Ka Manganya Kakuona Ngati Kasewela Game Yovuta | Koma Ndikamunthu Koipa | Watelo Khad

#manganya #chilima #malawi #trending #news #viral

Пікірлер: 218

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q5 күн бұрын

    Amene akususa ni wa amcp.amumasure.boni karindo chakwera nisataniki wamupha chirima

  • @JustinLipipa
    @JustinLipipa6 күн бұрын

    Mmmmm in politics palibe True friend, si game yonkhulupilirana

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y6 күн бұрын

    Good Messnge my brother

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe83956 күн бұрын

    I think it's wise to pick somebody from utm other than MCP

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI6 күн бұрын

    Chakwela wamupha chilima manganya amupha chakwela tiyeni tiziyang ana mezi ikubwelayi

  • @FelixBoss-yn9pe

    @FelixBoss-yn9pe

    5 күн бұрын

    Ndagwirizananawe

  • @KellyHart-pi4hd

    @KellyHart-pi4hd

    5 күн бұрын

    Ineso ndikugwilizana na we

  • @sharonicier001

    @sharonicier001

    4 күн бұрын

    You're right brother 🤔🤔coz manganya anachenjera kwambiri 🤷🤷🤷

  • @DivineMercy-df2pu
    @DivineMercy-df2pu5 күн бұрын

    Manganya his cup will b full soon ... imagine MPs shouting m'boma ilo when we have just barried Chilima n I'm sure those MPs are not Utm ,UDF or DPP it can only b MCP . Your down fall is near.

  • @VisianMw
    @VisianMw6 күн бұрын

    Inu nde mangoyankhula zilungamo zokhazokha boss 💪💪💪

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience22836 күн бұрын

    We have to pray for Malawi to be free from MCP and "satanic politics".

  • @Luxemaven8686

    @Luxemaven8686

    5 күн бұрын

    Facts!!!

  • @emmammatsa1284

    @emmammatsa1284

    19 сағат бұрын

    I am not a politician neither belong to any party, in Malawi every party belongs to someone besides MCP which is the party for everyone but lacks good leadership, MCP leaders now are weak, wicked and have tainted the party.

  • @IssaKapalamula
    @IssaKapalamula5 күн бұрын

    Mwauponda, mumaganiza kuti asankha wa mcp cholinga mudzetse mpungwe pungwe pakati pa utm ndi mcp 😂😂😂😂

  • @RabiaOsman-wy1ud
    @RabiaOsman-wy1ud5 күн бұрын

    Interview ya b.banda ndi manga'anya inanena yokha, he couldn't answer zogwira mtima, I was hoping to hear zogwira mtima. Koma palibe ananena. Anali atamugwiritsa buns . It makes sense now.

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe5 күн бұрын

    Ndipo manganya ngochenjeladi mix nka school kuposa anzawowo nde ndizovuta wina akhonza kuona madzi angazime

  • @user-kh4qp1ji1i
    @user-kh4qp1ji1i6 күн бұрын

    Iweyo ndi katundu olemera kwambiri. Your brain is sharp!

  • @IsaacsCapetown-hu8wh
    @IsaacsCapetown-hu8wh6 күн бұрын

    Potengela ndimmene wafela chilima muja olo akasankhidwa wina aliyese kupatula manganya bwezi tikuti wapha ndiyeyo

  • @yohanestainly6340

    @yohanestainly6340

    5 күн бұрын

    Zoona. Ndipo pena chilungamo chokakamiza sichikhala chilungamo

  • @Cathy-oc7vd

    @Cathy-oc7vd

    5 күн бұрын

    Ndipo zoona

  • @WezzieChimuzi-ek7bk

    @WezzieChimuzi-ek7bk

    3 күн бұрын

    Mawu abro

  • @augrinngunga8031

    @augrinngunga8031

    22 сағат бұрын

    Mbuli iwe

  • @TracyMutesi
    @TracyMutesi6 күн бұрын

    Zimene mwayankhulazo nde ndi zambola musiyeni manganya alamulire imeneyo ndi nsanje

