Nicholas Dausi at MCP, facing President Lazarus Chakwera

Honourable Nicholas Dausi speaking at the Mwanza development rally where the president of Malawi, Dr Lazarus Chakwera was present

Пікірлер: 361

  • @KennedyTchauya-fl5yk
    @KennedyTchauya-fl5yk5 ай бұрын

    The king is back🌋🌋 welcome Mr Dausi , home is best

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata69335 ай бұрын

    Anthu akuononga malawi ndi amenewa

  • @user-kp6ng8bc2f

    @user-kp6ng8bc2f

    5 ай бұрын

    Day wa one kuzachimanga Kaye chikachapike mutu ku maulako

  • @innocentissah2636
    @innocentissah26365 ай бұрын

    Anthu adyera amakhala ndi mbalume ndikuonera chitsiru chimenechi chotchedwa Nicholas Dausi

  • @innocentchapotera7416

    @innocentchapotera7416

    5 ай бұрын

    adzafa imfa yowawa kwambiri

  • @petereliezer3795

    @petereliezer3795

    5 ай бұрын

    Osapsa mtima ndale za ku malawi ndi part of entertainment 😂

  • @patrickmasa7145

    @patrickmasa7145

    5 ай бұрын

    Uziwa et zongovela izi dausi macheza awa ahaaa kuwatengela upusa adha​@@petereliezer3795

  • @DokotalaPhungu-lk4kn
    @DokotalaPhungu-lk4kn5 ай бұрын

    Dausi kujiya kumeneko. Limbikira akupasa u minister. Udyeretu. This is your last term.

  • @InnocentKapesi-gx7yf
    @InnocentKapesi-gx7yf5 ай бұрын

    Awa ndi achitsiru kwabasi

  • @carlossadimba595
    @carlossadimba5955 ай бұрын

    That's great move Mr president and braval to Mr Dausi you are taking a good choice .....

  • @user-qh5jo5qh3b
    @user-qh5jo5qh3b5 ай бұрын

    Apm my vote

  • @EmmanuelMbilu
    @EmmanuelMbilu5 ай бұрын

    Ill never stop following him or atasitha chipani🔥💯...... He's just a vibe person 😂

  • @jacobjerome6538

    @jacobjerome6538

    5 ай бұрын

    😂😂😂😂😂😂 munthu osokoneza ngati uyu ine sindimamuonepo ayi,kuchenjela kwake koopya heavy

