Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r
14 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@IshumaelMbewe-d4t14 күн бұрын
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@PetersenjMwale14 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@RobertCosmas-bo1uo13 күн бұрын
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@HastingsJonathan13 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@blessingsfalamenga457511 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@FosterMatchano13 күн бұрын
I like the conversation
@GiftNyirenda-q9d12 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@louisgolden14 күн бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@lastonmasoatenganji-bs5gf12 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@kotking-xg7pp14 күн бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@dumisanimoyo315214 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@PetersenjMwale14 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@user-sw6rz4tz3z11 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@user-to5of3ks3g14 күн бұрын
Nice message
@EugeneChiyenda14 күн бұрын
Kma iyiyi mwang'alula🥳
@user-un8yq1gg2i13 күн бұрын
Hahahaha koma iyiyi nde ndiyong'alura kuyipatu kkkkkkk
@user-mh7cc8up4i13 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@nellybruhan583414 күн бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t
14 күн бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834
14 күн бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
@MemoryKamanga-jv4jh14 күн бұрын
Number one brothers
@user-sw6rz4tz3z11 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@GraceZumazuma14 күн бұрын
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
@xinalungu961613 күн бұрын
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@Erickasonya-uw8yw11 күн бұрын
Bravo guys mumakwana
@sungirenikampu863014 күн бұрын
Guys mumatha keep it up
@OssmanAbubaker-l5s10 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@user-zo3bf3ec3g12 күн бұрын
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
@sulleahmnyimbili136214 күн бұрын
Well spoken
@SolokingChimzy-yt7dj11 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@gracemkandawire876913 күн бұрын
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
@jelsonmlowoka861114 күн бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala
14 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
Ife timamva nanu kukoma chifukwa mumayankhula chilungamo ,ndipo nthawi ya program yanuyo muionjezele mabwana
@user-si7po9sd5i14 күн бұрын
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala
14 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i
14 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r
14 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r
14 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
@ShagaFologonya14 күн бұрын
Mmakwana uzo ndi mzao
@EllenChione14 күн бұрын
Ndakutayilani kamtengo guys
@user-im7sc2my4w14 күн бұрын
Komadi ma junior police akuvutika ,srs
@raytavares225614 күн бұрын
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
Пікірлер: 123
❤❤❤iyiyi mwanena zogwila mtima lero mwaonetsa u independent wa times keep it up
Iyiyi nde yandifikapo ndithu big up Hot current 💪💪
Ulamuliro wa nkhanza inde pano school fees anthu tikulephera kulipira ndiye Ana aphunzire motan mmmm ambuye atithandize
@user-zq3li3qw1m
14 күн бұрын
Zoonadi
For the first time Malawi can see great roads not just miyala ya madziko. I pray that Malawi wakes up. We should wake up n balance our forums
Kuyakhula mopanda mantha. Komaso mwaphawi zofunikira kwaose amalawi pabwino mkuyamikirana. Poipapo dzuzurani, rangizani akapanda kumva arekeni!!!!🎉
Apa ponkhapa mwawalakhulila amalawi🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r
14 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
I like the conversation
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
U guys u talking the really truth
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
Nice message
Kma iyiyi mwang'alula🥳
Hahahaha koma iyiyi nde ndiyong'alura kuyipatu kkkkkkk
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t
14 күн бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834
14 күн бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
Yeah! This is hot for sure.
