Kodi alibe medical aid?sagwada zomwe amuthyolazo apite ku mwai wathu hospital or Adventist ,osati zowatengera amalawi kuntoso ai
@JohnMatope49 Жыл бұрын
Anthuwatu ali pa pikisanu and zawathu sakuwelengaso ayi
@blandinabonaventure5474 Жыл бұрын
Zitsiru zimenezi misokho yathu kma aliyese Ali ndi ufulu zikomo kwambiri mbuzi a utm nonse, +mcp tonse zipani 9 zero
@dijayusuf2918 Жыл бұрын
This is not fair
@jimmyzgambo9928 Жыл бұрын
Akupanga zopusa kwambiri
@princedetbozsmallboy1749 Жыл бұрын
Zikuchita kuwoneka kuti anthuwa ndi akumazidi wotumidwa ndi satana, munthu wamzelu sungawononge ndalama yoseyi pamene athu akulila za njala, mankhwala muzipatala, kukwela kwa zinthu, feteleza, koma ndiye yah asiyeni gahena linayasama kale kudikilila anthu ankhazawa, Chilimayo malipilo ake akugwila ntchito yanji? Shame to my fellow poor Malawians
@alickhassan181 Жыл бұрын
Kalanga ine malawi ine chete🇬🇹
@stevinmuhone877 Жыл бұрын
Akwanilitse zimene akufuna
@brendadumisan2526 Жыл бұрын
Mmmmmm koma nde mwatiseweresa ife amalawi zafikapa mukutiuza kuti muzipataramo odwara ndi nkazi chilima yekha kuti muziseweresa ndarama chonchi mmalo mokonza mavuto koma mwatizunza ife amalawi Mulungu akakulangani inu
@chifundonkhoma3642 Жыл бұрын
But these are their entitlements, don't compare the amount of money to the living standards of a commoner.... Guys we need to think, asagwiritse ntchito ma entertainments awo chifukwa wina aganiza kuti a kuwononga ndalama, izi ndi chimodzi modzi kuti musawalipire ogwira ntchito m'boma chifukwa a Malawi ena omwe Sali pa ntchito akuvutika ku mudziku... Ayi it's high time we need to change thinking like idiots....
Пікірлер: 35
If thats what his condition of service since he is vice president of Malawi and if your currency is devalued badly K312m malawi currency
Chilima hemust youz money from in his pocket this politicals the don't think for athars there Sany Of davors
Eish komatu Malawi ndiye wafikadi pa worse But i curse the coming of Lazarus Chakwera God is Watching you guys 😫😫
Komad ndilamayo yachuluka osangowasiya afe bwanji ndilamazo akagulile Fertiliser wadulayu
312milion thats tonse alliance
Iwowo salary zawo ntchito yake ndichani mmmmmm kma misokho yathu mmmmm mavuto kwambiri
Kodi alibe medical aid?sagwada zomwe amuthyolazo apite ku mwai wathu hospital or Adventist ,osati zowatengera amalawi kuntoso ai
Anthuwatu ali pa pikisanu and zawathu sakuwelengaso ayi
Zitsiru zimenezi misokho yathu kma aliyese Ali ndi ufulu zikomo kwambiri mbuzi a utm nonse, +mcp tonse zipani 9 zero
This is not fair
Akupanga zopusa kwambiri
Zikuchita kuwoneka kuti anthuwa ndi akumazidi wotumidwa ndi satana, munthu wamzelu sungawononge ndalama yoseyi pamene athu akulila za njala, mankhwala muzipatala, kukwela kwa zinthu, feteleza, koma ndiye yah asiyeni gahena linayasama kale kudikilila anthu ankhazawa, Chilimayo malipilo ake akugwila ntchito yanji? Shame to my fellow poor Malawians
Kalanga ine malawi ine chete🇬🇹
Akwanilitse zimene akufuna
Mmmmmm koma nde mwatiseweresa ife amalawi zafikapa mukutiuza kuti muzipataramo odwara ndi nkazi chilima yekha kuti muziseweresa ndarama chonchi mmalo mokonza mavuto koma mwatizunza ife amalawi Mulungu akakulangani inu
But these are their entitlements, don't compare the amount of money to the living standards of a commoner.... Guys we need to think, asagwiritse ntchito ma entertainments awo chifukwa wina aganiza kuti a kuwononga ndalama, izi ndi chimodzi modzi kuti musawalipire ogwira ntchito m'boma chifukwa a Malawi ena omwe Sali pa ntchito akuvutika ku mudziku... Ayi it's high time we need to change thinking like idiots....
Amalawi ochuluka akungodzifera mudzipatalamu kamba kosowa mankhwala pamene boma likukhuthula ndalama dzankhaninkhani pa munthu mmodzi😢😢😢
Athu akumwalila zimpatalamu kamba kosowa Panado ndiye Muthu mozi ndalama zosezo kusonyeza kuti miyo yanuyo ndiye yofunikila mumwalilabe mutisiya aphawife mulungu sowona chuma
Inu chakwera niamene wamuroza kuti afe dikirani muva kuti nayeso wamwarira
Mbola Kwantele boma
Musiyeni akwere ndege agwe naye afeso ngati chakwera wamuloza kaziyo.kuti apite
No sense full
@eranivesailesi9982
Жыл бұрын
Masewela eni eni awa
Mukuononga ma millions koma kukanika kutsitsa mtengo wa fertilizer....😩
Iwe voice yako si yabwino, ma videos akonso umawapanga mopusa. No interesting at all
Ai zikomo Mulungu azikuonani
That's bull sh*t
Wanthu wanyakhe wonjoya mchalo muno mweee mmmm
@roybanda5905
Жыл бұрын
Ndipo wazala
@roybanda5905
Жыл бұрын
Ndipo wazala
@user-rx2oh3rj7p
11 күн бұрын
Kkkkkk hahahaha
Yemwe azavotere chilima ndi chule
@hanifamw
Жыл бұрын
iiiii zomwezi lol