MCP vs DPP Cla$h? What happened at Mbowe, in Lilongwe today, 24 feb 2024
Members of the DPP (Democratic progressive Party) party have accused MCP (Malawi Congress Party) members of attacking them today and destroying their cars and other properties.
In this video, DPP National Deputy Director of Operations Hon. Levi Luwemba and Hon. Victor Musowa explain how alleged MCP thags attecked DPP supporters in Lilongwe today.
SUBSCRIBE here for more videos goo.gl/aYvIXK
Malawi videos in English and Chichewa
Пікірлер: 91
It's very unfortunate kuona izizi chikuchitika ku Malawi kuno yet pipo are suffering with hunger, economic crisis and the like. God is watching and will rescue His own pipo.
Ine ndikuonga ngati anthu angapange zimenezi eyenera kukhala anthu omutsatira Nankhumwa😢 chifukwa chomuchatsa my chipani cha DPP😢😢😢
Siianthu omusatira nankhumwa amenewa?
Ngati ndinu madolo bwanji osakalanda network yamapassport akuhagolani
Mumaziyamba alomwe pitirizani mwano muona nyenkhewe pitala agura Ina anzanu akukuphani kumangolira muziponyaso Nanu ugaru changamu patawuni
Grace Chinga anaulula kaye kuti utsogoleri uwuwu ndi wa mwazi ndi thukuta ndizimenezi Mulungu atithandize
Ambuye atithandidze, dxiko lathu la mkamka ndi uchi lija😢😢😢😢😢 lasanduka la tsabola ndi njuchi. Yoooo satana ndiolephera. Koma apolice mulikuti? Nanga malawi defence force muli kuti? Adzakhala ali makolo anu kapena akadzi anu, mudzamva bwanji😢😢😢😢
Kuno ndi ku Lilongwe panyo Mwayiwala ku Zomba
@edenngoma8214
4 ай бұрын
Zachamba izi , ayiwala momwe amazuzira anthu nthawi yomwe alimboma , amenyana okhaokha amenewo adanamizire MCP
Ndizi mene munafuna kubweresa MCP Lero mulimbe nazo koma kumeneko musama temane ayi, koma A polisi akungo yang'ana pamodzi Ndi asirikari m'mawa tu zimenezo ndi Ngozi inuso mukamapita muzi Tenga zikwanje akakupezani muzigwira m'modzi mpakana azau lure Amene wamutuma
Ana asukulu musalowerele ndale ,ndale nkanyama koipa ,nkasa song
Eeeeee zosayenda amatha bwanji kupweteka mnzawo pomwe anthu tikuvutika
DPP woyeeee
Zonsezi ndi Chilima ,potiuza tivotere kongiresi
@DngAisee
4 ай бұрын
Zoonadi ndichoncho
This boma instead of bringing development but chaos you will not going to rule again this country tibweza
Malawi😢
Ulamulilo wa mcp ndizimene timkafuna amalawi vote aythu yomwe chahta wakwiya mvula ndimenei ikusowa mudziwe yedu mcp
Anaziyamba olha ku Zomba
A mcp ndikuchenjezeni dziwani kuti tikamati Malawi Siku Lilongwe kokha. Timaona ngati dziko likulamulilidwa ndi a busa koma ichi mchinyama.achoke😢😢😢😢
Sorry guys
This aint fair for mw as acountry, where is this animality coming from?, the conclusion though
I think kufunika kuona was MCP munjila ndiye kumumenya bas zisilu Za anthu
He's the friend of Minangagwa if he wants to make onestate party this is coming from his friend munangagwa
DPP is very calculative.........
Pitani kadzilimani chifukwatu azanu omwe munawachotsa mchipani aja akuthani. Dont blame mcp ,bodza limeneli
0:43 don't include me in your nonsense 😂
Mwakhawula mufela zaeni😂😂😂😂
Malawi
Agalu a DPP athireni utsi amenewa
Sitigawa ma Sweet
Kom zosayenda yooo 😢😢😢
Iiiiiii chakwera watizuza mokwana inu muone uramuriro wachakwera.nimumene anthu afera nivula zaka zosezi kunaribe kufa ni vula.ayi uwu niuramuriro.wasataniki.chakwera.angofuna magazi.ndipo dpp oyeeeee
Kuno ku south Africa sangapange manyi amenewo ayi kuli futi kuno pipose khomo ndi khomo ndiye basop
Chilima ndiye adalondolera mavutowa
Midipiti yanu mzikapangila Ku Thyolo ndi Ku mangochi konko kwinako muphedwa nazo
akulila chan mu nthawi Yao anapha banja lose LA tambala ndi petrol bom nde angokhapidwa akudandaula chan
Futsegi
Izi tichepese zoona nkhondo imayambadi chonchi
Vuto amalawi mumasatira zinthu zimene simuzawina nazo zipani zosenzo ndizakuba zosathandidza
Km izizi mmmm sibwinoai .iiii ndio nkhondo
Dzitsilu mitumbo yanu nonse a dpp dzibwana dzimedzo mudzipangila kwanu konko ku mpanyila
Khope yonyasa
Very bad
Koma bwezela kuwawa mene anatimenyelaso DPP thawi yawo inja akukuthani mupangeso muone
Athu amenewa ayi km
