A UTM Bwezi Atapita Ku Kawonela Kumbila Kwa Michael Usi Ngati Vice President - Samuel Lwara
On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says it would have been nice if UTM members are leadership had attended the swearing in ceremony of Right Honourable Michael Usi as Vice President of the Republic of Malawi last friday.
Ku Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wati zikanakhala zabwino ngati mamembala a UTM ndi atsogoleri akadakhala nawo pamwambo wolumbiritsa Wolemekezeka Michael Usi kukhala wachiwiri kwa Purezidenti wa Republic of Malawi lachisanu lapitali.
#malawi
Пікірлер: 42
Genuine UTM members wouldn't go there just to clap hands and rejoice for someone who was a member of the party but due to his misconduct in the party divided people, party politics and sided with the MCP all the time than his party UTM
This man can talk eish
Usi was born in Zimbambwe.
Kodi mumaonangati mukamalankhula ndiyekuti muli ndi nzelu eti? Musamatinyase apa
@AdoptedNaijaBoy
13 күн бұрын
He’s even contradicting himself
Chakwela you mast go watikwana
APM my VOTE
@actuarialscience2283
12 күн бұрын
Ndine wa MCP koma ndidzavotera Peter
Iwe kape ungamuuze chochita ndani chifukwa wadya banzi aaaaa fisi
Don't answer for people, they know what they are doing
Zaziii!
Usi is always MCP supporter.
Mwadya banzi
@KenDuweh
12 күн бұрын
Iyu ali banja koma ?😅😅😅 fundo zosagwira mtima 😊
Waboza uyuyu analandira ndarama u can't be mcp and support utm
Iwe rwala and maikolo usi ndinu ma hypocrites, amthira kuwiri inu, you betrayed saulos chilima, Iwe rwala u r talking rubbish!
Za ziii,,
Sadayenera kupita ku meneko kamba koti adali pa maliro achilima
Uyunso alibe nzeru amayankhula zopanda nzeru
Ndiye ife tikulira mpaka 40 dez
My vote is for apm zingavute bwanji chifukwa ndi munthu wodekha oziwa kuyendesa bwino Boma komanso sanaphe munthu wina aliyense chifukwa chandale ...Apm ndiye vote ya ine .chakwera wandinyansa kwambili pa 4 years yokha
Ifeyo amalawi tikungofuna chilima wathu basi zaziiizo zopanda mutu uko mkazi wake ndi ana makola komanso abale ukuona ngat tikumva kukoma fusteck
Uyu ndi doba doba uyu
Monga mwa dzina lako Warwala ukudwala iweyo..
APM boma basi
Kkkkkk koma kumalawiko!!!!!
Zovuta kwambiri khoswe wakhala pa mkate.
Kodi uyu siuja amupasa ndalama a MCP
Uyu chimene akunena sakuchiziwa
Achitsilu inu munadya chibazi apa mukufuna mwatenge anthu ngat zitsilu ediot nthawi yoseija unalikut Galu iwe
Chitsiru Cha munthu
Chisilu cha munthu ichi
Pantumbopako Lwala,tufuna za kalindo ife atuluke mxiiii
Mmachende ako iwe galu
This guy he new nothing about politics.
Iwe galu osow chochita fisi
Zoonadi aliyese amafuna kudya
Ukusokosela zopanda nzeru who is usi after all? Ukumuchemelera ukuona ngati akutengela pena pake pomwe a mcp sanakufikisepo useless man depending on other's sweating. Dig yourself you will find gold on your own.
Waste of my data mxiew
There is no sense in your statement