Za meeting yoyamba ya UTM atamwalira Chilima yemwe anali mtsogoleri wao zili motele

Пікірлер: 13

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience228313 күн бұрын

    Chakwera kupha munthu kamba ka udindo? Ayi ndithu Mulungu akukhathe.

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w11 күн бұрын

    Nkhani imeneyo ndi yabwino, koma Manganya awatangwanikitsa chabe, mwamunva mzimai uja, Usi ndi wa independent, awapusitsa chabe apa.

  • @UsenLashid
    @UsenLashid12 күн бұрын

    Ulemu wanu akaliyati team yonse ya UTM pitiliza kusunga ulemu wanu komaso ndi kukweza mbendela ya Malawi komaso mokomela amalawi chezezo la ndilakuti samalani kwambiri musagulitse chipani chanu Ku MCP Ayi foundation ya UTM chakwela sakuyidziwa Ayi, chomwe akudziwa iye tonse alayasi koma zofetsa chisoni Kuti chakwela Anantchola bridge yowolokela tonse alayasi zomwe zikutathauza Kuti chakwela sakuwelengaso Za tonse alayasi chonde chonde ndalama zimene akukoza a MCP including president Kuti akupatse inu ndikuopa mulungu wanu Musalandile Ayi chifukwa zimenezo sindalama ayi Koma ndi mwazi wa president wanu komaso Kuti Ife amalawi tipitilize kukusapotani , ndi mbili ya bwino inuso mukuona amalawi ndi Mene alusila musakhale mu gulu lonyozedwa ndi amalawi chifukwa cha ndalama mudzakhala wosowa mtendele Moyo wanu , tikumbukile Kuti silikali wa kuzomba uja Anati ine ndinali komweko Ku chikangawa ndipo tibapatsidwa ma 10,000000 Koma ine ndenkha ndikulemphela kudya ndalama iyi chifukwa cha mwazi wa chilima Muthu wosalakwa god bless UTM party including all the members

  • @rashidadan2533
    @rashidadan253313 күн бұрын

    UTM ikakamila chingalawa chá tonse alliance ngati m'mene anachikakamilila Cláuds Chilima , ndithudi chipani cha UTM chizathela pomwepo mu 2025 , 😊

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q13 күн бұрын

    Moto buuu akaliyati tiyeni nazo poti inu ndi omwe mumakhala pafupi ndi chilima

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma12 күн бұрын

    Usi ndi crook musiyeni ameyo pangani zanu a utm plz

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda871112 күн бұрын

    Awa adziwona kuyipa kowombela fiti manja UTM Iithela pops asaganidze kuti .MCP yasekela aaa ngati sanalemekedze chilima awa asalawa adzingodikila kuchosedwa limodzi ndi MCP 2025 UTM adzathela popo basi dziiiii

  • @MisheckNtanbalika
    @MisheckNtanbalika13 күн бұрын

    Atuluke kaye ku tonse kut fundo zawo zikhal zamphavu km akapanda kutuluka akhozelaso maplani ngt president wawo chilima tsogolo labwino la utm liyime palokha osati ndi mcp

  • @AyamMkango
    @AyamMkango12 күн бұрын

    Kd mesa kuli vp kumeneko

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg13 күн бұрын

    Chakwela nd fiti

  • @DalitsoMbalanje-n2p
    @DalitsoMbalanje-n2p12 күн бұрын

    Osanyengela yudasi kut adye nafe imfa ija ikutiwawa.

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi12 күн бұрын

    Chakwera phudzo lelo Chilima kulibe

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi13 күн бұрын

    Zitakuchitikitala zimenezi ja ndizokaikisa ngati mungakhale ndi zonveka Kaya simuli ku chipani chakuphacho 😭😭😭😭😭😭😭😭😭

Келесі