  • @AchinaKellz

    @AchinaKellz

    5 күн бұрын

    Kape iwe mfiti

  • @harrisbanda5891

    @harrisbanda5891

    5 күн бұрын

    Alamulile ng'ona zimzake not amalawife, he betrayed his President chilima, even the vp itself doesn't suit him, udindo ukumukana😂😂😂😂😂

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox28655 күн бұрын

    Manganya ndiwa mcp ever since....ka spy

  • @user-sh5wq4uf6r
    @user-sh5wq4uf6r5 күн бұрын

    Your massage is very straight thank you my brother

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e5 күн бұрын

    Manganya ndi oipa kwambiri waphesa chilima pofuna kukhala vice President

  • @OlgaChirezi-qt1pg
    @OlgaChirezi-qt1pg5 күн бұрын

    l Congolese from USA🇺🇸 but so sad guys in Malawi muchenchele

  • @user-sh2hr2cw8b
    @user-sh2hr2cw8b5 күн бұрын

    You don't know Michael Usi, Jelous sikuthandiza bwera ku Malawi iwe

  • @user-gg6uh2wo4x
    @user-gg6uh2wo4x3 күн бұрын

    Respect mr man

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h5 күн бұрын

    A Malawi chonde tiyeni tizuke chakwela watopesa, uyu satanic president

  • @ElonBlack1999
    @ElonBlack19996 күн бұрын

    Thanks for your video

  • @ChisomoKandikole
    @ChisomoKandikole6 күн бұрын

    Mmmm Mulungu tu a kuona ndipo mmm munthu oipa mmm amamusungira kampeni kumphasa kuti afe chirima, mwanxi wake ubwexera ndinthu mmm

  • @patricksamson4852
    @patricksamson48525 күн бұрын

    Chakwera watenga slow poison coz of frustration

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI6 күн бұрын

    Manganya ndi pulendeti chakwela akafa mezi ikubwelayi

  • @Emmanuelisraelsimbi

    @Emmanuelisraelsimbi

    5 күн бұрын

    Kkkk

  • @PetroJack

    @PetroJack

    4 күн бұрын

    Ndipo amupha Chakwera ndiwokhwima amupondesa kasapa Chakwera

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly6 күн бұрын

    Nkhani ndi ya tonse Alliance asakha bwino, game imeneyiyi tiyimalize isathele panjila aaaaaaaaaaaaaa inu tiyimalize basi UTM WOYEEEEEEEEE osadanda timalize gameyi

  • @ellahmwams831
    @ellahmwams8315 күн бұрын

    😂😂😂 dziko lalowa chisawawa ili

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm3 күн бұрын

    Km akulu inu ndi munthu oganiza mumalankhura chilungamo ndpo simumaopa munthu ambuye akuze malire amoyo wanu timakunyadiran❤

  • @user-kl9id7kx3m
    @user-kl9id7kx3m6 күн бұрын

    Enough of the hate, bro! Get a life and try to be objective in your criticism of the leaders back here. You can't just be sitting there saying things that have no proof for the sake of the views. The leaders are not without flaws because they're only human but make sure your criticism has to be founded on truth and constructive enough.

  • @fazeerchisamia4371
    @fazeerchisamia43716 күн бұрын

    Lero wabwera ndimbola heavy,vuto mukupanga za personal kwambiri kusiya 20 million people.Sopano umafuna asankhe ndani. Akuti kovuta munthu kundipha ineyo kkkkk childish

  • @user-kx3en7hy5j

    @user-kx3en7hy5j

    5 күн бұрын

    Panyapako

  • @CharlesmakveliNyirenda
    @CharlesmakveliNyirenda6 күн бұрын

    Kkkkk zoona bwana ka manganya ndikafiti 😂😂😂

  • @SangwaniKawawa
    @SangwaniKawawa5 күн бұрын

    Only God will save us from the misery

  • @danielsaidi7230
    @danielsaidi72305 күн бұрын

    Pitani muzangolima musamangokhalila zolandila. Timagwirantchito kuti zinthuzipezeke, ndiye pamenepo uzingotayapo nthawi, ulankhule usalankhule koma manganya akulamulilabe, chakwela akulamulilabe.

