisomoNyimbo7 күн бұрын

    Inu ndi osokoneza ndthu palipose kubweretsa negative altitude mxiew

  • @estherkambewa7791
    @estherkambewa77918 күн бұрын

    Nsanje a Malawi uyu amangidwe Sizisintha kanthu he is still the VP Dziko likamva kuti litani?

  • @chitenjepatriq3338

    @chitenjepatriq3338

    8 күн бұрын

    Video ndiya kalekale

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9dКүн бұрын

    Following

  • @AmulatDenis
    @AmulatDenis6 күн бұрын

    Manganya ndi wamdede

  • @WatsonAmon
    @WatsonAmon7 күн бұрын

    Ndangowona kuti akulu awawa amadana ndi manganya

  • @KennyMathank
    @KennyMathank8 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 koma nkhani zili umu eeeeeh bakili muluzi tv ndi wakulu

  • @sandramkaligida1163
    @sandramkaligida11636 күн бұрын

    Enafe tikamati uyu wa bakili muluzi tv ndi chitsiru mumati tsutsa Nanga zoona akanenene za chokodzela cha munthu pano

  • @levisonchagona7232
    @levisonchagona72328 күн бұрын

    Mumafukula nkhan

  • @Mphatso-jr1fb
    @Mphatso-jr1fb7 күн бұрын

    😂😂😂😂 Ndizakale izi uyu ndiamene bwela nazo lero mobgokumbutsana

  • @user-yg9rs7tp2x
    @user-yg9rs7tp2x8 күн бұрын

    Izi ndizakalekale worakwa ndi wotuzayo

  • @mikechingamba3088
    @mikechingamba30886 күн бұрын

    Everyone has a dark side of history but we don't need to start digging such as if the woman has chosen to bring it to the public.. Nkhani zanutu pango'nopang'ono zayamba kumamveka ngati zija za m;maboma pa MBC.

  • @alicechigamba1751
    @alicechigamba17517 күн бұрын

    Mbili yonyasa anthu a seventhday ndiachisawawa I can tell

  • @RABSONSIKELO
    @RABSONSIKELO7 күн бұрын

    Inunso tiuzen mbili yanu ...

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano4736 күн бұрын

    Bakili Muluzi channel adayotulutsa video some years back go and check Bakili muluzi platform you may realised he produced this video two to three-years ago l started watch some years ago so don't be upset.

  • @davidjames679
    @davidjames6795 күн бұрын

    nonse imakubhowan tulukan ndipo musamamvele

  • @HusseinMachemba
    @HusseinMachemba6 күн бұрын

    Guyz vedio iyi ndi yakale kwambili nde chonde musaluse ayi

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg8 күн бұрын

    😂😂😂😂 chakwera ndi wamisala kusiya nsonda kusiya dausi kusiya uladi Musa

  • @masterkachingwe7448

    @masterkachingwe7448

    8 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @EstherZintambira-sq3yy

    @EstherZintambira-sq3yy

    8 күн бұрын

    Aaaah oduka mutu achna uladi kuononga chani

  • @amosbula1249
    @amosbula12498 күн бұрын

    Perekani mbiri yabwinobwino ngati munthu woti mumatiuza nkhani pano. Zinazo ndi zosafunikira

  • @jumbradoone4164

    @jumbradoone4164

    8 күн бұрын

    Ndi mbiri ya Munthu-tu iyi, palibe cholakwika.

  • @TheresaKuluwemba

    @TheresaKuluwemba

    8 күн бұрын

    Izinso ndizofunika

  • @isaacchipatala1618
    @isaacchipatala16186 күн бұрын

    Nonse amene mukhulupilila izi ndinu opusa

  • @user-cb5me8wp1k

    @user-cb5me8wp1k

    6 күн бұрын

    Iweyo nd opusa cos iz anatulutsa kare kare ndipo ndizoona iwe umangomudziwa manganese lero fuse athu akhala naye

  • @danielkhinguirossejuliasse6106
    @danielkhinguirossejuliasse61068 күн бұрын

    tatiuzani za south africa mavoti aribwanji?

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b7 күн бұрын

    Manganya uhule ankapanga pomwe anali mphawi sono ndi u vice aupedzawo

  • @CatherineDesire

    @CatherineDesire

    7 күн бұрын

    🤣🤣🤣🤣akupangabe wachake tsasiya komaso d,zoti angakonze dzinthu ndakaika bola Bon kalindo kkkk

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev8 күн бұрын

    Pamtumbopako galu wa munthu lwe satana ukutipatsa mbili kapena zoyipa za manga nya..

  • @YoungKhakhizo

    @YoungKhakhizo

    8 күн бұрын

    Naweso panyero pako garu

  • @walesbanda4959
    @walesbanda49598 күн бұрын

    Kkkkkkk koma akulu inu bodza simudzasiya

  • @BatisonKalonga
    @BatisonKalonga7 күн бұрын

    Uyu amangokamba zomwe akuganiza niwabodza

  • @ancientnkhata1137

    @ancientnkhata1137

    6 күн бұрын

    Ndipo nchabodza osati masewera .

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata11376 күн бұрын

    Nthawi yomwe waipa ?

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire7 күн бұрын

    Utsilu basi a chimanganya Kuyaluks basi A K A 47

  • @yamikanichibungwe2315
    @yamikanichibungwe23158 күн бұрын

    Ukufusa kuti titani?

