Chifukwa Chenicheni Chomwe Shepherd Bushiri Akumangira Mzinda Wa GOSHEN CITY

if you like my content and would like to support me further, please
PayPal
➡️To Donate please use PayPal www.paypal.me/hanifamalawi
Business/Sponsor Inquiries //hanifamw.suggestions@gmail.com
Mu November mchaka cha 2021, pamene mlaliki Shepherd Bushiri pamodzi ndi mkazi wake Mary anathawa belo mdziko la South Africa mkubwera kuno ku Malawi, anthu ambiri anayesa kuti basi watha ndipo sangapangenso chilichonse cholozeka. Hotel yake yotchedwa Sparkling and Spa yomwe ili mu dera wa Rustenburg mdzikolo inayamba kupita pansi popeza malonda sankayenda. Ndalama zomwe amkazipeza kuchoka mu chopereka chaku tchalichi kamba kakuthawaku izi zinayima. Kenako ali ku Malawi analengeza za scholarship yomwe iye akufuna kuthandiza ana osowa fees mma sukulu osiyanasiyana. Apa anthu sanamukhulupilire popeza amkati alibe ndalama ndipo amapanga izi pongofuna kutchuka.
Komatu Bushiri wadabwitsa ndikututumutsa anthu ambiri posachedwapa atalengeza kuti akumanga mzinda m’boma wa Mangochi womwe akuwutcha kuti Goshen City.

Пікірлер: 121

  • @LovenessLester
    @LovenessLester21 күн бұрын

    That's a great city for many Malawians let's learn how to appreciate this our man of God 🙏

  • @alfednjolobvi1591
    @alfednjolobvi15912 жыл бұрын

    Bushiri ur a great man that's why ur very blessed I wish if Malawi having too many people like u Bushiri who thinking about there homeland ur great indeed keep it up God bless you more

  • @richardchaupe7231
    @richardchaupe72312 жыл бұрын

    I salute Bushiri, he is one of a kind Creating jobs for the young people

  • @josephkaputa8502
    @josephkaputa85022 жыл бұрын

    He is agood man coz he is dealing with poverty,big up B

  • @teddybanda8989
    @teddybanda89892 жыл бұрын

    That guy has got gold mines here in zambia 🇿🇲 and different countries

  • @allenchilekw5698

    @allenchilekw5698

    Жыл бұрын

    Where in Zambia?

  • @lucksonlongwe1658
    @lucksonlongwe1658 Жыл бұрын

    Best wishes to man of God. Continue your work. God is with you.

  • @michealmwimba6084
    @michealmwimba6084 Жыл бұрын

    I just like the way you express yourself in chichewa its so amazing and keep up the good work

  • @madakasosoch4322
    @madakasosoch4322 Жыл бұрын

    He is going great work to develop Malawi

  • @stevechizaka9908
    @stevechizaka99082 жыл бұрын

    Dziko la malawi silimatukuka ndi nkhani ngati zimenezi. Munthu ngati akumanga town yamakono ngati imeneyi mudziko lathu.ife bwezi tikuonesa chikondi kwaiye ndikumulimbikisa osati kumufookesa pazinkhani zopanda Pache. Anthu akatangale akuwaziwa kale bwanji osamakawafufuza amenewo

  • @naongarluhanga3218
    @naongarluhanga3218 Жыл бұрын

    Hard workers always think about changing things .All the best man

  • @maxwellmustaffaalickalick1745
    @maxwellmustaffaalickalick17452 жыл бұрын

    Ife anthu akuda ndichoncho sanje kwambiri i respect him a lot

  • @joebanda3732
    @joebanda37322 жыл бұрын

    You are doing extremely well Sir I like your tone. U got a very bright future. God will exalt you this year. Stay focused and pray more

  • @mussawilliam5684
    @mussawilliam56842 жыл бұрын

    Vuto ndilokuti ife a malawi makamaka kumipandoko kwachuluka achule kwambili mwachisanzo ine ndili kuno ku south Africa ndapedza ndalama ndithawile dziko lakwathu adzafuna kundifufudza ndiye uchulewo ugalu a aphaka Bushili akufuna kutukula dziko lakumalawi ndiye pakupedzeka agalu ena monga amulaka malilo ndijelasi yao kudzolowela kuvutika ugalu basi Bushiri akufuna kutukula dziko lamalawi