  • @PempheroKaunde
    @PempheroKaunde2 күн бұрын

    Koma mukuti chan aaa zopanda mutu zokhazokha inu mukutani kutenga dzikoli mutilamulire bwanj😂😂😂😂😂😂

  • @jacksonmaliro
    @jacksonmaliro6 күн бұрын

    Mmmm inayo ndi nsanje akulu inu, manganya walakwa chani? Komanso mukamatchula dzina la munthu mudzikhala ndi ulemu, osamakhala ngati ndinu olenga munthu

  • @DennisDonework

    @DennisDonework

    5 күн бұрын

    Koma manganya nduichenjela atha kumulanga chakwera kumuonesa athakubweza imfa yachilima dekhani muone

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko5 күн бұрын

    Kaduku,wudzafa choncho ndiye kuti iweso ukupatsidwaso ndalama, ukunama chilichose chimene chili ndi SIGNAL chikhoza kupangidwa hack,iwe akupeza!!!!

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly6 күн бұрын

    Asakha bwino TSOPANO TIONERENO GAME APAPANO YANGOYAMBA KUMENE

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika67845 күн бұрын

    Chakwera naye mulungu akuwona sakhalitsa mulungu atilangira😢😢

  • @doreenkaliati3166

    @doreenkaliati3166

    5 күн бұрын

    Amen atilangire

  • @user-nv3rf7bl7r

    @user-nv3rf7bl7r

    4 күн бұрын

    Zaziii mulungu wake utiyo osamusewelesa mulungu

  • @AlinafePililani
    @AlinafePililani6 күн бұрын

    Nanuso ndinu achitsilu

  • @nancynyirenda6774
    @nancynyirenda67745 күн бұрын

    Wopani Mulungu a chimwene kutukwana uku mukafa muzapita kuti? A siyeni anzanu ndi nthawi yawo. Cha nzeru mwachitapo inu ndi chiti?

  • @CholapitsaSamson
    @CholapitsaSamson5 күн бұрын

    Iwe ndiye umangoying'alula uli phe umakwana

  • @IsaacsCapetown-hu8wh
    @IsaacsCapetown-hu8wh6 күн бұрын

    Chintchito chilipo pa home pano tiyeni tizingong'ana mwina zinalembedwa kale

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox28655 күн бұрын

    Miya was not a malawian to run for a president....yes manga is a sellout....just look at the jacket mbuzi yakumuzi 😂😂

  • @johnman4619
    @johnman46196 күн бұрын

    Ukunena zoona bloh chakwera inso asamale

  • @JTUPHIRI
    @JTUPHIRI4 күн бұрын

    Ndiye titani kuti tikonze? Osamangotokota apa kumapeto no solution, kumpusa kumeneko tikunva kuwawa ife. Tokotani mukamaliza tipaseni solution zizitikanika tokha. Inunso ngati mMalawi okhuzidwa muzitenganso gawo mma solutions wooo.

  • @thokozanichabwera5658
    @thokozanichabwera56586 күн бұрын

    I used to see sense in your videos but today I have been let down 😢

  • @bwenguking3894

    @bwenguking3894

    6 күн бұрын

    He is on illegal drugs

  • @gladyschisomo4324

    @gladyschisomo4324

    5 күн бұрын

    😂😂😂😂😂​@@bwenguking3894

  • @SheenahMwalabu-iz3pr

    @SheenahMwalabu-iz3pr

    5 күн бұрын

    Ndipo nane wandifoola sanaiganizile shape and wandikhumudwitsa. Manganya zapaimfa ya Chilima sikumukhudza, tiyeni timufunile zabwino mulungu salakwitsa atha kudzagwetsa mcp ndiwanzeru plus alibe 2koloko

  • @thokozanichabwera5658

    @thokozanichabwera5658

    5 күн бұрын

    Choosing manganya is the only right thing because ndi vice president wa UTM. Lamulo limati VP replacement should be done within 7 days so there is nothing to wrong to be considered as a traitor

