Oimba omwe ananyozapo Bushiri

Музыка

anthu omwe anaimbapo nyimbo zonyoza bushiri

Пікірлер: 232

  • @sammalvitha
    @sammalvitha Жыл бұрын

    Zikomo poonera, chonde Ngat simunachite subscribe.. kumbukiran kutero ... Muchite like ...video iyi .... Zikomo

  • @muyabasamson

    @muyabasamson

    Жыл бұрын

    Akupanga sanjechabe

  • @starlonjamus

    @starlonjamus

    Жыл бұрын

    👍

  • @gordonmatsagopane

    @gordonmatsagopane

    Жыл бұрын

    1qq

  • @Dyson.chibaloh

    @Dyson.chibaloh

    10 ай бұрын

    ​@@starlonjamusHy Hy hyhy

  • @bahatichirwa7601

    @bahatichirwa7601

    10 ай бұрын

    😊😊😊😊😊😊😊

  • @harryhara6217
    @harryhara6217 Жыл бұрын

    Oyimba onse amanyoza Bushiriwa, nkhani,yake ndi umphawi. Iwowo amafuna kukhala oweruza?ine si fan wa Bushiri and i've never been. Koma sindingamamuweruze.

  • @greshammshelera5344

    @greshammshelera5344

    Жыл бұрын

    True bro

  • @peterjcndolo5644
    @peterjcndolo5644 Жыл бұрын

    I like him, he has a humanitarian motivation, big up Shepherd Bushiri. Ngati zintchito ndizonyasa kuseli let God do His of Judging

  • @judywilliams2349
    @judywilliams2349 Жыл бұрын

    That’s true, blood money. Magician full time.

  • @judywilliams2349
    @judywilliams2349 Жыл бұрын

    That’s true, Bushiri is a magician and I can’t understand how people are so brainwashed.

  • @keniekaipa1997
    @keniekaipa199711 ай бұрын

    Mbuzi iwe umanama......usiye kupanga za anthu

  • @user-tf2ri2sl5s
    @user-tf2ri2sl5s10 ай бұрын

    Thanks for your true report about the Prophet Shepherd Bushiri and his beloved wife (Prophetess... As well as the Malawian musicians who composed their music despising, criticize, or contempt the Prophet Shepherd Bushiri!!! Anyway... Only God knows... HE'S THE RIGHTEOUS GUDGE IN HEAVEN AND AND ON EARTH.

  • @kalunguhelias
    @kalunguhelias3 ай бұрын

    I've ukutiuza za bushir KT titaninaye

  • @musicoftheviolinstudios.1109
    @musicoftheviolinstudios.1109 Жыл бұрын

    zofotokoza zanu zili bwino,ndizosakolana zachindunji bwino bwino.mulipo awiri ndi big mani enake samazitchula dzina lake .

  • @yassinrashid7012

    @yassinrashid7012

    Жыл бұрын

    Mkulu wa bakili Muluzi tv

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Жыл бұрын

    Very much Best bro please ceep it up good job bro

  • @sammalvitha

    @sammalvitha

    Жыл бұрын

    I will try my best

  • @sonnymasandi1748
    @sonnymasandi1748 Жыл бұрын

    Ndayikonda so much keep up agood work

  • @AuthenticV
    @AuthenticV Жыл бұрын

    Pastor David Kalirani Amayenera kukhala pa number 1

  • @chrissjunior8342
    @chrissjunior8342 Жыл бұрын

    Proudly you my brother " nd nkhan ngat zmenez 🤟

  • @ElizaNyirongo

    @ElizaNyirongo

    Жыл бұрын

    Love it

  • @godfreybiziweck1224
    @godfreybiziweck1224 Жыл бұрын

    Ndizoonadi anamunyoza prophet shepherd bushiri

  • @gracephiri1203
    @gracephiri1203 Жыл бұрын

    Mwaitha bro muzibwelabwela

  • @ashraffmidu7837
    @ashraffmidu7837 Жыл бұрын

    Piksy didn't liar he only says the truth moreover that song of him it's my favorite song....akutithera mtundu m'malawi ameneyo...#MartseKeepRip😥

