Patricia Kaliati Ndi khwimbi La UTM kusangalala ''Athyola dance''
SKC Boma motooo buuu 🔥🔥🔥🔥
Amazing inu mulibe nzelu kwambili
Chilima keep it up bwana
SKC🎉🎉🎉❤❤
Zikakunyasa uwone zochita UTM 🔥🔥🔥
Wakwiya ndi mfiti SKC 2025 BOMA ❤❤❤❤❤
Muyambeso kutinamiza...kulakwatu uku aMalawi
Kkkk koma kaliyati sazatheka😂😂
Mwaiwala kale a Malawi ayi zikomo
Basi tu a zimayi 😂kumadikura 😅
Aaaa agalu nokha nokha ndi ndi MCP yanuyo okuba okha okha zauchitsilu mene wathelano malawi pano kumanyadila idzi thembelelo chiyani amalawi
SKC my vote❤❤❤❤
Ukukup sakokakoka kukala ngamti opandazelu kusangalila chakumba chilima ndi mbusi chkwera palukundu pao iya yausilu uweiyai chatap
anthu amene akuononga dziko ndi azimayi amangokondwera zilizonse,Koma pamapeto pake amayambaso kulira ndiyiwowo
Anthony inu mukungovomeleza zosalongosoka mukafika kunyubako mukukangona ndi njala
Komatu aMalawi kumachilapa chilima ndi chakwera nzawo ndi zimodz pls kumaganiza mwakuya popanga chisakho chanu mutipwetekesaq
Kusangalarila Muthu okuba a Malawi amaganiza mopeoera
Bola loho chakwera mbava
A dpp akuwona nyekhwe kaye ku bagamoyo nyekhwe inatembenukira😂😂😂
Bravo
UTM yabwera kudzakhala,, take it or leave it, afune asafune. Next government ndi UTM led by SKC
🔥🔥🔥🥳
Inu munawona okuba okha okha akumangana uchisilu mudzalowabe mundende bola moyo
🔥🔥🔥
Koma mukusowa zochita chosecho maluzi alitho
Panyapanu agalu
Ayi zikomo anthu inu koma ndi chani???
Asowa nazo kolowa kd .?
MCP amatelo inu muli ku kenani anzanu kuwasiya kwa pilato zaka zonsezi, ulendo onyamukira limodzi.
Ndikamaona anthu akumasapotabe chilima ndi tonse alliance ndimangot amalawife tilindivuto lalikulu.koma zoona anthu amenewa atipusisa kale 5 years for nothing still kumawaomberabe manja.agalu amenewa 2019 amabwebwetuka kut anzawo anali olephera lero iwo alowa mkat zero kwa 10 lero anthu akutengekabe nawobenso.amalawi ndife ofa kuzimu ndithu ndi thupi lomwe ndife osaganiza timangooneka ochenjera koma tulo lilindife Mmmm zosaoneka.timatengeka ndizazing'ono kwambili even tishirt imene sitichedwa kuiwala ndife agalu eni eni.atipusisenso kachikena makapewanso tiwaikenso pampando for 5 yrs again zoona?iwo alibwalo akulephera kumenya mpila pomwe ama bulema anzawo kumati olephera.timilomo tawoti tinabwebwetuka kwambili mu 2020 muja apatayambanso kunamiza anthu 😂😂😂😂 mayo I cry for my mother land Kaya nabadwilanji kumalawi ine ambuye tikhululukileni ndithu sitidziwa chomwe timatsatila ndife akhungu mmalawi muno.and sitidziwa chomwe timafuna ife pokavota timangopangila kupsa ntima basi osalingalira zamawa.
