Ka Manganya Kakuona Ngati Kasewela Game Yovuta | Koma Ndikamunthu Koipa | Watelo Khad
#manganya #chilima #malawi #trending #news #viral
Жүктеу.....
Пікірлер: 218
@user-gs7wc3nx3q5 күн бұрын
Amene akususa ni wa amcp.amumasure.boni karindo chakwera nisataniki wamupha chirima
@JustinLipipa6 күн бұрын
Mmmmm in politics palibe True friend, si game yonkhulupilirana
@user-nf3ik3ff6y6 күн бұрын
Good Messnge my brother
@webstermbewe83956 күн бұрын
I think it's wise to pick somebody from utm other than MCP
@BENSONRANGWANI6 күн бұрын
Chakwela wamupha chilima manganya amupha chakwela tiyeni tiziyang ana mezi ikubwelayi
@FelixBoss-yn9pe
5 күн бұрын
Ndagwirizananawe
@KellyHart-pi4hd
5 күн бұрын
Ineso ndikugwilizana na we
@sharonicier001
4 күн бұрын
You're right brother 🤔🤔coz manganya anachenjera kwambiri 🤷🤷🤷
@DivineMercy-df2pu5 күн бұрын
Manganya his cup will b full soon ... imagine MPs shouting m'boma ilo when we have just barried Chilima n I'm sure those MPs are not Utm ,UDF or DPP it can only b MCP . Your down fall is near.
@VisianMw6 күн бұрын
Inu nde mangoyankhula zilungamo zokhazokha boss 💪💪💪
@actuarialscience22836 күн бұрын
We have to pray for Malawi to be free from MCP and "satanic politics".
@Luxemaven8686
5 күн бұрын
Facts!!!
@emmammatsa1284
19 сағат бұрын
I am not a politician neither belong to any party, in Malawi every party belongs to someone besides MCP which is the party for everyone but lacks good leadership, MCP leaders now are weak, wicked and have tainted the party.
@IssaKapalamula5 күн бұрын
Mwauponda, mumaganiza kuti asankha wa mcp cholinga mudzetse mpungwe pungwe pakati pa utm ndi mcp 😂😂😂😂
@RabiaOsman-wy1ud5 күн бұрын
Interview ya b.banda ndi manga'anya inanena yokha, he couldn't answer zogwira mtima, I was hoping to hear zogwira mtima. Koma palibe ananena. Anali atamugwiritsa buns . It makes sense now.
@FelixBoss-yn9pe5 күн бұрын
Ndipo manganya ngochenjeladi mix nka school kuposa anzawowo nde ndizovuta wina akhonza kuona madzi angazime
@user-kh4qp1ji1i6 күн бұрын
Iweyo ndi katundu olemera kwambiri. Your brain is sharp!
Nkhani ndi ya tonse Alliance asakha bwino, game imeneyiyi tiyimalize isathele panjila aaaaaaaaaaaaaa inu tiyimalize basi UTM WOYEEEEEEEEE osadanda timalize gameyi
@ellahmwams8315 күн бұрын
😂😂😂 dziko lalowa chisawawa ili
@HappyAbyssinianCat-xt2bm3 күн бұрын
Km akulu inu ndi munthu oganiza mumalankhura chilungamo ndpo simumaopa munthu ambuye akuze malire amoyo wanu timakunyadiran❤
@user-kl9id7kx3m6 күн бұрын
Enough of the hate, bro! Get a life and try to be objective in your criticism of the leaders back here. You can't just be sitting there saying things that have no proof for the sake of the views. The leaders are not without flaws because they're only human but make sure your criticism has to be founded on truth and constructive enough.
