Limpopo FM katswiri Ntanyiwa watiuza dzina la vice president watsopano uja tazidziwa nawo

Пікірлер: 71

  • @marryphili5419
    @marryphili5419Ай бұрын

    Achakwera zeru mulibe ndani sakuziwa Kuti ndinu munapha achilima manyazi mulibe

  • @wonganichakakanyirenda3299

    @wonganichakakanyirenda3299

    Ай бұрын

    Awuzeee

  • @ChrispoGawani
    @ChrispoGawaniАй бұрын

    😢 Malawi wavunda basi azisogoleri saganizanso nkomwe za anthu osauka onani kwacha pano momwe yathera Limpopo ndi massive keep it up we Love Limpopo fm

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4yАй бұрын

    Keep it up broo. Chakwera munthu wakupha uyu.Wapha abale athu ngati agalu

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gzАй бұрын

    Angosowa zochita a mcp wo

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533Ай бұрын

    We don't trust MDF and malawi Police for internal security , As Malawians we will defend ourselves from this evil government of MCP . ALLAH will protect every malawian .

  • @user-lf6qf2tw5o

    @user-lf6qf2tw5o

    Ай бұрын

    True

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3qАй бұрын

    Kmatu chakwera manyazi akhare nawo akapita kuja ndikukonda ndege kwakekuja azikamusala azungu

  • @yasitafuphiri-nw2he
    @yasitafuphiri-nw2heАй бұрын

    Kodi limpopo fm nkhani zaku malawi basi 😮.?

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2czАй бұрын

    Chakwela tulapansi udindo mwansanga

  • @GenialaChalera
    @GenialaChaleraАй бұрын

    Mzosatheka zimenezo ukukamba zosaveka galu iwe noman akufuna mpando

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomonАй бұрын

    Iwe ukati ntanyiwa chisiru wakulakwira chani cadet iwe, chirungamo akuyankhula

  • @user-kw7wr4kq9w
    @user-kw7wr4kq9wАй бұрын

    That's why you mislead people from Ntcheu and they got killed, it's a shame

  • @ChrispoGawani
    @ChrispoGawaniАй бұрын

    Congeresi ndiyokupha kuyambira kale koma pano Malawi wasukusula zivuta kwambiri

  • @babranzima8120
    @babranzima8120Ай бұрын

    Azunguladi muthu mwazi wamuthu uwazunguza chakwera ndi mbuzi pamodzi ndinduna zake zonse

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6yАй бұрын

    Chakwela you mast go

  • @HagEva1
    @HagEva1Ай бұрын

    Akuazunza ngati mmne anazunzila marefugie!!😢😢

  • @davidkayangemakala7957
    @davidkayangemakala7957Ай бұрын

    Enanu mukulipilidwa fees ndi MCP Ena mukudyesedya ndi MCP yomweyi chifukwachake yifa yachilima cmakukhuzani musadane ndi ntanyiwa

  • @user-lf6qf2tw5o

    @user-lf6qf2tw5o

    Ай бұрын

    Zoona

  • @Alliechamolie
    @AlliechamolieАй бұрын

    Kodi mukamadana ndi social media ,msikulomwe ndige inasowa social media inakambakut achilima amwalila pemene amboma amakana kenako mumamvomeledza Mawa wake , ndiye athu adzimvela dziti

  • @user-is3jt9el8l
    @user-is3jt9el8lАй бұрын

    Tifufuzireniko za magalimoto alowa munowa

  • @MercyNyachi
    @MercyNyachiАй бұрын

    Mcp is 😈 👿 indeed I hate this party with my soul😢

  • @alimamandra7115
    @alimamandra7115Ай бұрын

    😊😊😊anhaino munthu amwalila sapanoyapa atha thathtu muakhaly osachithe mwafuna muina kuthy azakhale vc presidente a bala azaganizia chyani.

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8oАй бұрын

    Ayenera amangidwe

  • @user-jb5yb9wq3y

    @user-jb5yb9wq3y

    Ай бұрын

    Pamtumbo pako

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9twАй бұрын

    Musileni mulungu aweluze monga mwantchito yake pali mwazi wamunthu sipanama ayi chilima ayakha yekha mulungu umboni akuwuziwa

  • @charlesbanda7594
    @charlesbanda7594Ай бұрын

    Kodi anthu mudana ndi chilungamo bwanji isiyeni Limpopo FM a lone

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517Ай бұрын

    Koma aganyu achakwera muli mmabvuto amakutumani ndani kuti mudzvera limpompo

  • @ChawingaMwaseteza
    @ChawingaMwasetezaАй бұрын

    Olo utikwane chosangalasa ndichoti ukumusatila bwino ntanyuwa..zilibwino udziwadziwitsa anyapapi akowo zomwe akulankhula,,ntanyiwa emweyooooooo

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023Ай бұрын

    Mulungu akuona misozi yathu

  • @user-wg8tp8in1v
    @user-wg8tp8in1vАй бұрын

    Apa zikugwirizana ndi zomwe zatuluka?

  • @SaidiMilaji-dk8sr
    @SaidiMilaji-dk8srАй бұрын

    Tikulila CHILIMA ife misozi ilikugwela mmimba mmesa mumati olila samutseka pakamwa?

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6noАй бұрын

    Uyambe ndiwe ukolozera motowe, adakulakwira chian a president ?