  • @MacDonaldkachala-cm5gc

    @MacDonaldkachala-cm5gc

    5 ай бұрын

    Dausi greatest of all times, good vibes😁😁😁

  • @towerankhoma1380

    @towerankhoma1380

    5 ай бұрын

    Ndipo inenso sindidzasiya kumukonda 😂😂😂

  • @user-jq1gy5ds9n

    @user-jq1gy5ds9n

    5 ай бұрын

    Kwambiri kumalowa chipani chabwino osati chipani chamunthu

  • @DickLinje

    @DickLinje

    4 ай бұрын

    ❤😮 of😢😢 ​@@jacobjerome6538😅😅🎉😢😅😅🎉

  • @user-oh5vs1gl4n
    @user-oh5vs1gl4n5 ай бұрын

    chisilu chimenechi ife pambuyo pa adadi

  • @NgomaRaheem

    @NgomaRaheem

    5 ай бұрын

    Ako nde wasiya kut nawe bwampini

  • @joeljere4385
    @joeljere43855 ай бұрын

    Chakwera ❤ Dausi❤

  • @smokeestery1101
    @smokeestery11015 ай бұрын

    Ukalande mcp,, DDp waikanika, sungaithe dpp ase wachepa

  • @DanielJuly-dj2ji
    @DanielJuly-dj2ji5 ай бұрын

    Dausi is too clever. Eish ! 🤐🙌

  • @HarveyMhango
    @HarveyMhango5 ай бұрын

    ❤❤❤❤ Ambwana umatha

  • @patrickmpinganjira3099
    @patrickmpinganjira30995 ай бұрын

    My man Hon. Nicholas Harry Dausi

  • @StevenPongolani-pp9by
    @StevenPongolani-pp9by5 ай бұрын

    Politics is the game of thrones

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    5 ай бұрын

    Ndipo kwambiri

  • @WilfredMathews-yl6ij
    @WilfredMathews-yl6ij5 ай бұрын

    Politics is the game of Numbers 😂😂❤

  • @GeorgeFwanthaphiri-ov4bt
    @GeorgeFwanthaphiri-ov4bt5 ай бұрын

    ❤❤❤❤❤

  • @noelcheonga8247
    @noelcheonga82475 ай бұрын

    Dausi I like this politician whether he changes side to MCP I like his character

  • @Johnfrank-gi5uc
    @Johnfrank-gi5uc5 ай бұрын

    Imeneyo ndiyo Democracy aliyense ali ndi ufulu wopita komwe akufuna ineso ndiponso ku UDF don't blame it's my rights to do so, thanks

  • @khaleedsaidi6232

    @khaleedsaidi6232

    5 ай бұрын

    Democracytu taionatu ife ndipo ndakulupilila kuti anthu a dpp analidi ademocracy ndipo anthu aja asakhala ademocracy. Nthawi ya dpp akaitana amcp kuti akhale pamonsi amakana lelo Iwo aliboma akawaitana a dpp akumabwela semene zikuoneselatu kuti dpp ndi imene imaziwa democracy ndiime phopo bwanji

  • @IbrahimWezely-qd4vj
    @IbrahimWezely-qd4vj5 ай бұрын

    Feel free this is your original party, takulanfirani madala

  • @rodglae6657
    @rodglae66575 ай бұрын

  • @josephngoliwa
    @josephngoliwa5 ай бұрын

    Hon. Dausi thank you simunanyoze Dpp and APM.. Zikomo.

  • @MatthewsPhiri-jh7zl
    @MatthewsPhiri-jh7zl5 ай бұрын

    Welcome back

  • @kha6068
    @kha60685 ай бұрын

    Abambowa ndi achitsilu chonchi kani

  • @mcbethmbewe5421
    @mcbethmbewe54215 ай бұрын

    A rolling stone gathers no moss...

  • @issahabdullah7186
    @issahabdullah71865 ай бұрын

    These Greedy politicians doesn't care for the Needy

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x5 ай бұрын

    Mbalame yokuba iyi achita Manyazi APM akulowa boma❤❤❤

  • @ulemubanda3934

    @ulemubanda3934

    5 ай бұрын

    Boma lake liti?😂😂

  • @websterkausiwa8919

    @websterkausiwa8919

    5 ай бұрын

    Zokaikisaa kwambri ku dpp kukuchitika za nsete kwambri zikundikhumudwisaa kwambri

  • @georgemmeto9722

    @georgemmeto9722

    5 ай бұрын

    Osakaika....DPP ikulowanso boma...khulupiliran anthunu

  • @user-fh3dn8kt2j

    @user-fh3dn8kt2j

    5 ай бұрын

    Never

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    4 ай бұрын

    Ndipo kwambiri 😮

  • @user-hm1bf6cw8t
    @user-hm1bf6cw8t5 ай бұрын

    Dausi ndi machine ayiseye 🔥

  • @evancenasoro922
    @evancenasoro9225 ай бұрын

    Ukatelo afuna malo ukoooo😂😂😂😂 ichiiiiii

  • @baziliobwanali4753
    @baziliobwanali47535 ай бұрын

    Keep going Dausi

  • @user-oo5bx1rl3j
    @user-oo5bx1rl3j5 ай бұрын

    Iweyo Dausi ukuganiza kuti anthu angadye stadium. Ndikupempha inuyo a MCP don't trust Dausi olo anthu akwào samàmukonda ai monga ndanenela kale kuti he is a sweet talker

  • @luciuschigoga2607

    @luciuschigoga2607

    5 ай бұрын

    Inu mmafuna anene kuti chani chomwe bomali siikudziwacho?