  • @NIDYBANDA-iz7xz

    @NIDYBANDA-iz7xz

    Жыл бұрын

    Pakut tilibe mphavu zopangila judge km mmmmmm

  • @jaymilazi2937
    @jaymilazi2937 Жыл бұрын

    Muzibwezerabwera ndi nkhani ngat izi

  • @fradahmakwinja3835
    @fradahmakwinja3835 Жыл бұрын

    Major one is Great

  • @JuniorAbasi-eb5ce
    @JuniorAbasi-eb5ce8 ай бұрын

    A Malawi ife tilibe ulemu Mr Bushiri zawo dzidayela khale chofunika ndi ulemu basi monga ine ndikuti ulemu wanu mr Bushiri .kodi A Malawi tinakhala bwanji munthu aliyitse akalemela.ali ndi vuto

  • @user-qk9ib7hb4l
    @user-qk9ib7hb4l9 ай бұрын

    That's very gorgeous

  • @user-gr6zh9zr9b
    @user-gr6zh9zr9b8 ай бұрын

    TNM super rige malawi

  • @thembalungani9347
    @thembalungani9347 Жыл бұрын

    proud to him man of God...enawa yakula ndi nsanje...m'nyamata ali ndi mphatso ya utumiki uyu congratulations to major 1

  • @kennethkaunda3636
    @kennethkaunda3636 Жыл бұрын

    Ndi zoona bro

  • @rasheedjaffali6674
    @rasheedjaffali6674 Жыл бұрын

    Nice one brood good work

  • @mosesjoni2542
    @mosesjoni2542 Жыл бұрын

    Best one bos

  • @TamandaniIssa
    @TamandaniIssa22 сағат бұрын

    He is still a prophet of God whether you like it or not

  • @amontchuwa6876
    @amontchuwa6876 Жыл бұрын

    Nanga iwe ukt bwanji Ine ai akuziwa ndi Yahweh

  • @yusufelliotanalidodoloooma9685
    @yusufelliotanalidodoloooma9685 Жыл бұрын

    Chimandisangalasa ndichoti bushiri utsogoleri ali nao sapsa ayii. Anthu ndie amathoka zaiye siku ndi siku. Koma mumpeza Alii pee . Iye bola ubale wake ndi mulungu uli bwino

  • @mastersubiri7934

    @mastersubiri7934

    Жыл бұрын

    Mulungu wake utii nanu kutengeka ndi zili zonse

  • @tichezechitukula5352

    @tichezechitukula5352

    Жыл бұрын

    @@mastersubiri7934 Mwandifusilako boss!!

  • @KatsekelaHassan
    @KatsekelaHassan2 ай бұрын

    Am still love bushiri

  • @eliasleonard9448
    @eliasleonard9448 Жыл бұрын

    Moyo ndikamozi ndagwirana ndinamdingo

  • @AffectionateFoliage-gh6bf
    @AffectionateFoliage-gh6bf5 ай бұрын

    Keep it up

  • @NavitchaBanda
    @NavitchaBanda23 күн бұрын

    Mukasowa chati usamalimbane ndi man of god

  • @JenniferRonnex
    @JenniferRonnex2 ай бұрын

    Haji❤

  • @ibulakimu9380
    @ibulakimu9380 Жыл бұрын

    Enewa ndi zanje

  • @user-tu6ph6wh2z
    @user-tu6ph6wh2z11 ай бұрын

    I like him he has a humanitarian

  • @KimuBanda
    @KimuBanda3 ай бұрын

    Tnx for the good report

  • @MercyMachipisaMunthali
    @MercyMachipisaMunthali2 ай бұрын

    Tose tapachalu chapasi ndise wakuchimwa Bushiri nayo wali ngat lwee pala wamanya lchi suzapanga zamuthu uzamukonda kwa mbiri. God bless Bushiri so that forex yisamasowe lfeso tikapulumusike

