Limpopo kupha Chilima zinachoka kutali tamvani bwino bwino Ntanyiwa wabweletsa

Пікірлер: 95

  • @tanishadias
    @tanishadias23 күн бұрын

    Ineyo a Limpompo fm ndili pa mbuyo pano ❤❤❤❤❤ mumatiuza zoona ndithu

  • @FazilCastin
    @FazilCastin23 күн бұрын

    Ine Langa ndi Funso Kwa inu Mr ntanyiwa Kodi Radio yanuyi imafikira anthu akumudzi. Chifukwa enafe tili ndi mwayi womvera komanso tili moyenda Monga out off country. Chifukwa akumudzi ndi amene akufunika Kuti adzidzitsata komanso ndi amene Anga Vote

  • @VeronicaChirwa-ct4os

    @VeronicaChirwa-ct4os

    23 күн бұрын

    Zoonadi akumudzi akufunika azizidziwa chilungamo cheni-cheni. Ndi amene amathamanga kukavota.

  • @Vwalavwata

    @Vwalavwata

    21 күн бұрын

    Ndipo ndimaisata kwambiri radio imeneyi from Malawi mzimba

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu23 күн бұрын

    Koma a chakwela mukuwoneka mulibe mtendere ndipo simunati mzimu wa munthu ndiwoopsa soseji mukuimva kunyung''unyatu ngati madimu musova😂😂

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn23 күн бұрын

    A UTM mukalola manyiwo musalamo nokha mu mgwilizano wanuwo ife zikwangwani talodza kale ku DPP mutsalanaye RUTO wanuyo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b23 күн бұрын

    Kkkkkkk koma apatu misala yayambika😂muziwona munakhetsa mwazi wa anthu osalakwa

  • @Stewartchikoja
    @Stewartchikoja23 күн бұрын

    Respect sibonda

  • @MaxWell-d7o

    @MaxWell-d7o

    23 күн бұрын

    Ine sindipitako

  • @BlessingKimu-yk8uj
    @BlessingKimu-yk8uj23 күн бұрын

    Moto wachilungamo tilinanu limodzi ifemso before amthu tikudziwa amthu okudana ndi chilungamo.

  • @IsmaelBilal-lh1pi
    @IsmaelBilal-lh1pi23 күн бұрын

    Jumah Mubarak. Our beloved Ntanyiwa ❤ freedom fighter 💪

  • @benbanda19
    @benbanda1919 күн бұрын

    Respect you Ntanyiwa Kumulakwira Chilima ndiena onse anafela mundege😢😢😢

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l23 күн бұрын

    Lipopo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ fire 🔥

  • @georgesmart3791
    @georgesmart379122 күн бұрын

    Kutha kwa Shasha... Apm 2025❤❤❤❤

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i20 күн бұрын

    Zinakanika kukambilana naye chilima chifukwa amaziwakuti chilima ndimuthu wachilungamo koma ngakhale mwamumpha zimu wa chilima ulamula ziko lamalawi ngakhale anachoka pakatipathu koma muchisomo chamulungu tilamulidwa ndi chilima S K C still I remember you 💔💔😭😭😭

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona22 күн бұрын

    Koma Malawi Chikangawa Party ikusavuka sinati . Mimbulu yoyipa iyi, Mwazi wa anthu osalakwa ukupengesani. Tiye nawo Mchimwene NTANYIWA kuwayika pambalambanda basi.

  • @Vwalavwata
    @Vwalavwata21 күн бұрын

    A khristu a CCAP ena ndi opusa amangosapota zilizonse even akuiziwa kuti akuzipereka yekha kwazigawenga kuti zimuphe

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto22 күн бұрын

    Limpopoooooooooo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj23 күн бұрын

    Mtanyiwwa ulemu wanuw bassi mulungu ationesa nkena kalikose iyyemwini ankubissa bwanj mulungu atiphasa nkuwona shoonad 🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲🤲

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm23 күн бұрын

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa ndi dolo kwambiri uyu akhalise Malawi.

