Kodi ufulu ulikuti, ku malawi kulibe ufulu chifukwa achina kamulepo ndi kalindo mudawamanga chifukwa chomenyera ufuluo, komatu Boma ili litipweteka ndithu
@JacksonChayibu6 күн бұрын
Ife tikufuna bon kalindo mawa atulusidwe
@user-vm7iz6oz6r6 күн бұрын
Muchoseko zaka 4 zomwe mwalamulilaz kulibe ufulu ndiye kt tili ndi zaka 56 xaufulu
@user-lr5bz7qk2d6 күн бұрын
Ukuona ngati anthu akukukhululukini mwanya akupha
@GiftManuel-er7yh6 күн бұрын
Amaio akunama mwana sangabadwe kutha miyedzi 6 asanamupitenao ku chipatala ku scale
@Trancy-xt4py6 күн бұрын
Ofufuza akhare a independent osati oziwana ndi mcp ai sipamveka black box ili kutiko choyamba?
@chimwemwekamwana7876 күн бұрын
Mukuopa kut anthu akutukwanani.. nanga mmene mukuoneramu amalawi tili pa ufulu ifeeee.. ai muli ndi manyazi ndithu
@user-lr5bz7qk2d6 күн бұрын
Agalu kumkuyu mapwala ako
@ZungeniBanet6 күн бұрын
Iwe mukuyu matako yako wapulika chakwel nayo pathako pake
@user-lr5bz7qk2d6 күн бұрын
Agalu mumuziwaso Mulungu
@JamesOsman-cz9cw6 күн бұрын
Mcp people machende anu nonse
@user-mj2te7vl6p5 күн бұрын
Bodza limenero manyazi achakwera
@yusufbakali6 күн бұрын
Kukhuyu zikhare chimwendo chakwela osewa adyeretu chaka chamawa chawoo palibe anthu tinavota kare kufa kwa chilima
@robertnambazo99365 күн бұрын
Akuziwa kuti anthu sazapitako awatuluka anthu awa
@josephchirwa-jt7jx6 күн бұрын
Kodi ku malawi kuliso ufulu?
@eliaskhofielias81526 күн бұрын
Ngakhale atapanga zokoma bwanji a mcp kuphiphilitsa za imfa ya chilima even atati apereka nseu wot chilima road sadzawinabe awa.ndinu okupha okupha basi munapha nzanu mbili sizafufutika.
@LamieTiger-ff7cj6 күн бұрын
Chakwera mukanangot kukhala Za satanic metsa inu ndi satana
@ulemujumbe85015 күн бұрын
Bring back Bon Kalindo
@hanifahmponda87115 күн бұрын
Aaa atenga anthu osadziwika cholinga choti adzattwudze mabodza ANTHU AKADZAMANENA KUTI CHILUNGAMO ACHIBUTSA ADZIMANGIDWA NDE MCP IMENEYO NDEGE YOTI DZIPANGIDZO DZINA ANACHOTSA MO MA PHONE KUTENGA KUMAFUFUDZA POKAPELEKA MA FON AFUTAMU CHILICHOTSE AAAAA amalawi mufunilanji omboni wina apa zawoka dzokha kuti chiwembu chokodza MR CHIHANA THANKS U SO MUCH KOMA A MCP AKATULUTSA BODZA LAWOLO ngati inu mudzayankhule potsusana a MCP mudzayembekedzele kumangidwa CHIFUKWA PANO DZIKO LA MALAWI LAFIKA ULAMULILO WACHIPANI CHIMODZI CHAKAKA NYALENDA NDADZANU ENA MUNATILAKWILA AMALAWI MUDZIWE DZIMENEDZO
@ElizabethKhosa-gx3wt5 күн бұрын
Chingawenga choopya cha chakwela panopa chikufuna kuphe bon kalindo
@dysonfysonchifundo22846 күн бұрын
Ndipo ofufudza sakuyenera kuitanidwa kuchoka ku boma cos ndiwomwe analephela kupulumutsa anthu, in other way, boma ndilimwe lapha anthu
Afiti inu palibe ufulu nanga born kalindo akutani ku selo
@user-rd2ft5uk3q6 күн бұрын
Ufulu wake utiwo
@geraldtuwaga-iz6ll6 күн бұрын
Opemphera ake ndani zigawenga inu?
@EdwardMathuwa5 күн бұрын
Dzaka 60 za democracy minus 4 ya chakwela tikusangala dzaka 56 coz dzaka 4 za chakwela kulibe ufulu
@marryphili54194 күн бұрын
Musatinyasepo apa ufulu womwe mukunena ndiye wuti Malawi wake wuti womwe Muli wufulu za ziiiii
@AleksaWilliams-qc6cn6 күн бұрын
Mukut mulira maliro nanga chowangira anthu mukulira maliro ndi chan?
@user-nn7sv5yb8h6 күн бұрын
Kunkuyu udzinena kuti presdent wakoyo wanena kuti osati walamula ai
@GeraldMkwewu-gd5eb6 күн бұрын
Chakwera ndi lwe nkukuyu agalu nose mapemphera achani fiti lnu nose ndi manganya tikulira chilima wanthu lnu mumumasure bon kalindo ndi kamulepu boma lakhaza lri mwayiwara kt mupeze ma udindo ndi chilima nose 😢
@AndrewMukhwapa-qj4vo6 күн бұрын
Very good a Chihana
@storytambala60885 күн бұрын
Hmm iwe Kunkuyu, ndi Chakwera musatiputsitse apa.
@feehasaidid.r.d6 күн бұрын
Wanena zoona chihana
@patrickmacheso50626 күн бұрын
Iweyo Kumkuyu ndi Chakwera wakoyo God must punish you, Mukukamba za kukhudza Maliro a Dr Chilima chonsecho mukungotiphimba kumaso.
@victorauwana72585 күн бұрын
Ziko la Malawi lakwanisa zaka 60 pokweza pasogolo umphawi wathu
@ShaliyaMusa5 күн бұрын
Ndiwomwewo mfiti. Chikwelayo paribe kikna
@ZungeniBanet6 күн бұрын
Inu ti onana 2025 mukutuluka inu
@viennasamuel29765 күн бұрын
Mwamasukatu mpaka zikhulupiliro zosakhala bwino? Globe vaccine akukupatsani thandizowo ndi ayesu? OK.
@user-nl5nk2wx1q6 күн бұрын
KOMA BOMA LA MCP 😢😢😢 AWA SI ANTHU KOMA AFITI ASATANIKI
@AlexKaunda-ny2eg6 күн бұрын
Chokani ana amahule inu kungokhalira umoyo wauchigawenga
@SarahMusama-eu7wt6 күн бұрын
Koma kachere anachulukitsa kulibe dzina lina
@TwayibuChimbama6 күн бұрын
Kusilamulila kwake kopa anthu
@richardManemba5 күн бұрын
Ayii akupangila kt ufulu wa amalawi uchoke km osalola kungolola bas zabwelela zakale
@ThomasMunyolowa6 күн бұрын
Osati kuopa ku kuwizidwa
@isaaczuze3 күн бұрын
Kunkuyu uzipemphela kwambili kuti boma lisasinthe ...boma kungosintha iwe uzafela kumdende ....unapha allan witika chifukwa cha mkazi .....munthu wopusa iwe kwambili mbuzi
@user-xm3zl5cg6x5 күн бұрын
Muvesen akunena ufulu obela a malawi galuyu okukuda kukeqma
Akuopa kuti akakuwidwa ku 6 July 😂😂😂😂 mwabalalika makape
@QueneteCatundulo6 күн бұрын
Good
@VanPaul-sv9yx5 күн бұрын
Nanu tazingodurani nkhani zofunikirazo ndikumaponya apa osati ndi nkhani zopoira zomwe
@user-mk3fy9nl2u5 күн бұрын
Inunso mukuziziwa zimenezo
@thulanimpphiri68736 күн бұрын
Well done Enoch chihana utsogoleri ndiumeneo. Tikufuna tiwaziwe anthu amene achoka ku Germany ofufuza za ngozi ya vice president ndi azathu 9. Awapeza bwanji anthu aku Germany owo aboma anene.
@isaaczuze3 күн бұрын
Mulila bwanji poti mwachita kumupha chilima koma ndizokhumudwisa kwambili
@MatiasChimsakasa5 күн бұрын
Komano bwanji anthu anasangalala polumbilitsa olemekezeka a vp koma 6jly ayi Kodi undiuthenga wanji mukupeleka kwa ife achinyamata
@user-nr4mi7pt8g5 күн бұрын
Ma billion chikondwererowo nde tigawanepotu sizausiru apa
@Eric-gb9ms5 күн бұрын
Akuti muli wufulu m'malawi zoona
@mussakathumba1283 күн бұрын
Komanotu kunena chilunga amalawife tikufatsa kwambiri plus ulemu too much.chakwera wationjeza akungopha anthu ngati khuku tinayenera kumuchotsa before mavoti
@FionaKhoma5 күн бұрын
Masiran born kalindo kaye mukubisa chan pomumanga iyeyo
@user-xf6dn7pv9b5 күн бұрын
Chakwera ndiwe mbuzi wamva , galu , nyani chittsru cha munthu
@user-lr2wx5xd9d6 күн бұрын
Following
@user-jl6sq3ph1b5 күн бұрын
Mufika kumeneko nonsenu kumeneko za chamba 6 July muzakhalamulibe moyo inu agalu eti mboloyako
@yusufbakali6 күн бұрын
Mbudzi iwe
@Trancy-xt4py6 күн бұрын
Inet imfa yachilima ndalota utsiku tapephera mosweka mtima akundilakhula kuti pangoz damulumuka koma anthu adandipha pondikhapa mendo zanga ndiy achakwera musamalet enafe ndi daniel tikapephera mulungu amayakha kumaloto athu mudapha inu pomukha chilima ndi zikwanje munyaaaaa nane daniel omasulira maloto kuuulurani
@ChristinaLigomeka
6 күн бұрын
😭😭😭 Km kulakwatu uku ayaluka awa akusewera ndi Mulungu km😭😭😭😭
@ManifoldPhiri
6 күн бұрын
Usatchure dzina la mulungu wako pachabe mingochimwa nazo izi
Пікірлер: 126
Nduona ngati akuopaa kkk ufulu weni weni tilibe kweni kweni
Big up Mr Chihana though sinamveere zomwe mwayankhula ndangowona anthu akuyamikira
Mawa lisathe kalindo amasulidwe chakwera &usi tionana 2025
Dzaka 60 really 😢😢😢 Malawi udzakula liti 60 years still kuvala pampaz shame on you kunkuyu
Amene adzapite ku mapephero amenewo mutu wake suyenda bwino mwalo mopangitsa mapephero olapa mudzikapephera chani Mulungu akamva zimenezo magazi akuyenda Malawi mo simukuwawona, mwazi wa anthu osalakwa ukufuulawo simukuoona mapephero achani mudziwerenga bible before kuchita zithu za ziiii mudzikapha Ana azanu ngati khuku mtendere simudzaupeza mpaka mutabwera poyera kulula
@user-eh1mg3ww6d
5 күн бұрын
Sure
Anthu amenewo ofufuzawo pls Mr Chihana muwonetsetse kuti asachokele ku Butchery kumene amatinamiza kuja kuti akagura Feteleza anthu akuba awa ndi kupha oyipa a MCP
Straight to the point Mr Chihana
Ufulu wake ndiye wutiwo mungomanga adzanu ndi kuphaso azanu
Memories will remain fresh even after 100 years. Let's remember them in a special way and continuously pray for their Souls to rest in eternal peace.
Nankhumwa wayamba kulankhula chifukwa sanamusankhe kukhala vp
Good Mr Chihana
A kunkuyu mzimu wa witika muli nao pamutupo
Nkukuyu ungotaya nthawi kulankhula zopusazo asakuziwa kuti Chakwera ndi nsogoleri ndani sangalalani ndi gulu lanulo LA uchigawenga mcp 😭😭😭😭😭🐊🐊🐊🐊
Iwowa mituyao sigwira kunkuyu ndi chakwera wakoyo ndinu mbuzi mukati ufulu odziramulira what do you mean? Momwe mukuyendetsera boma lero mukuona ngati dziko liri pa ufulu popeza muli busy kupha anthu komaso kumanga anthu omwe akukudzudzulani ndiye nkumati dziko liri pa ufulu inu agalu kwabasi zigawenga
Chihana well spoken,
Chihana very good
Boon kalindo ndikumufuna osat inuo,chokan apaaaa
Akuna adzakondwerere kuti zomwe.amafuna zatheka pokupha chilima
@IshmaelDouglas-j5i
7 сағат бұрын
Ol
Chihana anamumana udindo ku tonse allias
Anawo akhala osabereka
Nanga anthu amene mukuwamangao mukutathauza kuti mukulira bodza bwanji Mr president
Kodi ufulu ulikuti, ku malawi kulibe ufulu chifukwa achina kamulepo ndi kalindo mudawamanga chifukwa chomenyera ufuluo, komatu Boma ili litipweteka ndithu
Ife tikufuna bon kalindo mawa atulusidwe
Muchoseko zaka 4 zomwe mwalamulilaz kulibe ufulu ndiye kt tili ndi zaka 56 xaufulu
Ukuona ngati anthu akukukhululukini mwanya akupha
Amaio akunama mwana sangabadwe kutha miyedzi 6 asanamupitenao ku chipatala ku scale
Ofufuza akhare a independent osati oziwana ndi mcp ai sipamveka black box ili kutiko choyamba?
Mukuopa kut anthu akutukwanani.. nanga mmene mukuoneramu amalawi tili pa ufulu ifeeee.. ai muli ndi manyazi ndithu
Agalu kumkuyu mapwala ako
Iwe mukuyu matako yako wapulika chakwel nayo pathako pake
Agalu mumuziwaso Mulungu
Mcp people machende anu nonse
Bodza limenero manyazi achakwera
Kukhuyu zikhare chimwendo chakwela osewa adyeretu chaka chamawa chawoo palibe anthu tinavota kare kufa kwa chilima
Akuziwa kuti anthu sazapitako awatuluka anthu awa
Kodi ku malawi kuliso ufulu?
Ngakhale atapanga zokoma bwanji a mcp kuphiphilitsa za imfa ya chilima even atati apereka nseu wot chilima road sadzawinabe awa.ndinu okupha okupha basi munapha nzanu mbili sizafufutika.
Chakwera mukanangot kukhala Za satanic metsa inu ndi satana
Bring back Bon Kalindo
Aaa atenga anthu osadziwika cholinga choti adzattwudze mabodza ANTHU AKADZAMANENA KUTI CHILUNGAMO ACHIBUTSA ADZIMANGIDWA NDE MCP IMENEYO NDEGE YOTI DZIPANGIDZO DZINA ANACHOTSA MO MA PHONE KUTENGA KUMAFUFUDZA POKAPELEKA MA FON AFUTAMU CHILICHOTSE AAAAA amalawi mufunilanji omboni wina apa zawoka dzokha kuti chiwembu chokodza MR CHIHANA THANKS U SO MUCH KOMA A MCP AKATULUTSA BODZA LAWOLO ngati inu mudzayankhule potsusana a MCP mudzayembekedzele kumangidwa CHIFUKWA PANO DZIKO LA MALAWI LAFIKA ULAMULILO WACHIPANI CHIMODZI CHAKAKA NYALENDA NDADZANU ENA MUNATILAKWILA AMALAWI MUDZIWE DZIMENEDZO
Chingawenga choopya cha chakwela panopa chikufuna kuphe bon kalindo
Ndipo ofufudza sakuyenera kuitanidwa kuchoka ku boma cos ndiwomwe analephela kupulumutsa anthu, in other way, boma ndilimwe lapha anthu
Inu nosenu ndinu agalu kwabasi ifetu tikungo funa kuti bon Kalindo wathuyo tipaseni achainiyakefe
Afiti inu palibe ufulu nanga born kalindo akutani ku selo
Ufulu wake utiwo
Opemphera ake ndani zigawenga inu?
Dzaka 60 za democracy minus 4 ya chakwela tikusangala dzaka 56 coz dzaka 4 za chakwela kulibe ufulu
Musatinyasepo apa ufulu womwe mukunena ndiye wuti Malawi wake wuti womwe Muli wufulu za ziiiii
Mukut mulira maliro nanga chowangira anthu mukulira maliro ndi chan?
Kunkuyu udzinena kuti presdent wakoyo wanena kuti osati walamula ai
Chakwera ndi lwe nkukuyu agalu nose mapemphera achani fiti lnu nose ndi manganya tikulira chilima wanthu lnu mumumasure bon kalindo ndi kamulepu boma lakhaza lri mwayiwara kt mupeze ma udindo ndi chilima nose 😢
Very good a Chihana
Hmm iwe Kunkuyu, ndi Chakwera musatiputsitse apa.
Wanena zoona chihana
Iweyo Kumkuyu ndi Chakwera wakoyo God must punish you, Mukukamba za kukhudza Maliro a Dr Chilima chonsecho mukungotiphimba kumaso.
Ziko la Malawi lakwanisa zaka 60 pokweza pasogolo umphawi wathu
Ndiwomwewo mfiti. Chikwelayo paribe kikna
Inu ti onana 2025 mukutuluka inu
Mwamasukatu mpaka zikhulupiliro zosakhala bwino? Globe vaccine akukupatsani thandizowo ndi ayesu? OK.
KOMA BOMA LA MCP 😢😢😢 AWA SI ANTHU KOMA AFITI ASATANIKI
Chokani ana amahule inu kungokhalira umoyo wauchigawenga
Koma kachere anachulukitsa kulibe dzina lina
Kusilamulila kwake kopa anthu
Ayii akupangila kt ufulu wa amalawi uchoke km osalola kungolola bas zabwelela zakale
Osati kuopa ku kuwizidwa
Kunkuyu uzipemphela kwambili kuti boma lisasinthe ...boma kungosintha iwe uzafela kumdende ....unapha allan witika chifukwa cha mkazi .....munthu wopusa iwe kwambili mbuzi
Muvesen akunena ufulu obela a malawi galuyu okukuda kukeqma
Dzaka 60 yoh bwanji dziko lili paumphawi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 shame
Akuopa kuti akakuwidwa ku 6 July 😂😂😂😂 mwabalalika makape
Good
Nanu tazingodurani nkhani zofunikirazo ndikumaponya apa osati ndi nkhani zopoira zomwe
Inunso mukuziziwa zimenezo
Well done Enoch chihana utsogoleri ndiumeneo. Tikufuna tiwaziwe anthu amene achoka ku Germany ofufuza za ngozi ya vice president ndi azathu 9. Awapeza bwanji anthu aku Germany owo aboma anene.
Mulila bwanji poti mwachita kumupha chilima koma ndizokhumudwisa kwambili
Komano bwanji anthu anasangalala polumbilitsa olemekezeka a vp koma 6jly ayi Kodi undiuthenga wanji mukupeleka kwa ife achinyamata
Ma billion chikondwererowo nde tigawanepotu sizausiru apa
Akuti muli wufulu m'malawi zoona
Komanotu kunena chilunga amalawife tikufatsa kwambiri plus ulemu too much.chakwera wationjeza akungopha anthu ngati khuku tinayenera kumuchotsa before mavoti
Masiran born kalindo kaye mukubisa chan pomumanga iyeyo
Chakwera ndiwe mbuzi wamva , galu , nyani chittsru cha munthu
Following
Mufika kumeneko nonsenu kumeneko za chamba 6 July muzakhalamulibe moyo inu agalu eti mboloyako
Mbudzi iwe
Inet imfa yachilima ndalota utsiku tapephera mosweka mtima akundilakhula kuti pangoz damulumuka koma anthu adandipha pondikhapa mendo zanga ndiy achakwera musamalet enafe ndi daniel tikapephera mulungu amayakha kumaloto athu mudapha inu pomukha chilima ndi zikwanje munyaaaaa nane daniel omasulira maloto kuuulurani
@ChristinaLigomeka
6 күн бұрын
😭😭😭 Km kulakwatu uku ayaluka awa akusewera ndi Mulungu km😭😭😭😭
@ManifoldPhiri
6 күн бұрын
Usatchure dzina la mulungu wako pachabe mingochimwa nazo izi
@ChristinaLigomeka
6 күн бұрын
@@ManifoldPhiri atchula pacha be pempherani nanu mosweka mtima Mulungu sapepusa PEMPHELO losweka mtima Koditu amakani nu choona muchidziwa posachedwapa mwazi ukufula ohoooo wanthu 9 mmmmmm anthu mimba zamangidwa kufuna kudziwa choona chochoka kumwamba anthu kukugonedwa mapili kufuna kudziwa nchoonadi chochoka kumwamba inu ngati mafoloko alimanja daily musaganize ngati dziko lonse anthu avula dzuwa liliphweeee mukucheza ndi Mulungu
@SheenahMwalabu-iz3pr
6 күн бұрын
@@ChristinaLigomekakunena zoona imfa iyiyi sikundigonetsa tulo ndizowawa ndipo ngati bodza Chilima kulibe zoona. Mulungu munaloleranji? 😢 ndikufuna tidziwe zoona
Or mpunga wa nyama tisadyenso?? 😢😢😢
Mapemphero ake ati komanso abusa achokera mpingo uti Please leave God alone please
Zaziiii
Stupid you guys in chakwera team Mwapha chilima anthu inu mukukayankhula zautsiru
Malawi muno mulibe umfulu
Iwe kumkuyu ndiiwe mbuz et ufulu wake ulikut popeza mungomanga aliyese brushit zako
Ufulu wake ulikut???
Anthu tili ndi mafunso kumene
Kodi July yili Liti Koti muyambe kunena Za 6 July
Ufulu wake utiwo?????
Mbolo zanu
Kunkuyu panyapako galu iwe
Chakwera is a mbolicious guy.
😂😂😂😂😂
Akunkuyu machende
Zoona akufunikadi kunthandizidwa