  • @NIDYBANDA-iz7xz
    @NIDYBANDA-iz7xz Жыл бұрын

    Km mwatzindkilisa zambili man sam

  • @NjabuloMKhize501pro
    @NjabuloMKhize501pro20 күн бұрын

    Pwedo

  • @Ishriss1999
    @Ishriss1999 Жыл бұрын

    Koma Mthuzi ija simaseweratu 😂🙌

  • @sammalvitha

    @sammalvitha

    Жыл бұрын

    Anaswa

  • @hanifrego2744

    @hanifrego2744

    10 ай бұрын

    True chilugamo akuchiziwa iye urendo wa kumwamba ndi one one so let God be God

  • @danielkhinguirossejuliasse1214
    @danielkhinguirossejuliasse1214 Жыл бұрын

    Ina ija amati musamamange nhumba kwapongozi

  • @user-sc1ef6bb8i
    @user-sc1ef6bb8i10 ай бұрын

    ATHU AMAMUNYOZA BUSHIRI CZ CHUMA CHAKE CHOCHOKERADI KWAMULUNGU (ziwan kuti Dziko lapasi limadana ndizochokera kwayehova}

  • @MabvutoManjolo-hl6px
    @MabvutoManjolo-hl6px9 ай бұрын

    Number one bushili

  • @HAWAHANDRWE
    @HAWAHANDRWE Жыл бұрын

    Zikomo kwambili sam malvitha zaveka bwino

  • @MercyMachipisaMunthali
    @MercyMachipisaMunthali2 ай бұрын

    Ndimamukonda Bushiri chifukwa samanyoza munthu sayakhula mau opusa kwa munthu. Inu muli Holly lnu mukumaimba nyimbo atsikana atavula ndee oipisisa lnu mwawalimbikisa athu kut God will bless them kapena mwawatengerathu kwasatana

  • @michaelkhunga3676
    @michaelkhunga3676 Жыл бұрын

    keep it up .though am late to comment

  • @sammalvitha

    @sammalvitha

    Жыл бұрын

    Thanks so much

  • @user-ru4mq5bw8i
    @user-ru4mq5bw8i9 ай бұрын

    Only God knows

  • @EnockNyirenda-nr2uj
    @EnockNyirenda-nr2uj13 күн бұрын

    Ayizikomo

  • @tawanisolungu
    @tawanisolungu Жыл бұрын

    Great

  • @AnnahNyirenda-gl1ke
    @AnnahNyirenda-gl1ke Жыл бұрын

    Love it

  • @MercyMachipisaMunthali
    @MercyMachipisaMunthali2 ай бұрын

    God have mercy on you

  • @zainabchikakuda6297
    @zainabchikakuda6297 Жыл бұрын

    Komatu bushir ngodekha akayankha ndiye kuti zavuta mmmmh

  • @isaachara1861
    @isaachara1861 Жыл бұрын

    Bushiri Salimbana ndi mafana opanda vision

  • @evasakelebone3144
    @evasakelebone3144 Жыл бұрын

    Mmmmmmh mmmmh ndizapamwambadi well explained

  • @DeOffice-zz7rb
    @DeOffice-zz7rb9 ай бұрын

    Like

  • @jamesbanda5633
    @jamesbanda5633 Жыл бұрын

    Osamanyoza atumiki amulungu

  • @user-ur1uh4sr7k
    @user-ur1uh4sr7k8 ай бұрын

    God will judge am just a mere person and our lord said let millet grow together with glass separation shall be done at the end