Honestly mcp yalephera kukonza zinthu kwasala ndikubera anthu zosowetsa information ku immigration mcp ikuziwapo kanthu the aim yawo ndiofuna kuti anthu amene ali maiko ena athamangisidwe 2025 azavote then information izatuluka after vote izi mudziwe a Malawi amzanga,sine wandale koma pankhani iyi yachitika ku Lilongwe its part of the war instead to help poor citizens of Malawi,you send people kukaononga galimoto za anzawo what is that, pastor can't ruling the country that is big mistake,GOD watch this see you bye
A dpp mokhozeke mupangeso mukapangeso musatope
Ufela zaeni, ozavutika nfi ama 😂😂nyamundola I ndi mukazi wako
Naye ndi president lero chifukwa amapanga kampen yomweyo lero iyeyo akukanisa anzake kupanga kampen komaso akukanisa mademo chifukwa Chan galu wamunthu chimfiti wasatanic uja
SIMATHA AYI KOMA SIMUNAKOZEKE NDIYE NDIZDOVUTA MADALA
Malangalanga yapeza zochitaa
Komatu zimenezi sikulina adzakumana ndi futi chikwanje nifuti sizinga fane adzvulala
Chakwera shame on you Kodi wunali mu busa wotani Koma wuziwe mulungu si munthu akuwona zosezi atimenyera nkhondo amalawi 😭😭
@sharifmbali7240
4 ай бұрын
kunalibe chakwera ukuinu
MCP waziputa uzitsirize tibwexa
Akuchitabwino
@petersoko4283
4 ай бұрын
Ukuyala manyi😂😂
Defamation
Inuyotu Alomwe ,kuziyamba dala
Mwayiwala thawi yanu, Shipiti koza Chipani chanu Agalu Inu munya muona
Tisaope Malawi ndiwatonse Dpp ikuptira kuda phiri kasungu DDP WOYE KODI CHAKWERA ADZAPITA KUMWERA MUGWIRE MAU ANGA
KU MALAWI KULIBE CHIKONDI UDF INKAPANGA ZOMWEZI KUPHA ANTHU NTHAWI YAO, DPP NAYONSO POSACHEDWAPA IMAPHASO ANTHU , NAYONSO MCP IKUYAMBASO ZOMWEZI,VUTO NDI SANJE KU MALAWI ANTHU SAMAKONDWERA KUONA WINA AKUSANGALALA,
Inu mukudzayamba dala mku Lilongwe bwanji osakayambila kwalomwe anzanu komweko
Mpaka ugula Ina eeeee ilimpogwila etiiii tichixulaso imeneyo
Mmm nkhopeyotu ikuwonetsa kutupa muridi ready kufa etiii..komatu muzikonzekeranso za umfumu wa kumwamba..chifukwa mukuwonetsa kuti mankhwala simukumwa..pliz mukufunika kumamwa mankhwala kuti mudyelere chipani chanuchi chikawina 2025 ...anga ndi malangizo chabe..
Osawajambula anthu oyipawo bwanji zigawengazo anthu azione.
Innoyotu ndi Central
Akukhawulisani DPP...... Akanakhapa pamodzi ndi😂😂 madala wanu... Mcp UTM Moto
@user-nj5vu8cd5l
16 күн бұрын
Ndiakuba muzichenjela pa tauni
Koma mpaka kutsegula car breaking pomweposo shaaaa anthu anafasa eeeeeeh., koma yu see mtima umeneu omati tikalowa m'boma kumawapanga nkhaza anzathu ukanachepako chonde a Malawi amzanga, padzana paja DPP ndiyo inali patsogolo ndi nchitibwe wochifwamba oterewu kumawakhapa ma activist kuwagenda miyala kuwaswera galimoto zawo apolisi alipompo koma osapamgapo kanthu . Makolo dating nkhonya yobwezera kuwawa lero ndinu mawa ndi ife. Kodi tikifunapadzafe kaye mzungu kuti mw8na mkup3za polekera
Kom ndye kunapita ma car breakers2 kkkkkkkkk
Ndala zimene mwapasidwazo zokwana thumba lachimanga zaiii andalewa siyanthu
Kkkkkkk akulu awa kuwaimba mulandu nkulakwa. Anamwa mowa wambiri. Umayankhulawo ndi mowawo
Simuli m'boma ndiye Inu mukupanga chani?
Panyapanu ,tilinanu
Mmmmmm km MCP ikufuna nkhondo sopano
😂😂😂 anthu opusa inu
Abambo inu zikanakhala zamlulungu beta kuchikamwa kakau mzafela zaziko
Central mwayidziwa
Wavuta Malawi Kodi mulephela kumuthirila poison muchakudya
Munatha jauju
Alomwe Zitsilu Inu munya muona
Dpp inatha Izo mudziwe
Cakwera akufuna magazi amalawi titha ndithu afuna magazi akapereke kumidima cakwera chakwera cakwera sindife ana ako komanso udzikamwa magazi aana ako muthu oipa mtima ngati iwe sitinamuone chiyambireni mmalawi komaso ukangowina udziwe kuti khondo idzayamba wamva satana
Nkhalamba yili phee kunyumba kwake inu mwa banja lanu inuyo mkafa agogo anuwo azasamalia ana anu koma ndale ndiuchilu mkafa banja lanu lizavutika ndinu zisilu
Very bad
Mumaziyamba alomwe pitirizani mwano muona nyenkhewe pitala agura Ina anzanu akukuphani kumangolira muziponyaso Nanu ugaru changamu patawuni
@hendiemailosi7824
4 ай бұрын
Mapwala ngati alomwe iwe ndi opusa eti
@AckimKachiluwe
4 ай бұрын
You guys mufera dziko asiyeni andale azipanga zao khala ngat kumalawi ndinu achilendo bwnji zooona mukuonongesa katundu wanu choncho za ziiiiii aaaaaaaaaaaaa mbava zapezelapo mwai apo