Kuyankhula zomveka bwino ndipo zaphindu zokhazokha congratulation boss
@BinwelLukali7 күн бұрын
The DC bon kalindo the great 💪💪💪💪
@WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un7 күн бұрын
The DC akamuna okakha NDI mawaya
@JafaliAkimu-ll1bf7 күн бұрын
azibale athu amene anaphedwa ndi chakwera kuchikangawa ndi zomvesa chison kudziko lino chakwera ndi chigawenga
@MacreaChilingulo-ob9gb7 күн бұрын
Long live Boooon Kalindo !!!!! The D C ccc !!!! The Wise Guy !!! Iweyo palibenso !!
@owenmanda17417 күн бұрын
The problem with Malawi is nkhondo timawasiira anthu ochepa kumenyera ufulu,no wonder akalowa mu boma amakasakaza chuma.We all need to fight for our freedom
@AustinMangani7 күн бұрын
Mbambande Mr
@pempheroraynnoxmpesi87137 күн бұрын
Ati bon Kalindo amangidwebe😂
@harrisbanda58917 күн бұрын
Akhwakhwananda amenewa 🐊🐊🐊🐊 atitola kwambiri
@DanielChima-zl2uo7 күн бұрын
zoona Bon kalindo ngakhale kuno ku south Africa zimatikwana kwa basi zimene akupanga president
@harrisbanda58917 күн бұрын
60 years subtract 4 years yamazumzo ya chakwela
@JosephMichael-x7v7 күн бұрын
Bon kalindo our president
@ShaibMusa7 күн бұрын
My Hero..The Dc
@DYSONKUMPEREMBE6 күн бұрын
Machine bon kalindo ❤❤❤❤
@HallimaMakwinja7 күн бұрын
Zoonadi Mr Kalindo simukunama Chakwera ndi gulu lake they are mbunzi za anthu they are fools
@ChikumbutsoTsalangu7 күн бұрын
Iwo andale si bola akhutitsa mimba zawo
@GraceZumazuma6 күн бұрын
Or abadwe mwatsopano Koma mizimu ya anthu anapha ija imufafanthabe Mulungu wake uti okumba mapemphero a munthu opondeleza oipa wakupha okondela ngati ameneyo
@BeatrizUlanda-ht2th7 күн бұрын
Mumakwana Avon karindo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@AbondBolbo7 күн бұрын
Abon kuyilawilira😂😂😂
@RichardMedi7 күн бұрын
😅😅😅😅😅 Kakakakakakakakaka DC 😂 our president kkkkmwana owopsa heav😂😂😂
@TecksonKaima-dr6er7 күн бұрын
Mumakwana boss,osawanyengerera makape achina kumkuyu,zikhale ndi chakwera yemwe😙😙
THE D C BOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOON KALINDO 💪💪💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@user-ve7rx7vj1g7 күн бұрын
I agree with Kalindo..the #thinkalike
@blessingsmwale60075 күн бұрын
Izoooh Hankonnani pwiya aleleni iiwesese😂
@user-ty5zh2xi9b6 күн бұрын
Sowuna auseni agalu amenewa achakwera
@GraceZumazuma6 күн бұрын
President omvetsa chisoni chakwera ulamuliro wake ngati dzaka 100 chifukwa cha dyera
@SilverMkwatula7 күн бұрын
Bon muuzeni chakwera kuno ku mangochi asazafike tizapha tokha ndi galu
@chadreckchibwithala14937 күн бұрын
kkkk mwakumana usazindikila nokha nokha vuto mli busy pa ma phone mwayiwala kuti azanu ali pa ground . zoti peter analamula bwino mkunama matha ma albino ambiri
@EllenPhiri-xt8pt6 күн бұрын
Bon k amatha ❤
@user-le9su3mt7r7 күн бұрын
Chakwela mhuzi ya muthu
@trifoniachilunda62637 күн бұрын
Iweyo umandiwaza chifukwa umayankhula chilungamo. Palisouyu Limpopo FM NDI bakili muluzi TV anthuinu ndinu madolo❤
@TorshKadango7 күн бұрын
Iweyo ndi one
@IanChidothe7 күн бұрын
You saying the truth
@EliaMhone6 күн бұрын
Koma opposition ikalowa mu boma imasinthanso kuiwala zomwe ife amalawi tinkalira .