  • @GladysGwaza
    @GladysGwaza5 ай бұрын

    The servant of the people ( do service to the people)

  • @user-qq3ip1od6i
    @user-qq3ip1od6i5 ай бұрын

    Munthu oipaaaaa,, wadyela.. Osakonda dziko

  • @luciuschigoga2607

    @luciuschigoga2607

    5 ай бұрын

    And when he left MCP for dpp he did well neh? Wise up

  • @user-dv7ht6vn9s
    @user-dv7ht6vn9s5 ай бұрын

    Ku Mwanza samufuna uyu.... Kubisa mawanga mbuzi iyi... Fisi wachabechabe.... Sadzawinanso ku Mwanza

  • @lazaruschitsamba8394
    @lazaruschitsamba83945 ай бұрын

    no this is politics

  • @HenzelPat-vd8cz
    @HenzelPat-vd8cz5 ай бұрын

    🔥🔥🔥🔥

  • @franciscazuwawo3426
    @franciscazuwawo34265 ай бұрын

    Dausi ndikatundu 😂😂😂🙌🙌🙌

  • @user-nj3pv2wc1n
    @user-nj3pv2wc1n5 ай бұрын

    Zoona boss

  • @yamikanijames6915
    @yamikanijames69154 ай бұрын

    Welcome to MCP Mr dausi

  • @TimbaTv001
    @TimbaTv0015 ай бұрын

    Nkhope kunyasa ngati manyi

  • @JamesSaidi
    @JamesSaidi5 ай бұрын

    ineso ndikumva sugar ndima comment dpp is winning this game

  • @robertrichman9376
    @robertrichman93765 ай бұрын

    Mbuzi iyi

  • @mijerimasiye7310
    @mijerimasiye73105 ай бұрын

    Malawi walero womvetsa chisoni zedi nkhalamba zingotipusitsa zili pheeeee

  • @stevegowa7940

    @stevegowa7940

    4 ай бұрын

    😂

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg5 ай бұрын

    Dausi, Dausi, Dausi..........ayi zikomo Ambuye akuone ndithuuu.

  • @user-fh3dn8kt2j

    @user-fh3dn8kt2j

    5 ай бұрын

    😂😂😂

  • @HelvBen-sc1zu
    @HelvBen-sc1zu4 ай бұрын

    Ichi nd chitsiruuuuu

  • @user-ir5xk2sw3k
    @user-ir5xk2sw3k5 ай бұрын

    Uyu ndi swiswili uyu Dausi!

  • @user-cm5pv8dn7k
    @user-cm5pv8dn7k5 ай бұрын

    Machende ako chi nicholasi dausi omafuna udindo ku dpp mukuziwa kuti APM sakucheza ndi ana

  • @InnocentNkhonyo-rs9lq
    @InnocentNkhonyo-rs9lq5 ай бұрын

    Malawian politics

  • @TrimaMpima
    @TrimaMpima4 ай бұрын

    Yee

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i5 ай бұрын

    Olo chakwera sakumutorela kuyankhula ichichi aaaaahhh

  • @user-bg3rt8dy8u
    @user-bg3rt8dy8u4 ай бұрын

    Nice

  • @chifundokumbali-nv7fz
    @chifundokumbali-nv7fz5 ай бұрын

    Awa ngadyera

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl5 ай бұрын

    Ndausi ndi opusa kwambili

  • @chesterphiri7523

    @chesterphiri7523

    5 ай бұрын

    Why???

  • @StiveriaChikonga-rh3fi

    @StiveriaChikonga-rh3fi

    4 ай бұрын

    Ndipo ndi mbuzi yachabe chabe

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g5 ай бұрын

    🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️

  • @user-ft9ex5gy5c
    @user-ft9ex5gy5c5 ай бұрын

    Even president akuziwa Kuti ndi tambwali uyu.kuthwa pakamwa zaziiiiiii

  • @BlessingsButao-cm8sx
    @BlessingsButao-cm8sx5 ай бұрын

    All the best

  • @user-kz3ps1je1n
    @user-kz3ps1je1n5 ай бұрын

    Sadziwa chomwe amafuna uyu

  • @yamikanijames6915

    @yamikanijames6915

    4 ай бұрын

    Mwamuchosa ndiye umafuna azifinyika

  • @TamandaniMwale-sr8vd
    @TamandaniMwale-sr8vd5 ай бұрын

    Shaaaaa Kalulu

  • @kubengovender6996
    @kubengovender69965 ай бұрын

    Nonsense!!

