ali ndi makhutu afe good speech DR USI 100%
A Michael Usi mwamugulisa mzano, mwaphesa chilima ndinu
Malawi 🇲🇼 akufunika anthu ngati awa osangoti yes yes zili zonse
Awa zowayenera nzomwe zija ku masewero not izi ayi adzingopeleka azinzao nchimbuli mbuli
Kod zoti yona anamutsitsila pakat pa nyanja sanawelengeko
A usi mwaiwala chimodzi muzikumbukira nkhani ya Yona muchombo muja zinthu zikavuta sitimasankha katundu oponya mmadzi ai muziwe zimenezo Hon USI
Wandale ndi munthu omuyamikila, ndiye utsiluwo Kodi a Malawi mudzachangamuka liti???? Anthu olilitsa inu😭😭😭😭
Well said
Ausi mumatiimilila kumauzadi zowona anyozele okha achakelawo akazaluza azakhale okha chifukwa chosamva kwao 👍
A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD WE WILL END ALL NONSENSE GARBAGE FOOLISHNESS HAPPENING TO OUR LAND
Good Message ❤
michael usi you have to be our president ,cause you know exactly what malawians want
Yaaa neeee Mr usi
Mau abwino okonza dziko Dr Michael Usi
Good speech
a usi kumeneko ndiko kulankhula kwamphavu takunyadilani more fire 😂😂
Goog Message
👍👍
Yona komatu anamutsitsa zitavuta apatu zinthu zavuta 😀😀😀😀
Zoona ❤
This is true
Amakoma asanalowe udindo koma akasakhidwa amasitha
yes bwana yes bwana cholinga kufuna kuononga dzina lanu
Allah knows best
100% my president
Lelo asiya kuyankhula kut muboma muli mbuz zokha zokha kkkk ndale icant follow
Kuswa kuswa basi kkkkk
Siku lachigawenga muchizungu amati chigawenga day
Anayakhula koma osamanamizana chekwera anazivera okhatu apa
Bwato likamamira sitimaona chotsitsa. Mwambi otsutsana nawo
Dr usi amanveka motelomo
NDIMAONA NGATI THABWALA AKULU MUNASIYATU KKKKKKKKKKKK AYI NDITHU ,ITS NOT ALL UNITY THAT STAND WHICH IS OUT SIDE THE TRUTH OR JESUS CHRIST
Makape awa
No comment yet
Amenentchito sakugwira achosedwedi akuyipisa mbiri chakwera wanuyo
Kkkkk true
Zanveka ndithudi munthu wankulu ndithudi!,,,
Koma malawi walero ndi nyatwa!😆
Zoona zake manganya muuze Chakwerayo mbuzi yamunthu
Kkkk usi mukukana kusika bwato? Kkkk mumila limodzitu chifukwa ndie APM akulowanso mwatinamiza tinakuvotelani kwatha amalawi anachenjela sitingamvelenso bodza lanuli bola ki Egypt than ku bagamoyo
Chilungamo ndi chimenechi
Zopepela zanuzo osamagwilisa ntchito baibulo
Kkkk mawu mawu abwino kwambili
Ndipo musayelekeze kutsika. Mumira.
Kumeneko ndiye kulangula
Koma Mkulu uyu 😂😂😂😂😂
Iwe mbuzi munthu wopanda nzeru iwe chitsilu boma lake liti lakuthaithalo
Zonazake mbwiyache
Kamuzu wakupha anthu uja
Madzi achita katondo 😂😂😂
Chili Ndi mutu muli dzeru
Ngalu
😂😂😂😂
If ndiye timasitsila pakati popo iyaaa asambila ngati satha aona plan
Пікірлер: 58
ali ndi makhutu afe good speech DR USI 100%
A Michael Usi mwamugulisa mzano, mwaphesa chilima ndinu
Malawi 🇲🇼 akufunika anthu ngati awa osangoti yes yes zili zonse
Awa zowayenera nzomwe zija ku masewero not izi ayi adzingopeleka azinzao nchimbuli mbuli
Kod zoti yona anamutsitsila pakat pa nyanja sanawelengeko
A usi mwaiwala chimodzi muzikumbukira nkhani ya Yona muchombo muja zinthu zikavuta sitimasankha katundu oponya mmadzi ai muziwe zimenezo Hon USI
Wandale ndi munthu omuyamikila, ndiye utsiluwo Kodi a Malawi mudzachangamuka liti???? Anthu olilitsa inu😭😭😭😭
Well said
Ausi mumatiimilila kumauzadi zowona anyozele okha achakelawo akazaluza azakhale okha chifukwa chosamva kwao 👍
A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD WE WILL END ALL NONSENSE GARBAGE FOOLISHNESS HAPPENING TO OUR LAND
Good Message ❤
michael usi you have to be our president ,cause you know exactly what malawians want
Yaaa neeee Mr usi
Mau abwino okonza dziko Dr Michael Usi
Good speech
a usi kumeneko ndiko kulankhula kwamphavu takunyadilani more fire 😂😂
Goog Message
👍👍
Yona komatu anamutsitsa zitavuta apatu zinthu zavuta 😀😀😀😀
Zoona ❤
This is true
Amakoma asanalowe udindo koma akasakhidwa amasitha
yes bwana yes bwana cholinga kufuna kuononga dzina lanu
Allah knows best
100% my president
Lelo asiya kuyankhula kut muboma muli mbuz zokha zokha kkkk ndale icant follow
Kuswa kuswa basi kkkkk
Siku lachigawenga muchizungu amati chigawenga day
Anayakhula koma osamanamizana chekwera anazivera okhatu apa
Bwato likamamira sitimaona chotsitsa. Mwambi otsutsana nawo
Dr usi amanveka motelomo
NDIMAONA NGATI THABWALA AKULU MUNASIYATU KKKKKKKKKKKK AYI NDITHU ,ITS NOT ALL UNITY THAT STAND WHICH IS OUT SIDE THE TRUTH OR JESUS CHRIST
Makape awa
No comment yet
Amenentchito sakugwira achosedwedi akuyipisa mbiri chakwera wanuyo
Kkkkk true
Zanveka ndithudi munthu wankulu ndithudi!,,,
Koma malawi walero ndi nyatwa!😆
Zoona zake manganya muuze Chakwerayo mbuzi yamunthu
Kkkk usi mukukana kusika bwato? Kkkk mumila limodzitu chifukwa ndie APM akulowanso mwatinamiza tinakuvotelani kwatha amalawi anachenjela sitingamvelenso bodza lanuli bola ki Egypt than ku bagamoyo
Chilungamo ndi chimenechi
Zopepela zanuzo osamagwilisa ntchito baibulo
Kkkk mawu mawu abwino kwambili
Ndipo musayelekeze kutsika. Mumira.
Kumeneko ndiye kulangula
Koma Mkulu uyu 😂😂😂😂😂
Iwe mbuzi munthu wopanda nzeru iwe chitsilu boma lake liti lakuthaithalo
Zonazake mbwiyache
Kamuzu wakupha anthu uja
Madzi achita katondo 😂😂😂
Chili Ndi mutu muli dzeru
Ngalu
😂😂😂😂
If ndiye timasitsila pakati popo iyaaa asambila ngati satha aona plan
Good Message ❤