CHIHANA NDI NANKHUMWA AVUTA UKU |

Пікірлер: 126

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt6 күн бұрын

    Nduona ngati akuopaa kkk ufulu weni weni tilibe kweni kweni

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri5 күн бұрын

    Big up Mr Chihana though sinamveere zomwe mwayankhula ndangowona anthu akuyamikira

  • @Edson-sj8vn
    @Edson-sj8vn6 күн бұрын

    Mawa lisathe kalindo amasulidwe chakwera &usi tionana 2025

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h6 күн бұрын

    Dzaka 60 really 😢😢😢 Malawi udzakula liti 60 years still kuvala pampaz shame on you kunkuyu

  • @ChristinaLigomeka
    @ChristinaLigomeka6 күн бұрын

    Amene adzapite ku mapephero amenewo mutu wake suyenda bwino mwalo mopangitsa mapephero olapa mudzikapephera chani Mulungu akamva zimenezo magazi akuyenda Malawi mo simukuwawona, mwazi wa anthu osalakwa ukufuulawo simukuoona mapephero achani mudziwerenga bible before kuchita zithu za ziiii mudzikapha Ana azanu ngati khuku mtendere simudzaupeza mpaka mutabwera poyera kulula

  • @user-eh1mg3ww6d

    @user-eh1mg3ww6d

    5 күн бұрын

    Sure

  • @user-jd9yz5hp7y
    @user-jd9yz5hp7y6 күн бұрын

    Anthu amenewo ofufuzawo pls Mr Chihana muwonetsetse kuti asachokele ku Butchery kumene amatinamiza kuja kuti akagura Feteleza anthu akuba awa ndi kupha oyipa a MCP

  • @JIMMYWATHONJE
    @JIMMYWATHONJE6 күн бұрын

    Straight to the point Mr Chihana

  • @JohnsonRannel18
    @JohnsonRannel186 күн бұрын

    Ufulu wake ndiye wutiwo mungomanga adzanu ndi kuphaso azanu

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf6 күн бұрын

    Memories will remain fresh even after 100 years. Let's remember them in a special way and continuously pray for their Souls to rest in eternal peace.

  • @PaulMwachande
    @PaulMwachande6 күн бұрын

    Nankhumwa wayamba kulankhula chifukwa sanamusankhe kukhala vp

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y6 күн бұрын

    Good Mr Chihana

  • @user-zi8pj5ey4t
    @user-zi8pj5ey4t6 күн бұрын

    A kunkuyu mzimu wa witika muli nao pamutupo

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf5 күн бұрын

    Nkukuyu ungotaya nthawi kulankhula zopusazo asakuziwa kuti Chakwera ndi nsogoleri ndani sangalalani ndi gulu lanulo LA uchigawenga mcp 😭😭😭😭😭🐊🐊🐊🐊

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon5 күн бұрын

    Iwowa mituyao sigwira kunkuyu ndi chakwera wakoyo ndinu mbuzi mukati ufulu odziramulira what do you mean? Momwe mukuyendetsera boma lero mukuona ngati dziko liri pa ufulu popeza muli busy kupha anthu komaso kumanga anthu omwe akukudzudzulani ndiye nkumati dziko liri pa ufulu inu agalu kwabasi zigawenga

  • @OmarManjawira-up3ns
    @OmarManjawira-up3ns6 күн бұрын

    Chihana well spoken,

  • @user-hp4rl8cv3h
    @user-hp4rl8cv3h5 күн бұрын

    Chihana very good

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN6 күн бұрын

    Boon kalindo ndikumufuna osat inuo,chokan apaaaa

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e6 күн бұрын

    Akuna adzakondwerere kuti zomwe.amafuna zatheka pokupha chilima

  • @IshmaelDouglas-j5i

    @IshmaelDouglas-j5i

    7 сағат бұрын

    Ol

  • @HeedsonJere
    @HeedsonJere5 күн бұрын

    Chihana anamumana udindo ku tonse allias

  • @user-kr4wb2th9i
    @user-kr4wb2th9i5 күн бұрын

    Anawo akhala osabereka

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi5 күн бұрын

    Nanga anthu amene mukuwamangao mukutathauza kuti mukulira bodza bwanji Mr president

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo5 күн бұрын

    Kodi ufulu ulikuti, ku malawi kulibe ufulu chifukwa achina kamulepo ndi kalindo mudawamanga chifukwa chomenyera ufuluo, komatu Boma ili litipweteka ndithu

  • @JacksonChayibu
    @JacksonChayibu6 күн бұрын

    Ife tikufuna bon kalindo mawa atulusidwe

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r6 күн бұрын

    Muchoseko zaka 4 zomwe mwalamulilaz kulibe ufulu ndiye kt tili ndi zaka 56 xaufulu

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d6 күн бұрын

    Ukuona ngati anthu akukukhululukini mwanya akupha

  • @GiftManuel-er7yh
    @GiftManuel-er7yh6 күн бұрын

    Amaio akunama mwana sangabadwe kutha miyedzi 6 asanamupitenao ku chipatala ku scale

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py6 күн бұрын

    Ofufuza akhare a independent osati oziwana ndi mcp ai sipamveka black box ili kutiko choyamba?

  • @chimwemwekamwana787
    @chimwemwekamwana7876 күн бұрын

    Mukuopa kut anthu akutukwanani.. nanga mmene mukuoneramu amalawi tili pa ufulu ifeeee.. ai muli ndi manyazi ndithu

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d6 күн бұрын

    Agalu kumkuyu mapwala ako

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet6 күн бұрын

    Iwe mukuyu matako yako wapulika chakwel nayo pathako pake

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d6 күн бұрын

    Agalu mumuziwaso Mulungu

  • @JamesOsman-cz9cw
    @JamesOsman-cz9cw6 күн бұрын

    Mcp people machende anu nonse

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p5 күн бұрын

    Bodza limenero manyazi achakwera

  • @yusufbakali
    @yusufbakali6 күн бұрын

    Kukhuyu zikhare chimwendo chakwela osewa adyeretu chaka chamawa chawoo palibe anthu tinavota kare kufa kwa chilima

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo99365 күн бұрын

    Akuziwa kuti anthu sazapitako awatuluka anthu awa

  • @josephchirwa-jt7jx
    @josephchirwa-jt7jx6 күн бұрын

    Kodi ku malawi kuliso ufulu?

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias81526 күн бұрын

    Ngakhale atapanga zokoma bwanji a mcp kuphiphilitsa za imfa ya chilima even atati apereka nseu wot chilima road sadzawinabe awa.ndinu okupha okupha basi munapha nzanu mbili sizafufutika.

  • @LamieTiger-ff7cj
    @LamieTiger-ff7cj6 күн бұрын

    Chakwera mukanangot kukhala Za satanic metsa inu ndi satana

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe85015 күн бұрын

    Bring back Bon Kalindo

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda87115 күн бұрын

    Aaa atenga anthu osadziwika cholinga choti adzattwudze mabodza ANTHU AKADZAMANENA KUTI CHILUNGAMO ACHIBUTSA ADZIMANGIDWA NDE MCP IMENEYO NDEGE YOTI DZIPANGIDZO DZINA ANACHOTSA MO MA PHONE KUTENGA KUMAFUFUDZA POKAPELEKA MA FON AFUTAMU CHILICHOTSE AAAAA amalawi mufunilanji omboni wina apa zawoka dzokha kuti chiwembu chokodza MR CHIHANA THANKS U SO MUCH KOMA A MCP AKATULUTSA BODZA LAWOLO ngati inu mudzayankhule potsusana a MCP mudzayembekedzele kumangidwa CHIFUKWA PANO DZIKO LA MALAWI LAFIKA ULAMULILO WACHIPANI CHIMODZI CHAKAKA NYALENDA NDADZANU ENA MUNATILAKWILA AMALAWI MUDZIWE DZIMENEDZO

  • @ElizabethKhosa-gx3wt
    @ElizabethKhosa-gx3wt5 күн бұрын

    Chingawenga choopya cha chakwela panopa chikufuna kuphe bon kalindo

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo22846 күн бұрын

    Ndipo ofufudza sakuyenera kuitanidwa kuchoka ku boma cos ndiwomwe analephela kupulumutsa anthu, in other way, boma ndilimwe lapha anthu

  • @user-tn2qg1vs9j
    @user-tn2qg1vs9j6 күн бұрын

    Inu nosenu ndinu agalu kwabasi ifetu tikungo funa kuti bon Kalindo wathuyo tipaseni achainiyakefe

  • @DennisDonework
    @DennisDonework6 күн бұрын

    Afiti inu palibe ufulu nanga born kalindo akutani ku selo

  • @user-rd2ft5uk3q
    @user-rd2ft5uk3q6 күн бұрын

    Ufulu wake utiwo

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll6 күн бұрын

    Opemphera ake ndani zigawenga inu?

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa5 күн бұрын

    Dzaka 60 za democracy minus 4 ya chakwela tikusangala dzaka 56 coz dzaka 4 za chakwela kulibe ufulu

  • @marryphili5419
    @marryphili54194 күн бұрын

    Musatinyasepo apa ufulu womwe mukunena ndiye wuti Malawi wake wuti womwe Muli wufulu za ziiiii

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn6 күн бұрын

    Mukut mulira maliro nanga chowangira anthu mukulira maliro ndi chan?

  • @user-nn7sv5yb8h
    @user-nn7sv5yb8h6 күн бұрын

    Kunkuyu udzinena kuti presdent wakoyo wanena kuti osati walamula ai

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb6 күн бұрын

    Chakwera ndi lwe nkukuyu agalu nose mapemphera achani fiti lnu nose ndi manganya tikulira chilima wanthu lnu mumumasure bon kalindo ndi kamulepu boma lakhaza lri mwayiwara kt mupeze ma udindo ndi chilima nose 😢

  • @AndrewMukhwapa-qj4vo
    @AndrewMukhwapa-qj4vo6 күн бұрын

    Very good a Chihana

  • @storytambala6088
    @storytambala60885 күн бұрын

    Hmm iwe Kunkuyu, ndi Chakwera musatiputsitse apa.

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d6 күн бұрын

    Wanena zoona chihana

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso50626 күн бұрын

    Iweyo Kumkuyu ndi Chakwera wakoyo God must punish you, Mukukamba za kukhudza Maliro a Dr Chilima chonsecho mukungotiphimba kumaso.

  • @victorauwana7258
    @victorauwana72585 күн бұрын

    Ziko la Malawi lakwanisa zaka 60 pokweza pasogolo umphawi wathu

  • @ShaliyaMusa
    @ShaliyaMusa5 күн бұрын

    Ndiwomwewo mfiti. Chikwelayo paribe kikna

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet6 күн бұрын

    Inu ti onana 2025 mukutuluka inu

  • @viennasamuel2976
    @viennasamuel29765 күн бұрын

    Mwamasukatu mpaka zikhulupiliro zosakhala bwino? Globe vaccine akukupatsani thandizowo ndi ayesu? OK.

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q6 күн бұрын

    KOMA BOMA LA MCP 😢😢😢 AWA SI ANTHU KOMA AFITI ASATANIKI

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg6 күн бұрын

    Chokani ana amahule inu kungokhalira umoyo wauchigawenga

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt6 күн бұрын

    Koma kachere anachulukitsa kulibe dzina lina

  • @TwayibuChimbama
    @TwayibuChimbama6 күн бұрын

    Kusilamulila kwake kopa anthu

  • @richardManemba
    @richardManemba5 күн бұрын

    Ayii akupangila kt ufulu wa amalawi uchoke km osalola kungolola bas zabwelela zakale

  • @ThomasMunyolowa
    @ThomasMunyolowa6 күн бұрын

    Osati kuopa ku kuwizidwa

  • @isaaczuze
    @isaaczuze3 күн бұрын

    Kunkuyu uzipemphela kwambili kuti boma lisasinthe ...boma kungosintha iwe uzafela kumdende ....unapha allan witika chifukwa cha mkazi .....munthu wopusa iwe kwambili mbuzi

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x5 күн бұрын

    Muvesen akunena ufulu obela a malawi galuyu okukuda kukeqma

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg6 күн бұрын

    Dzaka 60 yoh bwanji dziko lili paumphawi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 shame

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d5 күн бұрын

    Akuopa kuti akakuwidwa ku 6 July 😂😂😂😂 mwabalalika makape

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatundulo6 күн бұрын

    Good

  • @VanPaul-sv9yx
    @VanPaul-sv9yx5 күн бұрын

    Nanu tazingodurani nkhani zofunikirazo ndikumaponya apa osati ndi nkhani zopoira zomwe

  • @user-mk3fy9nl2u
    @user-mk3fy9nl2u5 күн бұрын

    Inunso mukuziziwa zimenezo

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri68736 күн бұрын

    Well done Enoch chihana utsogoleri ndiumeneo. Tikufuna tiwaziwe anthu amene achoka ku Germany ofufuza za ngozi ya vice president ndi azathu 9. Awapeza bwanji anthu aku Germany owo aboma anene.

  • @isaaczuze
    @isaaczuze3 күн бұрын

    Mulila bwanji poti mwachita kumupha chilima koma ndizokhumudwisa kwambili

  • @MatiasChimsakasa
    @MatiasChimsakasa5 күн бұрын

    Komano bwanji anthu anasangalala polumbilitsa olemekezeka a vp koma 6jly ayi Kodi undiuthenga wanji mukupeleka kwa ife achinyamata

  • @user-nr4mi7pt8g
    @user-nr4mi7pt8g5 күн бұрын

    Ma billion chikondwererowo nde tigawanepotu sizausiru apa

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms5 күн бұрын

    Akuti muli wufulu m'malawi zoona

  • @mussakathumba128
    @mussakathumba1283 күн бұрын

    Komanotu kunena chilunga amalawife tikufatsa kwambiri plus ulemu too much.chakwera wationjeza akungopha anthu ngati khuku tinayenera kumuchotsa before mavoti

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma5 күн бұрын

    Masiran born kalindo kaye mukubisa chan pomumanga iyeyo

  • @user-xf6dn7pv9b
    @user-xf6dn7pv9b5 күн бұрын

    Chakwera ndiwe mbuzi wamva , galu , nyani chittsru cha munthu

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d6 күн бұрын

    Following

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b5 күн бұрын

    Mufika kumeneko nonsenu kumeneko za chamba 6 July muzakhalamulibe moyo inu agalu eti mboloyako

  • @yusufbakali
    @yusufbakali6 күн бұрын

    Mbudzi iwe

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py6 күн бұрын

    Inet imfa yachilima ndalota utsiku tapephera mosweka mtima akundilakhula kuti pangoz damulumuka koma anthu adandipha pondikhapa mendo zanga ndiy achakwera musamalet enafe ndi daniel tikapephera mulungu amayakha kumaloto athu mudapha inu pomukha chilima ndi zikwanje munyaaaaa nane daniel omasulira maloto kuuulurani

  • @ChristinaLigomeka

    @ChristinaLigomeka

    6 күн бұрын

    😭😭😭 Km kulakwatu uku ayaluka awa akusewera ndi Mulungu km😭😭😭😭

  • @ManifoldPhiri

    @ManifoldPhiri

    6 күн бұрын

    Usatchure dzina la mulungu wako pachabe mingochimwa nazo izi

  • @ChristinaLigomeka

    @ChristinaLigomeka

    6 күн бұрын

    @@ManifoldPhiri atchula pacha be pempherani nanu mosweka mtima Mulungu sapepusa PEMPHELO losweka mtima Koditu amakani nu choona muchidziwa posachedwapa mwazi ukufula ohoooo wanthu 9 mmmmmm anthu mimba zamangidwa kufuna kudziwa choona chochoka kumwamba anthu kukugonedwa mapili kufuna kudziwa nchoonadi chochoka kumwamba inu ngati mafoloko alimanja daily musaganize ngati dziko lonse anthu avula dzuwa liliphweeee mukucheza ndi Mulungu

  • @SheenahMwalabu-iz3pr

    @SheenahMwalabu-iz3pr

    6 күн бұрын

    ​@@ChristinaLigomekakunena zoona imfa iyiyi sikundigonetsa tulo ndizowawa ndipo ngati bodza Chilima kulibe zoona. Mulungu munaloleranji? 😢 ndikufuna tidziwe zoona

  • @JosephKuyeli-rc9on
    @JosephKuyeli-rc9on4 күн бұрын

    Or mpunga wa nyama tisadyenso?? 😢😢😢

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3f5 күн бұрын

    Mapemphero ake ati komanso abusa achokera mpingo uti Please leave God alone please

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy17496 күн бұрын

    Zaziiii

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi6 күн бұрын

    Stupid you guys in chakwera team Mwapha chilima anthu inu mukukayankhula zautsiru

  • @charlesvenacio9773
    @charlesvenacio97735 күн бұрын

    Malawi muno mulibe umfulu

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem5 күн бұрын

    Iwe kumkuyu ndiiwe mbuz et ufulu wake ulikut popeza mungomanga aliyese brushit zako

  • @ClementMinyanga
    @ClementMinyanga4 күн бұрын

    Ufulu wake ulikut???

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda98305 күн бұрын

    Anthu tili ndi mafunso kumene

  • @louisgolden
    @louisgolden4 күн бұрын

    Kodi July yili Liti Koti muyambe kunena Za 6 July

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal4 күн бұрын

    Ufulu wake utiwo?????

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w6 күн бұрын

    Mbolo zanu

  • @isaaczuze
    @isaaczuze3 күн бұрын

    Kunkuyu panyapako galu iwe

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm6 күн бұрын

    Chakwera is a mbolicious guy.

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k6 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma5 күн бұрын

    Akunkuyu machende

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro6 күн бұрын

    Zoona akufunikadi kunthandizidwa

Келесі