  • @isaacschamatwa3596
    @isaacschamatwa35962 жыл бұрын

    such a very good tone,Bushiri is doing such a good job

  • @joeljere4385
    @joeljere43852 жыл бұрын

    He is doing great work to develop Malawi

  • @andersonmasamba457

    @andersonmasamba457

    Жыл бұрын

    t

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Жыл бұрын

    Goshen City is a product of powerful vision

  • @biggyk7740
    @biggyk77402 жыл бұрын

    I will always support bushiri he is a true citizen of Malawi

  • @williamlahman2787
    @williamlahman27872 жыл бұрын

    Let him to fulfill his duties,. He's so young, hope will do mo than that. All those jealous people must fall. Almighty bless him

  • @mollymadzibane
    @mollymadzibane Жыл бұрын

    My Father My Prophet you are doing great job . You are creating work also for Malawians generation . I tap into your Annointing my Prophet . May God bless you all your Enemies will Scarter one by one Molly limpopo

  • @hoekboy1102
    @hoekboy11022 жыл бұрын

    I salute you Bushiri I will be Uber driver there

  • @harrietmwika8695
    @harrietmwika8695 Жыл бұрын

    Love the Bushiris keep it up and God bless.

  • @machonabanda5752
    @machonabanda57522 жыл бұрын

    Hanifa you are the best ♥️♥️🙏🙏

  • @simonndou5236
    @simonndou5236 Жыл бұрын

    Good work Prophet Bushiri

  • @agnessmpungalume1446
    @agnessmpungalume1446 Жыл бұрын

    Just wow Beautiful masophenya

  • @willardakidy6916
    @willardakidy69162 жыл бұрын

    Akulephera mapulesident kutukura dziko lanthu ineyo ndingoti Malawi mwana tingathe kumaloza chala kwaathu kuti town yakwathu iyo mulungu pasongolo basi

  • @jestinanamkonda1495
    @jestinanamkonda14952 жыл бұрын

    The annointing of Papa Bushiri breaks the yokes of poverty. Try it. You don't know the businesses Bushiri has. Why being so rough without the knowledge of his wealth and Riches. He is the third richest person in Malawi nde mumati ndalama azitani nazo? They devil will never be happy with a progressive person

  • @benitozack6523
    @benitozack6523 Жыл бұрын

    Don't be jealous with someone who is doing great work,because that city will change many Malawians

  • @mederinausain6913
    @mederinausain6913 Жыл бұрын

    Bushili ndi one akupotsa president ulemu wanu a bushili za ndare simupanga nawo koma kukwedza malawi pa sogolo ..koma muzandilembeko tchito

  • @chifundonkhoma3642
    @chifundonkhoma36422 жыл бұрын

    Komatu anthu mupole moto... Mmalo mopanga njira zothana ndi umphawi omwe satana anakutembererani nawowo.. Mukulimbana ndiwo mulungu adawadalitsa, kutaya nthawi ndi za zii limbikirani kupemphera siyani msanje, mulungu adzaona mokudalitsira musiyeni Shepherd Bushiri apange zothandiza human kind

  • @bashiriyusufu1224
    @bashiriyusufu12242 жыл бұрын

    🔥🔥🔥Wabwela ngat coming 💪💪💪

  • @englishboy6570
    @englishboy65702 жыл бұрын

    Vuto la amalawi ndinsanje basi

  • @jestinanamkonda1495

    @jestinanamkonda1495

    2 жыл бұрын

    That is the problem of Malawians

  • @jtpi8362

    @jtpi8362

    2 жыл бұрын

    Ndi izi mukuziona ku ma comments kuno, anthu a nsanje akumunyozabe m'malo moyamikila kuti a Malawi ambiri apeza ntchito kumeneko, komanso dziko lathu litchuka ntchito imeneyi ikatha.

