Ineyo a Limpompo fm ndili pa mbuyo pano ❤❤❤❤❤ mumatiuza zoona ndithu
@FazilCastin23 күн бұрын
Ine Langa ndi Funso Kwa inu Mr ntanyiwa Kodi Radio yanuyi imafikira anthu akumudzi. Chifukwa enafe tili ndi mwayi womvera komanso tili moyenda Monga out off country. Chifukwa akumudzi ndi amene akufunika Kuti adzidzitsata komanso ndi amene Anga Vote
@VeronicaChirwa-ct4os
23 күн бұрын
Zoonadi akumudzi akufunika azizidziwa chilungamo cheni-cheni. Ndi amene amathamanga kukavota.
@Vwalavwata
21 күн бұрын
Ndipo ndimaisata kwambiri radio imeneyi from Malawi mzimba
@JeanBanda-zy6wu23 күн бұрын
Koma a chakwela mukuwoneka mulibe mtendere ndipo simunati mzimu wa munthu ndiwoopsa soseji mukuimva kunyung''unyatu ngati madimu musova😂😂
@MarthaMbewe-uk5nn23 күн бұрын
A UTM mukalola manyiwo musalamo nokha mu mgwilizano wanuwo ife zikwangwani talodza kale ku DPP mutsalanaye RUTO wanuyo
@user-do2cs8nf4b23 күн бұрын
Kkkkkkk koma apatu misala yayambika😂muziwona munakhetsa mwazi wa anthu osalakwa
@Stewartchikoja23 күн бұрын
Respect sibonda
@MaxWell-d7o
23 күн бұрын
Ine sindipitako
@BlessingKimu-yk8uj23 күн бұрын
Moto wachilungamo tilinanu limodzi ifemso before amthu tikudziwa amthu okudana ndi chilungamo.
Respect you Ntanyiwa Kumulakwira Chilima ndiena onse anafela mundege😢😢😢
@user-ny3it3jp9l23 күн бұрын
Lipopo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ fire 🔥
@georgesmart379122 күн бұрын
Kutha kwa Shasha... Apm 2025❤❤❤❤
@user-mh7cc8up4i20 күн бұрын
Zinakanika kukambilana naye chilima chifukwa amaziwakuti chilima ndimuthu wachilungamo koma ngakhale mwamumpha zimu wa chilima ulamula ziko lamalawi ngakhale anachoka pakatipathu koma muchisomo chamulungu tilamulidwa ndi chilima S K C still I remember you 💔💔😭😭😭
@MandalaChaona22 күн бұрын
Koma Malawi Chikangawa Party ikusavuka sinati . Mimbulu yoyipa iyi, Mwazi wa anthu osalakwa ukupengesani. Tiye nawo Mchimwene NTANYIWA kuwayika pambalambanda basi.
@Vwalavwata21 күн бұрын
A khristu a CCAP ena ndi opusa amangosapota zilizonse even akuiziwa kuti akuzipereka yekha kwazigawenga kuti zimuphe
Ubwino wake mgwilizano anthu anavota zaka 5 nde zaka 5 zikatha anthu akavotanso sikuti avotelanso alliance ayi akavotela kumene akufuna kaya avotela DPP kaya avotela AFORD kaya MCP kaya UTM sikuti akavotela alliance
@user-pp6kf6vu2y22 күн бұрын
Nyimbo yu tigairen inu❤❤
@mathewsmbaluko852223 күн бұрын
Zikachitika timvela kwainu ❤❤
@cacksygustarf626023 күн бұрын
Ntanyiwa❤
@Mrssamalanngwira23 күн бұрын
Limpopo ❤❤❤❤ 🔥
@user-vw7tj2ss3l23 күн бұрын
Mbiri yoipa mpaka kale kale
@FocusGeorge-qz4sh23 күн бұрын
Yomweyo chikangawa
@InnocentNitamanMilanzi4 күн бұрын
Ngati zinali zonama kuti anapha chilima nchifukwa chani akumamanga anthu kodi nkhani yokunamizira umalimbana nayo?ndikunama ndi iwe sataniki chilima anthu azifa ndi nhlaka chifukwa cha iwe
@GeraldChisokeza-er5cf23 күн бұрын
Zilungamo zokhazokha
@UsenLashid23 күн бұрын
What is that Kuti anthu akasiye matelefone uyaluka galu iwe Sunati mulungu wathu wanthu ndi wa Moyo amene anafafaniza aiguputo ndipo Lero mulungu wemweyo akufuna kufafaniza chakwela ndi chipani chake zichitike mulungu wanthu wa Moyo timakudalilani sitimadalila chakwela Ayi zichitike mudzina la yesu khristu nanuso azibusa muzayankha mulandu Kwa mulungu
@Jamesmwale-iz4ri23 күн бұрын
Koma muti nichani
@giftwankhama991423 күн бұрын
Comrade mumatha.