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMulesoКүн бұрын

    Big man continue to give us information

  • @MussaJohn-gt8ep
    @MussaJohn-gt8ep4 күн бұрын

    mr khad always with you. may Allah guide you

  • @user-cs5dh3yl8w
    @user-cs5dh3yl8w5 күн бұрын

    Keep it up My brother ♥️♥️

  • @ElizabethTrapens
    @ElizabethTrapens4 күн бұрын

    Ndioipadi ndinthira kuwiri, wampeni kumphasa ndipo uyu imfa yachilima akudziwapo kanthu km iwowa siamuyaya zidzaululika ndipo adzafanso

  • @samdiverson9733
    @samdiverson97335 күн бұрын

    Ana a look sharp like inu ndamene mungatukule dziko come to Malawi

  • @leviefeston7626

    @leviefeston7626

    3 күн бұрын

    Mufuna akamuphe ku Malawi

  • @HappyAutumnTrees-cd9ye
    @HappyAutumnTrees-cd9ye4 күн бұрын

    Chonena ife tilibe adziwe ndimulungu 🙏🙏🙏🙏

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg4 күн бұрын

    Machende ao bwanji kupha anthu like that😢😢😢

  • @jonathankumalasa
    @jonathankumalasa5 күн бұрын

    Aliyese wokhala vp bwezi tikuti wamupha chirima ndi iyeyo,ukunenazo tabweretsa tangible evidence

  • @DoraTembo
    @DoraTembo5 күн бұрын

    Very very true bro

  • @ChifuniroChintengo
    @ChifuniroChintengo2 күн бұрын

    Well said

  • @violetpotani
    @violetpotani4 күн бұрын

    Ambuye kumwamba ko ife ana anu imvani kulira kwathu.. Kuno ku malawi zinthu sizili bwino

  • @MadaKanene
    @MadaKanene5 күн бұрын

    Perfect 👌 said

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko45345 күн бұрын

    Yaaa manganya is clever really clever ka kalulu

  • @user-nv3rf7bl7r
    @user-nv3rf7bl7r4 күн бұрын

    Nsanje iyi musamayese ku joni kuno ndikwanu kutchuka ndiza ziiiii

  • @FatsaniNgolomi-xn4mo
    @FatsaniNgolomi-xn4mo5 күн бұрын

    Kape iwe Ufuna dziko ikhale lopanda president kudikila wina awole kae? Bingu Anamwalira jb anatenga malo ake bwanj simunalankhule

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3di5 күн бұрын

    Abwana olo mwana akudziwa kuti zachitika pamenepo ndi mbola olo munve kayankhidwe ka mai kaliyati utm ikudziwa kale kuti ndi mbola yachitika apa abwana amalawife ndi mbuzi timawombela m"manja oti atimphe

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz5 күн бұрын

    Charlie Chaplin at war comedy

  • @marvinhanke5520
    @marvinhanke55206 күн бұрын

    Si zonse zomwe mumayankhula ndi zanzeru.

  • @ethusiasts
    @ethusiasts4 күн бұрын

    kamunthu koyipa😢😢

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj5 күн бұрын

    U r very brave bro

  • @user-rt7ye1gt8x
    @user-rt7ye1gt8x4 күн бұрын

    So u mean chilima sanali ochenjera...imfa sithawika....I think wina aliyese akapita kunja ndkuziwa chizungu amazitenga wanzeru..ngati muli ndi zeru kuno munachoka chifukwa chani...anthu anzeru amalemera konkuno Boss

  • @brianntonya5319
    @brianntonya53195 күн бұрын

    Muli ndivuto mwene

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw5 күн бұрын

    Big up

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim6 күн бұрын

    We know that inu mukusapota chakwera ndiinu a mcp are u sure chakwera ndi manganya the lead malawi chakwera mbuli osaona manganya ndi wamadrama lero ndalama yanu ndi k10,000 to $1 next year $1 k50 000

  • @Jele-mk9ip
    @Jele-mk9ip6 күн бұрын

    But its the construction. There is no basis of accusing Michael Usi.

  • @Jele-mk9ip

    @Jele-mk9ip

    6 күн бұрын

    Sorry l wanted to say constitution.

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMulesoКүн бұрын

    Koma imfa yachilima ndi yosaiwalika ngakhale a MCP akufuna kuifuta nsanga chilima anafa ngati galu munthu oti anali olemekezeka koma kumupanga chinchija anthu inu ndi amfiti tikat kuipa ndiye kut tachepesa

  • @MorrisMapiri
    @MorrisMapiri5 күн бұрын

    Good lucky to chakwera for he has been warned.

