Komatu apa zikuoneka kuti,mtolankhani uyu sakumvetsa zomwe a Namalomba akukamba.
@Chikulamayembe577 ай бұрын
This Journalist, Leah Malekano, just cuts it for me! 👏👏👏
@AndrewNtombosola-ur7vh
7 ай бұрын
Kodi pamene sakuwamvetsa a Namalombawa ndipati?
@enerstmwakhundi44007 ай бұрын
mbambande Leah 👏Good questions
@rashidsaid22327 ай бұрын
Mr Namalomba good answers without hiding God bless u if u love DDP us we love it Chakwela must removed in 2025 akuononga too much our country
@kha60687 ай бұрын
This guy is very smart 🎉
@AlexisKantondo7 ай бұрын
Ntchito ya utolikhani adona simayitanidwe anu
@HappyMphande7 ай бұрын
One step at a time Leah 🎉
@brinokalemba45037 ай бұрын
Leah ndiwe dolo🔥🔥🔥🔥🔥
@whitethamangar29507 ай бұрын
😂😂😂😂Namalomba 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@JohnKamanga-tu2il7 ай бұрын
All the best mr
@georgesmart37917 ай бұрын
More fire Nambalomba fire 🔥 🔥
@DICKSY-kz1qd7 ай бұрын
Love you namalomba
@user-xq5ju2uo9h7 ай бұрын
Namalombe ndi mbuli uyu saziwa zamaundindo 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@patrickmacheso5062
7 ай бұрын
Paja mbuli zilipo maguru angapo, Umbuli wa Namalomba uli better than wanuwo coz simungamufikile or pang'ono even mutatengana nonse ku family yanu.
@patrickmacheso50627 ай бұрын
Namalomba is a very smart guy and he deserve to be the spokes person for APM and DPP, Nankhumwa, Dausi, G Jeffrey and other empty tins that there making noise including Ken Msonda are Just making Jealous for him.
@hopeskafumbi2246
7 ай бұрын
thank you so much indeed he is wise man
@emmanuelmukondia3568
7 ай бұрын
He is good for this evil party. Nepostic
@user-kr1kg5hy9l7 ай бұрын
Bravo Namalomba.
@user-kx5uk8vj1j7 ай бұрын
Namalomba kuchikamwa
@edsonnyasulu53946 ай бұрын
Namalomba naye akusaka ya deya kuti azikadya ndi Ana aka palibe cha zeru apa
Ndipo anthu amenewa akutumidwa ndi boma kuti azivuta ndicholinga aboma azapeze polowela do you think panopa tilindi a opposition nankhumwa
@user-pn7ek7wb7n
7 ай бұрын
Iwe sudziwa kalikose time ndiye ya mcp
@markhamdaddy6 ай бұрын
Muthu wamkulu namalomba kuyakhula zamchere
@user-wt4hl4ps2k7 ай бұрын
Namalomba, a mere rift raff...Such position suit well level head persons.. always avoiding questions... deliver lacks substance... exposing the party gone to wayawaya wading in Chikangawa forest..Namalomba is the one brewing problems in the party...Unless replaced, party problems and confusion will never die until 2025 and the party will walk out again with tail tapped between the two legs...Namalomba amaopa Nankhumwa kwambiri...Analephera kumchotsa Nankhumwa as Leader of Opposition ku Parliament. Akuopa party convention...Is this not litmus to show Nankhumwa is powerful and threat to APM...Namalomba and gang are the ones forcing APM to stand stand...Zawo zaima...zosolola zija zatha..akufuna azizasololanso kumbuyo Kwa APM... These people are denting the image of APM... Shame..
@user-rk4ch1ly3z7 ай бұрын
Namalomba iwe ndi katswiri palibeso chipani wachigwira bwino ,ife tili pambuyo pa APM dpp woyee!
@paulmakaula49377 ай бұрын
This is the caliber of politician Malawi needs onwards wadzake wolemera, full of politics. He can thoroughly present Malawi before international bodies like IMF, World Bank, bilateral donors and ably convince on behalf of Malawians...actually bomali can tap his talents....DPP please let Nankhumwa and APM amicably solve this wrangle with few reputable clergy as moderators...Nankhumwa should not be underrated has support base pa ground...reach out possible new intellectual faces who should help clear image yomwe inaonongeka in the last reign...otherwise Malawians akufuna izizi squabbles zithe! However odana ndi Namalomba akudana ndi progressive minds, he's simply the best!
@BENSONRANGWANI24 күн бұрын
Ulemu upite kwa Namalomba
@clintonhodda98307 ай бұрын
Namalomba ndi machine onse otumidwa ndi Mcp ali madzi
@bichardmoises96857 ай бұрын
Nthawi zina ndizofunika osamapitako uku
@MisterBanda-pl8ct7 ай бұрын
Thank you
@JOHNSANGWALI-ox8mu7 ай бұрын
Live from Kimberley Km vuto palibe no sound
@user-mj3ms4jt3b7 ай бұрын
Namalomba sioyenela udindo umenewu anapatdidwila kukachipinda. Leya wangoiwala kuwafusa kuti Kodi 2018 ku convention ya DPP anthu anapikisana pa udindo wa spokesperson? Nanga ena anapikisana pa udindo wa publicity secretary? Nanga ngati anapikisana mumaudindo onsewa pa convention, iwowa anatenga udindo omwe unali wandani yemwe anasakhidwa pa convention yo?