  • @ChesterBanda-qm8fh
    @ChesterBanda-qm8fh9 ай бұрын

    Fire up otsogoleri

  • @frankleeliwonde6221
    @frankleeliwonde6221 Жыл бұрын

    Namadingo sanalengezepo kuti wasiya kuyimba nyimbo zauzimu

  • @sammalvitha

    @sammalvitha

    Жыл бұрын

    Watch my next video

  • @ChalivaIchu-zs1ed
    @ChalivaIchu-zs1ed Жыл бұрын

    Mosezi makawa and tomozichibade

  • @LukaSaulula-kt7bu
    @LukaSaulula-kt7bu3 ай бұрын

    Oooh okay

  • @tamarachipokosa9633
    @tamarachipokosa9633 Жыл бұрын

    Muchedwa nazo limbikirani ntchito

  • @romanslungu
    @romanslungu Жыл бұрын

    Proud of u

  • @user-mc9ce2ug7g
    @user-mc9ce2ug7g3 ай бұрын

    Simungapezemo ndalama

  • @twarichissah4222
    @twarichissah4222 Жыл бұрын

    Nyimbo ya namadingo ya wabwela muli uthenga wabwino kwambiri ndipo kwa munthu wawumunthu pamenepo Palibe vuto lililonse 🤔🤔

  • @ipyanamwanyongo4169
    @ipyanamwanyongo4169 Жыл бұрын

    don't worries about this guy they have pay him big money thus why he is supporting him

  • @MadjidMatola
    @MadjidMatola3 ай бұрын

    Za zii kumangolimbana ndi anthu, that's sighn of poverty 😢

  • @user-id7dj6uk7t
    @user-id7dj6uk7t3 ай бұрын

    Piksy ndi mfauna oziwika ndi bouma😂

  • @user-bh7xr1hz5t
    @user-bh7xr1hz5t9 ай бұрын

    😂😂😂😂😂 chilungamo chimawawadi anthu a bushili akuwoneka olusa tuu samala aise

  • @SelemaniSabiti
    @SelemaniSabiti11 ай бұрын

    ❤❤

  • @aaronphiri5992
    @aaronphiri5992 Жыл бұрын

    Nysaland will always be Nysaland

  • @rhodrickchingoli3636
    @rhodrickchingoli3636 Жыл бұрын

    aMalawi timakodwa wina akamavutika

  • @BlessingsWakhutamoyo
    @BlessingsWakhutamoyoАй бұрын

    If today mulungu says iam whom i

  • @user-rd3ml9qw2x
    @user-rd3ml9qw2x10 ай бұрын

    Be careful with a word of God and don't make a mistake to follow wrong things that you will know that this is a wrong. read jobs 13 verse 14

  • @user-iu4kk6em5k
    @user-iu4kk6em5k9 ай бұрын

    Thax for information❤

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Жыл бұрын

    Ngati ndi wasitaniki mulung ndiye adzamuweluza, osati ine kapena iwe, chotsa chitsotso chili mmanso mwako, uwona bwanji chitsotso chili mmanso mwamzako, chako usanachotse.

  • @shotsfired588
    @shotsfired588 Жыл бұрын

    Wasatanic uyu, ngozi mmene zikuchitikira ku malawi mukuyesa ndi chani, ngozi zoopsya zikuchitikazi chibwerere bushiri kumalawi, magazi akuwukha mwakathithi anthu akufa moopsya and tinanena bushiri atangobwera ku malawi, kuzichitika ngozi zoopsya munthu Wasatanic ameneyi akabwera.

  • @mastersubiri7934

    @mastersubiri7934

    Жыл бұрын

    True that brother

  • @ipyanamwanyongo4169

    @ipyanamwanyongo4169

    Жыл бұрын

    Yes was satanic uyo too since Ali ku Malawi everyday I hear accident why her please bro don't defense him hey,but follow Jesus Christ not men

  • @IsraelMwamvani-ig5fj
    @IsraelMwamvani-ig5fj Жыл бұрын

    🤝

  • @user-qo9dp7vv5s
    @user-qo9dp7vv5s10 ай бұрын

    So nice

  • @RaimundoMuquiale-yc7lf
    @RaimundoMuquiale-yc7lf6 ай бұрын

    Koma ndiye

  • @daudigodfrey1369
    @daudigodfrey136910 ай бұрын

    Nde kuuluka mwamba ndiphamvu yaumulungu ndiyesu yekha adapang zimenezija aise plibeso akuenera kupang paziko lapasi

