Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe
@MikeKanyaza-bm5tp13 күн бұрын
Osamasowa antanyiwa please 😊
@GanizaniKamvazaana13 күн бұрын
Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA
@DavidJackson-ox4xm13 күн бұрын
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
@esaMoha-dm4kj13 күн бұрын
ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always
@meganabigail-ye7fw13 күн бұрын
Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu. Ondikumbila dzenje agwelamo yekha. Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.
@VaseleMsiska13 күн бұрын
Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.
@JosephHill-fy1bb13 күн бұрын
We are here already comrade ✌️
@MaxwellumbiriLumbiri
13 күн бұрын
Zakwanitsa tate akuona zonse
@MaxwellumbiriLumbiri
13 күн бұрын
Yehova akuona chilichonse afa yekha
@zimmekapachika678413 күн бұрын
Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura
Muzina la yesu christu achakwera kungopha modzi muziona ndithuuu😭😭😭😭
@AnusaNkhoma13 күн бұрын
Waying'alura kuno mtanyiwa
@MebleNgulinga-hi6rg13 күн бұрын
Oh Lord have mercy on us Malawians Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu
Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya
@user-wl4nd7ic1s13 күн бұрын
GOD bress u Mr mtanyiwahhh!!
@user-hg5oj3ko1o13 күн бұрын
Iiiii ndiye atipha tonsetu
@originalblack10012 күн бұрын
aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@kondwaniwhite287113 күн бұрын
Nice 👍 nndinakusowani
@HusseinMoffatt-mi1fl13 күн бұрын
Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu
@GraceZumazuma10 күн бұрын
Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko
@augustinechibbalazi889713 күн бұрын
My gracious heavenly Father have mercy on Malawians
WHEN YOU ARE PLAYING THE MUSIC OR OTHER VOICES WE CAN NOT HEAR CLEAR PLS TELL YOUR TEACHINIAN
@ZionekaMember13 күн бұрын
Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa Kut chachitika chan
@cynthiakananji160813 күн бұрын
Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.
@Extratremendouszeus13 күн бұрын
Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅
@AminahMussah13 күн бұрын
anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa
@CharlesPhiri-ds1rk13 күн бұрын
Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa
Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa
@user-lj7lm6ly7z13 күн бұрын
Palibe so kuphedwa apa Inu ambuye akukutetezerani a ntanyiwa ndi azinzanu onse timakuikizani mmapephero
@AnaffSayamika-uh6vg13 күн бұрын
💥💥💥💥
@user-wo2kh4xe8q13 күн бұрын
futi yomwe akufuna aphere azawo apita ndi iwoo mulungu simunthu
13 күн бұрын
Okupha nayeso azafa... palibe kuopa mcp ndi azitsogoreli ikagwere
@AminAbbass-xc4qk13 күн бұрын
🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@PetroMatias13 күн бұрын
👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍
@PatrickMtira13 күн бұрын
Tinakusowani Boss
@VanessaGwangwa13 күн бұрын
❤❤
@user-hj5oq5jm9v13 күн бұрын
Ing'alureni fadah
@edmorswalley666313 күн бұрын
Mulungu sichejemu auzeni
@user-bw2cv9sd7x13 күн бұрын
a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa
@user-mv8vy3ht3n13 күн бұрын
God is able
@user-oq5rg5mz7q13 күн бұрын
Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji
@ChiefJustin-cl8jl13 күн бұрын
Nthatha za njaladi
@ArnoldBinali13 күн бұрын
Koma chakwela eeee
@LouisKanje13 күн бұрын
Chilango
@ZionekaMember13 күн бұрын
Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu
@Uncle_B26513 күн бұрын
Komatuu tili pa ululu eeeeee
@hanifahmponda871113 күн бұрын
MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU
Пікірлер: 83
Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe
Osamasowa antanyiwa please 😊
Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always
Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu. Ondikumbila dzenje agwelamo yekha. Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.
Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.
