BON KALINDO 7 JULY 2024 KUKHDZULASO PA CHI SUNDAY

Пікірлер: 115

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg7 күн бұрын

    Nanuso bwanji Joyce Banda mbuzi yamunthu chakwera mutu ngati phwala lambuzi

  • @limbanimtitima9170
    @limbanimtitima91707 күн бұрын

    Born you always talk the truth ❤❤😂

  • @chiefjusticie
    @chiefjusticie7 күн бұрын

    Ulemu wanu

  • @KelvinMangwengwe
    @KelvinMangwengwe6 күн бұрын

    Kuyankhula zomveka bwino ndipo zaphindu zokhazokha congratulation boss

  • @BinwelLukali
    @BinwelLukali7 күн бұрын

    The DC bon kalindo the great 💪💪💪💪

  • @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un
    @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un7 күн бұрын

    The DC akamuna okakha NDI mawaya

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf7 күн бұрын

    azibale athu amene anaphedwa ndi chakwera kuchikangawa ndi zomvesa chison kudziko lino chakwera ndi chigawenga

  • @MacreaChilingulo-ob9gb
    @MacreaChilingulo-ob9gb7 күн бұрын

    Long live Boooon Kalindo !!!!! The D C ccc !!!! The Wise Guy !!! Iweyo palibenso !!

  • @owenmanda1741
    @owenmanda17417 күн бұрын

    The problem with Malawi is nkhondo timawasiira anthu ochepa kumenyera ufulu,no wonder akalowa mu boma amakasakaza chuma.We all need to fight for our freedom

  • @AustinMangani
    @AustinMangani7 күн бұрын

    Mbambande Mr

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi87137 күн бұрын

    Ati bon Kalindo amangidwebe😂

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58917 күн бұрын

    Akhwakhwananda amenewa 🐊🐊🐊🐊 atitola kwambiri

  • @DanielChima-zl2uo
    @DanielChima-zl2uo7 күн бұрын

    zoona Bon kalindo ngakhale kuno ku south Africa zimatikwana kwa basi zimene akupanga president

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda58917 күн бұрын

    60 years subtract 4 years yamazumzo ya chakwela

  • @JosephMichael-x7v
    @JosephMichael-x7v7 күн бұрын

    Bon kalindo our president

  • @ShaibMusa
    @ShaibMusa7 күн бұрын

    My Hero..The Dc

  • @DYSONKUMPEREMBE
    @DYSONKUMPEREMBE6 күн бұрын

    Machine bon kalindo ❤❤❤❤

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja7 күн бұрын

    Zoonadi Mr Kalindo simukunama Chakwera ndi gulu lake they are mbunzi za anthu they are fools

  • @ChikumbutsoTsalangu
    @ChikumbutsoTsalangu7 күн бұрын

    Iwo andale si bola akhutitsa mimba zawo

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma6 күн бұрын

    Or abadwe mwatsopano Koma mizimu ya anthu anapha ija imufafanthabe Mulungu wake uti okumba mapemphero a munthu opondeleza oipa wakupha okondela ngati ameneyo

  • @BeatrizUlanda-ht2th
    @BeatrizUlanda-ht2th7 күн бұрын

    Mumakwana Avon karindo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @AbondBolbo
    @AbondBolbo7 күн бұрын

    Abon kuyilawilira😂😂😂

  • @RichardMedi
    @RichardMedi7 күн бұрын

    😅😅😅😅😅 Kakakakakakakakaka DC 😂 our president kkkkmwana owopsa heav😂😂😂

  • @TecksonKaima-dr6er
    @TecksonKaima-dr6er7 күн бұрын

    Mumakwana boss,osawanyengerera makape achina kumkuyu,zikhale ndi chakwera yemwe😙😙

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx7 күн бұрын

    Zakeyu powonetsa kubadwa mwatsopano anabweza theka lachuma cheke kwawomwe anawabera ndiye Chakwera pamodzi ndi amithenga Ake onse abweze zomwe atiberazo powonetsa kubadwa mwatsopano