  • @UsenLashid
    @UsenLashid23 күн бұрын

    Inu mahule chokani sindinu mulungu muziona 2025 komaso iwe chakwela usamati uzafela mbendela ya Malawi Ayi iwe uzafela tambala wakuda osati frug ya malawi Ayi

  • @user-yh3ys3qn6p
    @user-yh3ys3qn6p23 күн бұрын

    Km atanyiwa ndi kachilombo paka fukufuku kkkkkkk

  • @tanishadias
    @tanishadias23 күн бұрын

    Adamphadi Muthu uja basi palibeso kukanika konse 😭😭mcp chipani chakupha

  • @AsiyatuPoya
    @AsiyatuPoya23 күн бұрын

    Limpopo oyeee

  • @4ourcusworldwide426
    @4ourcusworldwide42620 күн бұрын

    Ndipo azibusa ambiri atayadi chilungamo..kukhala osauka mpimgo siukuwerengera. Mpake alibusy kusaka chikwamq.. rip chilima

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw23 күн бұрын

    Limpopo fm listening from Botswana comred number one

  • @JeremiahKainga-rm2np

    @JeremiahKainga-rm2np

    22 күн бұрын

    😅😅😅 2:14 2:16 2:17 😅😅 2:23 2:25 2:29 2:36 has been 2:41 2:42 2:43 2:44 2:44 2:46 2:48 2:49 😅 3:04 3:07 3:07 3:09 3:09 2 3:10 3:11 3:11 3:13 your 3:16 3:17 😊 3:19 3:20 9 3:23 3:2 6:31 6:40 6:51 7:02 7:02 7:10 7:12 7:17 7:18 7:18 7:19 8 5:45 😅 5:55 5:57 6:01 6:02 ,, 6:06 , 6:13 6:13 6:28 6:30 3:32 3:34 99😅 5:25 5:25 😅 5:44 3:50 3:51 3:54 3:56 😅 4:59 :38 2:39 2:41

  • @JeremiahKainga-rm2np

    @JeremiahKainga-rm2np

    22 күн бұрын

    7:37 7:37

  • @JeremiahKainga-rm2np

    @JeremiahKainga-rm2np

    22 күн бұрын

    African 9

  • @JeremiahKainga-rm2np

    @JeremiahKainga-rm2np

    22 күн бұрын

    What 😮

  • @JeremiahKainga-rm2np

    @JeremiahKainga-rm2np

    22 күн бұрын

    😊😊😊😊and

  • @MahallaMinistries-fv1hw
    @MahallaMinistries-fv1hw22 күн бұрын

    Sadly, we've moved from having men of God to men of gold.😮😮

  • @AlexGomani-ss5nj
    @AlexGomani-ss5nj23 күн бұрын

    Apa yalimba nkandilo basi, ma plan onse kumangopanga ngati openga Mulungu atachotsa nzeru.

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal23 күн бұрын

    Ndiye mwati chikangawa ikupita kukalapa ndiye anthu asatenge ma phone mm anagula ndiyeyo kkkk koma misala yayambika basi 😂😂😂

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du23 күн бұрын

    Mai gotani Hala amachindana ndi mkulu wanga

  • @JosephMaduka-i9s

    @JosephMaduka-i9s

    23 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @sammynkata5461

    @sammynkata5461

    21 күн бұрын

    Ing'alule basi ķkkk

  • @Hellenistic109

    @Hellenistic109

    20 күн бұрын

    Kkkkkkkkkiest

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j23 күн бұрын

    Akuyopa chani galu ameneyu pothimitsa malamya

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q23 күн бұрын

    Mulungu ndimboni pagwilizano wa tose Koma ngati chinali chiwembu ine ndikunena kuti mulungu abwezela chiwembu mboni dzilipo ndipo zinalakhula ndale amapanga usiku onsakhala masana mpepa azisogoleli tiyeni tiziopa mulungu amaona dzose

  • @NONELWANAMANYI
    @NONELWANAMANYI22 күн бұрын

    💪 tiyeni timenyele ufulu ziko lathu Mr mtanyiwa

  • @louismagongwa
    @louismagongwa23 күн бұрын

    😂😂😂😂 kma ku malawi kwafikapo

  • @BwanaGD
    @BwanaGD23 күн бұрын

    Kwawilira mafon timayankha uku tikuva mawu amulungu nde buzi yachabechabe akati Fon izime whay kapena akupita ndi poyison mwina akufuna akatinthemo anthuwo mkachisimo iiiii mayooo munthuyutu watsala pang'ono kufa kapena zimu wa chilima ukumutsata ndiye akuwonagati kutseka zitseko zimuwo sumupeza iiiii kkkk atate mwayambatu kuvetsa chisoni iiiii kkkk