  • @gloriabanda6552
    @gloriabanda6552 Жыл бұрын

    this is great💯

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q28 күн бұрын

    Akurephera chakwera kutukura ziko.rino angoononga ndarama chakwera chito zamanja ako zikuchitire umboni bushiri

  • @richardchaupe7231
    @richardchaupe72312 жыл бұрын

    Please do the same content in English to enable none Malawians understand Unless you are from Zambia and some Zimbabwians can understand

  • @brucewarchild2156

    @brucewarchild2156

    2 жыл бұрын

    It's none of foreigners business

  • @chifundonkhoma3642

    @chifundonkhoma3642

    2 жыл бұрын

    Kkkkkkk OK fine.... Please people stop being jealous,instead of focusing on your demonic poverty , you waste time with whom YAHWE blessed... Learn to love one another.. Learn to thank God......

  • @williamjusten6646
    @williamjusten66462 жыл бұрын

    Great job

  • @limpopolimpopo2623
    @limpopolimpopo26232 жыл бұрын

    A Malawi sanje mlekeni atukule dziko lathu la Malawi

  • @mbumbajilowele6511
    @mbumbajilowele65112 жыл бұрын

    Greatest man

  • @AllanChingwazala
    @AllanChingwazala12 күн бұрын

    Ndimafunisisa utazakhara president malawi ikhoza kukhala yopambana ngat wakwanisa kumanga ndalama zayekha kulibwanji athakhala president buchiri ndimakufila kuzakhala president ndizabwerera kumalawi

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth29472 жыл бұрын

    A Malawi Munatani kodi kumangovuta pa zinthu zopanda pake MAJOR 1 akufuna kutimagira Town mukufuna kumufufuza chiyani at least he's creating jobs zomwe Atsogoleri athu saangakwanitse koma kuba basi ndi ma slangs and fluent English opanda pake hands of BUSHIRI Manga Town SHEPHERD...👏👏💪 Let Them Talk, Idiot's come on Homies If you want someone to investigate I'm gonna show you where to go Pitani ku TONSE ALLIANCE that's where you'll find thieves,mbava,akamatule,matsotsi,wawii,🤞😊

  • @praisemkutumula3348
    @praisemkutumula3348 Жыл бұрын

    Great ideas

  • @trymoo8479
    @trymoo84792 жыл бұрын

    Ohhh? At least

  • @anthuochukapazambiaelishas4978
    @anthuochukapazambiaelishas49782 жыл бұрын

    Perfect

  • @johnboscozgambo71
    @johnboscozgambo712 жыл бұрын

    Thanks for budget

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q28 күн бұрын

    Bushiri uzangokhara president

  • @mikegoodblessyoumenofgoodm3482
    @mikegoodblessyoumenofgoodm34822 жыл бұрын

    Moti musangalale akubwelesa Chitukuko ku malawi sanjebasi

  • @wisdomktitus660
    @wisdomktitus660 Жыл бұрын

    Aaa pajatu Malawi is full of kaduka,,enawa angofuna amudyere

  • @innocentkandulu2825
    @innocentkandulu28252 жыл бұрын

    That's great

  • @simonndou5236
    @simonndou5236 Жыл бұрын

    We need ro underatand in english too. Inam in South Africa.

  • @promise3693
    @promise36932 жыл бұрын

    Nsanje aMalawi iiiii munthu akapanga chinthu basi zokamba mbweeee

  • @duduzilesimelane9208
    @duduzilesimelane9208 Жыл бұрын

    I like profet he only does God mind not his

  • @duduzilesimelane9208
    @duduzilesimelane9208 Жыл бұрын

    Man of God who only does God mind not him

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw5 ай бұрын

    Zoona zake afufuzidwee munali asadiki miya muzikomo olemera oti amatha kukuthandiza boma lo koma sanafikepo apo fufuzani ndithu

  • @geoffreychimutu6654
    @geoffreychimutu6654 Жыл бұрын

    More fire

  • @beautyandnatureofafrica5334
    @beautyandnatureofafrica53342 жыл бұрын

    Nsanje amalawi.. Musiyen bushiri atukule dzulo lathu

  • @phikamomo9755
    @phikamomo9755 Жыл бұрын

    Nice job

  • @webbyasterchengo4006
    @webbyasterchengo40062 жыл бұрын

    That's why ziko lamalawi lizakalabe losauka mphaka kale kale amufufuza bwanji ngati ziko lamalawi labeledwapo nsaja basi ziko losafuninara anthu zabwino

