ZAYAMBIKA TSOPANO/ TIONA ZINTHU CHAKA CHINO.

Пікірлер: 29

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah8 күн бұрын

    Chakwera tell Malawian gets money for rooting compain 2019 ngati simuulula anthuso zangaulule

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d8 күн бұрын

    Ambuye ndikupempha please mtengeni chakwera afe asanamalidze Malawi please please

  • @user-uh5ef4cr8d
    @user-uh5ef4cr8d8 күн бұрын

    First MCP and chakwela where did he gets Money for rooting compain in 2019 he must tell Malawian

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g7 күн бұрын

    Mbewu zokhazo tengo ufike pa k1000

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms7 күн бұрын

    Mr a chatsika 2025 chanu palibe samalani akulu

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms7 күн бұрын

    Boma kugula chimanga kwa alimi and then azigulisa kunja

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p8 күн бұрын

    Ok ndiyeoyambakuulula ankhale palipanoyo

  • @user-ii2sh1mz3r
    @user-ii2sh1mz3r8 күн бұрын

    Ziwani Kuti mau amalenga , samalani ndi kamwa yanu iyo a Richard Chimwendo Banda ,

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovita8 күн бұрын

    ndalama zomwe azikhale ng,oma Ritchard chimunthu kunkuyu chitchyola ndi apresident akumafupa anthu kuwatuma azipanga zosayenela akumazitenga kuti

  • @jameskachulu8141
    @jameskachulu81415 күн бұрын

    Ku family ya sadc miya

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh8 күн бұрын

    Wayankhula ndi chakwale opusa iweti a chaima ndi chakwera zikugwilizina

  • @lungisanishezi1023
    @lungisanishezi10237 күн бұрын

    Zimenezi zingathandize chani guyes?

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu8 күн бұрын

    Aaaaaa zaka zingati zakapeni izi zoputsitsa athu

  • @GrantYohane-zd4qy
    @GrantYohane-zd4qy7 күн бұрын

    Koma boma kagulidwe kake ka chimanga aaa ku admark amafunatu chotsuka. Koma mbewu sabweletsa ya chimanga chimene amafunachi.

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu8 күн бұрын

    Aaaaamugulila ndani chimanga palibe 2025 tikumanabe basi. Chimanga gulani

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp8 күн бұрын

    Dziko achakwera lakanika 4 Yes palibe chimene apanga kusowaso kamba

  • @user-ii2sh1mz3r
    @user-ii2sh1mz3r8 күн бұрын

    Kodi uni ukuti tili pa ufulu wozilamulira , Koma bwanji nthawi zonse tikudalira chuma kuchokera Ku maiko akunja, economically we are still colonised, politically we are dependent, but full of witchcraft , instead of serving people political leaders are busy shouting at their fellow leaders , akuti ,ine mungandifanizire ndi a Kuti , ine ndi kumtunda , muona uja ndithana naye mmmmm

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w8 күн бұрын

    Kkkkkkk mbolo zanu

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef8 күн бұрын

    😊😊😊😊😊

  • @homeremedys3748
    @homeremedys37488 күн бұрын

    Chakwela Uchenjele Ndi Nzimu wachilima ndi Ena 8 unawapha aja ndicholinga uimenso 2025, Ndalamazo Zakoma Chotani Zochita Kuphela Nanzo Anzako. Amalawi Munapusa Kwambili Izi zinachita poyela simunapangepo kanthu Only Born Kalindo Amene Amaona Zinthu Ndikuyankhulapo Ena Nonse Zitsilu

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne8 күн бұрын

    Ayambe kaye kuulura chakwera panthawwi ya campaign yake ya 2019, stupiet thinking

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo7 күн бұрын

    Km Chakwera ndi anthu ako mukubweretsa mfundo zopanda Pake, iwe mmene umalowa m'boma ndalama unatenga kut?

  • @RedeemaKachali

    @RedeemaKachali

    7 күн бұрын

    Ndipo inu

  • @FaressPatel
    @FaressPatel8 күн бұрын

    Zoopsa kwabasi

  • @Mahamudu-q6b
    @Mahamudu-q6b8 күн бұрын

    😮😮😮😂😂😂

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovita8 күн бұрын

    ndalama zomwe amaitanitsaila asilikali aku isalael ndi Rwanda akumazitenga kuti zomwe akumatumiza anyamata kokasaka atolankhani alimpopo fm ndi bakili muluzi tv akuzitenga kuti

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo71538 күн бұрын

    Iyyeyo chakwerayo ankazitenga kuti?

  • @user-nw6ie3xx8b
    @user-nw6ie3xx8b8 күн бұрын

    Leave us alone as mcp ask dpp how norman chisale got rich

  • @Eric-gb9ms

    @Eric-gb9ms

    7 күн бұрын

    Mcp yanyanya mwa mmodzi ndiweyo wakuba iwe

Келесі