@GanizaniKamvazaana7 күн бұрын
Koma thawi ikubwera ndithu mlungu atiyakha ndithu mlungu wathu salephera❤
@AliceMpaso6 күн бұрын
Kkkkkk winiko samatopa mumamuseweletsa😂
@charlesmataka17007 күн бұрын
Machende awo awa
@marychavula6987 күн бұрын
Our Hero
@MarkinaJohn5 күн бұрын
The DC
@inessmsiyambiri85177 күн бұрын
Mwana oopsa kwambiri
@oskidooscar74687 күн бұрын
Koma why sakuyamkhulapo za manganya vice president ku mcp
@KennethChazama7 күн бұрын
Inetu ndi mchewa koma nyasi izii sitikukondwa Nazo ,from nathenje
@HarryYottam-ft1bo7 күн бұрын
Ulemu wanu comrade
@CollinsHala6 күн бұрын
Vuto a Malawi ife mantha
@mayesojameskatete7 күн бұрын
The D.C.
@chestermajora7 күн бұрын
awa akungolankhula Loma palibe zomwe zikuchitika.mmalo mot tipange zinthu ngat kukenya.
@hanifahmponda87117 күн бұрын
Aaaa kuba mistake kuyika MCP papando iiiiiii tinalakwitsa
@AustinMangani7 күн бұрын
Morning
@AffickChaona7 күн бұрын
The DC Bon kalindo ❤
@user-hm9nc7lz6e7 күн бұрын
Kodi cakwera akufuna anthu amuvotere 2025 afuna adzidzatani poti iye sadziwa kanthu akufuna adzapitilidze kuba conde. Cakwera usavutike amalawi sitikukufuna ngakhale pangono watilidzatu iwe watidzudza dzaka 5 ngati dzaka hundred
@rhinovaheke66147 күн бұрын
I just watch so that kalindo can make some money
@JeremiahChilenje7 күн бұрын
Dziko lamkaka ndi uchi lija pano ndi sabora ekhaekha😢😢😢😢
@AnaffSayamika-uh6vg7 күн бұрын
The DC 💥💥💥💥💥
@AndrewChitsamba6 күн бұрын
We respect fools so no need to reply... 😂😂😂😂
@user-ss9bj5eh6b7 күн бұрын
madala madala born k
@ClementChisemphele7 күн бұрын
Wamsala iwe amalawi umanenawo ndi ati? enafetu sutifuna zolandila zimene umafuna iwezo ife amene timalima tikusangalala kabwebweta ndi misala yakoyo
@PatronChanza7 күн бұрын
The dc
@user-do2cs8nf4b7 күн бұрын
Komanso boma ili manyaka eni eni koma ndlama zikuwonongedwazi ndi zabwino bwino? Mzipatala mulibe mankhwala koma ndlama zogula anthu muli nazo shame Malawi government shame Mulungu kumwambako muzimutetezera Bon kalindo kwina kuli konse angapite
@HamitonFrank7 күн бұрын
60years of independence but nothing to show
@IbrahimRaphael-z3l7 күн бұрын
💪💪💪💪
@KennethChazama7 күн бұрын
Nkhani ya ma ID muikokomeze kt apart from mcp zipani Zina taonetsetsani zomwe zikuchika mmaderamu,tabwerani kunathenje midzi ngati monga mphete village,mtsotsa, sanjiko,nyama ,kaphala ,matapira,Chatha ana osafikamo Zaka,
@AndrewChitsamba6 күн бұрын
Empty tins
@ShafieIdrissah7 күн бұрын
❤❤❤❤❤
@user-kw7wr4kq9w7 күн бұрын
Let's not be negative for everything. Peter was also useless
@yobesaikonde61667 күн бұрын
Chamba kkkkkkkkkk
@feehasaidid.r.d7 күн бұрын
Koma akamati abadwa mwasopani akuyesa kuti ndiopusa Never ever changes my mindset
Пікірлер: 115
Nanuso bwanji Joyce Banda mbuzi yamunthu chakwera mutu ngati phwala lambuzi
Born you always talk the truth ❤❤😂
Ulemu wanu
Kuyankhula zomveka bwino ndipo zaphindu zokhazokha congratulation boss
The DC bon kalindo the great 💪💪💪💪
The DC akamuna okakha NDI mawaya
azibale athu amene anaphedwa ndi chakwera kuchikangawa ndi zomvesa chison kudziko lino chakwera ndi chigawenga
Long live Boooon Kalindo !!!!! The D C ccc !!!! The Wise Guy !!! Iweyo palibenso !!