  • @AlexMakweza
    @AlexMakweza23 күн бұрын

    Respect you

  • @UsenLashid
    @UsenLashid23 күн бұрын

    Ma mfumu akuntcheu chilima sanayikidwe Ku start house Ayi ngati akufuna akupezeni Ku ntcheu komweko osati inu mupiteko Ayi akoza poison wa kumpha ziwaro musapiteko Ayi

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel23 күн бұрын

    Iweee ndiwabodza umakonda kunaniza amarawi

  • @John-to8gl

    @John-to8gl

    23 күн бұрын

    😂

  • @julietbanda5203
    @julietbanda520323 күн бұрын

    Limpopo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @Mrssamalanngwira
    @Mrssamalanngwira23 күн бұрын

    Limpopo f m my feveret

  • @AnnaElisha-b4h
    @AnnaElisha-b4h23 күн бұрын

    More fire mtanyiwa

  • @PeterMillimbo
    @PeterMillimbo23 күн бұрын

    Kodi nchifukwa chiyani a silikali amakhala mbali ya olamulila kusiya kuteteza mzika za Malawi

  • @benjaminjobo3525
    @benjaminjobo352523 күн бұрын

    Bwana Ntanyiwa nyimboyi tikuifuna ngati pali link tipatseni ndaikonda 🔥🔥🔥🔥

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f23 күн бұрын

    Ife tikufuna tiwadziwe amene anapita kuchikangawa kukamalizitsa anthu 9 mwachinsisi ,aaa ife sitikumvesa anta ndipo sitikugona 😭😭😭

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x23 күн бұрын

    Buddy Ntanyiwa ♥️🔥

  • @RodgersPhiri-ju1eo
    @RodgersPhiri-ju1eo19 күн бұрын

    Ubwino wake mgwilizano anthu anavota zaka 5 nde zaka 5 zikatha anthu akavotanso sikuti avotelanso alliance ayi akavotela kumene akufuna kaya avotela DPP kaya avotela AFORD kaya MCP kaya UTM sikuti akavotela alliance

  • @user-pp6kf6vu2y
    @user-pp6kf6vu2y22 күн бұрын

    Nyimbo yu tigairen inu❤❤

  • @mathewsmbaluko8522
    @mathewsmbaluko852223 күн бұрын

    Zikachitika timvela kwainu ❤❤

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf626023 күн бұрын

    Ntanyiwa❤

  • @Mrssamalanngwira
    @Mrssamalanngwira23 күн бұрын

    Limpopo ❤❤❤❤ 🔥

  • @user-vw7tj2ss3l
    @user-vw7tj2ss3l23 күн бұрын

    Mbiri yoipa mpaka kale kale

  • @FocusGeorge-qz4sh
    @FocusGeorge-qz4sh23 күн бұрын

    Yomweyo chikangawa

  • @InnocentNitamanMilanzi
    @InnocentNitamanMilanzi4 күн бұрын

    Ngati zinali zonama kuti anapha chilima nchifukwa chani akumamanga anthu kodi nkhani yokunamizira umalimbana nayo?ndikunama ndi iwe sataniki chilima anthu azifa ndi nhlaka chifukwa cha iwe

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf23 күн бұрын

    Zilungamo zokhazokha

  • @UsenLashid
    @UsenLashid23 күн бұрын

    What is that Kuti anthu akasiye matelefone uyaluka galu iwe Sunati mulungu wathu wanthu ndi wa Moyo amene anafafaniza aiguputo ndipo Lero mulungu wemweyo akufuna kufafaniza chakwela ndi chipani chake zichitike mulungu wanthu wa Moyo timakudalilani sitimadalila chakwela Ayi zichitike mudzina la yesu khristu nanuso azibusa muzayankha mulandu Kwa mulungu

  • @Jamesmwale-iz4ri
    @Jamesmwale-iz4ri23 күн бұрын

    Koma muti nichani

  • @giftwankhama9914
    @giftwankhama991423 күн бұрын

    Comrade mumatha.

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d23 күн бұрын

    Koma chakwela sutizamuiwala ndithu muchita kusowa chiyakhula mmm ndipo watikwana

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon19 күн бұрын

    KUYALUKA BOMA LA MCP KUSAFUNA KUVOMEREZA KUTI ZAWAVUTA

  • @Fatima-f5c
    @Fatima-f5c23 күн бұрын

    Chakwela akusekesa athuu bwanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂🎉

  • @DanNzima
    @DanNzima22 күн бұрын

    Crocodile party ,

  • @jamessheki4293
    @jamessheki429323 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂 kubwera olonjezedwa

  • @samuelazumah1050
    @samuelazumah105023 күн бұрын

    Limpopo inu ndinu katundu waboma

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r23 күн бұрын

    Kwakula kudzidzimbaitsa kwa ciombankhanga kufuna kuoneka ngati njiwa. Ciwanda ngati m'ngelo wakuunika. Zavuta basi.

