This is true and he was warrior and may his saul rest in peace 😢😢😢😢😢😢😢. Chakwera akutinyasa. Chakwera ndiopa kwambiri ndipo akulitenga dzikori ngat ndilamake.
@sulleahmnyimbili13627 күн бұрын
Rest well SKC, thanks for the information
@patrickmacheso50628 күн бұрын
Well spoken Mr Man,, tikufuna anthu olimba mtima ngati inuyo Mr,, Mmene mukuyankhula chonchi ma Members a MCP akusakani bwana.
@AliceChipeta-pc3nb8 күн бұрын
Mzimu wachilima mmmm ndi waukali
@Kilocssreaction8 күн бұрын
Amene akudana ndi voice iyi machende ake ndichakwera manyi ake
Chilungamo ndi mwano amene ikumukhuza nkhani imeneyi audio iyi sakupuma nawo bwino akuwona ngati awanyoza koma ayi wayankhula chilungamo Zimveka bs any time chilungamo chizatuluka
@user-wb5ym2qm6y3 күн бұрын
Komaditu a Huwa Mkaka adalankhula kuti ndale za kuMalawi timapanga ndi usiku.
@babranzima81208 күн бұрын
Idalidi nyambo pama plan athuwadi😢😢
@Pangolinimw8 күн бұрын
😢😢😢😭😭😭 mcp ndi yakumpa
@nephitalychitedze21188 күн бұрын
Kusokosera pano sikuthandiza china chilichonse nkhani ndiyakuti. Ngati muli ndi umboni pitani ku Court. Sizomangosokosera zotibweretsera misozi ayi... RIP my Veep SKC
@OFG-th3st8 күн бұрын
Chippewa chija Ndichoopsa😢
@Hong_sing8 күн бұрын
Excellent 😭😭😭😭😭
@kubengovender69968 күн бұрын
We are together big man!!
@MillieMalakam6 күн бұрын
Cakwela ndiwosalakwa anavomeleza kt cilima zayimila koma nduna xakezi ndizimene zikumuzocelesa kt azipanga zoipa koma mcp must go akazizi achabecabe afiti osekelera
@KelvinPhiri7508 күн бұрын
zosakhala bwino...i do know when we will change a s a country 😭
@CharlesBanda-kv8bh8 күн бұрын
Ndiwe chitsiru amene ukutukwanawe udikire uwone cho me mulungu amanita ndizitsiru ngati iwe
@KelvinJpchimphepo-sh6nc2 күн бұрын
Umbuli wakudanawo osaziwa chimene akuchita
@SaidiMdoka-pn3zm8 күн бұрын
Mfiti yayikulu ndi Chakwela m'busa wonyenga
@FortuneAndrew-nb2im8 күн бұрын
Respected may his soul rest in peace
@reymondpetermaster56973 күн бұрын
Skc rest in peace, only God knows about your early departure.
@chitanibenito11096 күн бұрын
Mawu onse amayankhura a mcp aphelezera anthuwa ngakupha basi ngakhale zi siru za anthu ena zikubakira as if they don’t see wat is happening n it’s just only few people amene akumusokoneza president.
Vuto lanu a Malawi 🇲🇼 Kusankha kwanu kuti mumulande Boma Peter Mthalika.....wakwiya mzimu wa Bingu,Munya muzingophana shupiti....
@andrewmaluwa2713
8 күн бұрын
aaa uja adationjeza kwambili APM, nkhaza zomwe ma cadet amachita zija muona ngati tayiwala? aliyense adzafatu including APM yo, osamalakhula motumbwa, dzikoli si la amuthalika, chakwela naye 2025 akadzaluza ndekuti amalawi samufuna osati adzidzati andilanda boma
@PRECIOUSMKUTE
8 күн бұрын
Lero akutifuna okhatu. Ankatinyoza
@sokojane4015
8 күн бұрын
Zinthu zimayenda bwino only with Bingu. Munthu uja aaaa anathesa njala ndipo zinthu zambiri zimaoneka ndi maso. Bingu wa Mthalika miss him always@@PRECIOUSMKUTE
Пікірлер: 214
This is true and he was warrior and may his saul rest in peace 😢😢😢😢😢😢😢. Chakwera akutinyasa. Chakwera ndiopa kwambiri ndipo akulitenga dzikori ngat ndilamake.
Rest well SKC, thanks for the information
Well spoken Mr Man,, tikufuna anthu olimba mtima ngati inuyo Mr,, Mmene mukuyankhula chonchi ma Members a MCP akusakani bwana.