  • @EstherNangomba
    @EstherNangomba7 күн бұрын

    😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥kuti buuuuuuuuuuuuuu

  • @eliaschinoko2086
    @eliaschinoko20867 күн бұрын

    THE D C BOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOON KALINDO 💪💪💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-ve7rx7vj1g
    @user-ve7rx7vj1g7 күн бұрын

    I agree with Kalindo..the #thinkalike

  • @blessingsmwale6007
    @blessingsmwale60075 күн бұрын

    Izoooh Hankonnani pwiya aleleni iiwesese😂

  • @user-ty5zh2xi9b
    @user-ty5zh2xi9b6 күн бұрын

    Sowuna auseni agalu amenewa achakwera

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma6 күн бұрын

    President omvetsa chisoni chakwera ulamuliro wake ngati dzaka 100 chifukwa cha dyera

  • @SilverMkwatula
    @SilverMkwatula7 күн бұрын

    Bon muuzeni chakwera kuno ku mangochi asazafike tizapha tokha ndi galu

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala14937 күн бұрын

    kkkk mwakumana usazindikila nokha nokha vuto mli busy pa ma phone mwayiwala kuti azanu ali pa ground . zoti peter analamula bwino mkunama matha ma albino ambiri

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt6 күн бұрын

    Bon k amatha ❤

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r7 күн бұрын

    Chakwela mhuzi ya muthu

  • @trifoniachilunda6263
    @trifoniachilunda62637 күн бұрын

    Iweyo umandiwaza chifukwa umayankhula chilungamo. Palisouyu Limpopo FM NDI bakili muluzi TV anthuinu ndinu madolo❤

  • @TorshKadango
    @TorshKadango7 күн бұрын

    Iweyo ndi one

  • @IanChidothe
    @IanChidothe7 күн бұрын

    You saying the truth

  • @EliaMhone
    @EliaMhone6 күн бұрын

    Koma opposition ikalowa mu boma imasinthanso kuiwala zomwe ife amalawi tinkalira .

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana7 күн бұрын

    Koma thawi ikubwera ndithu mlungu atiyakha ndithu mlungu wathu salephera❤

  • @AliceMpaso
    @AliceMpaso6 күн бұрын

    Kkkkkk winiko samatopa mumamuseweletsa😂

  • @charlesmataka1700
    @charlesmataka17007 күн бұрын

    Machende awo awa

  • @marychavula698
    @marychavula6987 күн бұрын

    Our Hero

  • @MarkinaJohn
    @MarkinaJohn5 күн бұрын

    The DC

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri85177 күн бұрын

    Mwana oopsa kwambiri

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar74687 күн бұрын

    Koma why sakuyamkhulapo za manganya vice president ku mcp

  • @KennethChazama
    @KennethChazama7 күн бұрын

    Inetu ndi mchewa koma nyasi izii sitikukondwa Nazo ,from nathenje

  • @HarryYottam-ft1bo
    @HarryYottam-ft1bo7 күн бұрын

    Ulemu wanu comrade

  • @CollinsHala
    @CollinsHala6 күн бұрын

    Vuto a Malawi ife mantha

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete7 күн бұрын

    The D.C.

  • @chestermajora
    @chestermajora7 күн бұрын

    awa akungolankhula Loma palibe zomwe zikuchitika.mmalo mot tipange zinthu ngat kukenya.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda87117 күн бұрын

    Aaaa kuba mistake kuyika MCP papando iiiiiii tinalakwitsa

  • @AustinMangani
    @AustinMangani7 күн бұрын

    Morning

  • @AffickChaona
    @AffickChaona7 күн бұрын

    The DC Bon kalindo ❤

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e7 күн бұрын

    Kodi cakwera akufuna anthu amuvotere 2025 afuna adzidzatani poti iye sadziwa kanthu akufuna adzapitilidze kuba conde. Cakwera usavutike amalawi sitikukufuna ngakhale pangono watilidzatu iwe watidzudza dzaka 5 ngati dzaka hundred