@fazeerchisamia43716 күн бұрын
Lero wabwera ndimbola heavy,vuto mukupanga za personal kwambiri kusiya 20 million people.Sopano umafuna asankhe ndani. Akuti kovuta munthu kundipha ineyo kkkkk childish
I used to see sense in your videos but today I have been let down 😢
@bwenguking3894
6 күн бұрын
He is on illegal drugs
@gladyschisomo4324
5 күн бұрын
😂😂😂😂😂@@bwenguking3894
@SheenahMwalabu-iz3pr
5 күн бұрын
Ndipo nane wandifoola sanaiganizile shape and wandikhumudwitsa. Manganya zapaimfa ya Chilima sikumukhudza, tiyeni timufunile zabwino mulungu salakwitsa atha kudzagwetsa mcp ndiwanzeru plus alibe 2koloko
@thokozanichabwera5658
5 күн бұрын
Choosing manganya is the only right thing because ndi vice president wa UTM. Lamulo limati VP replacement should be done within 7 days so there is nothing to wrong to be considered as a traitor
Ambuye kumwamba ko ife ana anu imvani kulira kwathu.. Kuno ku malawi zinthu sizili bwino
@MadaKanene5 күн бұрын
Perfect 👌 said
@lytonmaseko45345 күн бұрын
Yaaa manganya is clever really clever ka kalulu
@user-nv3rf7bl7r4 күн бұрын
Nsanje iyi musamayese ku joni kuno ndikwanu kutchuka ndiza ziiiii
@FatsaniNgolomi-xn4mo5 күн бұрын
Kape iwe Ufuna dziko ikhale lopanda president kudikila wina awole kae? Bingu Anamwalira jb anatenga malo ake bwanj simunalankhule
@MaryChavula-jz3di5 күн бұрын
Abwana olo mwana akudziwa kuti zachitika pamenepo ndi mbola olo munve kayankhidwe ka mai kaliyati utm ikudziwa kale kuti ndi mbola yachitika apa abwana amalawife ndi mbuzi timawombela m"manja oti atimphe
@AchinaKellz5 күн бұрын
Charlie Chaplin at war comedy
@marvinhanke55206 күн бұрын
Si zonse zomwe mumayankhula ndi zanzeru.
@ethusiasts4 күн бұрын
kamunthu koyipa😢😢
@SolokingChimzy-yt7dj5 күн бұрын
U r very brave bro
@user-rt7ye1gt8x4 күн бұрын
So u mean chilima sanali ochenjera...imfa sithawika....I think wina aliyese akapita kunja ndkuziwa chizungu amazitenga wanzeru..ngati muli ndi zeru kuno munachoka chifukwa chani...anthu anzeru amalemera konkuno Boss
@brianntonya53195 күн бұрын
Muli ndivuto mwene
@TopoTopo-bm4vw5 күн бұрын
Big up
@MustaphaCassim6 күн бұрын
We know that inu mukusapota chakwera ndiinu a mcp are u sure chakwera ndi manganya the lead malawi chakwera mbuli osaona manganya ndi wamadrama lero ndalama yanu ndi k10,000 to $1 next year $1 k50 000
@Jele-mk9ip6 күн бұрын
But its the construction. There is no basis of accusing Michael Usi.
@Jele-mk9ip
6 күн бұрын
Sorry l wanted to say constitution.
@AlinafeMulesoКүн бұрын
Koma imfa yachilima ndi yosaiwalika ngakhale a MCP akufuna kuifuta nsanga chilima anafa ngati galu munthu oti anali olemekezeka koma kumupanga chinchija anthu inu ndi amfiti tikat kuipa ndiye kut tachepesa
@MorrisMapiri5 күн бұрын
Good lucky to chakwera for he has been warned.
@giftdulamkalenga73445 күн бұрын
Amalawi Kusanva 😢😢😢
@user-xi6sr7kd7p4 күн бұрын
😂😂😂 fact ka munthu kameneka
@AminAbbass-xc4qk6 күн бұрын
🎉🎉🎉👏👏👏👏
@NACNAC-fg5yd5 күн бұрын
Mumafuna akanasankha inuyo? Kuchita kuvalira jacket ndi tie kulankhula zopusaZo? Kodi akuluwa alibe zochita Zina za nzeru than kulankhula za ndale?