  • @victormsika1538

    @victormsika1538

    8 ай бұрын

    Ndipo iyi nde ndi mfundo ndithu

  • @newdavidomw
    @newdavidomw Жыл бұрын

    bushiri ndi munthu modzi wachuma yemwe akuyika pa map malawi

  • @johnbihali9883
    @johnbihali9883 Жыл бұрын

    But your report doesn't relate with the title of your presentation. Improve pliz

  • @hendmorsoni32
    @hendmorsoni32 Жыл бұрын

    Malawi akukanika kutukuka chifukwa chansanje

  • @mabvutochimkondenji910
    @mabvutochimkondenji910Ай бұрын

    uyu akhale vice

  • @nelsonkausiwa4754
    @nelsonkausiwa4754 Жыл бұрын

    Major one

  • @manuelsamuel293
    @manuelsamuel293 Жыл бұрын

    Let him to do what he want to do and moreover he is doing that in his country, so let those dogs who has jealous with him to smile urine

  • @kondwanileonard9868
    @kondwanileonard9868 Жыл бұрын

    Is right

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Жыл бұрын

    Maiko azathu anthu ngati amene ndi amene amatukura dziko,

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson14432 жыл бұрын

    Gays tangoyamikilani muthuyu popangachiganizo chotukula zikolovesa chisonili ngati palizolakwika aakoze ndimulungu

  • @olipamaseko2693

    @olipamaseko2693

    8 ай бұрын

    Zokaikitsa ndalama zake aaa

  • @victormsika1538

    @victormsika1538

    8 ай бұрын

    @@olipamaseko2693and so???? Nde mukufuna kuti munthu atani kodi. Olo Chakwera atasiya kupusa kwakeku this country can’t still go further because of people like you. Bitter and pathetic person

  • @thekuhespodcast
    @thekuhespodcast2 жыл бұрын

    The first to comment and hopefully will be the first resident of Goshen 😂

  • @lilianmazila7688

    @lilianmazila7688

    2 жыл бұрын

    L

  • @bonimpoya1439
    @bonimpoya1439 Жыл бұрын

    Malawi goas on

  • @giftphiri595
    @giftphiri5952 жыл бұрын

    A Malawi ambiri amadana ndi chitukuko amafuna kuba chabe, Bushiri asaope munthu.

  • @victormsika1538

    @victormsika1538

    8 ай бұрын

    Nzoona ndithu

  • @tuntufyesichinga1071
    @tuntufyesichinga1071 Жыл бұрын

    Okay?

  • @VincentChikopa-mm6ig
    @VincentChikopa-mm6igАй бұрын

    Muuze bushili mon

  • @phirisandfore643
    @phirisandfore643 Жыл бұрын

    Papa help me to change my life

  • @naongarluhanga3218
    @naongarluhanga3218 Жыл бұрын

    No need of AcB because he z not apolitician

  • @marcelolemos1484
    @marcelolemos14842 жыл бұрын

    Humm

  • @squatmansaidi561
    @squatmansaidi561 Жыл бұрын

    Kkkk kma guys mawu awa akuyenera munthu wa ndemvu ku face

  • @innocentchirwa3677
    @innocentchirwa36772 жыл бұрын

    Wabwera mwa coming

  • @snetawailiyasa3215
    @snetawailiyasa32152 жыл бұрын

    Ok

  • @olipamaseko2693
    @olipamaseko26938 ай бұрын

    Aaaa ndalamazi aaaa

  • @frankkamunde4575
    @frankkamunde45752 жыл бұрын

    nsanje ndimene yakula nsinkhu

  • @lonmediatech5864
    @lonmediatech58642 жыл бұрын

    Iwe anthu azakumangisa.

  • @fedinadisakala2380
    @fedinadisakala23802 жыл бұрын

    Sanje amalawi musiyeni munthu atukulemalawi

  • @vitumbikochirwa2830
    @vitumbikochirwa2830 Жыл бұрын

    Enemies of progress.Bushiri is doing this for the betterment of the country. This is malawi property,bushiri is just engineering.its the government which is going to benefit

  • @mustafailanga5010
    @mustafailanga50102 жыл бұрын

    Sanje amalawi

  • @user-vo4yj7vz2r
    @user-vo4yj7vz2r6 ай бұрын

    Wabodza iwe

  • @rasheedbanert7086
    @rasheedbanert7086 Жыл бұрын

    Zasatanic basi mboli yako iwe

  • @sidickbadat1086
    @sidickbadat10862 жыл бұрын

    You have to screen this man the so called Prophet, whenever he got his money and how he made it, because this doesn’t look normal at all.