The problem with Malawi is nkhondo timawasiira anthu ochepa kumenyera ufulu,no wonder akalowa mu boma amakasakaza chuma.We all need to fight for our freedom
Mbambande Mr
Ati bon Kalindo amangidwebe😂
Akhwakhwananda amenewa 🐊🐊🐊🐊 atitola kwambiri
zoona Bon kalindo ngakhale kuno ku south Africa zimatikwana kwa basi zimene akupanga president
60 years subtract 4 years yamazumzo ya chakwela
Bon kalindo our president
My Hero..The Dc
Machine bon kalindo ❤❤❤❤
Zoonadi Mr Kalindo simukunama Chakwera ndi gulu lake they are mbunzi za anthu they are fools
Iwo andale si bola akhutitsa mimba zawo
Or abadwe mwatsopano Koma mizimu ya anthu anapha ija imufafanthabe Mulungu wake uti okumba mapemphero a munthu opondeleza oipa wakupha okondela ngati ameneyo
Mumakwana Avon karindo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Abon kuyilawilira😂😂😂
😅😅😅😅😅 Kakakakakakakakaka DC 😂 our president kkkkmwana owopsa heav😂😂😂
Mumakwana boss,osawanyengerera makape achina kumkuyu,zikhale ndi chakwera yemwe😙😙
Zakeyu powonetsa kubadwa mwatsopano anabweza theka lachuma cheke kwawomwe anawabera ndiye Chakwera pamodzi ndi amithenga Ake onse abweze zomwe atiberazo powonetsa kubadwa mwatsopano
😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥kuti buuuuuuuuuuuuuu
THE D C BOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOON KALINDO 💪💪💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
I agree with Kalindo..the #thinkalike
Izoooh Hankonnani pwiya aleleni iiwesese😂
Sowuna auseni agalu amenewa achakwera
President omvetsa chisoni chakwera ulamuliro wake ngati dzaka 100 chifukwa cha dyera
Bon muuzeni chakwera kuno ku mangochi asazafike tizapha tokha ndi galu
kkkk mwakumana usazindikila nokha nokha vuto mli busy pa ma phone mwayiwala kuti azanu ali pa ground . zoti peter analamula bwino mkunama matha ma albino ambiri
Bon k amatha ❤
Chakwela mhuzi ya muthu
Iweyo umandiwaza chifukwa umayankhula chilungamo. Palisouyu Limpopo FM NDI bakili muluzi TV anthuinu ndinu madolo❤
Iweyo ndi one
You saying the truth
Koma opposition ikalowa mu boma imasinthanso kuiwala zomwe ife amalawi tinkalira .
Koma thawi ikubwera ndithu mlungu atiyakha ndithu mlungu wathu salephera❤
Kkkkkk winiko samatopa mumamuseweletsa😂
Machende awo awa
Our Hero
The DC
Mwana oopsa kwambiri
Koma why sakuyamkhulapo za manganya vice president ku mcp
Inetu ndi mchewa koma nyasi izii sitikukondwa Nazo ,from nathenje
Ulemu wanu comrade
Vuto a Malawi ife mantha
The D.C.
awa akungolankhula Loma palibe zomwe zikuchitika.mmalo mot tipange zinthu ngat kukenya.
