No video

Kachikenaso Born Kalindo 😂🙌😂😂🙌 pa Chi Sunday 14 July 2024

Пікірлер: 85

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4bАй бұрын

    Ndalama zingowonongedwa anthu angofa mdzipatalamu mankhwala kulibe anthu angofa sisawawa Mulungu akuwoneni mwapaderadera

  • @user-nz7bd7lm4i
    @user-nz7bd7lm4iАй бұрын

    Born mulungu azikudalitsa kwambiliiiiiiiiiiii ndipo azikuteteza🙏🙏🙏

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassimАй бұрын

    Chakwera akuwalipira azungu pa ntchito yomwe adagwila pakupha chilima

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zbАй бұрын

    Achakwera akuwononga dziko lathu kwambiri.

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9nАй бұрын

    Dziko lochitisa manyanzi, nkumati achakwera akugwira ntchito ngati president.

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3fАй бұрын

    Tiyamike kubwera kwa tonse Alliance anthu mukung'alula kuti anthu tiziwe zenizeni more 🔥 🔥

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hzАй бұрын

    Koma this very very shameful 😢😢😢😢😢

  • @cjaymw496
    @cjaymw496Ай бұрын

    Ya balance I think so too😂😂😂

  • @fredsemu7136
    @fredsemu7136Ай бұрын

    KOMA CHIKANGAWA ATIPWETEKA NDITHU

  • @MisheckAselo
    @MisheckAseloАй бұрын

    Chakwera mchifukwa chake anakapemphera ku CCAP kamutu kataya mission yapheduka, umkaona ngati wapha chilima zako ziziyenda, chilima sanafe akanalipo muona zakuda inu😂

  • @ThokozaniMunkhondia
    @ThokozaniMunkhondiaАй бұрын

    A born kalindo,inu ndi mbambande😢😢

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394Ай бұрын

    Koma bon mulungu akuteteze

  • @ClearKondowe-m3j
    @ClearKondowe-m3j28 күн бұрын

    Very sorry a Malawi kaya dziko lathu likonzedwa. Yoooo

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bmАй бұрын

    Mulungu wakiya nawe chakwera waona mulungu wakwiya ndpo mulungu achita nawe iweyo

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9iАй бұрын

    Ati akukonza zinthu!....😅😅😅😅😅😅😅...koma kukonza kunasintha..

  • @ZettaImuranYunusu
    @ZettaImuranYunusuАй бұрын

    Osati Ifeyo Amalawi ai.... But all opposition party's we are with you Trap

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6fАй бұрын

    Ima poyela ndipo aliyense azimva ndithu.Tinasankha satana

  • @crosbeygondwe5403
    @crosbeygondwe5403Ай бұрын

    Kung'alulaaaa😂😂😂😂

  • @robertkamtimaleka4394
    @robertkamtimaleka4394Ай бұрын

    a Born Kalindo 42 million yommweyi basi

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299Ай бұрын

    Chakwera iweyooo

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9eАй бұрын

    Auze DC ❤ agaru amenewo

  • @SumanJames
    @SumanJamesАй бұрын

    Akalindo sakunama

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665Ай бұрын

    Tiuzeni zambiri bwana .kma dziko lathu lomwe kuzunzika

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomelaАй бұрын

    Ma mafia ati😂😂😂

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9eАй бұрын

    The DiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiCiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @JamesTeacher-b3o
    @JamesTeacher-b3oАй бұрын

    Bwana inuyo mmatha kuyankhula ulemu wanu

  • @AufiThera
    @AufiTheraАй бұрын

    Wathu wathu born kalindo ✌️🔥 Kung,alula💯💪

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomonАй бұрын

    KKKKKKKKKK BALANCE KUWAMALIZIRA PANTCHITO YOMWE ANAGWIRA PAKUPHA CHIRIMA NDI ANZAKE SHAME CHAKWERA

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7vАй бұрын

    Munyengo yakung'alula

  • @Mikekajawo-pq9nr
    @Mikekajawo-pq9nrАй бұрын

    At we are building Malawi yet ndalama zikutuluka

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5dАй бұрын

    Ndalamq zathu misokho yutha ukupeleka kwazigawenga azipha azibale anthu osalakwa Chakwera sukuwina ase ndakuuza

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850Ай бұрын

    Malawi akulowera kuti abale? Long live the DC

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomoleАй бұрын

    The DC ❤❤❤

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomelaАй бұрын

    Ma mafia 😂

  • @Pangolinimw
    @PangolinimwАй бұрын

    The DC 😅😅😅

  • @user-xx4mt8ox8e
    @user-xx4mt8ox8eАй бұрын

    Mwati ndi Balance?

  • @RitaKainga
    @RitaKaingaАй бұрын

    Ulemu wanu the DC

  • @GeoffreyMaulana-rh5rx
    @GeoffreyMaulana-rh5rxАй бұрын

    Ng'ona zalusa kufuna kusaulisa Malawi

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062Ай бұрын

    Mr Bon Kalindo ndinu oyankhuliradi a Malawi tonse, keep it up the DC.

  • @WilliamKawaza
    @WilliamKawazaАй бұрын

    Tell them DC

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489Ай бұрын

    Ayi zikomo

  • @BlessingsMikeyasi
    @BlessingsMikeyasiАй бұрын

    Nazoooo

  • @adzonzicomedy
    @adzonzicomedyАй бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4bАй бұрын

    Chili chonse chingowululika kumwamba kulandire ulemu

  • @AnnastasiaChakwiya
    @AnnastasiaChakwiyaАй бұрын

    Ai zikomo achakwera

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gzАй бұрын

    😢😢😢😢😢

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1kАй бұрын

    Koma what is the use of our currency in Zambia? I don't understand this.

  • @BornfiyesignalSignalmtema
    @BornfiyesignalSignalmtemaАй бұрын

    The dc

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713Ай бұрын

    Ya balance 😢 RIP SKC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1rАй бұрын

    Choka iwe mbuli zokhazokha zomwe ziimakunvera iwe gawanani ndlmazo paja ndiyo ntchito yanu 😂😂😂mwayi ndi MCP ukudya bwino kamba ka mabodza akowo azipani akumakulipila 😅😅😅uziyamklika wamva

  • @tingamasi106

    @tingamasi106

    Ай бұрын

    Mbuli ndiwe mavuzi okhwimawo

  • @Dysonkhofi

    @Dysonkhofi

    Ай бұрын

    Iwenso ndiwe galu,chitsiru

  • @user-bd5kw8oq1r

    @user-bd5kw8oq1r

    Ай бұрын

    @@Dysonkhofi fisi,chule,mbuzi,,bulu munayiwala zimenezo zikomo God bless you 😊😊❤️❤️❤️ work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

  • @ednakaluwa5414

    @ednakaluwa5414

    Ай бұрын

    ​@@user-bd5kw8oq1rutukwana anzako..opanda chifukwa ena akubwexera utchula dzina la Mulungu shame on you.

  • @ednakaluwa5414

    @ednakaluwa5414

    Ай бұрын

    Vuto u need attention

  • @JamesAlinafe
    @JamesAlinafeАй бұрын

    Tha DDDDD ccccccccc

  • @katalamajames4947
    @katalamajames4947Ай бұрын

    Koma keni nsonda amadya mutu nkhope the same sekeleton ma R. V.sakugwira nchito

  • @zimmekapachika6784

    @zimmekapachika6784

    Ай бұрын

    😅😅😅😅😂😂😂mankwala anapima sakugwila 😅😅😅😅😅😂😂😂yomweyo galu iwe

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7noАй бұрын

    Kukuyu nyamayake

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9nАй бұрын

    Komanso chibadwireni ine ntchito ya asilikali athu muno mu malawi sindikuiziwa, chifukwa ngati nkuteteza dziko .bwezi atalipanga boma ili held responsible pa nkhani iyi infact predent akadamuchosa.

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2gАй бұрын

    Balance

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4soАй бұрын

    koma amalawi

  • @LiamTennessee
    @LiamTennesseeАй бұрын

    Amazalandila malipilo a ntchito yomwe adagwila

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9clАй бұрын

    Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5sАй бұрын

    Zovetsa chisoni 😢

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hiАй бұрын

    The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔

  • @kelvinsibande8779
    @kelvinsibande8779Ай бұрын

    The DDDDDCCCCCCC

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWiliАй бұрын

    Mmmmm haa?

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gzАй бұрын

    Ma 20kwachawooo??

  • @MinhoMasanza

    @MinhoMasanza

    Ай бұрын

    Yah ndima mk20 koma each carton contains more than a million

  • @hudycorex1893

    @hudycorex1893

    Ай бұрын

    Mk20 Sindalama????? Iwe ndendiopepera bwanji!!!

  • @rhodricksalima5387

    @rhodricksalima5387

    Ай бұрын

    Paliso ma 5 pin tu

  • @CharityChikomo-hl1gz

    @CharityChikomo-hl1gz

    Ай бұрын

    Opepela ndi amako

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493Ай бұрын

    ANTHU PANO MMANGO PANGA MA COMMENT KOPANDA KUSATILA ZINTHU . NDALAMA ZOMWE ZAPEZEKA KU ZAMBIA NDI ZAMAYIKO ANGAPO KUPHATIKIZA MALAWI ANTHU OMWE APEZEKA NAZO NDIZINKA ZA KU RUSSIA OMWE AKUPANGA MA BUSSINES A MA DRUGS OSATI ZOTI BOMA AYI MMM KALINDO ECHI BOZA LENILENI ZINAMIZA ACHILOMWE AKOWO

  • @TysonMwenye

    @TysonMwenye

    Ай бұрын

    Ndiye anthu aku Russia wo angapeze ndi ndalama zathu chifukwa choti akugulitsa ma Drugs? Ifeyo tikamapita ku mayiko akunja timasintha ndalama zadziko lomwe tikupitako.Ndipo tikamaliza business yathuyo tisanatuluke mudzikolo timasinthilatu zamalawi.Ndiye awowo apezeka bwanji ndi ndalama zathu (Mwk) koma kudziko lina chinawakanikitsa kusintha kumalawi konko ndichani ngati ndizachilungamo ndalamazo

  • @tingamasi106

    @tingamasi106

    Ай бұрын

    Ndalama zama drug mpaka sealed? Iwe ndichimbutumwa wamva

  • @munashemoyo4190

    @munashemoyo4190

    Ай бұрын

    Kusonyeza kt zomwe zikuchitika dziko muno iwe zikukusangalasa et i uzaziwona ukazakwatila ukasiya kudyesedwako mbudzi yamunthu iwe kape

  • @AmosScott-z9x

    @AmosScott-z9x

    Ай бұрын

    Kape iwe

  • @chadreckchibwithala1493

    @chadreckchibwithala1493

    Ай бұрын

    mbutuma ndinu osaziwa zinthu alomwe matama basi tiyeni uko . mleke kutivuska mngalamuliraso yai chalo ichi jiiiiiiiii peter wanuyo no

  • @user-si8vm5vj8s
    @user-si8vm5vj8sАй бұрын

    Shame on you chakwera

  • @warrenmwambazi8342
    @warrenmwambazi8342Ай бұрын

    Very bad 😊😊😊

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2kiАй бұрын

    Kalindo ndi nyatwa auze zitsiru izi.

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomelaАй бұрын

    Ma mafia 😂

Келесі