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2czАй бұрын

    Adad oyeeeeeeeeee❤❤❤❤❤

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6noАй бұрын

    Uyambe ndiwe

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwelaАй бұрын

    Malawi kuimba kwa late matafale

  • @PetroMatias
    @PetroMatiasАй бұрын

    Sizigwilizana zimenedzo

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWOАй бұрын

    Mmmmm

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gyАй бұрын

    Usatana wa chakwera wafika popenga nawo

  • @EmmanuelMarko-lf1oz
    @EmmanuelMarko-lf1ozАй бұрын

    Wabodza iwe. Sitingakunvereso iwe.

  • @alfredchigwankhu7355
    @alfredchigwankhu7355Ай бұрын

    iwetu uimbidwa mulandu obweretsa chisoko ezo mdziko

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6rАй бұрын

    Chisilu chamunthu mmalo moti mzigwira ntchito ku o ku sa nfiwe chisilu kwabasi

  • @user-yv3jp3it2t
    @user-yv3jp3it2tАй бұрын

    Nonse amene akuyikila MCP kumbuyo ndinu athu opanda nzelu mukuvuti zomwe akubazo simudya nawo musiyeni Ntanyiwa alakhule zomwe akudziwa mukati umboni mukufunatso umboni wina Musamakhale athu opepela wake up guys dziko ndi lathu ili

  • @ChaloseMoyenda
    @ChaloseMoyendaАй бұрын

    Changu udindo pansi😂😂😂

  • @AticksonRevesonSemele-lk3du
    @AticksonRevesonSemele-lk3duАй бұрын

    Mmmmmmmmmmmmmmmmmm koma Nde malodzatu

  • @user-uz2wm9uq4g
    @user-uz2wm9uq4gАй бұрын

    Apenga zenizeni sanati avula

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    Ай бұрын

    Atola zosipe

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3qАй бұрын

    Anthu akucheu mukaona anthu akubwera kuzamanga mp wanu uko.muzawagendeso musawasekerere ayi koma chakwera niusataniki wake osazamuvoteraso ayi nimunthu oyipa chakwerayo bwanji iyeyu osamumanga boni karindo akurephera kumumanga bwanji

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2czАй бұрын

    Chakwela galu iwe

  • @JhdaLifi-vu9sd
    @JhdaLifi-vu9sdАй бұрын

    Limpompo fm

  • @alimamandra7115
    @alimamandra7115Ай бұрын

    Iweo simulila simukhaiankhula chonchi?

  • @isaacedsonmabulesi
    @isaacedsonmabulesiАй бұрын

    asamangidwe alakwachani

  • @FrancisDinala
    @FrancisDinalaАй бұрын

    Nde mwat azunguso akuziwa eti ine ndikuona kut mwapanga edit za mzunguzo sure ndi Edit iyi

  • @Alliechamolie
    @AlliechamolieАй бұрын

    Agalu awa mcp

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4wАй бұрын

    Mmmmm ,masiku ano kulibe zomangana chisawawa ABUSA mwatni ?? ADAD sadaphepo MUNTHU ,muziwona a MCP, anthu amakonda MUNTHU wabwino 😂😂😂😂

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumaniАй бұрын

    adadi❤❤❤❤❤❤

  • @Stewartchikoja
    @StewartchikojaАй бұрын

    Atiputa angoni dala

  • @user-tu8sv2pu9z
    @user-tu8sv2pu9zАй бұрын

    😂😂😂

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dhАй бұрын

    Wachamba iweti mesa wenkha umati avotela bushiri anapikisana ndinankhumwa lero ukuti chidati malunga wankhuta batata eti

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    Ай бұрын

    Wachamba ndiwe ukumvera zosakukonda

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6noАй бұрын

    Eyaa apanga bwino chifukwa zikuonjeza , kunyoza , kutukwana , si zooona , malo mopempherela wakufayo , pano mwapanga zomangotukwana , ayi zaonjeza koma ,

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    Ай бұрын

    Kupanda kumumpha anthu anakatukwana

  • @zebronchipate7297
    @zebronchipate7297Ай бұрын

    Wapala

  • @PreciousChiphwanya
    @PreciousChiphwanyaАй бұрын

    Asiyeni awamange, sadzaluza okha mlanduwo, ndi nkhani yopanda umboni imeneyo, chifukwa adzawauaza kut ndikufuna mundipatse umboni kut ndine amene ndinawatuma give me umboni ogwirika video yake y tione kut ndinawauza anthu kut adzikuwa, at the end Boma lidzapezeka kuti likuluza ndalama zankhani nkhani kulipira.

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8oАй бұрын

    Chitsiru Cha munthu ntanyiwa

  • @BrotherPaul-ln2ld

    @BrotherPaul-ln2ld

    Ай бұрын

    Zoonadi mmm. Mpaka kutiulula chonchi? Komanso MCP yathuyitu ikuonjeza mmm

  • @user-im7sc2my4w

    @user-im7sc2my4w

    Ай бұрын

    Mwanama ,walakwanji

  • @BeneditoMartinhoAlbano-yc9de

    @BeneditoMartinhoAlbano-yc9de

    Ай бұрын

    Nose a mcp simulibwino wakuchulukirani usatana

  • @user-nf3ik3ff6y

    @user-nf3ik3ff6y

    Ай бұрын

    Iwe ulibe zelu Chakwela you mast go

  • @user-nf3ik3ff6y

    @user-nf3ik3ff6y

    Ай бұрын

    Mutanyiwa amatiuza Zoona

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4yАй бұрын

    Keep it up broo. Chakwera munthu wakupha uyu.Wapha abale athu ngati agalu