  • @rhinovaheke6614
    @rhinovaheke66147 күн бұрын

    I just watch so that kalindo can make some money

  • @JeremiahChilenje
    @JeremiahChilenje7 күн бұрын

    Dziko lamkaka ndi uchi lija pano ndi sabora ekhaekha😢😢😢😢

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg7 күн бұрын

    The DC 💥💥💥💥💥

  • @AndrewChitsamba
    @AndrewChitsamba6 күн бұрын

    We respect fools so no need to reply... 😂😂😂😂

  • @user-ss9bj5eh6b
    @user-ss9bj5eh6b7 күн бұрын

    madala madala born k

  • @ClementChisemphele
    @ClementChisemphele7 күн бұрын

    Wamsala iwe amalawi umanenawo ndi ati? enafetu sutifuna zolandila zimene umafuna iwezo ife amene timalima tikusangalala kabwebweta ndi misala yakoyo

  • @PatronChanza
    @PatronChanza7 күн бұрын

    The dc

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b7 күн бұрын

    Komanso boma ili manyaka eni eni koma ndlama zikuwonongedwazi ndi zabwino bwino? Mzipatala mulibe mankhwala koma ndlama zogula anthu muli nazo shame Malawi government shame Mulungu kumwambako muzimutetezera Bon kalindo kwina kuli konse angapite

  • @HamitonFrank
    @HamitonFrank7 күн бұрын

    60years of independence but nothing to show

  • @IbrahimRaphael-z3l
    @IbrahimRaphael-z3l7 күн бұрын

    💪💪💪💪

  • @KennethChazama
    @KennethChazama7 күн бұрын

    Nkhani ya ma ID muikokomeze kt apart from mcp zipani Zina taonetsetsani zomwe zikuchika mmaderamu,tabwerani kunathenje midzi ngati monga mphete village,mtsotsa, sanjiko,nyama ,kaphala ,matapira,Chatha ana osafikamo Zaka,

  • @AndrewChitsamba
    @AndrewChitsamba6 күн бұрын

    Empty tins

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah7 күн бұрын

    ❤❤❤❤❤

  • @user-kw7wr4kq9w
    @user-kw7wr4kq9w7 күн бұрын

    Let's not be negative for everything. Peter was also useless

  • @yobesaikonde6166
    @yobesaikonde61667 күн бұрын

    Chamba kkkkkkkkkk

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d7 күн бұрын

    Koma akamati abadwa mwasopani akuyesa kuti ndiopusa Never ever changes my mindset

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx7 күн бұрын

    Truth must be told plainly without fear

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko7 күн бұрын

    Vuto amalawi mumawombele mmanje fiti kodi simudziwa kut mtambo ni akalindo vinanyeza kwambili pita muthali mpaka apita analuza masankho anazikambe amenewa

  • @yusufbreak905
    @yusufbreak9057 күн бұрын

    Kkk

  • @KhumboMunthali-jx5me
    @KhumboMunthali-jx5me7 күн бұрын

    Terelini

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn7 күн бұрын

    Wapenga chakwerayu

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z7 күн бұрын

    6 July ndiye chani

  • @elishamael-shadai
    @elishamael-shadai7 күн бұрын

    Tell them where to get off your ass The DC. Chakwera amadya maliro

  • @FaruckMuhammad
    @FaruckMuhammad7 күн бұрын

    Mutayeni uko Joyce Banda ndihule wachabe chabe

  • @ChikuMatemba
    @ChikuMatemba7 күн бұрын

    ine Mchewa Koma Chakwera Guy osamuvoteraso

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc7 күн бұрын

    Wow

  • @user-dd1qq5xq1k
    @user-dd1qq5xq1k7 күн бұрын

    Ufulu unali mbuyomu koma pano ufulu uja anatilanda,kumangomangidwa ...Boma ili lankhaza zedi.

