BON KALINDO 8 JULY 2024 BIG MAN WAFIKASO PA MONDAY

Пікірлер: 74

  • @JosephMichael-x7v
    @JosephMichael-x7v13 күн бұрын

    Kungotiphera bon kalindo muzakhala nkhondo mmalawi

  • @MacleanKwacha
    @MacleanKwacha13 күн бұрын

    Our president komaso mukudziwa kuti kulilongwe kuno kukuyenda anthu akuitanisa chiphaso chauzika,kumat akuchita kalembera oti pakamachitika zitukuko zaboma asamavutike kupita kwamfumu azingotenga mukaundula?Tifufuzileni mutiuze zoona.

  • @JamesEuginio
    @JamesEuginio13 күн бұрын

    Bwana kalindo mugwirane mana ndi comrade mtambo chifukwa iwowo alibe tulo komaso ngati Malawi first itafuna kuima pa zisankho Malawi ambiri tikondwa inu bwana kalindo tikuona usogoleri mwa inu chifukwa kumuyankhulira mphawi yemwe alibe mawu sikophweka koma kuyankhulira olemera omwe pamapeto pake munthu amalipidwa choncho inu bwana timakupemphererani mulungu agwirise ntchito inu kuti satana achite manyazi kuno kumangichi makanjira

  • @EllenPhiri-xt8pt

    @EllenPhiri-xt8pt

    12 күн бұрын

    Bon kalindo and antanyuwa bolaso munakangoimila u president that anthu amenewa angokhala chete akusekelela zomwe chakwelayu akuchitazi😢😢😢

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt12 күн бұрын

    Keep it up mr DC

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w13 күн бұрын

    UTM, AFORD, DPP and UDF must make an alliance and win government, Chakwera out, useless government.

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    13 күн бұрын

    Koma otsutsa akewa makape

  • @MikeArthur-jd2ij

    @MikeArthur-jd2ij

    13 күн бұрын

    You are right

  • @JinishgiftMbalaka

    @JinishgiftMbalaka

    12 күн бұрын

    Km za alliance zikumabweresa udani mmmm better aliyese azpangile yekha

  • @user-pv9uk6sc3w

    @user-pv9uk6sc3w

    12 күн бұрын

    @@JinishgiftMbalaka vuto payekha payekha sangafike 50+1 yomwe yikufunika.

  • @MastonStanley

    @MastonStanley

    11 күн бұрын

    Maganizo abhoo

  • @EVERSONGalatia
    @EVERSONGalatia13 күн бұрын

    UTM PDP AFORD CFT PP and UDF must make alliance

  • @HenryKeyala
    @HenryKeyala12 күн бұрын

    Loud and clear

  • @DavieMuziwo
    @DavieMuziwo13 күн бұрын

    Best DC

  • @watsonmhango8794
    @watsonmhango879412 күн бұрын

    Zoona Mr DC president wa Anthu osauka

  • @taneesharkamwendo8710
    @taneesharkamwendo871011 күн бұрын

    president wanga wanga vote yanga

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o13 күн бұрын

    Bon kalindo machine,, koma Aford, UDF, Aford komaso DPP khalan maso

  • @SigoMw
    @SigoMw13 күн бұрын

    Onse mapulezidenti opuma Ali nkhwinthi ngati akumetetsa kwa kaondo ku 36, akupweteketsadi mtima chifukwa palibe akumveka kupatula inu akalindo. Ma radio ndi ma TV pa Malawi kulibe ife tikudalira inu akalindo, amtanyiwa ndi Wa bakili muluzi.

  • @BlessingswazaDyress
    @BlessingswazaDyress13 күн бұрын

    Fantastic DC

  • @FaithDonald-ts2pp
    @FaithDonald-ts2pp12 күн бұрын

    The dc❤

  • @peterchimatiro4093
    @peterchimatiro409312 күн бұрын

    The DC

  • @voicedumathindwa
    @voicedumathindwa13 күн бұрын

    Mnthuyi ambuye amdalise akumenyadi ufulu

  • @JefulyPesulo
    @JefulyPesulo13 күн бұрын

    Keep up DC

  • @MwanundaEmmanuel-nb5dk
    @MwanundaEmmanuel-nb5dk13 күн бұрын

    Keep it up the dc

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli13 күн бұрын

    This government must go out we don't need this mcp

  • @IssahAluba
    @IssahAluba12 күн бұрын

    ndipo Pena gati useke president mpaka kuligawa dziko ai zikomo kuphandoko mulungu akudalitseni

  • @trustchiwalo9225
    @trustchiwalo922513 күн бұрын

    Eiish!!