@user-eh1mg3ww6d23 күн бұрын
Koma chakwela sutizamuiwala ndithu muchita kusowa chiyakhula mmm ndipo watikwana
@HalisonSolomon19 күн бұрын
KUYALUKA BOMA LA MCP KUSAFUNA KUVOMEREZA KUTI ZAWAVUTA
To honest this government it's full or shit n evil....munthu ukamayandikil kumwalira sunvaa kapena ndinene kut mbuzi ikakondwa amalonda Ali pafupi.....tionana nthawi yovotaa
@JackNagoli23 күн бұрын
Km guys mukutinyamula 🎉
@user-sm8gx4vf1v23 күн бұрын
Mafumu ena alibe fone aku ntcheu adziwa bwanji nanga
@SamukLungu-zg7fl23 күн бұрын
Kurikwabwino akhirisithu apite koma ma phone awo aka wayike since azika record zose chifukwa ngati sapita sitiziwakuti akufuna kurapachani
@mellipherjohn715823 күн бұрын
Limpopo moto kut buuuuuu🎉🎉
@MosesKalenge22 күн бұрын
📺📡❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤👑
@vincentbarnes587222 күн бұрын
Sitikufuna DPP, MCP, UDF kapena PP ayi. Tikufuna kupitiliza vision ndi passion ya Dr Saulos Klaus Chilima with UTM basi. The grace of God is upon UTM party
@DanielJuwawo23 күн бұрын
Mantha kwambir
@GraceZumazuma23 күн бұрын
Ali ndi tsoka chikangawa ndi banja lake mpaka kufikila m'bado wake wa chi 4 otembeleledwa ulibe mwai
@MarthaMbewe-uk5nn23 күн бұрын
Koma ameneyu GALU kwambiri wamiyitana ndani NYANI ameneyo apite akapemphere ku Assembles kwake komweko GALUUUU!
Пікірлер: 95
Ineyo a Limpompo fm ndili pa mbuyo pano ❤❤❤❤❤ mumatiuza zoona ndithu
Ine Langa ndi Funso Kwa inu Mr ntanyiwa Kodi Radio yanuyi imafikira anthu akumudzi. Chifukwa enafe tili ndi mwayi womvera komanso tili moyenda Monga out off country. Chifukwa akumudzi ndi amene akufunika Kuti adzidzitsata komanso ndi amene Anga Vote
@VeronicaChirwa-ct4os
23 күн бұрын
Zoonadi akumudzi akufunika azizidziwa chilungamo cheni-cheni. Ndi amene amathamanga kukavota.
@Vwalavwata
21 күн бұрын
Ndipo ndimaisata kwambiri radio imeneyi from Malawi mzimba
Koma a chakwela mukuwoneka mulibe mtendere ndipo simunati mzimu wa munthu ndiwoopsa soseji mukuimva kunyung''unyatu ngati madimu musova😂😂
A UTM mukalola manyiwo musalamo nokha mu mgwilizano wanuwo ife zikwangwani talodza kale ku DPP mutsalanaye RUTO wanuyo
Kkkkkkk koma apatu misala yayambika😂muziwona munakhetsa mwazi wa anthu osalakwa
Respect sibonda
@MaxWell-d7o
23 күн бұрын
Ine sindipitako
Moto wachilungamo tilinanu limodzi ifemso before amthu tikudziwa amthu okudana ndi chilungamo.
Jumah Mubarak. Our beloved Ntanyiwa ❤ freedom fighter 💪
Respect you Ntanyiwa Kumulakwira Chilima ndiena onse anafela mundege😢😢😢
Lipopo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ fire 🔥
Kutha kwa Shasha... Apm 2025❤❤❤❤
Zinakanika kukambilana naye chilima chifukwa amaziwakuti chilima ndimuthu wachilungamo koma ngakhale mwamumpha zimu wa chilima ulamula ziko lamalawi ngakhale anachoka pakatipathu koma muchisomo chamulungu tilamulidwa ndi chilima S K C still I remember you 💔💔😭😭😭
Koma Malawi Chikangawa Party ikusavuka sinati . Mimbulu yoyipa iyi, Mwazi wa anthu osalakwa ukupengesani. Tiye nawo Mchimwene NTANYIWA kuwayika pambalambanda basi.
A khristu a CCAP ena ndi opusa amangosapota zilizonse even akuiziwa kuti akuzipereka yekha kwazigawenga kuti zimuphe
Limpopoooooooooo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Mtanyiwwa ulemu wanuw bassi mulungu ationesa nkena kalikose iyyemwini ankubissa bwanj mulungu atiphasa nkuwona shoonad 🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa ndi dolo kwambiri uyu akhalise Malawi.