Guys mwasiya kugawa ma sweet ulemu wanu. Timayesa nanuso akudyesani chibansi
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
Koma ndiye mwanena mosanyengeleratu
Hahahaha akuti 👇 "Sitidya kwanu!" 😅😅😅😅
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
Eeeeee anyamata relo mwatokota kkkkkk muli bho kwambiri mwaveka ❤❤❤
Iyi ndye hot current yen yen 🔥🔥🔥
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
Number one brothers
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
Bravo guys mumakwana
Guys mumatha keep it up
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
Well spoken
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala
14 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
Mmmmm tiyeni ticheze bwino
Lelotu anyamata mwawalankhulila amalawi pitilizani
Mmoziyi ndamene amalakwisa program amakonda kuwatchinga azinzakewo kuti asamasuke
Mwalakhulako zazerutu, mukamadya ma bazi guys times izakhala Ngati MBC yoonera achakwera okha
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
If yuo steal with sorrounded one day all will 😂😂
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
Koma zikhale ng'omayo nde ayi aaaaa
Iyi koma mwang,alulandi makosana abwana kutundako azizifusa makamaka achekwela ndimbava ndifukwa akopa ACB
Why big people wear tinted sun glasses
😂😂😂😂😂 apa mwatha manthatu
Vuto lolandililatu zanu tinkhope tanuto nditamanyaziii😢
Mmmm Zikhale Ng'oma nawoso akufuna u Vice President ku MCP? Mmmm awa ai body structure
@eliffagondewe8214
14 күн бұрын
Kkkkkkk 🔥🔥
Chanzelu apha chilima+anthu 8 kumphatizapo kasambala
Ife timamva nanu kukoma chifukwa mumayankhula chilungamo ,ndipo nthawi ya program yanuyo muionjezele mabwana
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala
14 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i
14 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r
14 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r
14 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
Mmakwana uzo ndi mzao
Ndakutayilani kamtengo guys
Komadi ma junior police akuvutika ,srs
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
Brilliant idea 💡
Ulemu
Ku painter eti?
anyamata musamale muphedwatu mcp sifuna anthu oyankhula chilungamo
Aaah koma ma boys inuyo mumakwana 😅
China chake kuseliku nkumati ndikupeleza 7 kwa ten mfiti 😢
Every day kusokesa uniform ya police zovuta zedi
Zofunika osambisala munda wa mtedza timadabwatu koma apa mwabwera
Ati sitidya kwanu kmatu Mr wonder
@eliffagondewe8214
14 күн бұрын
Watopera akanganya amenewa.
😂😂😂😂
Ayi palibe chabwino kulibwino undindo asiyile wena
Iyayi bomali linaziyipisila kale
Mukamatero tililimodzi pamenepo
Mtsogoleri yekhayo adali ndi kuthekera koteroko adali Akamuna a Bingu seconded by Akamuna Dr Saulosi
@RitaKainga
14 күн бұрын
Exactly!
Koma kumeneko
Mumakwana gayez
Thanks you 2 guys there,Komano kod mmesa achakwera anatiuza Kut adzamanga aliyense ochita katangale m'boma lawo? Ndy chilowele amenebanamuona mkumanga ndi achilima okha? Plz plz t mkwabwino kusangalatsa Mulungu than munthu mzako
Abodza awa sanena zoona komaso oopa kwabasi bwanji analephela kutuuza zoona nthawi ya maliro anyamata wanthu skc timakubukila zbs isakudziwa ndalama pa imfa ya bingu atolankhani amakwela mu tengo kuti anene zoona Koma pano mmmmmmmmmma radio ake cabbage oneka oliba koma mkati madzi okhaokha
More fire gentlemen, Malawi wathu ndiyemweyu,Osaopa kuzilangiza nkhutukumve ndi mbala zimenezi
Chakwera must go before September pls God is looking for us
bora bingu ndi ng'ono wake pta osati uyuyu chakwerayu ndimbzi
Hello Guys. Please continue hitting the nail on the head.
Chilungamo chimamasula, azibambo inuyo mulungu azikudalisani ndikutetezani mukugwila tchito, from cape town
Apapa ndiye mwabwera madolo ulemu wanu that is democracy
Pitilizani kumatiyakhulira chilungamo pa hot current
😂😂😂😂😂😂😂😂 ndemvu zamwayi apolice akumadula zikhadabo atavala nsapato kkkkkkkkkk
@CalvinThomson-ys5zf
14 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 uyu ndiwamwano ati kuwenga zikhadabo autavala nsapato
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
14 күн бұрын
@@CalvinThomson-ys5zf kkkkkkkkk akutero kuli kutha kwa nsapato kkkk
Pamene apolisi akusowa nsapato nawo ma pensioners sakulandira ndalama zawo ena mpaka zaka panopa katangale mbona wa chulukadi
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV❤
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
U guys u talking the really truth
@user-dc7qq9yz3v
14 күн бұрын
Matha
Koma kumeneko
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@GiftNyirenda-q9d
12 күн бұрын
Vuto lanu lopanga compare anthu awiri osiya, zolinga zosiya, koma kulephela kusiyanitsa.
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV