Man of God do not give up go ahead ngakhale mwamangidwa kuno kudziko musataye mtima ku umzimu ndinu omasulidwa 🙏
@Musa1828-l5d5 күн бұрын
Kaya Chakwera alamulira moyo wake onse koma chilungamo mchakuti wapha Chilima wapha munthu amene anamuthandiza kukhala president 💔💔💔💔
@Hong_sing
4 күн бұрын
Exactly osamati adziwa ndi mulungu yenkha chilichonse ai ifeso anthu timadxiwa timaopa kumagwidwa kapena 2025 kukamvotela ku maula ndinthu 😅😅😅
@MosesNyalugwe-ll8hh
3 күн бұрын
Osayiwaranxo miya
@MosesNyalugwe-ll8hh
3 күн бұрын
Osayiwaranxo miya
@henryibrahimsailes46385 күн бұрын
Aaa inu apolice ndi zitsiru kwambiri mumanga bwanji munthu osalakwa,kodi mukutenga ngati dziko ndi malamulo ali mmanja mwanu bwanji,kodi satana wanu chakwera akukupatsani zingati kuti muzikazunza anthu chonchi mukubwereza ulamuliro wachipani chimodzi wa kamuzu komatu ulendo zofuna zanu sizitheka chifukwa anthu tinatseguka mmaso ndipo izi mukupangazi malipiro ake nanu muwaona sikalenso ayi anthu opusa inu muphe ndi kumanga amalawi tonse if you can evils 😈
@cynthiakananji1608
5 күн бұрын
A police ndi abale anthu,Koma akupangidwa force kut azigwira ntchito yausatanayi
@user-xx4jb9se3z5 күн бұрын
Choonadi chimamasula anthu sachifuna chilungamo God is with you pastor nanga akatolika aja .uja adati mwagawana zovala zake.zazii.apolice alibe zochita Haas mcp woyeer 2025
@user-pv9uk6sc3w5 күн бұрын
Chakwera akungopitiliza kupeleka mkwiyo kwa a Malawi, anthu ndi okwiya kale ndi ulamuliro wa MCP ndi chakwera. Asamange anthu chonchi.
@user-hq6dq7zr1e5 күн бұрын
Chowamangila anthuwocho,nde kuti zoona wapha ndiye.akanakhala kuti sanaphe ndiye akanangokhala chete ndikuuza ntundu wa a malawi zoona zeni zeni
@Imtiyazkalikodole5 күн бұрын
Anakati aziyakhura Chichewa kapena English
@ulemujumbe85015 күн бұрын
Tsono watukwana ndani kuti mpaka amumange ????
@meeksonmkhala5 күн бұрын
This makes sense Sir, why MCP police???? Siku lina tizakuukiran muzathawa
Police sono yanyanyisa esh there is no reason kut amumange uyuyu
@LeendaDeborah20055 күн бұрын
Komatu nde mumanga ndi azungu omwe. Cos enanso akuyankhula zokuti ndegeyi mudaipangila plan kuti igwe
@ceciliathole5 күн бұрын
Mulungu si analume for tipemphele kuti mutuluke abusa chilungamo chimamasula
@user-ig9qk6gi6g5 күн бұрын
This pastor was saying the truth. Why mu kumumanga?
@thulanimpphiri68735 күн бұрын
Ine pamene ndavera audio ya busa anga cholakwa sindikuchiona. Ngati aboma or kalaya mayi yolamu akuti ndege inafika ku mzuzu apereke umboni kuti tipeze ngati abusa ndiwolakwa ndege kusowa 10 o'clock kufufuza kuziwisa 4 o'clock mmm ndiye muzimanga anthu wu police munaphuzira kuti wopanda nawo zeru
@dysonmsamba57784 күн бұрын
KOMA NGATI MULI NDI INFORMATION INA YAKE MUKAWAUZE A POLICE KAPENA ANY EMBASSY THAN KU POSITA IZI CHOMWE MUNGADZIWE MUKHOZA KUYAMBA KUMENYANA OPANDA CHIFUKWA CHENICHENI NONSE MUUPEZE MNTIMA
@CHIWSABINYAMBOSE5 күн бұрын
Chapha chilima chachakwerachi mfiti
@AchinaKellz4 күн бұрын
Kwacha Kwacha basi😂
@HsjsmzmHsjsnsjaja5 күн бұрын
Ndiye mumanga angati
@BlessMnyenyembe5 күн бұрын
Mulimosemo kumeneko chilungamo chioneke
@jomochirwa5 күн бұрын
Njee wamangidwa chonchi basi ?
@RhodneyBwa34 күн бұрын
Angomuttulusa mwaulemu
@SamuelMthengo5 күн бұрын
Kodi ufulu omwe timaukondwelera uja uli kuti?why are we still moving backward?
@user-mj2te7vl6p5 күн бұрын
Chakwera anapha chilima
@isaacchirwa95185 күн бұрын
Thanks you for arresting him, akanene bwino komanso akapereke dzina la police yemwe anamuuza kuti palivi zoti ndege ya vice president ikubwera ku mzuzu
😅😅😅😅😅 imwe mwaneneska ka mubusa nayo vikamukhuza nivi va ndege
@user-rm2xv8ys1i5 күн бұрын
Ineso ninamva same thing abusa anthu muwatuluse pls
@sinoiajamu94845 күн бұрын
Same thing is Wrong ndiboma, pamalilo people are free to say what ever they fell why arresting them government did you do anything on SKC if not stop this nonsense,MCP don't bring Kamuzu lifestyle to us
Palije apo chifukwa chakumangira mnthu mmalo mwakuti mlimbane namasuzgo ayo yali mumalawi imwe bizy wa mcp kukoma wanthu mwezi uno pera mwakoma wanthu 10 nakuyamba kukaka wanthu pala wamuzuzulani mapoli mose mlije no zeru yyi vimavi vinu this is no one party system this is democracy" how many people u need to kill?
@user-nv3rf7bl7r
5 күн бұрын
Imwe namwe zeru mulije mukuwa nga ndimwe wachewa kutinangila mutundu chaa ise wanthu wala wslikufwa kwithu ku mzuzu wakawa wa mcp
@user-nv3rf7bl7r
5 күн бұрын
Iye muliska va ndege vikamukhuza niviii ndiwo wakuwa waliska waboza awa wanyawo wakuwa busy kupemphelela malawi kuti muwe mutende iyo walibusy namilandu nawanthu wachita makola kumumanga wakayowoye chilungamo
Пікірлер: 73
Azibusa ambiri adzuka tsono mumanga ambiri kmso kupalamura mkwiyo wa mulungu.
Man of God do not give up go ahead ngakhale mwamangidwa kuno kudziko musataye mtima ku umzimu ndinu omasulidwa 🙏
Kaya Chakwera alamulira moyo wake onse koma chilungamo mchakuti wapha Chilima wapha munthu amene anamuthandiza kukhala president 💔💔💔💔
@Hong_sing
4 күн бұрын
Exactly osamati adziwa ndi mulungu yenkha chilichonse ai ifeso anthu timadxiwa timaopa kumagwidwa kapena 2025 kukamvotela ku maula ndinthu 😅😅😅
@MosesNyalugwe-ll8hh
3 күн бұрын
Osayiwaranxo miya
@MosesNyalugwe-ll8hh
3 күн бұрын
Osayiwaranxo miya
Aaa inu apolice ndi zitsiru kwambiri mumanga bwanji munthu osalakwa,kodi mukutenga ngati dziko ndi malamulo ali mmanja mwanu bwanji,kodi satana wanu chakwera akukupatsani zingati kuti muzikazunza anthu chonchi mukubwereza ulamuliro wachipani chimodzi wa kamuzu komatu ulendo zofuna zanu sizitheka chifukwa anthu tinatseguka mmaso ndipo izi mukupangazi malipiro ake nanu muwaona sikalenso ayi anthu opusa inu muphe ndi kumanga amalawi tonse if you can evils 😈
@cynthiakananji1608
5 күн бұрын
A police ndi abale anthu,Koma akupangidwa force kut azigwira ntchito yausatanayi
Choonadi chimamasula anthu sachifuna chilungamo God is with you pastor nanga akatolika aja .uja adati mwagawana zovala zake.zazii.apolice alibe zochita Haas mcp woyeer 2025
Chakwera akungopitiliza kupeleka mkwiyo kwa a Malawi, anthu ndi okwiya kale ndi ulamuliro wa MCP ndi chakwera. Asamange anthu chonchi.
Chowamangila anthuwocho,nde kuti zoona wapha ndiye.akanakhala kuti sanaphe ndiye akanangokhala chete ndikuuza ntundu wa a malawi zoona zeni zeni
Anakati aziyakhura Chichewa kapena English
Tsono watukwana ndani kuti mpaka amumange ????
This makes sense Sir, why MCP police???? Siku lina tizakuukiran muzathawa
Apolice nanuso ndinu zitsiru ,,,,chakwera chilima unamupha ndiweyo
Good voice
Khaniyiyi or ayipinda kaya kuopseza anthu zoona zake ndizoti athu aja ana chita kuphedwa Ngati sizoona akumangilanji anthu
@user-nv3rf7bl7r
5 күн бұрын
Akuwamanga kuti akapelekele umboni mesa iwo alinawo
Nothing but the truth was spoken here
@GreshamKadzembe-tn8cq
5 күн бұрын
Chilungamo chomwe wanenacho nkana amutenga kuti akaperekere ku police umboniwo, ndi umboni okwanira
This audio is for Kamlepo kalua can you share the audio of the pastor
Mumakwana big pamoza ndi DC tili pambuyo panu
Chilungamo mchimenecho palibe nkhani yowamangira akunena zimene akudziwa km panja ukankhala olakwa umafuna umboni udzibisika anthu atopa nanu anthu 9 pakamodzi ai mudaonjenza tulanidi pansi udindo bwanji kd anthu amamwalira ochuluka pa ulamuliro onkhaonkha wa mcp ena ifanzo zimankhala kt?
prophet liabunya wanena kuti chakwera ali crean sakukhusidwa ndi imfa ya chilima. n wanena kuti 2025 azawinaso . mnya alomwe mwauponda
All of us are angry 😡😡😡😡😡😡😡😡😡😡😡
Kodi mukufuna muzinamiza anthu Mesa imeneyo ndi voice ya kamulepu ndiye inu mukuti ya M'busa
😮sorry a Malawi ino indiyo nthawi yosiliza okamba choonandi sazapeza mtendere ndi dziko lapatsi bible ikutelo
This is not a bad voice
Jipangeni respect mwekha kuyowoya nge wana yayi, wana wasambizgeni makola
@user-nt4fr2le3f
4 күн бұрын
Iwe ndiwe ukulemba nge ndiwe mwana,chifukwa icho walemba uchimanya yay
@user-ms8tm3yf7d
3 күн бұрын
Imwe namwe ndiwe wachindere munthu waleke kuyowoya uwo mbunenesyo kupusa kwako iwe mumalenge mosi nthena na Boma ili mukuona yayi likukoma wanthu mwe mukopha
Ndingomva ngat nditukwane mwina mtima undiphwa chakwera asandiyakhulise pa mbali
Mr chakwera sinu amuyaya PA zomwe mukuchita
Ndipo chakwela waputa m,kwiyo wa mulungu kumanga azibusa ndiwe otembeleledwa ndi nduna zako
Achakwera mizimu yakwiya olo mutawamanga onse amene akulakhulawa koma akasiya anthu wa kulakhula Mlungu adzutsa myala kuti ilakhule za imfa ya Chilima
Kodi zikukhala bwanji voice imeneyi ndiyomweso anamangidwa nayoso Akamlepo Kalua ,? Ndiye koma atumbuka onse samangidwa
Nanunso apolice mwasowa zochita, mumangatu ndye amalawi onse hiyaaa osangozitsiya bwanji? Akukulipirani ma million angati?
Wayankhula chizungu chakumpoto amvana okhaokha
Choti muziwe dziko lino ndi la demokilase mphamvu ZOMWE muli manasozo tsiku lina sizatha ndie NDI pamene musalimve dziko kununkha agalu anu
Remember Bingu atakangana ndi Synod ,mkumanga anthu akupeleka maganizo awo inuyo ngat muli ndi umbon tiwuzen,munthu mwamuchita tintin Chakwera wopusa kwambiri
Kwachema akutapa.
Boma likupindukanji pomanga anthu amene AKULIRA MOBANGULA ?
Tonse alliance osawopa logo
Police sono yanyanyisa esh there is no reason kut amumange uyuyu
Komatu nde mumanga ndi azungu omwe. Cos enanso akuyankhula zokuti ndegeyi mudaipangila plan kuti igwe
Mulungu si analume for tipemphele kuti mutuluke abusa chilungamo chimamasula
This pastor was saying the truth. Why mu kumumanga?
Ine pamene ndavera audio ya busa anga cholakwa sindikuchiona. Ngati aboma or kalaya mayi yolamu akuti ndege inafika ku mzuzu apereke umboni kuti tipeze ngati abusa ndiwolakwa ndege kusowa 10 o'clock kufufuza kuziwisa 4 o'clock mmm ndiye muzimanga anthu wu police munaphuzira kuti wopanda nawo zeru
KOMA NGATI MULI NDI INFORMATION INA YAKE MUKAWAUZE A POLICE KAPENA ANY EMBASSY THAN KU POSITA IZI CHOMWE MUNGADZIWE MUKHOZA KUYAMBA KUMENYANA OPANDA CHIFUKWA CHENICHENI NONSE MUUPEZE MNTIMA
Chapha chilima chachakwerachi mfiti
Kwacha Kwacha basi😂
Ndiye mumanga angati
Mulimosemo kumeneko chilungamo chioneke
Njee wamangidwa chonchi basi ?
Angomuttulusa mwaulemu
Kodi ufulu omwe timaukondwelera uja uli kuti?why are we still moving backward?
Chakwera anapha chilima
Thanks you for arresting him, akanene bwino komanso akapereke dzina la police yemwe anamuuza kuti palivi zoti ndege ya vice president ikubwera ku mzuzu
Aaaaaa that's why kuzolozolo wanambembe muchalitchi
@user-nv3rf7bl7r
5 күн бұрын
😅😅😅😅😅 imwe mwaneneska ka mubusa nayo vikamukhuza nivi va ndege
Ineso ninamva same thing abusa anthu muwatuluse pls
Same thing is Wrong ndiboma, pamalilo people are free to say what ever they fell why arresting them government did you do anything on SKC if not stop this nonsense,MCP don't bring Kamuzu lifestyle to us
Police yakumalawi kupusa ndchifukwa mukumafa muli amphawi shit
Sorry abusa chakwera azafa chagada
M c p chimpani cha magazi
Mlw so bad
Palije apo chifukwa chakumangira mnthu mmalo mwakuti mlimbane namasuzgo ayo yali mumalawi imwe bizy wa mcp kukoma wanthu mwezi uno pera mwakoma wanthu 10 nakuyamba kukaka wanthu pala wamuzuzulani mapoli mose mlije no zeru yyi vimavi vinu this is no one party system this is democracy" how many people u need to kill?
@user-nv3rf7bl7r
5 күн бұрын
Imwe namwe zeru mulije mukuwa nga ndimwe wachewa kutinangila mutundu chaa ise wanthu wala wslikufwa kwithu ku mzuzu wakawa wa mcp
@user-nv3rf7bl7r
5 күн бұрын
Iye muliska va ndege vikamukhuza niviii ndiwo wakuwa waliska waboza awa wanyawo wakuwa busy kupemphelela malawi kuti muwe mutende iyo walibusy namilandu nawanthu wachita makola kumumanga wakayowoye chilungamo