Inu mahule chokani sindinu mulungu muziona 2025 komaso iwe chakwela usamati uzafela mbendela ya Malawi Ayi iwe uzafela tambala wakuda osati frug ya malawi Ayi
Km atanyiwa ndi kachilombo paka fukufuku kkkkkkk
Adamphadi Muthu uja basi palibeso kukanika konse 😭😭mcp chipani chakupha
Limpopo oyeee
Ndipo azibusa ambiri atayadi chilungamo..kukhala osauka mpimgo siukuwerengera. Mpake alibusy kusaka chikwamq.. rip chilima
Limpopo fm listening from Botswana comred number one
@JeremiahKainga-rm2np
22 күн бұрын
😅😅😅 2:14 2:16 2:17 😅😅 2:23 2:25 2:29 2:36 has been 2:41 2:42 2:43 2:44 2:44 2:46 2:48 2:49 😅 3:04 3:07 3:07 3:09 3:09 2 3:10 3:11 3:11 3:13 your 3:16 3:17 😊 3:19 3:20 9 3:23 3:2 6:31 6:40 6:51 7:02 7:02 7:10 7:12 7:17 7:18 7:18 7:19 8 5:45 😅 5:55 5:57 6:01 6:02 ,, 6:06 , 6:13 6:13 6:28 6:30 3:32 3:34 99😅 5:25 5:25 😅 5:44 3:50 3:51 3:54 3:56 😅 4:59 :38 2:39 2:41
@JeremiahKainga-rm2np
22 күн бұрын
7:37 7:37
@JeremiahKainga-rm2np
22 күн бұрын
African 9
@JeremiahKainga-rm2np
22 күн бұрын
What 😮
@JeremiahKainga-rm2np
22 күн бұрын
😊😊😊😊and
Sadly, we've moved from having men of God to men of gold.😮😮
Apa yalimba nkandilo basi, ma plan onse kumangopanga ngati openga Mulungu atachotsa nzeru.
Ndiye mwati chikangawa ikupita kukalapa ndiye anthu asatenge ma phone mm anagula ndiyeyo kkkk koma misala yayambika basi 😂😂😂
Mai gotani Hala amachindana ndi mkulu wanga
@JosephMaduka-i9s
23 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@sammynkata5461
21 күн бұрын
Ing'alule basi ķkkk
@Hellenistic109
20 күн бұрын
Kkkkkkkkkiest
Akuyopa chani galu ameneyu pothimitsa malamya
Mulungu ndimboni pagwilizano wa tose Koma ngati chinali chiwembu ine ndikunena kuti mulungu abwezela chiwembu mboni dzilipo ndipo zinalakhula ndale amapanga usiku onsakhala masana mpepa azisogoleli tiyeni tiziopa mulungu amaona dzose
💪 tiyeni timenyele ufulu ziko lathu Mr mtanyiwa
😂😂😂😂 kma ku malawi kwafikapo
Kwawilira mafon timayankha uku tikuva mawu amulungu nde buzi yachabechabe akati Fon izime whay kapena akupita ndi poyison mwina akufuna akatinthemo anthuwo mkachisimo iiiii mayooo munthuyutu watsala pang'ono kufa kapena zimu wa chilima ukumutsata ndiye akuwonagati kutseka zitseko zimuwo sumupeza iiiii kkkk atate mwayambatu kuvetsa chisoni iiiii kkkk
Respect you
Ma mfumu akuntcheu chilima sanayikidwe Ku start house Ayi ngati akufuna akupezeni Ku ntcheu komweko osati inu mupiteko Ayi akoza poison wa kumpha ziwaro musapiteko Ayi
Iweee ndiwabodza umakonda kunaniza amarawi
@John-to8gl
23 күн бұрын
😂
Limpopo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Limpopo f m my feveret
More fire mtanyiwa
Kodi nchifukwa chiyani a silikali amakhala mbali ya olamulila kusiya kuteteza mzika za Malawi
Bwana Ntanyiwa nyimboyi tikuifuna ngati pali link tipatseni ndaikonda 🔥🔥🔥🔥
Ife tikufuna tiwadziwe amene anapita kuchikangawa kukamalizitsa anthu 9 mwachinsisi ,aaa ife sitikumvesa anta ndipo sitikugona 😭😭😭
Buddy Ntanyiwa ♥️🔥
Ubwino wake mgwilizano anthu anavota zaka 5 nde zaka 5 zikatha anthu akavotanso sikuti avotelanso alliance ayi akavotela kumene akufuna kaya avotela DPP kaya avotela AFORD kaya MCP kaya UTM sikuti akavotela alliance
Nyimbo yu tigairen inu❤❤
Zikachitika timvela kwainu ❤❤
Ntanyiwa❤
Limpopo ❤❤❤❤ 🔥
Mbiri yoipa mpaka kale kale
Yomweyo chikangawa
Ngati zinali zonama kuti anapha chilima nchifukwa chani akumamanga anthu kodi nkhani yokunamizira umalimbana nayo?ndikunama ndi iwe sataniki chilima anthu azifa ndi nhlaka chifukwa cha iwe
Zilungamo zokhazokha
What is that Kuti anthu akasiye matelefone uyaluka galu iwe Sunati mulungu wathu wanthu ndi wa Moyo amene anafafaniza aiguputo ndipo Lero mulungu wemweyo akufuna kufafaniza chakwela ndi chipani chake zichitike mulungu wanthu wa Moyo timakudalilani sitimadalila chakwela Ayi zichitike mudzina la yesu khristu nanuso azibusa muzayankha mulandu Kwa mulungu
Koma muti nichani
Comrade mumatha.