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr23 күн бұрын

    Askhristu nonse akuligadzi muphedwa mwanvatu kuti zitseko zikatsekedwa zonse tchalitchi amatseka 😂😂😂😂😂 ma foni off ,ayi zikomo achakwela kupengatu uku kodi proglam yomphq chilima mumapanga monkha ndanga enawo mwayamba kupenga nonkha tu anakupakani manyi azinkhale akukunkhuyu achimwendo ,,

  • @AndrewSimakweli
    @AndrewSimakweli23 күн бұрын

    Mulingo umene umayeza nawo mzako ndi omwenso umakuyezela

  • @EsnartMalewa
    @EsnartMalewa23 күн бұрын

    Koma ziliko 😂😂😂😂😂

  • @AdamMwanza-rf6pd
    @AdamMwanza-rf6pd23 күн бұрын

    Nde utsi wafukila kut pamenepo UTM or akokoloka ndi mphepo ya pakati

  • @RodgersPhiri-ju1eo
    @RodgersPhiri-ju1eo19 күн бұрын

    Kodi Mtanyiwaso ndiokwiya tangobwela kuno kumalawi kuti uzawonese nkwiyowo ife zachilima woti anafakale sizitikhuza ndiposo sitikukwiya nazo okwiya ndiweyo bwela uzawonese nkwiyowakowo vutolake iweso ntanyiwa ndimbuzi chifukwa chilungamo ukuchiziwa koma ungokhala momyata ngati bwampini mmalo mobwela poyela kuti uwathandize anzakowa naweso ndi galu wachabechabe tikuwuzeni nose opandanzelunu pamozi ndi chilimayo timakuwuzani kuti tafasani koma kusanva amanamizidwanso ndi kaliyati kuti ayambise kachipani kawo agwese DPP aphwanga DPP siyolimbana nayo mwatitukwana yee a UTM pano mwasowa kolowela ife a DPP tiliphee ndipo a UTM kunoko ku DPP sitikukufunani nose ndinu agalu ndi chilima wanuyo mesa munkafuna adadi atafa lelo inu mulikuti muwona DPP 2025 boma

  • @CatherineKumwex
    @CatherineKumwex23 күн бұрын

    Uuuuu Shane

  • @user-gq9jg4vm2f
    @user-gq9jg4vm2f23 күн бұрын

    Azapanga ta15 minits thawi ikumachuluka tipepherekon

  • @user-gp2zp2dj1w
    @user-gp2zp2dj1w23 күн бұрын

    To honest this government it's full or shit n evil....munthu ukamayandikil kumwalira sunvaa kapena ndinene kut mbuzi ikakondwa amalonda Ali pafupi.....tionana nthawi yovotaa

  • @JackNagoli
    @JackNagoli23 күн бұрын

    Km guys mukutinyamula 🎉

  • @user-sm8gx4vf1v
    @user-sm8gx4vf1v23 күн бұрын

    Mafumu ena alibe fone aku ntcheu adziwa bwanji nanga

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl23 күн бұрын

    Kurikwabwino akhirisithu apite koma ma phone awo aka wayike since azika record zose chifukwa ngati sapita sitiziwakuti akufuna kurapachani

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn715823 күн бұрын

    Limpopo moto kut buuuuuu🎉🎉

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge22 күн бұрын

    📺📡❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤👑

  • @vincentbarnes5872
    @vincentbarnes587222 күн бұрын

    Sitikufuna DPP, MCP, UDF kapena PP ayi. Tikufuna kupitiliza vision ndi passion ya Dr Saulos Klaus Chilima with UTM basi. The grace of God is upon UTM party

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo23 күн бұрын

    Mantha kwambir

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma23 күн бұрын

    Ali ndi tsoka chikangawa ndi banja lake mpaka kufikila m'bado wake wa chi 4 otembeleledwa ulibe mwai

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn23 күн бұрын

    Koma ameneyu GALU kwambiri wamiyitana ndani NYANI ameneyo apite akapemphere ku Assembles kwake komweko GALUUUU!

  • @REXCHARLESKAJAWO
    @REXCHARLESKAJAWO22 күн бұрын

    Mukukwana antanyiwa 😂😂😂