  • @bensonchunga7258
    @bensonchunga7258 Жыл бұрын

    Thanks

  • @lysonkumbwezaabdullah6075
    @lysonkumbwezaabdullah607510 ай бұрын

    pamenepo zoyamikila zake ndi ziti

  • @steveal-banda2517
    @steveal-banda2517 Жыл бұрын

    How can you forget David kalilani anyambuti

  • @yamikanijames6915

    @yamikanijames6915

    9 ай бұрын

    Eeeeh l like that song it should be on number one for me because he went directly mentioning his name and that was a hit so many punches in that song

  • @christopherbanda1084

    @christopherbanda1084

    9 ай бұрын

    Osaopa

  • @Alimoyo-km2ps
    @Alimoyo-km2ps3 ай бұрын

    Following

  • @user-bm5fi7ui2g
    @user-bm5fi7ui2g Жыл бұрын

    Tikufuna Ena ngat mbiri ya bushiri

  • @ashiamaziti6523
    @ashiamaziti6523 Жыл бұрын

    Nice video

  • @AmosNephan
    @AmosNephan2 ай бұрын

    Bushili ndinthu wabwino kwambiri

  • @stevinmuhone877
    @stevinmuhone877 Жыл бұрын

    Machitidwe awo abushiri ndi amene tikuti samapemhphera mlungu ndipo ine sindizawakhulupirirapo ata

  • @hanabrighton9903

    @hanabrighton9903

    Жыл бұрын

    Alandililatu pasipano ameneyo kumwamba kulibe mark my words

  • @hanabrighton9903

    @hanabrighton9903

    Жыл бұрын

    Ineso chimodzimodzi alikuti Gracy Chinga cz of him ulemuumene mukuunenawo ndiyekuti mphotoyake

  • @petrozakeyo
    @petrozakeyo Жыл бұрын

    Zake izo bora zikumuthekera

  • @frankbanda3259
    @frankbanda3259 Жыл бұрын

    That one is a good person and he is a man of God

  • @wisdomchitseko5956

    @wisdomchitseko5956

    Жыл бұрын

    Yusf

  • @wisdomchitseko5956

    @wisdomchitseko5956

    Жыл бұрын

    Mandonda

  • @shonmikemtawa3262
    @shonmikemtawa3262 Жыл бұрын

    Ose oyimba sangakhare obonza koma ndi zen zen izi

  • @tichezechitukula5352

    @tichezechitukula5352

    Жыл бұрын

    Fact👍

  • @kennedykamoto5068
    @kennedykamoto50684 ай бұрын

    Umakwana sam

  • @judywilliams2349
    @judywilliams2349 Жыл бұрын

    I have no respect for the magicians. I can’t understand how people are so brainwashed. God help us.

  • @hendrixhendrickse1608

    @hendrixhendrickse1608

    Жыл бұрын

    me too .

  • @SIDDHARTPATRICK

    @SIDDHARTPATRICK

    4 ай бұрын

    Sure

  • @dhaoudhiabedinegomaseko2363
    @dhaoudhiabedinegomaseko2363 Жыл бұрын

    Adzabwera ngati akhristu koma kuti adzanyenge ochuluka.Mawu awa ali mu bible koma anthu eti kakakakaka

  • @reemoman-tr5wd
    @reemoman-tr5wd Жыл бұрын

    Woyimbawo amayimba zeni zeni ndipo zoona zonkha zonkha

  • @masekophiri
    @masekophiri Жыл бұрын

    Chilungamo chiyende ngat madzi so athu mumaopa chilungamo ndye kuti mumaopa pop

  • @mlezanyirenda2815
    @mlezanyirenda2815 Жыл бұрын

    Chilungamo chimawawa eti

  • @martinkapito9418
    @martinkapito9418 Жыл бұрын

    Chilungamo chimawawa

  • @tingoalex6370
    @tingoalex6370 Жыл бұрын

    Namadingo ndiwamabodza amakonda kulimbana ndi azizake aaa

  • @adamkabaghe9018

    @adamkabaghe9018

    Жыл бұрын

    Good one

Келесі