Zikomo poonera, chonde Ngat simunachite subscribe.. kumbukiran kutero ... Muchite like ...video iyi .... Zikomo
@muyabasamson
Жыл бұрын
Akupanga sanjechabe
@starlonjamus
Жыл бұрын
👍
@gordonmatsagopane
Жыл бұрын
1qq
@Dyson.chibaloh
10 ай бұрын
@@starlonjamusHy Hy hyhy
@bahatichirwa7601
10 ай бұрын
😊😊😊😊😊😊😊
@harryhara6217 Жыл бұрын
Oyimba onse amanyoza Bushiriwa, nkhani,yake ndi umphawi. Iwowo amafuna kukhala oweruza?ine si fan wa Bushiri and i've never been. Koma sindingamamuweruze.
@greshammshelera5344
Жыл бұрын
True bro
@peterjcndolo5644 Жыл бұрын
I like him, he has a humanitarian motivation, big up Shepherd Bushiri. Ngati zintchito ndizonyasa kuseli let God do His of Judging
@judywilliams2349 Жыл бұрын
That’s true, blood money. Magician full time.
@judywilliams2349 Жыл бұрын
That’s true, Bushiri is a magician and I can’t understand how people are so brainwashed.
@keniekaipa199711 ай бұрын
Mbuzi iwe umanama......usiye kupanga za anthu
@user-tf2ri2sl5s10 ай бұрын
Thanks for your true report about the Prophet Shepherd Bushiri and his beloved wife (Prophetess... As well as the Malawian musicians who composed their music despising, criticize, or contempt the Prophet Shepherd Bushiri!!! Anyway... Only God knows... HE'S THE RIGHTEOUS GUDGE IN HEAVEN AND AND ON EARTH.
@kalunguhelias3 ай бұрын
I've ukutiuza za bushir KT titaninaye
@musicoftheviolinstudios.1109 Жыл бұрын
zofotokoza zanu zili bwino,ndizosakolana zachindunji bwino bwino.mulipo awiri ndi big mani enake samazitchula dzina lake .
@yassinrashid7012
Жыл бұрын
Mkulu wa bakili Muluzi tv
@ayamijackson1443 Жыл бұрын
Very much Best bro please ceep it up good job bro
@sammalvitha
Жыл бұрын
I will try my best
@sonnymasandi1748 Жыл бұрын
Ndayikonda so much keep up agood work
@AuthenticV Жыл бұрын
Pastor David Kalirani Amayenera kukhala pa number 1
@chrissjunior8342 Жыл бұрын
Proudly you my brother " nd nkhan ngat zmenez 🤟
@ElizaNyirongo
Жыл бұрын
Love it
@godfreybiziweck1224 Жыл бұрын
Ndizoonadi anamunyoza prophet shepherd bushiri
@gracephiri1203 Жыл бұрын
Mwaitha bro muzibwelabwela
@ashraffmidu7837 Жыл бұрын
Piksy didn't liar he only says the truth moreover that song of him it's my favorite song....akutithera mtundu m'malawi ameneyo...#MartseKeepRip😥
@NIDYBANDA-iz7xz
Жыл бұрын
Pakut tilibe mphavu zopangila judge km mmmmmm
@jaymilazi2937 Жыл бұрын
Muzibwezerabwera ndi nkhani ngat izi
@fradahmakwinja3835 Жыл бұрын
Major one is Great
@JuniorAbasi-eb5ce8 ай бұрын
A Malawi ife tilibe ulemu Mr Bushiri zawo dzidayela khale chofunika ndi ulemu basi monga ine ndikuti ulemu wanu mr Bushiri .kodi A Malawi tinakhala bwanji munthu aliyitse akalemela.ali ndi vuto
@user-qk9ib7hb4l9 ай бұрын
That's very gorgeous
@user-gr6zh9zr9b8 ай бұрын
TNM super rige malawi
@thembalungani9347 Жыл бұрын
proud to him man of God...enawa yakula ndi nsanje...m'nyamata ali ndi mphatso ya utumiki uyu congratulations to major 1
@kennethkaunda3636 Жыл бұрын
Ndi zoona bro
@rasheedjaffali6674 Жыл бұрын
Nice one brood good work
@mosesjoni2542 Жыл бұрын
Best one bos
@TamandaniIssa22 сағат бұрын
He is still a prophet of God whether you like it or not
@amontchuwa6876 Жыл бұрын
Nanga iwe ukt bwanji Ine ai akuziwa ndi Yahweh
@yusufelliotanalidodoloooma9685 Жыл бұрын
Chimandisangalasa ndichoti bushiri utsogoleri ali nao sapsa ayii. Anthu ndie amathoka zaiye siku ndi siku. Koma mumpeza Alii pee . Iye bola ubale wake ndi mulungu uli bwino
@mastersubiri7934
Жыл бұрын
Mulungu wake utii nanu kutengeka ndi zili zonse
@tichezechitukula5352
Жыл бұрын
@@mastersubiri7934 Mwandifusilako boss!!