  • @SACHAMAGIC
    @SACHAMAGIC5 ай бұрын

    Politricking at crimax

  • @MacDonaldkachala-cm5gc
    @MacDonaldkachala-cm5gc5 ай бұрын

    Dausi , leaving DPP, knowing that it's worn out and no direction, it just moving like a dragon fly, Martha😂😂😂😂

  • @AnnoyedCaptainHat-ol4dj

    @AnnoyedCaptainHat-ol4dj

    5 ай бұрын

    Koma Dausi ndi mbuzz eti

  • @backfordrowanlwazi7892

    @backfordrowanlwazi7892

    4 ай бұрын

    Mukunama mufunseni Dr Joyce Banda mpaka kuthawa mudziko muno

  • @backfordrowanlwazi7892

    @backfordrowanlwazi7892

    4 ай бұрын

    Late Nelson Chikalamba Khonje anali waku Khondowe Nkhata-Bay north anakana mai ake omubereka

  • @MacDonaldkachala-cm5gc

    @MacDonaldkachala-cm5gc

    4 ай бұрын

    You can't join your mother, it's not a choice It's by nature, you can join the party 'coz it's a choice, just because DPP it's not a party, it's Mutharikas family business that's why things are going this way, I understand it's not a problem for jobseekers, the yes bwanas 😂😂😂

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi17 сағат бұрын

    Musavotere anthu woyenda ndi mphepo ngati amenewa

  • @StiveriaChikonga-rh3fi
    @StiveriaChikonga-rh3fi4 ай бұрын

    A chitsiru awah 😎 ndiye ukuwona ngati mene wa choka ku dpp ife tikukusowa umatipasa bzy saname buzi iwe

  • @user-wi9hz8fk8i
    @user-wi9hz8fk8i5 ай бұрын

    Wakulizani Dausi makape

  • @YusuffuDaud-cs7yu
    @YusuffuDaud-cs7yu5 ай бұрын

    Monica ndiye watchena ndipatse number yako

  • @user-qe2lv3hs8q
    @user-qe2lv3hs8q5 ай бұрын

    typing....

  • @user-oe5vb2in3e
    @user-oe5vb2in3e5 ай бұрын

    Dausi abambo oputsa heavy

  • @timothylipenga8413
    @timothylipenga84135 ай бұрын

    Chi Vibe 🎉🎉

  • @ChikondiChikwakwa-if7du
    @ChikondiChikwakwa-if7du5 ай бұрын

    Kkkkkk ndale zimampangisa munthu kukhala chitsiru ndithu

  • @user-kp6ng8bc2f

    @user-kp6ng8bc2f

    5 ай бұрын

    Ichi ndi chisilu ndithu.

  • @geraldmtika7961
    @geraldmtika79614 ай бұрын

    Kodi vice anajomba this day?

  • @Phill-nh8ru
    @Phill-nh8ru5 ай бұрын

    A president akukupusitsani ameneyu wadyela mndalama uyu. Koma palibe oposa DPP pa chitukuko olo kumwamba kukudziwa mulungu ndi mboni

  • @dicksoncassim1954
    @dicksoncassim19545 ай бұрын

    Iwe ndi wa congress iwe wachita bwino kukuthothora ku mcp

  • @merviselias6230
    @merviselias62305 ай бұрын

    Tinakutulukani adausi ahule pa ndale,,😂😂😂😂

  • @user-kp6ng8bc2f
    @user-kp6ng8bc2f5 ай бұрын

    Ulibe mfundo Nicholas dausi. Iwe ndiwadyela basi palibe chimene unachita cha nzelu ku mtundu wa a Malawi. Ndiwe mbuzi ya munthu masikini weni weni

  • @madalitsoonale5338
    @madalitsoonale53385 ай бұрын

    This man is stupid, with such kind of these people thus y Malawi is going nowhere

  • @user-nm8gp1du2m
    @user-nm8gp1du2m5 ай бұрын

    Awa ndiwosokonekera awa,,, zakuziwa chimene akufuna panoyo pa moyo wawo.. Akungosokoneza Malawi

  • @user-cm7zw6pk6d
    @user-cm7zw6pk6d5 ай бұрын

    Amadyera mphotho bambo Nicolas Dausi .Amakometsa kumene kuli madyo .