  • @AbondBolbo
    @AbondBolbo7 күн бұрын

    Abon kuyilawilira😂

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo7 күн бұрын

    Chakwera wationjedza

  • @mikeasmachine4581
    @mikeasmachine45817 күн бұрын

    Chakwera ndi pa msete seriously

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t7 күн бұрын

    Kuyankhula mwachulumgamo

  • @MphatsoGowero
    @MphatsoGowero7 күн бұрын

    😂😂100%

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb7 күн бұрын

    😂😂 telelini

  • @nafejonga972
    @nafejonga9727 күн бұрын

    Kodi zinachitikira kuti? Sindizisate nane 😂😂😂

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness7 күн бұрын

    Kodi aborn kalindo mapemphero ndikuti ndichinthu choyipa kodi nayesa unali mwambo wamapemphero koma inuso zina mumangolankhura zopepela zokhazokha ndipo amene amakupasani ma coment okutamandani nkupanda nzeru pa inuyo tikuwona ndipanja zowona dairy kubwera pa air basi nkhani za ziii zopanda phindu

  • @StanleyChirwa-d6b

    @StanleyChirwa-d6b

    7 күн бұрын

    Kungosiya kuvera bas coz mutopa🥺

  • @WisdomMaseko-fi5sv

    @WisdomMaseko-fi5sv

    7 күн бұрын

    Koma muli nkuchikanwa kosatopa now it's boring

  • @InnocentKandaya
    @InnocentKandaya6 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

  • @ChisamiMalota
    @ChisamiMalota7 күн бұрын

    Kkkkkkkk Born K the DC

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole7 күн бұрын

    Pangoline the DC ❤❤

  • @HamitonFrank
    @HamitonFrank7 күн бұрын

    Bon kalindo the great💪💪💪💪💪

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn7 күн бұрын

    Wapengatu chakwelayu😂😂😂😂is Dog.

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko7 күн бұрын

    Kalinda mtambo niamene anayika chakwela paudindo vitsilu vimenevi vikutenga ngati amalawi opusa amene omatsatila zokamba zanu nose awili ndinu munayika amcp pampando mwemwe vitsilu amalawi osavela viwanthu vimenevi😅😂😊😊

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere7 күн бұрын

    Mumuuze Kalindoyo kuti ndiodwala komaso ndichitsiru kwabasi zinthu zinaipa kuyambila pa Bakili mpaka pano

  • @felixmaluku5077

    @felixmaluku5077

    7 күн бұрын

    Iwe osamuudza wekha bwanji

  • @JosephChatama

    @JosephChatama

    7 күн бұрын

    Iwe ndi mbudzi kwabasi, zitaipa nthawi imeneyo unapangapo chani😂😂

  • @user-hm9nc7lz6e

    @user-hm9nc7lz6e

    7 күн бұрын

    Iwe ndi chisiru nthawi ya maprezdent enawo fanta timagula 200 kwaca nthawi yachakwera 750 wakumudzi angamugulire mwana fanta manyi amako wava cakwera waononga dziko kukwera kwa zinthu ndiye anthu tikamalira iwe wati tikunama mbusa wasatanic akucoka 2025 mdipo adzamumanha ndende yace tikumba dzenje mpaka adzafera momwemo munthu oipa mtima ngati konyera

  • @ChrisMsonyo-yq2ko

    @ChrisMsonyo-yq2ko

    7 күн бұрын

    @@user-hm9nc7lz6e galu kwabas

  • @ShamilahSaizi

    @ShamilahSaizi

    7 күн бұрын

    Mwapenga inu eti

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki7 күн бұрын

    Chakwera ndi bakha weniweni.

  • @jamesmsonkho4830
    @jamesmsonkho48307 күн бұрын

    Wandiwazaso ndi busa ujayo wamzeru kwambiri kulalikila mwaphavu

  • @AbondBolbo
    @AbondBolbo7 күн бұрын

    Abon kuyilawilira😂

Келесі