Mzimu wachilima mmmm ndi waukali
Amene akudana ndi voice iyi machende ake ndichakwera manyi ake
@user-hs6sh3xz1f
8 күн бұрын
Upole mototu koma kkkkk
@peterjailos1879
6 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@McneverMauwa
5 күн бұрын
Ndipo live brother nkhani ya straight iyi
@christophergibson72
5 күн бұрын
Naweso akowo pali chotukwanila apa? Mutul ngati chibonga
UTM ndi Malawi Tapya kusogolo ndi pansanapomwe. MHSRIP 😭😭😭
MUSIYENI CHAKWERA ABALE AKUZIWA NDI MULUNGU, R.I.P BOSS MAN CHILIMA
Incompetent leader Malawi ever hard........ Lazarus chakwera
True bigman live and direct
Muziika zinthuzi zizipanga slide, zimapangitsa munthu kuonjezela chidwi pomvetsera. Thanks for the information
@gomesavirgo3987
6 күн бұрын
That's very true, I think uli ngat ine
imfa yapweteka iyi eeeh!
@nancynkumbira1466
6 күн бұрын
Ndipo yowawa eee sinazionepo ,,i feel for the family
Chilungamo chomveka bwino kwambiri 😢😢😢
Koma eeeeeeee chîungamo kuwawa or kuli agule Pena mudzivesa chilungamu
Nice massage
Dziko tengani ili achakwela ndi anthu anu, anthu opanda chisoni, Now Mukufuna Kupha APM ndi Born Kalindo, Zonsezo tikuzidziwa
Chilima rest well ,until we meet u again
Chimenetu amaiwala, Technology,ili ponseponse,si nthawi imene anaphedwa nduna,4 zija kunalibe, technology.lero.kutelo,ungoonekela, poyela.si,izi.mabvutotu, awayamba,okha.
Munthu wanyau chakwera .my br chakwera akudziwa imfa yachilima
Chonde chonde tibweretsereni poyera zigawengazi ziyaluke
Good Messnge Chakwela you mast go
We are to gether brother
I salute u for good update only God knows, mmm malawi
@Willardpiches-ci4yi
8 күн бұрын
Ili ndi pemphero ameen
Thanks my lady 😊😊
MCP chawo palibe azakawinila kumwamba chakwerayo
Utsi sufuka popanda moto
Kumalawi kulibe fiti iyaaah 😂😂 amalakwa chani chakwera
@user-re7fo3be2z
8 күн бұрын
Do you have humanity?
MCP yatipweteka kwambili
@user-qf7jw4ho3h
8 күн бұрын
Only God knows the truth
@princedetbozsmallboy1749
8 күн бұрын
@@user-qf7jw4ho3h to know about now because it's obvious chakwera killed Chilima umbuli kapena ufiti inuso nanu aaaaaa
@SolomonNjolomole
8 күн бұрын
Criminal party mcp.
@JamesNgwaya-vz1ox
8 күн бұрын
Wapha ndi chakwera akutsutsawo ndani mbolo yake yosadulayo foolish
Ziyankhule zitsilu zozala ndimagazi kuyambila kale mpakav kale
This is reality big man
Like my dad also ananena choncho kuti kumukhulukira uku inali nyambo
💯 %true brother 😢
Amuphela Dala chilima sazawinaso 2025
Winayo masoti ngati mphaka , mr kilimora
Tienazoni,angotsola kunjira,ndipo njira sadatseke aí,inunso mutero basi sinu Mulungu aí.
Komatu Chakwerayu atafuna kukubwezelani mutha kuona zosaona
Chilungamo ndi mwano amene ikumukhuza nkhani imeneyi audio iyi sakupuma nawo bwino akuwona ngati awanyoza koma ayi wayankhula chilungamo Zimveka bs any time chilungamo chizatuluka
Komaditu a Huwa Mkaka adalankhula kuti ndale za kuMalawi timapanga ndi usiku.
Idalidi nyambo pama plan athuwadi😢😢
😢😢😢😭😭😭 mcp ndi yakumpa
Kusokosera pano sikuthandiza china chilichonse nkhani ndiyakuti. Ngati muli ndi umboni pitani ku Court. Sizomangosokosera zotibweretsera misozi ayi... RIP my Veep SKC
Chippewa chija Ndichoopsa😢
Excellent 😭😭😭😭😭
We are together big man!!
Cakwela ndiwosalakwa anavomeleza kt cilima zayimila koma nduna xakezi ndizimene zikumuzocelesa kt azipanga zoipa koma mcp must go akazizi achabecabe afiti osekelera
zosakhala bwino...i do know when we will change a s a country 😭
Ndiwe chitsiru amene ukutukwanawe udikire uwone cho me mulungu amanita ndizitsiru ngati iwe
Umbuli wakudanawo osaziwa chimene akuchita
Mfiti yayikulu ndi Chakwela m'busa wonyenga
Respected may his soul rest in peace
Skc rest in peace, only God knows about your early departure.