We are here already comrade ✌️
@MaxwellumbiriLumbiri
13 күн бұрын
Zakwanitsa tate akuona zonse
@MaxwellumbiriLumbiri
13 күн бұрын
Yehova akuona chilichonse afa yekha
Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura
Ndikamava kanyimboko ndiye ndimasangarara ndimazdziwa kuti chirungamo chirimunjira
I salute Comrade ntanyiwa,, ndiye titani Comrade amalawi tiyen titengen gawo tipemphere kwambiri
The best Radio station in the world. Big up Comrade
Koma dziko lathu tinalozedwa bas zoona kumuopa chakwela kamuthu kamodzi tiyen tipange ngat ku Kenya please zausilu zikuchitikazi
Loud n clear from Johannesburg
Pemphelo rathu ndichida chomwe timangonjesera adani zenje akuwakumbira athu onseo agweramo onse akupereka mayina awathu osarakwa imfa akunenayo atamwalire ndiwo 2025 isanafike mulungu akuona
Ntanyiwa wadzuka bwanji kumeneko ifetu tilibwino ndithu tiye nazoni
Comrade am 100% support u always ing'alure fadah
Angozinamiza anthu onsewa Mulungu sangalore kuti aphedwe.
I ❤ this program
Long liveNtanyiwa
Muzina la yesu christu achakwera kungopha modzi muziona ndithuuu😭😭😭😭
Waying'alura kuno mtanyiwa
Oh Lord have mercy on us Malawians Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu
Amalawi kumudziko tadzukani mumchotse chakwelayo......dziko silake
Atchela kumawa nkhangazaona anyanayo
long live Mtanyiwa here in capetown i support you❤
You are our head lamp Mr Mntanyinya tipempha mayiko ena atithandize kuchotsa president okuphayu
😂😂😂😂😂 nde mcp itsala yokhatu nanga anthu osewo akawapha ku opposition kudzakhala ndan mcp muzitenge bwino zithuzi vuto mwakhalitsa padzuwa muli kotsutsa😅😅😅😅😅😅😅😅
Antanyiwa nlipo abale osamasowa chonchi
Lord have Mercy
Iwe chakwela Mano kuyipa ngati nyemba ya pa nyini ya Monica wako uyo usatibowe ife
Okhesa mwazi yehova sakondwera naye olo nyama ikatero Mulungu amapereka Chicano paizo
Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu adalise wina aliyese astaguffllal yha Allah thallah brother
Comrade ntanyiwa ..great man ft kalindooooo
Achakwera ku state house atawako posachedwapa
We're always with you buddy Ntanyiwa.♥️🔥🔥
We love you comrade ..tell us more
Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya
GOD bress u Mr mtanyiwahhh!!
Iiiii ndiye atipha tonsetu
aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Nice 👍 nndinakusowani
Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu
Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko
My gracious heavenly Father have mercy on Malawians
Ndipo galu ameneyo siomuchula kuti mr iyayi chakwera akufuna amalawi atani 😂😂😂
I salute you comrade!
WHEN YOU ARE PLAYING THE MUSIC OR OTHER VOICES WE CAN NOT HEAR CLEAR PLS TELL YOUR TEACHINIAN
Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa Kut chachitika chan
Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.
Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅
anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa
Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa
Mr Chakwera pamtumbo panu ndinthu
Nsembe yomwe inapelekedwa zaka zapitazo ya ufulu chakwera waipangisa expire akufuna mwazi wina otchuluka
Komatu kulimbana ndi aNtanyiwa kuzipusisa ndithu. Awa ndi akatundu omangidwa ndizitsulo. Mbambande.
Lipopo ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤❤❤❤
Zosatheka athu APHA Aja sanakwane BaiBulo Linati okumba zenje agwelemo yekha ndiiiiiiithu amene watenga gawo lokupha athu amenewa agweramo okhaaaaa ambuye invani simunawalenge athu Kuti azuzike paziko pano inu mukule Ife tichepe
Lipopo support ❤ 💙
Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa
Palibe so kuphedwa apa Inu ambuye akukutetezerani a ntanyiwa ndi azinzanu onse timakuikizani mmapephero
💥💥💥💥
futi yomwe akufuna aphere azawo apita ndi iwoo mulungu simunthu
Okupha nayeso azafa... palibe kuopa mcp ndi azitsogoreli ikagwere
🎉🎉🎉🎉🎉🎉
👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍
Tinakusowani Boss
❤❤
Ing'alureni fadah
Mulungu sichejemu auzeni
a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa
God is able
Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji
Nthatha za njaladi
Koma chakwela eeee
Chilango
Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu
Komatuu tili pa ululu eeeeee
MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU
Wina watukwana chakwera uku 😂😂kzread.info/dash/bejne/iYZ4zbNxo8KZZM4.htmlsi=r_3Qm9tNpQwXfR0D