  • @Chiso2019
    @Chiso201913 күн бұрын

    Ine koma opposition yi.....imamunamizila kut akusokoneza ndi anankhumwa,nankhumwa anakuchokeraniko ife timayesa ziyamba kubebano koma manyaka okhaokha

  • @user-pn8lc7vq8b
    @user-pn8lc7vq8b13 күн бұрын

    Kodi mesa a UTM anachita kuchokera ku zipani opositionizo? Akukolola zimene anafesa amenewo.

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje13 күн бұрын

    Abale a dpp mukutani

  • @user-ri8em6my2e
    @user-ri8em6my2e13 күн бұрын

    Koma azipani zotsutsa tapanganipo kanthu inuuuuuu Bon Kalindo ndiye akuyesetsa kukutsinani khutu ndipo CHAKWERA ndinduna zake akufuna kupitiliza kuba mubomali😢😢

  • @AndrewKonondo
    @AndrewKonondo13 күн бұрын

    Bwana DC, ipatseni moto tili nanu, akapangaso chibwana zodzabera chisakhocho tidzangomenyanapo mmalawi muno, ndi mbuzi za anthu

  • @ZettaImuranYunusu
    @ZettaImuranYunusu13 күн бұрын

    Mr dc dziwani Izi... Zipani Izi DPP UDF AFORD ADD onsewo a kupanga zinthu zoti ayimile mu 2025 Ndipo inuyo musakayikenso ai

  • @user-wx1ri9xv3f
    @user-wx1ri9xv3f12 күн бұрын

    🙏🙏🙏🙏🙏

  • @ashrafffaque
    @ashrafffaque13 күн бұрын

    Machine athu The DC

  • @siphiwenyirongo2568
    @siphiwenyirongo256813 күн бұрын

    Mmm

  • @user-bo1kt3nq6j
    @user-bo1kt3nq6j13 күн бұрын

    Matiimilila DC Landilani ulemu wanu

  • @MuneerYusuf-py1lz
    @MuneerYusuf-py1lz13 күн бұрын

    Komadi afasa kwambiri azuzeni

  • @RobertKanaphwatiwa
    @RobertKanaphwatiwa13 күн бұрын

    Ulemu wanu mr Kalindo tulutsani ndondo nthawi yakwana bwana

  • @MikeArthur-jd2ij
    @MikeArthur-jd2ij13 күн бұрын

    Thus our DC 🔥

  • @AliciaMaphanga
    @AliciaMaphanga13 күн бұрын

    Powerful the DC❤❤❤

  • @PemphaChina
    @PemphaChina13 күн бұрын

    From njedza village

  • @user-xt5in6nu2h
    @user-xt5in6nu2h13 күн бұрын

    Ubwino wake achewawo ali m'boma

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z13 күн бұрын

    Awawa achoke a MCP

  • @MacleanKwacha
    @MacleanKwacha13 күн бұрын

    Ineyo ndkunena pano ,dzulo laliwisi moti akazanga achita kukana kuti mwina akufuna kubwera zisankho

  • @user-wu8kp7ui5j
    @user-wu8kp7ui5j13 күн бұрын

    The DC 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x13 күн бұрын

    The DC🔥🔥🔥

  • @LameckBanda-ph2nh
    @LameckBanda-ph2nh13 күн бұрын

    The DC ❤❤❤❤

  • @user-mv1wg2qd6i
    @user-mv1wg2qd6i13 күн бұрын

    Machine ❤❤❤DC

  • @user-rm2xv8ys1i
    @user-rm2xv8ys1i13 күн бұрын

    ❤❤❤❤

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi13 күн бұрын

    The DC 🔥💗🔥

  • @ThomasMlowoka
    @ThomasMlowoka13 күн бұрын

    DC 💪💪

  • @SmilingFishingRod-zc4wx
    @SmilingFishingRod-zc4wx13 күн бұрын

    Nkhani yonveka bwino Nanga a Mwananveka muli kwanikiii? Monga inu.