  • @tituskamsesa7274
    @tituskamsesa72745 күн бұрын

    Does this Bakili Muluzi T V have anything good to say in Malawi? Or they only see the wrongs

  • @MovableSoundSquad

    @MovableSoundSquad

    2 күн бұрын

    What about you do you have anything good to say?

  • @bridgetmasache5685
    @bridgetmasache56858 күн бұрын

    Koma nde mmakamba zabodza mkazi wamanganya nanga ndiameneyo mm

  • @TheresaKuluwemba

    @TheresaKuluwemba

    8 күн бұрын

    Mkazi wake ndindani nanga? Ndinuyo kapena???😅

  • @pusikanimwasinga6044
    @pusikanimwasinga60447 күн бұрын

    Eish

  • @isaacchipatala1618
    @isaacchipatala16186 күн бұрын

    Akulu mwatani kodi

  • @NemayiBandah
    @NemayiBandah7 күн бұрын

    Nenani zanu tinve

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w8 күн бұрын

    Auzen mn

  • @jamesgama5489
    @jamesgama54898 күн бұрын

    Ayi zikomo

  • @GladysMasasa
    @GladysMasasa8 күн бұрын

    Zauchitsimluzi izi mukadayankhula mmbuyomo pano mwachedwa mzanuyu mumuvule msamuvule pano ndi presedent basiiiiii wapitaaa!

  • @GladysMasasa

    @GladysMasasa

    8 күн бұрын

    Tisamatero Anthufe tiziopa mulungu.

  • @user-nr6po2cp4r

    @user-nr6po2cp4r

    8 күн бұрын

    Izi adayakhura kale kumene silero ai iwe nde oduka mawaya sukudziwa kathu

  • @TheresaKuluwemba

    @TheresaKuluwemba

    8 күн бұрын

    Video ndiyakalekaletu iyi, mwina inuyo bakili muluzi tv simumamutsatayi mmbuyomu, koma ndiyakale kwambiri

  • @Omwale
    @Omwale8 күн бұрын

    kkkkkk koma manga

  • @MrsMachewere
    @MrsMachewere8 күн бұрын

    Mbuzi ya Munthu Amangidwe basi

  • @ZIONEAMILU-oo6og
    @ZIONEAMILU-oo6og7 күн бұрын

    Zapakathawi 😂😂😂😂

  • @timothyntonga8256
    @timothyntonga82567 күн бұрын

    Kkkkkk

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x8 күн бұрын

    😂😂Koma malawi 😂😂😂😂 president etii😂😂😂

  • @MasterJailos-kv5sd
    @MasterJailos-kv5sd7 күн бұрын

    Usafooka

  • @user-rh3un3hv3j
    @user-rh3un3hv3j8 күн бұрын

    Kkkkkkkkk km ukooooo

  • @CharlesMateya
    @CharlesMateya7 күн бұрын

    Kkkkkkkk zamalisechezez

  • @RhodneyBwa3
    @RhodneyBwa38 күн бұрын

    Mmmmmmmmm km abale.

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata11376 күн бұрын

    Awa abakili Muluzi tawatulukira kuti ndi aDPP

  • @HusseinMachemba

    @HusseinMachemba

    6 күн бұрын

    Koma akulu muzifufuza kayetu video iyi ndi three years ago

  • @adzonzicomedy

    @adzonzicomedy

    6 күн бұрын

    video iyi ndiyakalekale

  • @adzonzicomedy

    @adzonzicomedy

    6 күн бұрын

    we love bakili muluzi TV

  • @gamammwenye
    @gamammwenye7 күн бұрын

    malawians we have to accept that in every person there is a dark side, aliyense ali ndi mbiri.... Bakili muluzi tv has just narrated what happened, but that does not imply kuti the current Manganya is a bad person. kutukwana mkozi ndi mwini wa channel chimenechi, sizingathandize.

  • @modestamhango611

    @modestamhango611

    7 күн бұрын

    Zoona

  • @MalumboMtaba
    @MalumboMtaba8 күн бұрын

    Zaziiiii

  • @MaryMakina-nh2eo
    @MaryMakina-nh2eo7 күн бұрын

    Kkkkkkkkkk

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon37567 күн бұрын

    Kkkkkkkkkkkkkkkkk

  • @RichardKumwenda-mz8qi
    @RichardKumwenda-mz8qi8 күн бұрын

    Kkkkkkkkk koma

  • @SwidiqLameck
    @SwidiqLameck7 күн бұрын

    Kt zimveke bwa

  • @Hudhayf

    @Hudhayf

    7 күн бұрын

    Kaya naonso awa

  • @CeniaMayeni
    @CeniaMayeni8 күн бұрын

    Uyu ndi bakili muluzi TV wa fake

  • @shukranhabibuh9928

    @shukranhabibuh9928

    6 күн бұрын

    Ndipo live sakumveka zenizeni

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo62518 күн бұрын

    Zakale kale izi lol

  • @thomsonchauluka
    @thomsonchauluka8 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @MemoryMbepula
    @MemoryMbepula5 күн бұрын

    Nonsense

  • @AlinafeNdalama
    @AlinafeNdalama7 күн бұрын

    A crook in deed

Келесі