@wittinessnkhokwe5 күн бұрын
Malawi akulamulidwa ndima Gamba ( mbava) kkkk
@user-nu3zg6pr1l5 күн бұрын
God bless Malawi
@ulemujumbe85015 күн бұрын
😂😂😂kkkkk amn"gamba pompo mkokonda ndalama Ka judasi
@mavmsusa13105 күн бұрын
Bwana, munayika sing’enge ndi sing’enge to surround you. Kkkkkkk
@WezzieNyasulu-cp7hy6 күн бұрын
This is funny kma experiencing someones life on other people so we can talk this is wrong
@Cathy-oc7vd5 күн бұрын
Panu ndi pakamwa pompo... tachitani ng'oooo.. siyani mabodza awa
Пікірлер: 218
Amene akususa ni wa amcp.amumasure.boni karindo chakwera nisataniki wamupha chirima
Mmmmm in politics palibe True friend, si game yonkhulupilirana
Good Messnge my brother
I think it's wise to pick somebody from utm other than MCP
Chakwela wamupha chilima manganya amupha chakwela tiyeni tiziyang ana mezi ikubwelayi
@FelixBoss-yn9pe
5 күн бұрын
Ndagwirizananawe
@KellyHart-pi4hd
5 күн бұрын
Ineso ndikugwilizana na we
@sharonicier001
4 күн бұрын
You're right brother 🤔🤔coz manganya anachenjera kwambiri 🤷🤷🤷
Manganya his cup will b full soon ... imagine MPs shouting m'boma ilo when we have just barried Chilima n I'm sure those MPs are not Utm ,UDF or DPP it can only b MCP . Your down fall is near.
Inu nde mangoyankhula zilungamo zokhazokha boss 💪💪💪
We have to pray for Malawi to be free from MCP and "satanic politics".
@Luxemaven8686
5 күн бұрын
Facts!!!
@emmammatsa1284
19 сағат бұрын
I am not a politician neither belong to any party, in Malawi every party belongs to someone besides MCP which is the party for everyone but lacks good leadership, MCP leaders now are weak, wicked and have tainted the party.
Mwauponda, mumaganiza kuti asankha wa mcp cholinga mudzetse mpungwe pungwe pakati pa utm ndi mcp 😂😂😂😂
Interview ya b.banda ndi manga'anya inanena yokha, he couldn't answer zogwira mtima, I was hoping to hear zogwira mtima. Koma palibe ananena. Anali atamugwiritsa buns . It makes sense now.
Ndipo manganya ngochenjeladi mix nka school kuposa anzawowo nde ndizovuta wina akhonza kuona madzi angazime
Iweyo ndi katundu olemera kwambiri. Your brain is sharp!
Potengela ndimmene wafela chilima muja olo akasankhidwa wina aliyese kupatula manganya bwezi tikuti wapha ndiyeyo
@yohanestainly6340
5 күн бұрын
Zoona. Ndipo pena chilungamo chokakamiza sichikhala chilungamo
@Cathy-oc7vd
5 күн бұрын
Ndipo zoona
@WezzieChimuzi-ek7bk
3 күн бұрын
Mawu abro
@augrinngunga8031
22 сағат бұрын
Mbuli iwe
Zimene mwayankhulazo nde ndi zambola musiyeni manganya alamulire imeneyo ndi nsanje
@AchinaKellz
5 күн бұрын
Kape iwe mfiti
@harrisbanda5891
5 күн бұрын
Alamulile ng'ona zimzake not amalawife, he betrayed his President chilima, even the vp itself doesn't suit him, udindo ukumukana😂😂😂😂😂
Manganya ndiwa mcp ever since....ka spy
Your massage is very straight thank you my brother
Manganya ndi oipa kwambiri waphesa chilima pofuna kukhala vice President
l Congolese from USA🇺🇸 but so sad guys in Malawi muchenchele
You don't know Michael Usi, Jelous sikuthandiza bwera ku Malawi iwe
Respect mr man
A Malawi chonde tiyeni tizuke chakwela watopesa, uyu satanic president
Thanks for your video
Mmmm Mulungu tu a kuona ndipo mmm munthu oipa mmm amamusungira kampeni kumphasa kuti afe chirima, mwanxi wake ubwexera ndinthu mmm
Chakwera watenga slow poison coz of frustration
Manganya ndi pulendeti chakwela akafa mezi ikubwelayi
@Emmanuelisraelsimbi
5 күн бұрын
Kkkk
@PetroJack
4 күн бұрын
Ndipo amupha Chakwera ndiwokhwima amupondesa kasapa Chakwera
Nkhani ndi ya tonse Alliance asakha bwino, game imeneyiyi tiyimalize isathele panjila aaaaaaaaaaaaaa inu tiyimalize basi UTM WOYEEEEEEEEE osadanda timalize gameyi
😂😂😂 dziko lalowa chisawawa ili
Km akulu inu ndi munthu oganiza mumalankhura chilungamo ndpo simumaopa munthu ambuye akuze malire amoyo wanu timakunyadiran❤
Enough of the hate, bro! Get a life and try to be objective in your criticism of the leaders back here. You can't just be sitting there saying things that have no proof for the sake of the views. The leaders are not without flaws because they're only human but make sure your criticism has to be founded on truth and constructive enough.
