Kodi ku chipatala anapita naye mwanayo kuti akamupime kuti chamumpha ndi chani? chifukwa achipatala akadanena ndithu chomwe champha mwan
@marianyirenda
11 ай бұрын
Zoona akanapitadi ku Chipatala kuti akaone chomwe chapha mwana kuti ndi chani koma vuto la anthu akewa umbuli ndi wambiri kwabasi za sukulu mitu yawo wonse mulibe
@confidencebanda109 Жыл бұрын
Zoopsa 🤭🤭🤭
@justinjason7262 Жыл бұрын
Sound pls sir
@adolfodamianotitiphiriadol5417
Жыл бұрын
Mumakwana ma bg man a balanço semanal ck and Govate.
Пікірлер: 51
These people can feel more at home in Malawi than Mozambique 😂
Thanks I'm with you balasco semanaro
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
thanks
Ndithokoze mamuna poyankha moopa Mulungu kuti kulanga mkwamwini namalenga Mulungu.komaso mwana sanama chifukwa sanadziwe tchimo ndipo ndiye wapha mtsikanayo komaso nkutheka kuti watumidwa ndi aanthu ena moti akhale tcheru ndi mtumbirawo ngati sufukulidwa.
@lovebinta6863
Жыл бұрын
Ambuye akudalitsen abambo inu tisaname munamulandilad Ambuye kukhala mpulumutsi wamoyo wanu
Azimayi Pena tizikhala serious ndi ubereki, inu zoona munthu wakusiyani Panja kulowa mnyumba inu osamusatira? Mwa njira Ina pepan kwabasi Mulungu ndamene akudziwa zonse
@estherdumbo
Жыл бұрын
Ndipo inu mmmm munthu wakudutsa osakiyakhula iwe nde pheeee osamulondola eti......... Mwina anamupha mtima make mwanayo
@estherdumbo
Жыл бұрын
Amen adad amwana Mulungu abwezera ndipo choonadi chidzadziwikaaa pangatalike pangafupike.
Koma dzikoli ladikapoooo iiiii
Koma Umboniwu mmmm penanso zitha kutheka mwina nso mwana sadaphe ndiyeyo
😊
Zosakhala bwno bwanj
So sad watching live from Kuwait
Notícias muito triste, k culpa tema criança, ela deve responder na barra da justiça
Nkhani yovetsa chisoni
Zosayenda mm Ndimakonda kunvere zomwe matipatsira
Ambuye amutsowetse mtendele komwe aliko mpaka atabwela yekha chifukwa wapha mwana osaziwa tchimo
Timakunyadirani a Balanco semanal potidziwitsa zomwe zikuchitika
Koma amayi awa nawo ndiwotani iwowa anangomusiya Staples muthu yotisamacheza naye
Aaaaa nakubalayu chisamaliro analibe ,😭😭
@ellahkapuma7908
10 ай бұрын
Imagine mwana obwera kumene kumusiya mpaka 1hr yekha opanda munthu kulowa munthu iye olo kusatila nakubala ali very careless😢
Mmmmm walakwitsa kwambili
Isso é muito triste .
Triste notícia 😢 💔💔
Mmmmh Shame on her😭😭😭
Sorry ku banja lonse lofedwa
Sad story, 😭
Zovuta izi iiiii zosamvetsetseka ayiii
This is very sad 😔
Isso é muito triste e sentimental 🥲
Mukuitha mabwana
Km ndizowawa kwambili ndisaname zandiwawa
Komaso Mai wamwayu sanali serious ndi mwanayo.Aaaa kom abale Inu😭
@joshuamtenje1900
Жыл бұрын
Eti munthu kulowa mnyumba 12 o'clock iwo kulowamo mma 3 aaàaa
No sound guys
Osamatchyula dzina plz
Nkhani zoyipa ngati zimenezi zikumveka ndipo zikuchitika tsiku ndi tsiku.
Chilungamo chizamutsata ,
Tathokodza Balanco semanayo mumagwira ntchito yotamandika kwambiri pitilidzani kutero
Abale talongosolani bwino
Very sad story amayenera kuwotchedwa basi
@user-ng2nu6xn9x
Жыл бұрын
Mumapemphera koma?
Kodi ku chipatala anapita naye mwanayo kuti akamupime kuti chamumpha ndi chani? chifukwa achipatala akadanena ndithu chomwe champha mwan
@marianyirenda
11 ай бұрын
Zoona akanapitadi ku Chipatala kuti akaone chomwe chapha mwana kuti ndi chani koma vuto la anthu akewa umbuli ndi wambiri kwabasi za sukulu mitu yawo wonse mulibe
Zoopsa 🤭🤭🤭
Sound pls sir
@adolfodamianotitiphiriadol5417
Жыл бұрын
Mumakwana ma bg man a balanço semanal ck and Govate.
@pioireneuvictorpio1391
Жыл бұрын
Pafunika apezeke aulura chomwe wapangira zimenezo.
Sizikumveka guys
@balancosemanalckgovate8464
Жыл бұрын
tipanga edition . sorry