@KatsekelaHassan2 ай бұрын
Am still love bushiri
@eliasleonard9448 Жыл бұрын
Moyo ndikamozi ndagwirana ndinamdingo
@AffectionateFoliage-gh6bf5 ай бұрын
Keep it up
@NavitchaBanda23 күн бұрын
Mukasowa chati usamalimbane ndi man of god
@JenniferRonnex2 ай бұрын
Haji❤
@ibulakimu9380 Жыл бұрын
Enewa ndi zanje
@user-tu6ph6wh2z11 ай бұрын
I like him he has a humanitarian
@KimuBanda3 ай бұрын
Tnx for the good report
@MercyMachipisaMunthali2 ай бұрын
Tose tapachalu chapasi ndise wakuchimwa Bushiri nayo wali ngat lwee pala wamanya lchi suzapanga zamuthu uzamukonda kwa mbiri. God bless Bushiri so that forex yisamasowe lfeso tikapulumusike
@NIDYBANDA-iz7xz Жыл бұрын
Km mwatzindkilisa zambili man sam
@NjabuloMKhize501pro20 күн бұрын
Pwedo
@Ishriss1999 Жыл бұрын
Koma Mthuzi ija simaseweratu 😂🙌
@sammalvitha
Жыл бұрын
Anaswa
@hanifrego2744
10 ай бұрын
True chilugamo akuchiziwa iye urendo wa kumwamba ndi one one so let God be God
Пікірлер: 232
Zikomo poonera, chonde Ngat simunachite subscribe.. kumbukiran kutero ... Muchite like ...video iyi .... Zikomo
@muyabasamson
Жыл бұрын
Akupanga sanjechabe
@starlonjamus
Жыл бұрын
👍
@gordonmatsagopane
Жыл бұрын
1qq
@Dyson.chibaloh
10 ай бұрын
@@starlonjamusHy Hy hyhy
@bahatichirwa7601
10 ай бұрын
😊😊😊😊😊😊😊
Oyimba onse amanyoza Bushiriwa, nkhani,yake ndi umphawi. Iwowo amafuna kukhala oweruza?ine si fan wa Bushiri and i've never been. Koma sindingamamuweruze.
@greshammshelera5344
Жыл бұрын
True bro
I like him, he has a humanitarian motivation, big up Shepherd Bushiri. Ngati zintchito ndizonyasa kuseli let God do His of Judging
That’s true, blood money. Magician full time.
That’s true, Bushiri is a magician and I can’t understand how people are so brainwashed.
Mbuzi iwe umanama......usiye kupanga za anthu
Thanks for your true report about the Prophet Shepherd Bushiri and his beloved wife (Prophetess... As well as the Malawian musicians who composed their music despising, criticize, or contempt the Prophet Shepherd Bushiri!!! Anyway... Only God knows... HE'S THE RIGHTEOUS GUDGE IN HEAVEN AND AND ON EARTH.
I've ukutiuza za bushir KT titaninaye
zofotokoza zanu zili bwino,ndizosakolana zachindunji bwino bwino.mulipo awiri ndi big mani enake samazitchula dzina lake .