Lero wabwera ndimbola heavy,vuto mukupanga za personal kwambiri kusiya 20 million people.Sopano umafuna asankhe ndani. Akuti kovuta munthu kundipha ineyo kkkkk childish
@user-kx3en7hy5j
5 күн бұрын
Panyapako
Kkkkk zoona bwana ka manganya ndikafiti 😂😂😂
Only God will save us from the misery
Pitani muzangolima musamangokhalila zolandila. Timagwirantchito kuti zinthuzipezeke, ndiye pamenepo uzingotayapo nthawi, ulankhule usalankhule koma manganya akulamulilabe, chakwela akulamulilabe.
Koma mukuti chan aaa zopanda mutu zokhazokha inu mukutani kutenga dzikoli mutilamulire bwanj😂😂😂😂😂😂
Mmmm inayo ndi nsanje akulu inu, manganya walakwa chani? Komanso mukamatchula dzina la munthu mudzikhala ndi ulemu, osamakhala ngati ndinu olenga munthu
@DennisDonework
5 күн бұрын
Koma manganya nduichenjela atha kumulanga chakwera kumuonesa athakubweza imfa yachilima dekhani muone
Kaduku,wudzafa choncho ndiye kuti iweso ukupatsidwaso ndalama, ukunama chilichose chimene chili ndi SIGNAL chikhoza kupangidwa hack,iwe akupeza!!!!
Asakha bwino TSOPANO TIONERENO GAME APAPANO YANGOYAMBA KUMENE
Chakwera naye mulungu akuwona sakhalitsa mulungu atilangira😢😢
@doreenkaliati3166
5 күн бұрын
Amen atilangire
@user-nv3rf7bl7r
4 күн бұрын
Zaziii mulungu wake utiyo osamusewelesa mulungu
Nanuso ndinu achitsilu
Wopani Mulungu a chimwene kutukwana uku mukafa muzapita kuti? A siyeni anzanu ndi nthawi yawo. Cha nzeru mwachitapo inu ndi chiti?
Iwe ndiye umangoying'alula uli phe umakwana
Chintchito chilipo pa home pano tiyeni tizingong'ana mwina zinalembedwa kale
Miya was not a malawian to run for a president....yes manga is a sellout....just look at the jacket mbuzi yakumuzi 😂😂
Ukunena zoona bloh chakwera inso asamale
Ndiye titani kuti tikonze? Osamangotokota apa kumapeto no solution, kumpusa kumeneko tikunva kuwawa ife. Tokotani mukamaliza tipaseni solution zizitikanika tokha. Inunso ngati mMalawi okhuzidwa muzitenganso gawo mma solutions wooo.
