Limpopo iiiih! ma demo ajatu kwabwela anthu akunja kudzaletsa atapangidwa hayala Ntanyiwa waulura

Пікірлер: 98

  • @ShaolinThomas-ow8yn
    @ShaolinThomas-ow8yn3 күн бұрын

    Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba2 күн бұрын

    Koma iweyo pokhapa pot awagwila ndakuimikila manja mwamba athuo agwidwad

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du2 күн бұрын

    Akulu akulu mukulankhula koma sitikumva 😢

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b3 күн бұрын

    We won't fear anything even as Zambian s were coming in Malawi guys to fight that evil man chakwela

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda2 күн бұрын

    Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o2 күн бұрын

    May God bless you comrade Ntanyiwa

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm3 күн бұрын

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du2 күн бұрын

    Koma chakwera wandikwana one day ndi kupedza people they call gringo

  • @UsenLashid
    @UsenLashid2 күн бұрын

    Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn7158Күн бұрын

    umakwana mtanyiwa tikuziwa zambili amalawi ambuye azikupasani moyo wautali 🎉🎉🎉🎉

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e2 күн бұрын

    Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi

  • @WatsonNtchito
    @WatsonNtchitoКүн бұрын

    Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du2 күн бұрын

    Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂

  • @priscillamangata4023

    @priscillamangata4023

    2 күн бұрын

    Umwa chani

  • @user-ht7vs3dp2u
    @user-ht7vs3dp2u3 күн бұрын

    Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee

  • @JaneLikome
    @JaneLikome2 күн бұрын

    Nice mr ntanyiwa

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns3 күн бұрын

    Pano malawi ndi North Korea 😭😭😭

  • @CadTafa2
    @CadTafa23 күн бұрын

    Apolici a malawi a kuzishipisa

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu2 күн бұрын

    Umakwana ya mtanyiwa tili nawenawe my brother

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi2 күн бұрын

    Apapa ndatanganidwa kuwerenga nkunvesera😂😂

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal2 күн бұрын

    Anthu nonse amene mukudana ndi nthanyiwa mitungati zoswera malambe inu zikukusangalasani mmene akuyendesela dzikoli gule wanuyi achoke alibe phindu

  • @DuntumaziyaDuntumaziya
    @DuntumaziyaDuntumaziya2 күн бұрын

    following you sir

  • @blacksonpeshes5057
    @blacksonpeshes50572 күн бұрын

    kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja

  • @BitonFred
    @BitonFred9 сағат бұрын

    Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon2 күн бұрын

    Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah2 күн бұрын

    Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,

  • @misoMoyo
    @misoMoyo2 күн бұрын

    Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt2 күн бұрын

    Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe

  • @IssahAluba
    @IssahAluba2 күн бұрын

    Chonde AMalawi asatiphimbe maso BOMA ilili osalivera tiyeni pansewu week yamawa osaopa gayz 💪💪🛶🛶🏹🏹⚒️⛏️

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon2 күн бұрын

    Ndipo chakwera tidzachita kuotcha pamoto chifukwa chankhanza akuchitazi

  • @NisharChibisa
    @NisharChibisa3 күн бұрын

    Mumakwana

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmaelКүн бұрын

    Zachamba basi dikilani 2025 vote yanu ndiye nuclear power osati zabibi zanuzi

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdezaКүн бұрын

    nkhanga zaonaaa

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukumaКүн бұрын

    Ntanyiwa woyeeeee

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo3 күн бұрын

    ❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata40232 күн бұрын

    Comredy mtanyiwa tikufuna number yanu tizipephela Nanu mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda

  • @JamesIsaac-zi4kb
    @JamesIsaac-zi4kb2 күн бұрын

    Chakwela ofuna adibwe kanyenya basi

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o2 күн бұрын

    Nde inu mukuganiza kut olo patabwera peteryo zinthu zingasinthe foundation ya Malawi kuvuta konseko ndi chipani Cha udf olo mutatani Malawi sazasintha

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o2 күн бұрын

    Ukanakhala kut mwina ukutiwuza munthu wozamuvotera koma nawenso ukumpangila peter kampen choti uziwe peter nayenso atatitopesa kale sitikunfunanso

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f2 күн бұрын

    Tisayembekezere kuti tingamve munthu wakuphayo kuti ndine ndapha mayz ? Munona kt wakupha kufufuza chifkwa chomwe wina wafera koma atapha ndiyeyo ? Mayankho ndiomwewa omwe tikumayankhulawa coz action ikuchitatu kuoneka yokha ndipo mwachindunji monga kumangidwa anthu then kulowesa zigawenga nde ngt akusakidwa anthuwa kuti aphedwe nde nkumat ena omwe adafa aja anafera zina ?

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili2 күн бұрын

    Mcp mukali kuyalukirayalukiratu

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona3 күн бұрын

    M C P -- Malawi Congress Party M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️

  • @maluli5691
    @maluli56912 күн бұрын

    Asilikali Aku malawi ndi asilikadzi.west Africa asilikali sakunyengelela kulanda boma

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o3 күн бұрын

    Anthu amenewo ngat agwidwa aphedwe ndinthu cifukwa iwowo anabwela kuzapha

  • @mipeacemakermw9501
    @mipeacemakermw950121 сағат бұрын

    Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣kzread.info/dash/bejne/iYZ4zbNxo8KZZM4.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p

  • @stanleychisasa4343
    @stanleychisasa43432 күн бұрын

    Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which Big man?