😂😂😂😂😂😂😂😂
Masanje eni,,eni,,kulephera kuimba njaratu imeneyo😢😅
😂😂😂😂
Koma campaign iyaka
CHIPANI musachichepetse ichi nchamoto
Nice
Пікірлер: 37
SKC Boma motooo buuu 🔥🔥🔥🔥
Amazing inu mulibe nzelu kwambili
Chilima keep it up bwana
SKC🎉🎉🎉❤❤
Zikakunyasa uwone zochita UTM 🔥🔥🔥
Wakwiya ndi mfiti SKC 2025 BOMA ❤❤❤❤❤
Muyambeso kutinamiza...kulakwatu uku aMalawi
Kkkk koma kaliyati sazatheka😂😂
Mwaiwala kale a Malawi ayi zikomo
Basi tu a zimayi 😂kumadikura 😅
Aaaa agalu nokha nokha ndi ndi MCP yanuyo okuba okha okha zauchitsilu mene wathelano malawi pano kumanyadila idzi thembelelo chiyani amalawi
SKC my vote❤❤❤❤
Ukukup sakokakoka kukala ngamti opandazelu kusangalila chakumba chilima ndi mbusi chkwera palukundu pao iya yausilu uweiyai chatap
anthu amene akuononga dziko ndi azimayi amangokondwera zilizonse,Koma pamapeto pake amayambaso kulira ndiyiwowo
Anthony inu mukungovomeleza zosalongosoka mukafika kunyubako mukukangona ndi njala
Komatu aMalawi kumachilapa chilima ndi chakwera nzawo ndi zimodz pls kumaganiza mwakuya popanga chisakho chanu mutipwetekesaq
Kusangalarila Muthu okuba a Malawi amaganiza mopeoera
@user-le9su3mt7r
Ай бұрын
Bola loho chakwera mbava
A dpp akuwona nyekhwe kaye ku bagamoyo nyekhwe inatembenukira😂😂😂
Bravo
UTM yabwera kudzakhala,, take it or leave it, afune asafune. Next government ndi UTM led by SKC
🔥🔥🔥🥳
Inu munawona okuba okha okha akumangana uchisilu mudzalowabe mundende bola moyo
🔥🔥🔥
Koma mukusowa zochita chosecho maluzi alitho
Panyapanu agalu
Ayi zikomo anthu inu koma ndi chani???
Asowa nazo kolowa kd .?
MCP amatelo inu muli ku kenani anzanu kuwasiya kwa pilato zaka zonsezi, ulendo onyamukira limodzi.
Ndikamaona anthu akumasapotabe chilima ndi tonse alliance ndimangot amalawife tilindivuto lalikulu.koma zoona anthu amenewa atipusisa kale 5 years for nothing still kumawaomberabe manja.agalu amenewa 2019 amabwebwetuka kut anzawo anali olephera lero iwo alowa mkat zero kwa 10 lero anthu akutengekabe nawobenso.amalawi ndife ofa kuzimu ndithu ndi thupi lomwe ndife osaganiza timangooneka ochenjera koma tulo lilindife Mmmm zosaoneka.timatengeka ndizazing'ono kwambili even tishirt imene sitichedwa kuiwala ndife agalu eni eni.atipusisenso kachikena makapewanso tiwaikenso pampando for 5 yrs again zoona?iwo alibwalo akulephera kumenya mpila pomwe ama bulema anzawo kumati olephera.timilomo tawoti tinabwebwetuka kwambili mu 2020 muja apatayambanso kunamiza anthu 😂😂😂😂 mayo I cry for my mother land Kaya nabadwilanji kumalawi ine ambuye tikhululukileni ndithu sitidziwa chomwe timatsatila ndife akhungu mmalawi muno.and sitidziwa chomwe timafuna ife pokavota timangopangila kupsa ntima basi osalingalira zamawa.
😂😂😂😂😂😂😂😂
Masanje eni,,eni,,kulephera kuimba njaratu imeneyo😢😅
@eliffagondewe8214
Ай бұрын
😂😂😂😂
Koma campaign iyaka
CHIPANI musachichepetse ichi nchamoto
Nice