I used to see sense in your videos but today I have been let down 😢
@bwenguking3894
6 күн бұрын
He is on illegal drugs
@gladyschisomo4324
5 күн бұрын
😂😂😂😂😂@@bwenguking3894
@SheenahMwalabu-iz3pr
5 күн бұрын
Ndipo nane wandifoola sanaiganizile shape and wandikhumudwitsa. Manganya zapaimfa ya Chilima sikumukhudza, tiyeni timufunile zabwino mulungu salakwitsa atha kudzagwetsa mcp ndiwanzeru plus alibe 2koloko
@thokozanichabwera5658
5 күн бұрын
Choosing manganya is the only right thing because ndi vice president wa UTM. Lamulo limati VP replacement should be done within 7 days so there is nothing to wrong to be considered as a traitor
Big man continue to give us information
mr khad always with you. may Allah guide you
Keep it up My brother ♥️♥️
Ndioipadi ndinthira kuwiri, wampeni kumphasa ndipo uyu imfa yachilima akudziwapo kanthu km iwowa siamuyaya zidzaululika ndipo adzafanso
Ana a look sharp like inu ndamene mungatukule dziko come to Malawi
@leviefeston7626
3 күн бұрын
Mufuna akamuphe ku Malawi
Chonena ife tilibe adziwe ndimulungu 🙏🙏🙏🙏
Machende ao bwanji kupha anthu like that😢😢😢
Aliyese wokhala vp bwezi tikuti wamupha chirima ndi iyeyo,ukunenazo tabweretsa tangible evidence
Very very true bro
Well said
Ambuye kumwamba ko ife ana anu imvani kulira kwathu.. Kuno ku malawi zinthu sizili bwino
Perfect 👌 said
Yaaa manganya is clever really clever ka kalulu
Nsanje iyi musamayese ku joni kuno ndikwanu kutchuka ndiza ziiiii
Kape iwe Ufuna dziko ikhale lopanda president kudikila wina awole kae? Bingu Anamwalira jb anatenga malo ake bwanj simunalankhule
Abwana olo mwana akudziwa kuti zachitika pamenepo ndi mbola olo munve kayankhidwe ka mai kaliyati utm ikudziwa kale kuti ndi mbola yachitika apa abwana amalawife ndi mbuzi timawombela m"manja oti atimphe
Charlie Chaplin at war comedy
Si zonse zomwe mumayankhula ndi zanzeru.
kamunthu koyipa😢😢
U r very brave bro
So u mean chilima sanali ochenjera...imfa sithawika....I think wina aliyese akapita kunja ndkuziwa chizungu amazitenga wanzeru..ngati muli ndi zeru kuno munachoka chifukwa chani...anthu anzeru amalemera konkuno Boss
Muli ndivuto mwene
Big up
We know that inu mukusapota chakwera ndiinu a mcp are u sure chakwera ndi manganya the lead malawi chakwera mbuli osaona manganya ndi wamadrama lero ndalama yanu ndi k10,000 to $1 next year $1 k50 000
But its the construction. There is no basis of accusing Michael Usi.
@Jele-mk9ip
6 күн бұрын
Sorry l wanted to say constitution.
Koma imfa yachilima ndi yosaiwalika ngakhale a MCP akufuna kuifuta nsanga chilima anafa ngati galu munthu oti anali olemekezeka koma kumupanga chinchija anthu inu ndi amfiti tikat kuipa ndiye kut tachepesa
Good lucky to chakwera for he has been warned.
Amalawi Kusanva 😢😢😢
😂😂😂 fact ka munthu kameneka
🎉🎉🎉👏👏👏👏
Mumafuna akanasankha inuyo? Kuchita kuvalira jacket ndi tie kulankhula zopusaZo? Kodi akuluwa alibe zochita Zina za nzeru than kulankhula za ndale?
Malawi akulamulidwa ndima Gamba ( mbava) kkkk
God bless Malawi
😂😂😂kkkkk amn"gamba pompo mkokonda ndalama Ka judasi
Bwana, munayika sing’enge ndi sing’enge to surround you. Kkkkkkk
This is funny kma experiencing someones life on other people so we can talk this is wrong
Panu ndi pakamwa pompo... tachitani ng'oooo.. siyani mabodza awa
Wabodza iwe ....... vuto lokhara kuja ndikumakolopa umalakhura zopanda zeru ngati izi
Khad ndi dolo!
Never give up
Woyipa ndiwe galu
Mwati kamung'amba?😂😂😂😂😂
@Betty-fe9ql
6 күн бұрын
😅😅😅
yes yes Comedy indeed
Zoonadi brother
What's the ways forward,, now?
Exactly
Uyu ndi mbuzi heavy zomwe amakhulupilira anthu zopanda umboni wogwilika
away ndiozungulila mutu ndachisilu
Odya naye mbare imodzi ndye amakupereka
Mumatha boss inuyo ndi one
Zovuta kwambili,malawi Sali bwino
One thing that I know is politics is evil only God knows about Malawian
Inuyo ndi ambuli amwene kulimbana ndima devo anzanu.bwanji?
Kkkkk 😂😂😂😂 aaaa iweso uli molalo bwanji kkkkk 😂😂😂😂😂