Mpungwepungwe pa kudwala kwa Mary Chilima ''zowona mpaka 312 million''

The K311 million doesn't include medical bills, folks. It's just pocket money.

Пікірлер: 35

  • @overcomers909
    @overcomers909 Жыл бұрын

    If thats what his condition of service since he is vice president of Malawi and if your currency is devalued badly K312m malawi currency

  • @hanafi4766
    @hanafi4766 Жыл бұрын

    Chilima hemust youz money from in his pocket this politicals the don't think for athars there Sany Of davors

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 Жыл бұрын

    Eish komatu Malawi ndiye wafikadi pa worse But i curse the coming of Lazarus Chakwera God is Watching you guys 😫😫

  • @ahamadulmbishana6629
    @ahamadulmbishana6629 Жыл бұрын

    Komad ndilamayo yachuluka osangowasiya afe bwanji ndilamazo akagulile Fertiliser wadulayu

  • @robenallie6985
    @robenallie6985 Жыл бұрын

    312milion thats tonse alliance

  • @blandinabonaventure5474
    @blandinabonaventure5474 Жыл бұрын

    Iwowo salary zawo ntchito yake ndichani mmmmmm kma misokho yathu mmmmm mavuto kwambiri

  • @emmanuelweja9606
    @emmanuelweja9606 Жыл бұрын

    Kodi alibe medical aid?sagwada zomwe amuthyolazo apite ku mwai wathu hospital or Adventist ,osati zowatengera amalawi kuntoso ai

  • @JohnMatope49
    @JohnMatope49 Жыл бұрын

    Anthuwatu ali pa pikisanu and zawathu sakuwelengaso ayi

  • @blandinabonaventure5474
    @blandinabonaventure5474 Жыл бұрын

    Zitsiru zimenezi misokho yathu kma aliyese Ali ndi ufulu zikomo kwambiri mbuzi a utm nonse, +mcp tonse zipani 9 zero

  • @dijayusuf2918
    @dijayusuf2918 Жыл бұрын

    This is not fair

  • @jimmyzgambo9928
    @jimmyzgambo9928 Жыл бұрын

    Akupanga zopusa kwambiri

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 Жыл бұрын

    Zikuchita kuwoneka kuti anthuwa ndi akumazidi wotumidwa ndi satana, munthu wamzelu sungawononge ndalama yoseyi pamene athu akulila za njala, mankhwala muzipatala, kukwela kwa zinthu, feteleza, koma ndiye yah asiyeni gahena linayasama kale kudikilila anthu ankhazawa, Chilimayo malipilo ake akugwila ntchito yanji? Shame to my fellow poor Malawians

  • @alickhassan181
    @alickhassan181 Жыл бұрын

    Kalanga ine malawi ine chete🇬🇹

  • @stevinmuhone877
    @stevinmuhone877 Жыл бұрын

    Akwanilitse zimene akufuna

  • @brendadumisan2526
    @brendadumisan2526 Жыл бұрын

    Mmmmmm koma nde mwatiseweresa ife amalawi zafikapa mukutiuza kuti muzipataramo odwara ndi nkazi chilima yekha kuti muziseweresa ndarama chonchi mmalo mokonza mavuto koma mwatizunza ife amalawi Mulungu akakulangani inu

  • @chifundonkhoma3642
    @chifundonkhoma3642 Жыл бұрын

    But these are their entitlements, don't compare the amount of money to the living standards of a commoner.... Guys we need to think, asagwiritse ntchito ma entertainments awo chifukwa wina aganiza kuti a kuwononga ndalama, izi ndi chimodzi modzi kuti musawalipire ogwira ntchito m'boma chifukwa a Malawi ena omwe Sali pa ntchito akuvutika ku mudziku... Ayi it's high time we need to change thinking like idiots....

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani20 күн бұрын

    Amalawi ochuluka akungodzifera mudzipatalamu kamba kosowa mankhwala pamene boma likukhuthula ndalama dzankhaninkhani pa munthu mmodzi😢😢😢

  • @OjesYahaya-zl4rx
    @OjesYahaya-zl4rx11 күн бұрын

    Athu akumwalila zimpatalamu kamba kosowa Panado ndiye Muthu mozi ndalama zosezo kusonyeza kuti miyo yanuyo ndiye yofunikila mumwalilabe mutisiya aphawife mulungu sowona chuma

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q15 күн бұрын

    Inu chakwera niamene wamuroza kuti afe dikirani muva kuti nayeso wamwarira

  • @lawrencenoson9777
    @lawrencenoson9777 Жыл бұрын

    Mbola Kwantele boma

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q15 күн бұрын

    Musiyeni akwere ndege agwe naye afeso ngati chakwera wamuloza kaziyo.kuti apite

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Жыл бұрын

    No sense full

  • @eranivesailesi9982

    @eranivesailesi9982

    Жыл бұрын

    Masewela eni eni awa

  • @customer4784
    @customer4784 Жыл бұрын

    Mukuononga ma millions koma kukanika kutsitsa mtengo wa fertilizer....😩

  • @charlesmuyaya8839
    @charlesmuyaya8839 Жыл бұрын

    Iwe voice yako si yabwino, ma videos akonso umawapanga mopusa. No interesting at all

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem2 ай бұрын

    Ai zikomo Mulungu azikuonani

  • @henzomanzo9158
    @henzomanzo9158 Жыл бұрын

    That's bull sh*t

  • @dysonmbizi9734
    @dysonmbizi9734 Жыл бұрын

    Wanthu wanyakhe wonjoya mchalo muno mweee mmmm

  • @roybanda5905

    @roybanda5905

    Жыл бұрын

    Ndipo wazala

  • @roybanda5905

    @roybanda5905

    Жыл бұрын

    Ndipo wazala

  • @user-rx2oh3rj7p

    @user-rx2oh3rj7p

    11 күн бұрын

    Kkkkkk hahahaha

  • @bonifacekanyinji2517
    @bonifacekanyinji2517 Жыл бұрын

    Yemwe azavotere chilima ndi chule

  • @hanifamw

    @hanifamw

    Жыл бұрын

    iiiii zomwezi lol