  • @masiyekalisitusidayton9210
    @masiyekalisitusidayton92102 жыл бұрын

    Apanga bwino nd2

  • @cadohjabu5565
    @cadohjabu55652 жыл бұрын

    Mlandu Ukudikila ku South Africa Aonetse chitsanzo chabwino

  • @user-ng2nu6xn9x
    @user-ng2nu6xn9x Жыл бұрын

    AKADAKHALA KUTI ANTHU ENANSO AMAKHOBILI AKU MALAWI ALI NDI MOYO AKUONETSA A SHEPHERD BUSHIRI PANOPA MALAWI AKADAKHALA ATATUKUKA KOOPSYA

  • @victormsika1538

    @victormsika1538

    8 ай бұрын

    Ndipo nzoona kunoku anthu ake ngansanje yauchitsilu nayo

  • @patchipanga8445
    @patchipanga84452 жыл бұрын

    Amange Malawi basi

  • @jonathandube9422
    @jonathandube9422 Жыл бұрын

    Bushili is a hill

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera72712 жыл бұрын

    Ppl are serious wth him ......for show bushiri is doing good jobs for better malawians

  • @FacekidofficialmozMoz
    @FacekidofficialmozMoz Жыл бұрын

    🇲🇿Hi

  • @fridayngungadaud731
    @fridayngungadaud7312 жыл бұрын

    Channel ichi sindichikhulupirila anta

  • @yamikanijames6915

    @yamikanijames6915

    10 ай бұрын

    Amaphatikiza choonadi ndi bodza vuto lake ndilimenelo

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw5 ай бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @amosnyirenda5712
    @amosnyirenda57122 жыл бұрын

    Zot zikuyenda chifukwa cha a Bushiri nde bodza the guy is bad luck kungobwera zinthu kuzsiiratu kuyenda kumalawi kuno. I dont like this guy

  • @victormsika1538

    @victormsika1538

    8 ай бұрын

    Nchifukwa chake this country can’t go further because of sick and twisted people like you. If you don’t like him very good but don’t shit on whatever good thing he’s doing. And he didn’t ask you to like him or not. Tabakhalabe pa umphawi wakowo mfiti iwe

  • @bryanfuimaono709
    @bryanfuimaono709 Жыл бұрын

    you need to speak in English

  • @KAIPAAA3211
    @KAIPAAA32112 жыл бұрын

    Mbava yoo pya

  • @cordilliachavula3912

    @cordilliachavula3912

    Жыл бұрын

    Anakubela chiyani????????????

  • @KAIPAAA3211
    @KAIPAAA32112 жыл бұрын

    Wakuba wabela anthu ambiri ku south aafrica, amawanamiza anthu ambiri aike ndalama ku acount yake miez itatu apeza ndalama zambili ku ma count ao, ambiri akulila

  • @jomonor4915

    @jomonor4915

    2 жыл бұрын

    Dziko likufunika kukhala ndi munthu ngati uyu,uyutu amadzigwilila ntchito pa yekha wosati zomaba misonkho ya anthu.papa yr great wishing yu best mwatimasula amalawife

  • @saudamwanyali8700

    @saudamwanyali8700

    2 жыл бұрын

    Do you hv a proof for wat u a sayin

  • @ronaldchirwa253

    @ronaldchirwa253

    Жыл бұрын

    Tazingogwirani ntchito apa... wakuberanipo chan chanu kapena cha makolo anu?

  • @yamikanijames6915

    @yamikanijames6915

    10 ай бұрын

    Then akuba bwinotu coz he is stealing to help others

  • @akiramlw
    @akiramlw2 жыл бұрын

    Hanifa give me your number ndufuna interview ya late Grace chinga ija

  • @louisbanda643
    @louisbanda6432 жыл бұрын

    Great job

Келесі