@yassinrashid7012
Жыл бұрын
Mkulu wa bakili Muluzi tv
Very much Best bro please ceep it up good job bro
@sammalvitha
Жыл бұрын
I will try my best
Ndayikonda so much keep up agood work
Pastor David Kalirani Amayenera kukhala pa number 1
Proudly you my brother " nd nkhan ngat zmenez 🤟
@ElizaNyirongo
Жыл бұрын
Love it
Ndizoonadi anamunyoza prophet shepherd bushiri
Mwaitha bro muzibwelabwela
Piksy didn't liar he only says the truth moreover that song of him it's my favorite song....akutithera mtundu m'malawi ameneyo...#MartseKeepRip😥
@NIDYBANDA-iz7xz
Жыл бұрын
Pakut tilibe mphavu zopangila judge km mmmmmm
Muzibwezerabwera ndi nkhani ngat izi
Major one is Great
A Malawi ife tilibe ulemu Mr Bushiri zawo dzidayela khale chofunika ndi ulemu basi monga ine ndikuti ulemu wanu mr Bushiri .kodi A Malawi tinakhala bwanji munthu aliyitse akalemela.ali ndi vuto
That's very gorgeous
TNM super rige malawi
proud to him man of God...enawa yakula ndi nsanje...m'nyamata ali ndi mphatso ya utumiki uyu congratulations to major 1
Ndi zoona bro
Nice one brood good work
Best one bos
He is still a prophet of God whether you like it or not
Nanga iwe ukt bwanji Ine ai akuziwa ndi Yahweh
Chimandisangalasa ndichoti bushiri utsogoleri ali nao sapsa ayii. Anthu ndie amathoka zaiye siku ndi siku. Koma mumpeza Alii pee . Iye bola ubale wake ndi mulungu uli bwino
@mastersubiri7934
Жыл бұрын
Mulungu wake utii nanu kutengeka ndi zili zonse
@tichezechitukula5352
Жыл бұрын
@@mastersubiri7934 Mwandifusilako boss!!
Am still love bushiri
Moyo ndikamozi ndagwirana ndinamdingo
Keep it up
Mukasowa chati usamalimbane ndi man of god
Haji❤
Enewa ndi zanje
I like him he has a humanitarian
Tnx for the good report
Tose tapachalu chapasi ndise wakuchimwa Bushiri nayo wali ngat lwee pala wamanya lchi suzapanga zamuthu uzamukonda kwa mbiri. God bless Bushiri so that forex yisamasowe lfeso tikapulumusike
Km mwatzindkilisa zambili man sam
Pwedo
Koma Mthuzi ija simaseweratu 😂🙌
@sammalvitha
Жыл бұрын
Anaswa
@hanifrego2744
10 ай бұрын
True chilugamo akuchiziwa iye urendo wa kumwamba ndi one one so let God be God
Ina ija amati musamamange nhumba kwapongozi
ATHU AMAMUNYOZA BUSHIRI CZ CHUMA CHAKE CHOCHOKERADI KWAMULUNGU (ziwan kuti Dziko lapasi limadana ndizochokera kwayehova}
Number one bushili
Zikomo kwambili sam malvitha zaveka bwino
Ndimamukonda Bushiri chifukwa samanyoza munthu sayakhula mau opusa kwa munthu. Inu muli Holly lnu mukumaimba nyimbo atsikana atavula ndee oipisisa lnu mwawalimbikisa athu kut God will bless them kapena mwawatengerathu kwasatana
keep it up .though am late to comment
@sammalvitha
Жыл бұрын
Thanks so much
Only God knows
Ayizikomo
Great
Love it
God have mercy on you
Komatu bushir ngodekha akayankha ndiye kuti zavuta mmmmh
Bushiri Salimbana ndi mafana opanda vision
Mmmmmmh mmmmh ndizapamwambadi well explained
Like
Osamanyoza atumiki amulungu
God will judge am just a mere person and our lord said let millet grow together with glass separation shall be done at the end
Fire up otsogoleri
Namadingo sanalengezepo kuti wasiya kuyimba nyimbo zauzimu
@sammalvitha
Жыл бұрын