Koma chakwela sutizamuiwala ndithu muchita kusowa chiyakhula mmm ndipo watikwana
KUYALUKA BOMA LA MCP KUSAFUNA KUVOMEREZA KUTI ZAWAVUTA
Chakwela akusekesa athuu bwanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂🎉
Crocodile party ,
😂😂😂😂😂😂 kubwera olonjezedwa
Limpopo inu ndinu katundu waboma
Kwakula kudzidzimbaitsa kwa ciombankhanga kufuna kuoneka ngati njiwa. Ciwanda ngati m'ngelo wakuunika. Zavuta basi.
Askhristu nonse akuligadzi muphedwa mwanvatu kuti zitseko zikatsekedwa zonse tchalitchi amatseka 😂😂😂😂😂 ma foni off ,ayi zikomo achakwela kupengatu uku kodi proglam yomphq chilima mumapanga monkha ndanga enawo mwayamba kupenga nonkha tu anakupakani manyi azinkhale akukunkhuyu achimwendo ,,
Mulingo umene umayeza nawo mzako ndi omwenso umakuyezela
Koma ziliko 😂😂😂😂😂
Nde utsi wafukila kut pamenepo UTM or akokoloka ndi mphepo ya pakati
Kodi Mtanyiwaso ndiokwiya tangobwela kuno kumalawi kuti uzawonese nkwiyowo ife zachilima woti anafakale sizitikhuza ndiposo sitikukwiya nazo okwiya ndiweyo bwela uzawonese nkwiyowakowo vutolake iweso ntanyiwa ndimbuzi chifukwa chilungamo ukuchiziwa koma ungokhala momyata ngati bwampini mmalo mobwela poyela kuti uwathandize anzakowa naweso ndi galu wachabechabe tikuwuzeni nose opandanzelunu pamozi ndi chilimayo timakuwuzani kuti tafasani koma kusanva amanamizidwanso ndi kaliyati kuti ayambise kachipani kawo agwese DPP aphwanga DPP siyolimbana nayo mwatitukwana yee a UTM pano mwasowa kolowela ife a DPP tiliphee ndipo a UTM kunoko ku DPP sitikukufunani nose ndinu agalu ndi chilima wanuyo mesa munkafuna adadi atafa lelo inu mulikuti muwona DPP 2025 boma
Uuuuu Shane
Azapanga ta15 minits thawi ikumachuluka tipepherekon
To honest this government it's full or shit n evil....munthu ukamayandikil kumwalira sunvaa kapena ndinene kut mbuzi ikakondwa amalonda Ali pafupi.....tionana nthawi yovotaa
Km guys mukutinyamula 🎉
Mafumu ena alibe fone aku ntcheu adziwa bwanji nanga
Kurikwabwino akhirisithu apite koma ma phone awo aka wayike since azika record zose chifukwa ngati sapita sitiziwakuti akufuna kurapachani
Limpopo moto kut buuuuuu🎉🎉
📺📡❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤👑
Sitikufuna DPP, MCP, UDF kapena PP ayi. Tikufuna kupitiliza vision ndi passion ya Dr Saulos Klaus Chilima with UTM basi. The grace of God is upon UTM party
Mantha kwambir
Ali ndi tsoka chikangawa ndi banja lake mpaka kufikila m'bado wake wa chi 4 otembeleledwa ulibe mwai
Koma ameneyu GALU kwambiri wamiyitana ndani NYANI ameneyo apite akapemphere ku Assembles kwake komweko GALUUUU!
Mukukwana antanyiwa 😂😂😂