MCP Change How You Treat SKC - Rwara
On Nyasa VoiceBox, a self declared card carrying member is appealing to members of the Malawi Congress Party (MCP) to show some respect to the Vice President Dr Saulos Klaus Chilima.
Ku Nyasa VoiceBox, chikalata chodzitcha kuti ndi membala wa chipani cha Malawi Congress Party (MCP) chikupempha kuti apereke ulemu kwa wachiwiri kwa Purezidenti Dr Saulos Klaus Chilima.
#malawi
Пікірлер: 158
You are very right brother. Chilima akuzunzika but he remains humble to to the president. God should see him through. If he was given a chance to implement the reforms, this Government would have been the best ever. Chilima, continue being humble.
I never thought I would hear a reasonable, fair voice.
Tifune tisafune Chilima will remain the genius whether him ruling Malawi or not. It's only Chilima who can change Malawi even the MCP gurus knows. He is a big threat to MCP not APM as it is put on the ground
@PhilomenaChikabadwa-dt6vy
4 ай бұрын
God save Malawi.
Mr Rwara is a reasonable Malawian who is fair and just. Chilima has been mistreated by mcp
Malawi lacks citizens who understand issues like the way you do. Big up i like the way you have voiced it out
@LearnsMussa
4 ай бұрын
. P
I am happy with your advice mr Rwara.
Well said. Paja chilungamo ndi mwano eti pa Malawi 😂😂❤❤
A'm a staunch supporter of MCP, but plz make sure, we must give SKC the presidency. He deserves it, whether one like it or not. Anzathu a kumpoto chonde nthawi zonse mumayambitsa zinthu zoti patsogolo timabvutika nazo. Musayiwale kuti ndinu amene munapanga kuti Kamuzu Banda akhale life president, so plz people from the North, stop being stupid by endorsing useless things.
@johnsimko2941
4 ай бұрын
North people are not stupid my friend, never been before. Remember they voted for chilima than any other region.
@StevenTembo-mb7rm
4 ай бұрын
That's true we as the northerners we don't favour useless and stupid politicians. Timavotera munthu wanzeru posatengera chigawo chomwe munthuyo akuchokera bola akhale mMalawi
Eeeya you are saying the truth. MCP ikukathera ku Convention.
Well said, from a well Matured person
Njoka yofatsa imalumira kumchila chilima is brilliant guy muzamulira atatulusa joka pamapeto pokuti Inu zose mwaika pa ground chifukwa Cha kulubwalubwa
Chilima ndi pangolini or ku mcp ko imadziwabwino za chilima
congrats to Mr vice President for the patience and owning to mcp members For they Bad actions Show to UTM president......
You have spoken very well
A'm from Dedza, the home of MCP, no one can question about that, my uncle managed to keep this party called MCP, even when stupid Bakili Muluzi tried to destroy it, its not negotiable, let us give it to Saulos Chilima. aChewa, chonde tisapange nsanje, munthu uyu adapanga kuti MCP idzuke kwa kufa, chonde pasapezeke m'chewa omunyoza Chilima, ndapota nanu. Musayiwale kuti Muluzi adalimbilira kuti mpaka adzalowe m'manda, adzawonetsetsa kuti MCP isadzalowenso m'boma.
Chilima will be president 2025
@sweeneykamwendo6251
4 ай бұрын
Mcp will not allow Chilima to be a torchbearer in 2025 believe me or not
@AmusedDimSum-hd5yp
4 ай бұрын
which country
Osamva asamve munthu wayankhula zothandiza chipani uyu, koma poti timasankha kutseka makutu, tiziona.
Mcp yatha iyi chilima simunthu oti angamutaye chonchi n kumunyoza honestly 2025 I see him winning his good reasoning n humbleness will bring joy to malawians
ALwara akunena zoona kupanda chilima anthu sakanavotera mcp
Respect the Vice president as per your advice. MCP if you loose Chilima you will fall by the nose.
Thats true voice, mcp must not put bhind chilima he is your position fighter.