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp13 күн бұрын

    Dc ❤❤wi love you

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope13 күн бұрын

    Munthu uyi mulungu azimutetedza until mcp out of power,,,,Dpp ,,Afford,,udf,,,,why are you not listen to kalindo

  • @SamsonWyson
    @SamsonWyson13 күн бұрын

    Dccccc

  • @mathewsnachuma8086
    @mathewsnachuma808613 күн бұрын

    Boooooooooooorn kalindoooooooooooooo

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg13 күн бұрын

    KING

  • @osaukaonjoya
    @osaukaonjoya13 күн бұрын

    Tokotani akolo

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d13 күн бұрын

    Koma abambo inuyo mukuyesesa kunja kukacha mulungu apitilize kukusungani ndi moyo koma ndimati ndi pephe inuyo simungambise chipani chani ndi achina m,tanyiwa bakili TV tikuvitelanitu chifukwa mumaoneka ndinu amaso m,phenya

  • @RachealHarawa-xc9gs
    @RachealHarawa-xc9gs13 күн бұрын

    Mulindimfundo zabwino

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb13 күн бұрын

    Azibambooooo

  • @DenisJamu
    @DenisJamu13 күн бұрын

    Fadah

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda871113 күн бұрын

    Ife UTM tsitiwelengela kuti chipani chotsusa ayi ichi ndi chipani cholamula boma ndi MCP itsewo alephelela lidzodzi kuyendetsa dziko NSONO A MCP KAYA APATSA NDALAMA KAYA TSAPATSA NDALAMA IDZO ZAWO AKUDZIWANI koma munthu wadzelu nsangasalale ndi munthu amene wapha bambo ako ndikumakuwudza kuti ndikutsamalilani bwino ana inu pomwe bombo wawoyo mumalephela kumutsamalila loko anawo bambo wawo ali moyo msimawathandidza UTM mistake yanu ndiyimene umalidze chipani chanu ndanena kuti kumalidza off course ifa ya CHILIMA yachepetsa mphamvu zanu mwina nsimukudziwa NDE MCP AMALAWI YAKWANO NDE OTSUNSA BOMA CHIHANA MUTHALIKA MAYI PATELO ATUPELE KALWUWA NDI ENA OTSE MUTSAKHELE CHETEEEEE KHALANI PAMODZI NDIKUPANGA CHIGANIDZO KUTI UKAMBELE MBELE AKUPANGANI A MCP NDI ARP muchita bwanji chifukwa kungopatsa pata kawili MCP kukhalatso boma amalawi OCHULUKA TiKUFA KOMATSO ULAMULILO UWU WACHIPANI CHIMODZI UDZAKHADZIKIKANO NDE MAMVUTO AKULU KU MALAWI

  • @user-sr4fe5bb2w
    @user-sr4fe5bb2w13 күн бұрын

    Pita iweyo ku khothi ko Mesa umati ndiwe president

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    13 күн бұрын

    Kape ukuti chani

  • @user-ej6tw9do2r
    @user-ej6tw9do2r13 күн бұрын

    Akufuna udindo uyu aaaaaa Popeza adamumana udindo. ndiye akuona kut aDPP azamupatsa?

  • @JamesEuginio

    @JamesEuginio

    12 күн бұрын

    @@user-ej6tw9do2r ndiye ukuganiza kuti what way followard if akalindo akufuna udindo iwe iwe tanena chabwino mchiti?

  • @DavieMuziwo
    @DavieMuziwo13 күн бұрын

    Best DC

  • @EmieMtendere
    @EmieMtendere13 күн бұрын

    The DC

  • @ISSAHKAINGA-zz1op
    @ISSAHKAINGA-zz1op13 күн бұрын

    ACHALUME KUTI CHUBWIIII

  • @FrancisGama-qb7ze
    @FrancisGama-qb7ze13 күн бұрын

    The DC

  • @SemuKaunda
    @SemuKaunda13 күн бұрын

    The DC