  • @dorisbutao4227
    @dorisbutao42272 күн бұрын

    Mmmh

  • @UsenLashid
    @UsenLashid2 күн бұрын

    Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please

  • @jangiya03
    @jangiya033 күн бұрын

    Ambuye tithandizeni Malawi waipa

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf3 күн бұрын

    Zoonad amalawi azimai tizingoyang'anira nyasizi bvuto azimai timatengrka ndi kathu kochepa

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala14932 күн бұрын

    mademo mpanga komweko ku lilongwe ayi mkanya

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe39583 күн бұрын

    Hahaha AAA, Malawi poison party, Wanthu anawa votera dala, bolani ife tiri kutali zina ukamva zina Leku kamba anga mwala.

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga3 күн бұрын

    😂😂😂😂😂 zabwino zonse wachita bwino wagwidwa tiakonzere konkuno

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri17993 күн бұрын

    If what comrade is saying is the truth,then Chakwera must be the worst president in Southern Africa.

  • @BitonFred
    @BitonFred10 сағат бұрын

    😂😂😂😂

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga3 күн бұрын

    Malawian kuwopa too much that’s why amakonda kulepheresa mademo so don’t tell us ngati muziwona zoti sizingatheke zochita mademo! Aaa why amakonda kulepheresa mademo

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga3 күн бұрын

    Limpopo FM ndi 1

  • @SeephyMfaume
    @SeephyMfaume3 күн бұрын

    MCP Pamtumbo pawo ndithu

  • @walesbanda4959
    @walesbanda4959Күн бұрын

    😂😂😂

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt2 күн бұрын

    Chakwela ndikanankhala kuti ndimatha ufiti ndinakamchosa ineyo manyi akee anthu

  • @EllenPhiri-xt8pt

    @EllenPhiri-xt8pt

    2 күн бұрын

    Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma3 күн бұрын

    Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq3 күн бұрын

    Koma chakwera anthawa wauyouyo mbwiyache.

  • @HappyMaolid
    @HappyMaolid3 күн бұрын

    It's time to figh now,osagona

  • @user-xi2vo4gc4u
    @user-xi2vo4gc4u3 күн бұрын

    Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg3 күн бұрын

    Chakwela ndigalu kwabasi

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq3 күн бұрын

    Asilikira akumalawi ndi wopusa.

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana3 күн бұрын

    8:30 musova mcp ,mulithawa dziko mukulifuna

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE3 күн бұрын

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala14932 күн бұрын

    zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa

  • @HalisonSolomon

    @HalisonSolomon

    2 күн бұрын

    Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera

  • @CharlesMateya
    @CharlesMateya3 күн бұрын

    Following

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto3 күн бұрын

    😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @user-td6qe4gr6w
    @user-td6qe4gr6w3 күн бұрын

    Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa

  • @GospelSoldiers-sr7np

    @GospelSoldiers-sr7np

    2 күн бұрын

    Ndipo kwambili eni dziko kumangosaukirabe

  • @FrankMulela-qt1wi
    @FrankMulela-qt1wi3 күн бұрын

    Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko3 күн бұрын

    Atanyiwa pathako pako

  • @ShentrycChinoko

    @ShentrycChinoko

    3 күн бұрын

    Yess

  • @ShentrycChinoko

    @ShentrycChinoko

    3 күн бұрын

    Zowonadi mchutsuludi chimenechi

  • @user-yc3ik9dq3x

    @user-yc3ik9dq3x

    3 күн бұрын

    Inu amenewo mungodziyankha nokha muli phee kugwiritsidwa ntchito ndi agaluwo 🥺mxieuw

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer3 күн бұрын

    Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz2 күн бұрын

    Achakwera vomelezani😂

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm3 күн бұрын

    Chakwera atha ngati Idi amin sizimuthera bwino ndithu.

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel3 күн бұрын

    Ndikut mambodza akowa Pali ine no comment ndizopusa zakozo tithana phwanga galimoto uma user ija nditha kukutumizira komaso pachikwangwani umakonda kucheza paj okay

  • @victorauwana7258

    @victorauwana7258

    3 күн бұрын

    Mwapemphedwa kutu mupange comment?

  • @NizigiyimanaChantal-c2p

    @NizigiyimanaChantal-c2p

    3 күн бұрын

    😢

  • @SoundmasterElectrical

    @SoundmasterElectrical

    3 күн бұрын

    Mbudzi iwe uthana ndindani usawone ngat ndife ogona wamva panyo pako

  • @MaryNyirenda-nq3mh

    @MaryNyirenda-nq3mh

    3 күн бұрын

    Chigawenga iwe chimunthu chopanda phindu chitsilu ulibe manyazi mulungu akukanthan

  • @LukaThawe

    @LukaThawe

    3 күн бұрын

    Anthu achoka Kuti iwe nawendimbuzi kwambiri ukukofuna kusokoneza amalawi ,chifukwa amalawi ndiopepera kale ndiye azikuvera nyasi zako sata yako

  • @user-tm3zh5zk4t
    @user-tm3zh5zk4t3 күн бұрын

    Paja ninakuwuza kale kuti upite kumalawi mabodza akowo mtanyiwa yiweyo niamene ukumasokoneza anthu infe timapeleka ulemu kwa boni kalindo osati mbuziyiweyo ayi

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko3 күн бұрын

    Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko3 күн бұрын

    Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi

  • @FrancisDay-br7xb

    @FrancisDay-br7xb

    3 күн бұрын

    Pain MCP

  • @user-yc3ik9dq3x

    @user-yc3ik9dq3x

    3 күн бұрын

    Dzidyani za magazizo. Mulungu akulangani nkhuku inu

  • @AminahMussah

    @AminahMussah

    2 күн бұрын

    ukatelo watumidwa nda nzako akuphawo

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE3 күн бұрын

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe