Wansembe wamkulu wa katolika anayankhula zonyoza boma zayambaso kuzungulira dzina ndi Fr Tamani
Жүктеу.....
Пікірлер: 75
@user-mj2te7vl6p6 күн бұрын
This is good massage
@augustMag6 күн бұрын
He is saying truth message he is advice the Government sananyoze kapena kutukwana ai❤
@DanMhone-iw6xg6 күн бұрын
Sananyoze koma amalakhula zona zokha zokha komasotu wanenelatu kuti zochezatu sono chomusakila nchani ndye akunama
@ChembeWaimba2 күн бұрын
Mwalalikazi mwatenga book liti lamulungu, kusochera ndikusocheresa uku, aneneri onyenga
@festonphiri3 күн бұрын
Good message fr
@scoobymatola83146 күн бұрын
Sakunyoza You can't run a government without knowing economics
@adammadi82486 күн бұрын
To speak the truth sikunyoza ,therefore tisiye mukalidwe woyika anzatu pamoto.
@MassPastor-bn8ck6 күн бұрын
Sindikuona chomwe Mkuluyu akuyankhula zonyoza boma koma kuti ambiri mwa ife timakondwa tikamalambalala chilungamo,koma chifukwa choti chilungamo chima pweteka ndichifukwa chake zikuveka ngati kunyoza kama ayi ndithu akukamba zona zake munthuyu. I wish if we can learn to stand for the truth like this Father..........
@erasmopedrombewe88424 күн бұрын
Esse padre falou a verdade, não é desprezo
@Maliko-bp1xn6 күн бұрын
Moyo wa munthu pali thupi ndi nzimu choncho thupi ngati likumana ndi mavuto akuyenera kulankhulapo kumene ,nkhristu ngati ali ndi njala angamve bwanji mau zikufunika zonse ziyende limodzi
@MphatsoMhoney-xn2ft6 күн бұрын
Very good and short speech
@sankhwe5 күн бұрын
Good one
@chrismezalumo56986 күн бұрын
Very profound 🔥🔥🔥
@samuelazumah10506 күн бұрын
Sananyoze koma chilungamo
@isaacpaulrabson20996 күн бұрын
Good point farther
@user-oc9vl9xz8e6 күн бұрын
This is great massages to the Malawi government if they have knowledge they have to change the direction
@FrancoKaunga-rq2ki6 күн бұрын
Father you are number one! Chakwera is a big failure. Indeed we made big mistake to put chakwera as a president.
@user-lw4hw9ce4w6 күн бұрын
Wakamba zoona wansembe amenei chakwera n boma lake sakuzaununkhanso mpando 2025 muzandivoera✋
@user-nf3ik3ff6y6 күн бұрын
Good Messnge Chakwela walephela you mast go
@uzaleuzale86036 күн бұрын
Ndiye kunyozako kuli pat
@shayrafernandeslatif95566 күн бұрын
Very true
@kondwamlungu83843 күн бұрын
Amen
@BeatGondwa6 күн бұрын
Good good
@clintonhodda98306 күн бұрын
Kwacha yagwa kumene ndipo akuti Chakwera ndi ophunzira koma akulephera kuyendetsa dziko
@mtimatrading7906 күн бұрын
Ameneyu saopa anayamba kupalamula nthawi ya Bingu, anamupuputitsa mkulu wina wake magilasi a mmaso pa msonkhano.
Ineyo sindikupeza vutoo and Chakwera alibenso mzotheka mchifukwa kumakhala cabinet members ntchito yawo kumuuza presedent pomwe sipakuyenda bwino ndipo amamva ndi munthu osamangoti presedent ali ndi vutoo vutoo ndaammbaliwa tere basi
@ThomsonNyirenda-df9io6 күн бұрын
Nothing wrong good
@RaphaelKweve6 күн бұрын
Palibe kunyoza apa ,,,,
@actuarialscience22836 күн бұрын
MCPigs ndi ufiti
@GreshamKadzembe-tn8cq6 күн бұрын
Kodi inu mesa ndi amene munalemba chikalata 1993 kuti mukufuna madipaty, ndiye mukuletsa chani zimenedzo ndiye ndarezo kuba basi onse akhara a kulowa aja ndi okuba ngakhare iweyo ukulankhula we kuti ukhare pampando utha kuba so
@adammadi82486 күн бұрын
Kodi povhota mumasanga kuti awa ndi abusa asavhote? Yet kufnyika and them there are experiencing the heat.
@user-pv9uk6sc3w6 күн бұрын
Kuswa kuswa, Chakwera ndi boma lake la MCP kumene aliko mutu waima, zoona zokha zokha, ndipo latikwana boma limeneli.
Nanuso musamakokomeze kuti zonyoza boma cholinga amangedwe akunena zoona aliyese pamene zafikapa olo mwana akudziwa kuti dzikoli sili bwino athu akufa ndi njala mwezi uno Kodi nangytifikile January athu akhala motani dzikoli lafika powawa tayendani m,mizimu athu afika pongomupepha mulungu kuti angowatenga chokhalilaso ndi moyo sakuchiona chifukwa Cha mavuto
@GanieAlidih-gu7no6 күн бұрын
Palibe kunyoza apa km kunenachilungamo
@user-ev4or2kg4z6 күн бұрын
Uthenga wabwino chifukwa anthu mukuwalikiralawo ali pamavuto mu dziko lawo
@rhodrickmpumila18206 күн бұрын
Ndi cadet wa DPP uyu ndikumudziwa bwino
@AllanChabwela6 күн бұрын
Chilungamo kkkkk
@jameschibwana27516 күн бұрын
Vuto anthu mumadana ndi chilungamo, wanyoza chiyani pamenepa?
@AllanaChiphazi6 күн бұрын
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@simeonbanda4240
6 күн бұрын
Rad the Book of Prophet Isaiah! He denounced the oppression of the poor and the injustices of the government. So its the responsibility of the pastors to denounce the envils of the government. Moreover the church has contributed significantly to the development of the country so it has a say where things go wrong
@abdukarimmponda56986 күн бұрын
Zimakutuzo amalawi kumataegula..anakuuzan ndani kut kutimikira mulungu nde kut azionelera zopusa zikuchitika aba ndalama za anthu zamisonkho kubako siusatana? Nde ena akalankhula alakwitsa...munthu wachinyamata mmutu mukadali ndale za 1990 zachisoniiio,👺🤔
@viennasamuel29766 күн бұрын
Pali kunyoza apa? Chilungamo ich
@owenmoses94346 күн бұрын
Zonyoza??? In what way??? Nananuso mwayambae???
@user-kw7wr4kq9w6 күн бұрын
Stop politics, mwayiwara ntchito yanu
@user-wt7ve3el5o
6 күн бұрын
Where is the politics in this speech?? Learn to accept when things went wrong.
@Jfphiri-w7b6 күн бұрын
Rev....mwasokonela a Revrend yambani ndale...mwakanika inu kuthana ndi Santana Zaka zonsez....musatchukile pa ndale ..simudziwanso kulalika inu
@user-wt7ve3el5o
6 күн бұрын
Osamangosusa zilizonse akulu ngati inu mukumwa tea daily si onse amene akumwa tea ngati inu. Choncho ndi udindo wake ngati m'busa kulangiza nkhosa zake zammene dziko likuyendera. Palibepo za ndale apa nchirungamo chokhachokha
@Jfphiri-w7b
6 күн бұрын
Its global...go to Zambia Kenya Haiti Amerika.....homeless...no tea r there....everyone must use his head to make things move urside
@user-kr1tf2tu7s6 күн бұрын
Kodi athu awa simadziwa,muve ndi toque yomweyo angakambe zabwino za mtundu wina?amafunana wokhawokha mtundu umeneu_
@RuthChilobwe6 күн бұрын
Kkkk koma politics yo sikuba. Sattargate @Cashgate @Achairs vashgate ..
Пікірлер: 75
This is good massage
He is saying truth message he is advice the Government sananyoze kapena kutukwana ai❤
Sananyoze koma amalakhula zona zokha zokha komasotu wanenelatu kuti zochezatu sono chomusakila nchani ndye akunama
Mwalalikazi mwatenga book liti lamulungu, kusochera ndikusocheresa uku, aneneri onyenga
Good message fr
Sakunyoza You can't run a government without knowing economics
To speak the truth sikunyoza ,therefore tisiye mukalidwe woyika anzatu pamoto.
Sindikuona chomwe Mkuluyu akuyankhula zonyoza boma koma kuti ambiri mwa ife timakondwa tikamalambalala chilungamo,koma chifukwa choti chilungamo chima pweteka ndichifukwa chake zikuveka ngati kunyoza kama ayi ndithu akukamba zona zake munthuyu. I wish if we can learn to stand for the truth like this Father..........
Esse padre falou a verdade, não é desprezo
Moyo wa munthu pali thupi ndi nzimu choncho thupi ngati likumana ndi mavuto akuyenera kulankhulapo kumene ,nkhristu ngati ali ndi njala angamve bwanji mau zikufunika zonse ziyende limodzi
Very good and short speech
Good one
Very profound 🔥🔥🔥
Sananyoze koma chilungamo
Good point farther
This is great massages to the Malawi government if they have knowledge they have to change the direction
Father you are number one! Chakwera is a big failure. Indeed we made big mistake to put chakwera as a president.
Wakamba zoona wansembe amenei chakwera n boma lake sakuzaununkhanso mpando 2025 muzandivoera✋
Good Messnge Chakwela walephela you mast go
Ndiye kunyozako kuli pat
Very true
Amen
Good good
Kwacha yagwa kumene ndipo akuti Chakwera ndi ophunzira koma akulephera kuyendetsa dziko
Ameneyu saopa anayamba kupalamula nthawi ya Bingu, anamupuputitsa mkulu wina wake magilasi a mmaso pa msonkhano.
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
aaaa kunyoza kwake..kulipati pamenepo akuyakhula chilungamo
Ulaliki wa kale uwu siwa pa 3 July 2024
Kaya ndizaliti koma he is saying the truth
True mssg
Pali kunyoza apa ichi ndi chilungamo cheni cheni
Powerful
Zoona kwambiri sikuwonapo cholakwika
Osati kuti wayankhula zonyoza anayankhula chilungamo osamadana ndikuuzidwa chilungamo ayi
🤗🤗🤗🤗
Andale ampingo
Sananyoz akunena chilungam uyu
Kunena zoona munthu wa mulungu sanafotokoze monyoza ayi ngati mukufuna kumutapa mkamwa mungomutapa mkamwa sindikuona chifukwa ayi.
another Dc
Koma akunena chilungamo
Ineyo sindikupeza vutoo and Chakwera alibenso mzotheka mchifukwa kumakhala cabinet members ntchito yawo kumuuza presedent pomwe sipakuyenda bwino ndipo amamva ndi munthu osamangoti presedent ali ndi vutoo vutoo ndaammbaliwa tere basi
Nothing wrong good
Palibe kunyoza apa ,,,,
MCPigs ndi ufiti
Kodi inu mesa ndi amene munalemba chikalata 1993 kuti mukufuna madipaty, ndiye mukuletsa chani zimenedzo ndiye ndarezo kuba basi onse akhara a kulowa aja ndi okuba ngakhare iweyo ukulankhula we kuti ukhare pampando utha kuba so
Kodi povhota mumasanga kuti awa ndi abusa asavhote? Yet kufnyika and them there are experiencing the heat.
Kuswa kuswa, Chakwera ndi boma lake la MCP kumene aliko mutu waima, zoona zokha zokha, ndipo latikwana boma limeneli.
Kunyoza boma ndie kuti chaani? Kudana ndichilungamo kapena?
Uthenga wa bwino zikomo
koma bwanji kunyoza wosatandiza maganizo
Nanuso musamakokomeze kuti zonyoza boma cholinga amangedwe akunena zoona aliyese pamene zafikapa olo mwana akudziwa kuti dzikoli sili bwino athu akufa ndi njala mwezi uno Kodi nangytifikile January athu akhala motani dzikoli lafika powawa tayendani m,mizimu athu afika pongomupepha mulungu kuti angowatenga chokhalilaso ndi moyo sakuchiona chifukwa Cha mavuto
Palibe kunyoza apa km kunenachilungamo
Uthenga wabwino chifukwa anthu mukuwalikiralawo ali pamavuto mu dziko lawo
Ndi cadet wa DPP uyu ndikumudziwa bwino
Chilungamo kkkkk
Vuto anthu mumadana ndi chilungamo, wanyoza chiyani pamenepa?
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@simeonbanda4240
6 күн бұрын
Rad the Book of Prophet Isaiah! He denounced the oppression of the poor and the injustices of the government. So its the responsibility of the pastors to denounce the envils of the government. Moreover the church has contributed significantly to the development of the country so it has a say where things go wrong
Zimakutuzo amalawi kumataegula..anakuuzan ndani kut kutimikira mulungu nde kut azionelera zopusa zikuchitika aba ndalama za anthu zamisonkho kubako siusatana? Nde ena akalankhula alakwitsa...munthu wachinyamata mmutu mukadali ndale za 1990 zachisoniiio,👺🤔
Pali kunyoza apa? Chilungamo ich
Zonyoza??? In what way??? Nananuso mwayambae???
Stop politics, mwayiwara ntchito yanu
@user-wt7ve3el5o
6 күн бұрын
Where is the politics in this speech?? Learn to accept when things went wrong.
Rev....mwasokonela a Revrend yambani ndale...mwakanika inu kuthana ndi Santana Zaka zonsez....musatchukile pa ndale ..simudziwanso kulalika inu
@user-wt7ve3el5o
6 күн бұрын
Osamangosusa zilizonse akulu ngati inu mukumwa tea daily si onse amene akumwa tea ngati inu. Choncho ndi udindo wake ngati m'busa kulangiza nkhosa zake zammene dziko likuyendera. Palibepo za ndale apa nchirungamo chokhachokha
@Jfphiri-w7b
6 күн бұрын
Its global...go to Zambia Kenya Haiti Amerika.....homeless...no tea r there....everyone must use his head to make things move urside
Kodi athu awa simadziwa,muve ndi toque yomweyo angakambe zabwino za mtundu wina?amafunana wokhawokha mtundu umeneu_
Kkkk koma politics yo sikuba. Sattargate @Cashgate @Achairs vashgate ..
@AllanaChiphazi
6 күн бұрын
Tidzangomvotera iyeyo, amalekeranji kukawadzudzula pamaso pa abomawo, lilipo boma lomwe linayamikiridwa ndi anthu amenewa? Popeza bolili lonse amalipezera zifukwa, zilalikani zoti anthu asiye kupanga ntchimo tiziopa tsiku lachimaliziro. Zamavote munayambitsa ndinu nomwe
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@FrancisDay-br7xb
6 күн бұрын
Iwe kumeneko sikusaniza ndale ndi mpingo koma kuzuzula zoipa za boma
@user-wt7ve3el5o
6 күн бұрын
Lalikani wanu tiumvere
@GiftSnoxy
6 күн бұрын
Nyani iwe wamva ukudziwa chan