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga73445 күн бұрын

    Amalawi Kusanva 😢😢😢

  • @user-xi6sr7kd7p
    @user-xi6sr7kd7p4 күн бұрын

    😂😂😂 fact ka munthu kameneka

  • @AminAbbass-xc4qk
    @AminAbbass-xc4qk6 күн бұрын

    🎉🎉🎉👏👏👏👏

  • @NACNAC-fg5yd
    @NACNAC-fg5yd5 күн бұрын

    Mumafuna akanasankha inuyo? Kuchita kuvalira jacket ndi tie kulankhula zopusaZo? Kodi akuluwa alibe zochita Zina za nzeru than kulankhula za ndale?

  • @wittinessnkhokwe
    @wittinessnkhokwe5 күн бұрын

    Malawi akulamulidwa ndima Gamba ( mbava) kkkk

  • @user-nu3zg6pr1l
    @user-nu3zg6pr1l5 күн бұрын

    God bless Malawi

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe85015 күн бұрын

    😂😂😂kkkkk amn"gamba pompo mkokonda ndalama Ka judasi

  • @mavmsusa1310
    @mavmsusa13105 күн бұрын

    Bwana, munayika sing’enge ndi sing’enge to surround you. Kkkkkkk

  • @WezzieNyasulu-cp7hy
    @WezzieNyasulu-cp7hy6 күн бұрын

    This is funny kma experiencing someones life on other people so we can talk this is wrong

  • @Cathy-oc7vd
    @Cathy-oc7vd5 күн бұрын

    Panu ndi pakamwa pompo... tachitani ng'oooo.. siyani mabodza awa

  • @user-dl2hs9mu2i
    @user-dl2hs9mu2i5 күн бұрын

    Wabodza iwe ....... vuto lokhara kuja ndikumakolopa umalakhura zopanda zeru ngati izi

  • @mr_bsoc
    @mr_bsoc3 күн бұрын

    Khad ndi dolo!

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo5 күн бұрын

    Never give up

  • @joshuankata6967
    @joshuankata69675 күн бұрын

    Woyipa ndiwe galu

  • @user-hw4yw7ex4j
    @user-hw4yw7ex4j6 күн бұрын

    Mwati kamung'amba?😂😂😂😂😂

  • @Betty-fe9ql

    @Betty-fe9ql

    6 күн бұрын

    😅😅😅

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz5 күн бұрын

    yes yes Comedy indeed

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe10385 күн бұрын

    Zoonadi brother

  • @user-qq3ip1od6i
    @user-qq3ip1od6i5 күн бұрын

    What's the ways forward,, now?

  • @user-vu9rt8gj3o
    @user-vu9rt8gj3o5 күн бұрын

    Exactly

  • @jonathankumalasa
    @jonathankumalasa5 күн бұрын

    Uyu ndi mbuzi heavy zomwe amakhulupilira anthu zopanda umboni wogwilika

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of6 күн бұрын

    away ndiozungulila mutu ndachisilu

  • @ChisomoKandikole
    @ChisomoKandikole6 күн бұрын

    Odya naye mbare imodzi ndye amakupereka

  • @WisdomBlack-uu7zt
    @WisdomBlack-uu7zt5 күн бұрын

    Mumatha boss inuyo ndi one

  • @LAKISSONEBINGOLOSSEMACUNHA
    @LAKISSONEBINGOLOSSEMACUNHA4 күн бұрын

    Zovuta kwambili,malawi Sali bwino

  • @Simangalisiwe
    @Simangalisiwe5 күн бұрын

    One thing that I know is politics is evil only God knows about Malawian

  • @user-wt9vb1vb5v
    @user-wt9vb1vb5v4 күн бұрын

    Inuyo ndi ambuli amwene kulimbana ndima devo anzanu.bwanji?

  • @PidoMaganga
    @PidoMaganga4 күн бұрын

    Kkkkk 😂😂😂😂 aaaa iweso uli molalo bwanji kkkkk 😂😂😂😂😂