Mawu onse amayankhura a mcp aphelezera anthuwa ngakupha basi ngakhale zi siru za anthu ena zikubakira as if they don’t see wat is happening n it’s just only few people amene akumusokoneza president.
ndakulakwila chani fuko langa lokondeka , mtima ukuwawa bwanji😢😢😢
Bwandeeeeeeeeee!!!!!!
Kkkkkkkk koma ya 2025 tidzawone kuti ndolo ndani
Wayakhula momveka bwino2 uyu..muciyakhulo cathu
Chooona chimamasula❤❤❤❤❤
Zoona
Sizingatheke kut achakwera osaidziwa opanga nde chakwerayo
Chilima R I P
Achewa ndinu oipa kwambili
Zomvetsa chisoni dziko lapita ili💔💔
Chipani choipa ichi ever in Malawi Kma thaw yawathera next year onse amangidwa after kuluza
Komaa!eeee dzikoli
Mukadakhala anzeru sibwenzi mukungolalata pamene Malawi ali pa moto.osatenga bomalo kuti amalawi tisiye kuvutika bwanji? Tatopa inu chilungamo mukuchidziwa koma mwabisala
True
Anthu awa amalawi zigewenga zikuluzikulu, dziko lino kulisiya mumanja mwa anthu amenewa ndiye kuti tiluza anthu ambiri ofunikira mdziko muno komaso amalawife titengelepo phunziro kuti sibwino kuvotera zigewenga kapena azibusa
Akutha thobwa akuluwa
True story brother
Chakwela achoke
This is Deus Sandram's voice
For sure biggman
Chilima dzathu wa chinyamata 80s 90s 2000
MCP should go
Or azipha nayenso kukumusidikila
Rest in peace legend
Chilungamo chimapweteka😢
Only God knows the truth
Rip acle😢😢
Ndipo khaniyi ndiyoona ndinthu koma mulungu alipo
Zomvesa chison + urem akurandira ndi mutharika
Go ahead brother
Gule kwao please
Tisaweluze timusiye Mulungu akhale yekhayo aweluza pansipompano Koma tikhale manso kwawo kwantha kwasala Kwa ine ndi inu
@user-qp8kh2hj9o
8 күн бұрын
Amen
Watsala ndiwe kufa ndiwe galu 😂😂😂
Mudziwa chani chakwera khaniyi ampaka mmodzi mwa ndunazake kenako iye aziyeretse basi kuteroko muona
Koma gayz m'dziko likuchita dzinthu yhoo
Rest in peace skc
Mcp ndiyakupha
No way chakwera ali momwemo
Mlahu.akibaru
Chilichose chomwe anachita anthu amenewa chiululika nzimu wachilima ndiwoophsa
Ulemu wanu Malume osaopa kunena chilungamo
Mulungu achitile chifundo dziko lathu la Malawi.
Vuto lanu a Malawi 🇲🇼 Kusankha kwanu kuti mumulande Boma Peter Mthalika.....wakwiya mzimu wa Bingu,Munya muzingophana shupiti....
@andrewmaluwa2713
8 күн бұрын
aaa uja adationjeza kwambili APM, nkhaza zomwe ma cadet amachita zija muona ngati tayiwala? aliyense adzafatu including APM yo, osamalakhula motumbwa, dzikoli si la amuthalika, chakwela naye 2025 akadzaluza ndekuti amalawi samufuna osati adzidzati andilanda boma
@PRECIOUSMKUTE
8 күн бұрын
Lero akutifuna okhatu. Ankatinyoza
@sokojane4015
8 күн бұрын
Zinthu zimayenda bwino only with Bingu. Munthu uja aaaa anathesa njala ndipo zinthu zambiri zimaoneka ndi maso. Bingu wa Mthalika miss him always@@PRECIOUSMKUTE
Dikilan wosat kumayakhula ngat wokhoza apa. Kuyakhula maganizo anu anthu ndikumakuwombelan m'manja
@user-rz9rm4cb8x
8 күн бұрын
Achitsilu inu
@Tenjklvtcy
8 күн бұрын
Ndiponso aaaa😅
@Tenjklvtcy
8 күн бұрын
@@user-rz9rm4cb8xamakuptsani Ufa kodi
Big up sir
Chakwera ndi satana amachita kuoneka pakhope mbudzi imene ija atipweteka fitsi imeneyi asazafe garu amneyi
Only God knows 🙏🙏
Sad
RIP skc