Watch my next video
Mosezi makawa and tomozichibade
Oooh okay
Muchedwa nazo limbikirani ntchito
Proud of u
Simungapezemo ndalama
Nyimbo ya namadingo ya wabwela muli uthenga wabwino kwambiri ndipo kwa munthu wawumunthu pamenepo Palibe vuto lililonse 🤔🤔
don't worries about this guy they have pay him big money thus why he is supporting him
Za zii kumangolimbana ndi anthu, that's sighn of poverty 😢
Piksy ndi mfauna oziwika ndi bouma😂
😂😂😂😂😂 chilungamo chimawawadi anthu a bushili akuwoneka olusa tuu samala aise
❤❤
Nysaland will always be Nysaland
aMalawi timakodwa wina akamavutika
If today mulungu says iam whom i
Be careful with a word of God and don't make a mistake to follow wrong things that you will know that this is a wrong. read jobs 13 verse 14
Thax for information❤
Ngati ndi wasitaniki mulung ndiye adzamuweluza, osati ine kapena iwe, chotsa chitsotso chili mmanso mwako, uwona bwanji chitsotso chili mmanso mwamzako, chako usanachotse.
Wasatanic uyu, ngozi mmene zikuchitikira ku malawi mukuyesa ndi chani, ngozi zoopsya zikuchitikazi chibwerere bushiri kumalawi, magazi akuwukha mwakathithi anthu akufa moopsya and tinanena bushiri atangobwera ku malawi, kuzichitika ngozi zoopsya munthu Wasatanic ameneyi akabwera.
@mastersubiri7934
Жыл бұрын
True that brother
@ipyanamwanyongo4169
Жыл бұрын
Yes was satanic uyo too since Ali ku Malawi everyday I hear accident why her please bro don't defense him hey,but follow Jesus Christ not men
🤝
So nice
Koma ndiye
Nde kuuluka mwamba ndiphamvu yaumulungu ndiyesu yekha adapang zimenezija aise plibeso akuenera kupang paziko lapasi
Thanks
pamenepo zoyamikila zake ndi ziti
How can you forget David kalilani anyambuti
@yamikanijames6915
9 ай бұрын
Eeeeh l like that song it should be on number one for me because he went directly mentioning his name and that was a hit so many punches in that song
@christopherbanda1084
9 ай бұрын
Osaopa
Following
Tikufuna Ena ngat mbiri ya bushiri
Nice video
Bushili ndinthu wabwino kwambiri
Machitidwe awo abushiri ndi amene tikuti samapemhphera mlungu ndipo ine sindizawakhulupirirapo ata
@hanabrighton9903
Жыл бұрын
Alandililatu pasipano ameneyo kumwamba kulibe mark my words
@hanabrighton9903
Жыл бұрын
Ineso chimodzimodzi alikuti Gracy Chinga cz of him ulemuumene mukuunenawo ndiyekuti mphotoyake
Zake izo bora zikumuthekera
That one is a good person and he is a man of God
@wisdomchitseko5956
Жыл бұрын
Yusf
@wisdomchitseko5956
Жыл бұрын
Mandonda
Ose oyimba sangakhare obonza koma ndi zen zen izi
@tichezechitukula5352
Жыл бұрын
Fact👍
Umakwana sam
I have no respect for the magicians. I can’t understand how people are so brainwashed. God help us.
@hendrixhendrickse1608
Жыл бұрын
me too .
@SIDDHARTPATRICK
4 ай бұрын
Sure
Adzabwera ngati akhristu koma kuti adzanyenge ochuluka.Mawu awa ali mu bible koma anthu eti kakakakaka
Woyimbawo amayimba zeni zeni ndipo zoona zonkha zonkha
Chilungamo chiyende ngat madzi so athu mumaopa chilungamo ndye kuti mumaopa pop
Chilungamo chimawawa eti
Chilungamo chimawawa
Namadingo ndiwamabodza amakonda kulimbana ndi azizake aaa
@adamkabaghe9018
Жыл бұрын
Good one