Koma choti muziwe chilima mukamuswaya mcp sangawine
Mr Lwara zimene mukulakhula ndi zoona BOMA lilipoli ndi la zipani zingapo zimene zinapangisa kuti Chakwera nd a Chilima tiwavotere koma vuto la MCP akadalibe ndi moyo wa one party system akanakhala Ena a MCP bwenzi pano akuwona zili pa Ground Chilima ma corner wose akukondedwa ndi anthu ndipo ngati akususana ndi mugwirizano ndiye kuti sanawina chifukwa sakulemekeza mu gwirizano umene ulipo and a Chakwera asataya chikhirisitu chawo chifukwa cha anthu amene akufuma kugwesa dziko la Malawi chifukwa chosafunira Malawi za bwino go ku Tanzania zinthu zikuvuta koma dziko zitukuko zikuwoneka koma ku Malawi ma family amene akusangalala ndiwokhawo ali close to president izi ndi zapa dziko la pansi tizisiya musamupange chipongwe lero Chilima otherwise muthera mu njira a MCP
Pangano linadulisa mutu wa yohane , MCP must know where the coming from ,Chilima must be respected he put the in power and He can take it back.
Very good speech
Mr Rwara is saying the truth.
The words without aparch mau Mau auzeni chilungamo MR AChirwa
Zoona brother
Chikondi ndi chabwino MCP isayiwale komwe achoka Chilima akuyenela Kulamulila basi
Exactly coz every knows that without Chilima mcp could fall down according to our vote percentage btwn tonse alliance and dpp
A MCP yakula ndi nsanje ndi Dr Saulosi Chilima. Akuyiwala kut a pambane anagwira ntchito ndi Dr Saulosi Chilima. Kusiya kuzitenga bwino ife a Malawi sitingakuloleni ndipo mukuwonga chipanidi.
Anthu a mcp ngati akunyoza chilima kuwona ngati awoloka sazapitilira 2025 and mcp ikuzaluza ndi kuntha komweko
Voice of the voice viva
Zoona zake MCP saziwa chomwe akuchita aziwona kusogoloko komwe tikurowelaku angolawawo atulukaso AWA chilima NDI solo
AKezzie Msukwa wakuvimanya yayi ivi wakuchita suzgo la ise kuno ku mpoto tikugwiritsidwa waka ntchito pala vyakukhumba vyawo vyafiskika mbwenu tikutayika waka ngati chiseru chakumala tikusambirapo kanthu yayi
Yes paja munthu akakhala kuti ndiwozindikira amadana naye.
Chilima ndi president wamasomphenya Koma zimene akuchita a MCP ndi zoyipa economic yagwa mumene chakwela alipampando
Amalawi tiyeni tiphunzire kulankhula mwaulemu,maka inu anzathu andale.Tikapita pamsonkhano ,timafuna kumamva zothandiza,anthu pamabvuto omwe tikukumana nawo,Osati mau onyozana.Ana athuwa tikuwapatsa chitsanzo chotani.Apresident analankhulapo kuti pali anthu omwe akufuna kumaso koneza pakati pa iwo nda Vice president,chonde ngati mulipodi,Mulungu akupatseni mtima wabwino wachikondi.A vice president ndi munthudi wopirira.Pitilizani khalidwe lanu la ulemu kwa president,Mulungu amadziwa zonse.
No one needs chakwera
Mukunena zoona Mr Rwara asiyeni a MCP akudzikumbila manda
Osataya kabudula wakale chifukwa mwagula wanyuwani, tsiku lina mudzafuna kuumba njerwa. Tread carefully.
Cape town streaming you live
Enough is enough mcp God will rescue Chilima one day. But know kuti mwathera pompo
There is need for power sharing deal not coalition in Malawi.
Chakwera will regret ,,, taking chilima for granted
❤❤❤❤ ya ndizoona
Mega farms, civil servants salariies, reform in civil service and soldiers new houses it's UTM / Chilima manifesto.😊😊
How do you attack north in this.That is not building our beloved mother land.We are one people,nomatter what
Chilungamo chokhachokha . MCP yakwera pamsana pa njobvu yaiwala kuti kunjaku kuli mame .
Ife amalawi ndi opusa kwambiri tikumayiwala bwanji za MCP
Mukuyankhula zowona zokha zokha chilima sakulemekezedwa
Mau mau. Chikondi chitsogole pakat pa azitsogoleri anthu.....