  • @markmanjonjo7916
    @markmanjonjo79165 ай бұрын

    Ndima politicians ngati amenewa dxiko silingatukuke

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh5 ай бұрын

    Atha bac

  • @AmusedOffroadCar-pg5xv
    @AmusedOffroadCar-pg5xv2 ай бұрын

    Anthu oipa awa ndiko akuzuza Malawi amenewa

  • @prestonkasito1815
    @prestonkasito18155 ай бұрын

    Akuluwa

  • @chikondipound5077
    @chikondipound50775 ай бұрын

    Be careful with him he is a snake in the village not in the grass ,he did a lot of bad things during kumuzu

  • @user-hq6bk9uv4m
    @user-hq6bk9uv4m5 ай бұрын

    Kaswiri Waza ndale akamuna Eni Eni

  • @JohnNyowani
    @JohnNyowani4 ай бұрын

    Uyu ndi waboza adamuvhosa kamba kamwano osati adaphempa stadium aii

  • @user-ft9ex5gy5c
    @user-ft9ex5gy5c5 ай бұрын

    Zamanyazi mr dausi

  • @user-fg1jk4qc3r
    @user-fg1jk4qc3r5 ай бұрын

    Akufuna angwetse MCP uyu,galu wachabechabe,,, Santana ( namzikambe

  • @user-xd2uz1bh3l
    @user-xd2uz1bh3l5 ай бұрын

    Dausi watha bas. Ndipo saoloka pa ndale ai😂😂😂😂

  • @user-vp8mr5ot7q
    @user-vp8mr5ot7q5 ай бұрын

    Mbava is shame to my motherland country, Guys we must know that we gonah be same like zim

  • @user-yu3bp8yq7f
    @user-yu3bp8yq7f5 ай бұрын

    Iikuthokoza adoctor chakwers kamba kachimanga chomwe atipasa mwa admric

  • @backfordrowanlwazi7892
    @backfordrowanlwazi78924 ай бұрын

    Back to one party system

  • @MartinoAmitoni
    @MartinoAmitoni4 ай бұрын

    I suilt you Dausi

  • @user-sp3iu3rv1t
    @user-sp3iu3rv1t5 ай бұрын

    Dawusi usazaende Dela lakwathu ku zomba tizakugenda ngati kwanuko anakwanisa kumubera chakwera wakoyo carpert ifekuno tizagenda conivo

  • @warrenmwambazi8342
    @warrenmwambazi83425 ай бұрын

    Adausi tikaziwa kuti ndinu a Congress basi,

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo33045 ай бұрын

    Kkkkk tizilpa koma, we are sinners, too much lies and hypocrisy

  • @user-nx7ot6vw7k
    @user-nx7ot6vw7k5 ай бұрын

    Tell Bakiri muluzi TV

  • @user-zm4vy5rs4v
    @user-zm4vy5rs4v5 ай бұрын

    Dpp ibakhala chipani sichokhachi choti chizingolamulira tisangowona za mavuto alero kuiwala zija ankachita pitala wanuyo

  • @giftelesoni
    @giftelesoni5 ай бұрын

    Kodii mwapita kale ku mcp bwana Dausi

  • @user-jk9hm1nt7l
    @user-jk9hm1nt7l5 ай бұрын

    Mbuzi zachabechabe owombela m'manja izizi ndiye chitsilu

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem5 ай бұрын

    Iyi ndembuzi yeni yeni ndithu machende ako galu

  • @victorbanda9039

    @victorbanda9039

    5 ай бұрын

    Mpaka kutukwanatu wasiya machende abambo ako kutchula aazako

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya85775 ай бұрын

    😂Ineyo sakomenteso 😂 ndikugonva kukoma ndi makoment ndawaonawa 😂😂😂zadziwika kut dpp ndi boma basi ❤ Apm woyeeeeeeeeeee❤❤

  • @user-ee6be5kl5o

    @user-ee6be5kl5o

    5 ай бұрын

    wapanga bwino dausi kuchitaedwa ku chipani Cha dpp , akunama uyo afuna kukudyelani ndalama chenjerani nayeni ameneyo akukupusitsani ndinthila kuwili mumasokoneza kwambiri

  • @LenzoChilek

    @LenzoChilek

    5 ай бұрын

    Oyee!!!!!!!!