Aaaa kuba mistake kuyika MCP papando iiiiiii tinalakwitsa
Morning
The DC Bon kalindo ❤
Kodi cakwera akufuna anthu amuvotere 2025 afuna adzidzatani poti iye sadziwa kanthu akufuna adzapitilidze kuba conde. Cakwera usavutike amalawi sitikukufuna ngakhale pangono watilidzatu iwe watidzudza dzaka 5 ngati dzaka hundred
I just watch so that kalindo can make some money
Dziko lamkaka ndi uchi lija pano ndi sabora ekhaekha😢😢😢😢
The DC 💥💥💥💥💥
We respect fools so no need to reply... 😂😂😂😂
madala madala born k
Wamsala iwe amalawi umanenawo ndi ati? enafetu sutifuna zolandila zimene umafuna iwezo ife amene timalima tikusangalala kabwebweta ndi misala yakoyo
The dc
Komanso boma ili manyaka eni eni koma ndlama zikuwonongedwazi ndi zabwino bwino? Mzipatala mulibe mankhwala koma ndlama zogula anthu muli nazo shame Malawi government shame Mulungu kumwambako muzimutetezera Bon kalindo kwina kuli konse angapite
60years of independence but nothing to show
💪💪💪💪
Nkhani ya ma ID muikokomeze kt apart from mcp zipani Zina taonetsetsani zomwe zikuchika mmaderamu,tabwerani kunathenje midzi ngati monga mphete village,mtsotsa, sanjiko,nyama ,kaphala ,matapira,Chatha ana osafikamo Zaka,
Empty tins
❤❤❤❤❤
Let's not be negative for everything. Peter was also useless
Chamba kkkkkkkkkk
Koma akamati abadwa mwasopani akuyesa kuti ndiopusa Never ever changes my mindset
Truth must be told plainly without fear
Vuto amalawi mumawombele mmanje fiti kodi simudziwa kut mtambo ni akalindo vinanyeza kwambili pita muthali mpaka apita analuza masankho anazikambe amenewa
Kkk
Terelini
Wapenga chakwerayu
6 July ndiye chani
Tell them where to get off your ass The DC. Chakwera amadya maliro
Mutayeni uko Joyce Banda ndihule wachabe chabe
ine Mchewa Koma Chakwera Guy osamuvoteraso
Wow
Ufulu unali mbuyomu koma pano ufulu uja anatilanda,kumangomangidwa ...Boma ili lankhaza zedi.
Abon kuyilawilira😂
Chakwera wationjedza
Chakwera ndi pa msete seriously
Kuyankhula mwachulumgamo
😂😂100%
😂😂 telelini
Kodi zinachitikira kuti? Sindizisate nane 😂😂😂
Kodi aborn kalindo mapemphero ndikuti ndichinthu choyipa kodi nayesa unali mwambo wamapemphero koma inuso zina mumangolankhura zopepela zokhazokha ndipo amene amakupasani ma coment okutamandani nkupanda nzeru pa inuyo tikuwona ndipanja zowona dairy kubwera pa air basi nkhani za ziii zopanda phindu
@StanleyChirwa-d6b
7 күн бұрын
Kungosiya kuvera bas coz mutopa🥺
@WisdomMaseko-fi5sv
7 күн бұрын
Koma muli nkuchikanwa kosatopa now it's boring
😂😂😂😂😂
Kkkkkkkk Born K the DC
Pangoline the DC ❤❤
Bon kalindo the great💪💪💪💪💪
Wapengatu chakwelayu😂😂😂😂is Dog.
Kalinda mtambo niamene anayika chakwela paudindo vitsilu vimenevi vikutenga ngati amalawi opusa amene omatsatila zokamba zanu nose awili ndinu munayika amcp pampando mwemwe vitsilu amalawi osavela viwanthu vimenevi😅😂😊😊
Mumuuze Kalindoyo kuti ndiodwala komaso ndichitsiru kwabasi zinthu zinaipa kuyambila pa Bakili mpaka pano
@felixmaluku5077
7 күн бұрын
Iwe osamuudza wekha bwanji
@JosephChatama
7 күн бұрын
Iwe ndi mbudzi kwabasi, zitaipa nthawi imeneyo unapangapo chani😂😂
@user-hm9nc7lz6e
7 күн бұрын
Iwe ndi chisiru nthawi ya maprezdent enawo fanta timagula 200 kwaca nthawi yachakwera 750 wakumudzi angamugulire mwana fanta manyi amako wava cakwera waononga dziko kukwera kwa zinthu ndiye anthu tikamalira iwe wati tikunama mbusa wasatanic akucoka 2025 mdipo adzamumanha ndende yace tikumba dzenje mpaka adzafera momwemo munthu oipa mtima ngati konyera
@ChrisMsonyo-yq2ko
7 күн бұрын
@@user-hm9nc7lz6e galu kwabas
@ShamilahSaizi
7 күн бұрын
Mwapenga inu eti
Chakwera ndi bakha weniweni.
Wandiwazaso ndi busa ujayo wamzeru kwambiri kulalikila mwaphavu
Abon kuyilawilira😂