Mwawuze asankhe chilima a mcp president
Achilima ndi munthu okhwima maganizo paja amati kufasa kumaonesa maso ankhono
Of course Mr Rwara is saying the truth. Dr Saulos Klause Chilima did a great job during 2020 campaign.
No more Alliance this time chilima must go alone ku election we MCP we're not afraid anything this time around
That is true what you saying bro
Mr Lwara is right.
MCP members plus mr Lazarus don't forget about chilima nfi yimodzi anakuwolotsani bwato
Mcp izaonazosaona muchaka. Chaka cha2025 ikuzagwa
Awo akulu akulu a chipani cha MCP asazathamangileso ku chipani china
Truth prevails
Ndizona chipanda chiliima sakanalowa palibe amafuna Mcp
Iweyo ndiwe wq chipani chanji chirwa??
Mcp as political party has right to have convention disregarding that it is in partnership with other parties hence being party has its constitution , on what you have highlighted concerning what Kezzie Msukwa stated on interview that no one will contest against Chakwera that's obviously, if you may recall that was the similar Scenario with DPP party the time they are in government . Mr Chirwa you are true citizen of Malawi and really you are indeed a member of MCP . I love Dr Chilima very much and 2025 surely he will be our president, Chilima and Chakwera are not fools they know what to do come 2025 , Chakwera being MCP party president will endorse Chilima at last minute believe me those guys are playing underground games
Ndipo iyeyo muti chakwera sangawine
Big Up
Koditu akulu akulu achipani cha mcp ndianthu osazidikila
Abambo inuyo mukanakhala nduna mwina Bwez mukumuuza kapena mukumuzuzula pano mbola Koma ndimulungu kufuna kutizwitsa Ife amalawi Kuti lazalo timudzwe
In the Bible there is a prodigal son who asked his father to given him his share and went away after using what he was given he went to ask for a job looking after nkhumba and eat together with nkhumba but after thinking wisely he decided to go back to the father and tell the father that I am not wealthy before you but the father prepared a feast for him . Why not Chilima go back to the father and say here I am😂😂
Ukunama yiwe pa ground pake party ngati anthu akumufuna chilima bwanji wosawinako mpando ku kalonga cadet wachabechabe
Very true munthu wankulu
Jealous Too Much Anthuwa !!! Chilima Arindi Moral Palipose
I guess the decision towards political alliance was genuine but lacked credibility. Remember whatever was agreed between the two does not rule out constitutions of the two parties. Unless otherwise there is an inclusion of such a clause in the constitutions validating powers of parties constitutions
Achakwera adaiwala koma ili ndi dziko
Sure mcp change mis treating SCK
Akumkhomelera chilima a mcp akudziwa kuti chilima amawaposa dzeru agaluwo
Izo mukulankhurazo zili choncho MCP sitikuyifunanso boma lakupha
Mkuulu uyu amalankhula zoona zokhazokha
Ukunama,owe si wa Mcp,usatinamize apa mmmmmmm
Pangolin skc
There's no one who can speak for chilima
Chilima ndi vice president Basi,whether you like or not, Mcp 2030 wooooo,tisapusitsane apa
Umakwana zoona zenizeni
Kuti zinthu zawo zayendele bwinu kupanda apo awona zokhomà achekwela
What we're waiting is the agreement that they did at the first time Olemekezeka aChakwera nthawi yao ikutha pompano aziwilethu
Zoona zokhazikha.
True
Facts
SKC 2025 boma.MCP take care behave like you have all your sense.
😢
He knows that what he feels in himself is more great that what MCP is doing.hyna is a hyna.
2025 kuli kanthu.
Mawu mawu mawu
Zoona chilima akunyozedwa
Chilima boma 2025
Zinduna ziwili izi zikuiwala kuti analowa bwanji m'boma
Bwato lija simunakwere nokha kuti muwoloke njanja ya Malawi
A kudziwa chimene a kupanga a Malawi wosagona imeneyo ndi ndale
NO PAIN NO GAIN NGAN YAVEKA BWIN BWIN BIG