@IsaacKachimanga2 ай бұрын
Mukuchoka ku mangoch South west
@archraphnkhoma-lw6wx7 ай бұрын
Palibe za Dausi apa Adadi Basi
@kingsleylabvulani55157 ай бұрын
😂😂😂😂😂 Namalomba ndi dolo
@user-hr2cg3ku1l7 ай бұрын
Mbuzi ya munthu Namalomba
@brianchimwaza7 ай бұрын
Mbambande namalomba
@victorbanda90397 ай бұрын
Namalomba nthata yanjala yaku dpp ati afuna azakhale a minister of information koma maloto achumba gogo wakoyo sangawineso
@brightngwira81707 ай бұрын
Mipandoyo tayikanipo ya bwino aaaaa nanga Professor Anthur adzakhalapo bwanji Pakhale mipando ya exuctives .. Wena adzakhala ataminula apa adzakhalapo bwanji🎉 Pilizi sinthani furniture apa 😮
@levisonmoyo13067 ай бұрын
About time she realized she just being used these politicians for their little funny games
@user-du9qs4tb6u7 ай бұрын
Iwe leya ndiwe kape usamafuse mafuso oyambanitsa anthu chomwe ungadziwe panopa amalawi akuvutika pa moyo watsiku nditsiku tikufuna mafuso opindulila amalawi kodi iweyo leya makolo ako sakuvutika kumudziko ndipo iweyo usamakhale pamenepo ngati azichimwene ako sakuvutika kodi ndiwe wa mcp. Ngati ukufuna kumva zokhudza amuthalika upite ku page house ukawafuse maganizo awo.
Akuti ,a spokesperson ndi amene amaitanitsa ,ma meeting,koma mopatsidwa mphamvu ,kapena kutumidwa ndi a President iiii siukumva pati?
@ndalamaandrew7 ай бұрын
Akuluwa ndi Solo kwambili 😂😂
@JamalNgumba-pe6xo7 ай бұрын
Grezeda,Nankhumwa ndi osokoneza
@patassonelucaszovuta34314 ай бұрын
Uyuyu ndi amene wagoneka Peter panopa madala aja ali ntulo akugona chifukwa uyuyu adawayika pa lo adzazindikila mochedwa chipani chitatha
@user-tq6pg7bv9x3 ай бұрын
Mbambande Namalomba
@greychizaka40887 ай бұрын
Genius shad
@user-uf1tz7bp5q7 ай бұрын
Kom ndiwambalumetu fira
@user-kr1kg5hy9l7 ай бұрын
Nankhumwa ndi wakuba...akufuna kuba chipani mgwilenj.
@ChisomoMsiska-oi2vg7 ай бұрын
Awa ndiwozikonda kwambiri ndichifukwa chake anzawo amathawako musonda ali ndi nzeru awa mmmm
@user-ty7mc9mg1f7 ай бұрын
Leya ,bwinobwino ee
@GreenFacksoncassim6 ай бұрын
Apm boma 💙💙💙💙2025
@martinkalaka26677 ай бұрын
Eish pano tapumulako za kupha alubino nde wina mkumati ndiwabwino kusaganiza kapena chani namalomba nda zake adpp amkapha alubino sitinayiwaletu agalu inu mwava😮
@user-gk6bf7xe9g7 ай бұрын
Anamalomba 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@GustavoBoloi-kz8js7 ай бұрын
Osaopa lakhula
@user-nw6ie3xx8b7 ай бұрын
Aaaaaa yai namalomba muli ndizifukwa ndi adaus, grizeda, ndi na nkhumwa
@user-nn5ug7ul4d
7 ай бұрын
Aaaaaa choka iweee kapr
@JohnKamanga-tu2il7 ай бұрын
Tell them
@user-tq6pg7bv9x3 ай бұрын
Matchin Namalomba
@henryphiri61007 ай бұрын
Komanso a Leah mudzipanga interview anthu oti afotokoza za nzeru.please anthu akuvutika.kuti tidzimva izi zamikanganozi ayiii it's an insults.zandalezo ayii chifukwa mwini chipani chimenechi ankakana kuti iyi siwandale ayi.ndiye please mudziyika zanzeru.mbuzi zimenezi tatopa nazo
@user-qi8xe7qh1e7 ай бұрын
Anamalomba zoti anthu akufuna zisankho 2024 zimenezo mukudziziwa? apa ndiye mudzitibhowa ndi 2025 mukukakamila 2025 bwanji uchitsiru kapena chani usadziwa malamulo kapena kodi bwanji a opposition nonse ndiopepela munadyetsedwa chani ndiye mukati 2025 mukuganiza kuti kwacha izakhala bwanji??
@user-km8ni2yk2c7 ай бұрын
Ndozitukumula chabe chilungamo mulibe umu
@SheenahMwalabu-iz3pr7 ай бұрын
Who else notice kuti Namalombwa voice kufanana ndia Chilima 😊
@user-lw4hw9ce4w7 ай бұрын
Udindo umakukhalani kwambiri inuyo anamalomba dausi ndiye mwana ndani
@henryphiri61007 ай бұрын
Kukanganirana chipani agalu inu.mwini wake yemwe anapanga mbiri yabwino yachipaniyi.Nankhumwa akupanga chiani chanzeru pano tikuvutika ndi Chakwera ngati mtsogoleri wa opposition.Ndiye akufuna adzatsogolere ndani wakeyo.
@user-xx5dc5wl7g7 ай бұрын
DPP sikulowanso m Boma akuchita kuoneselatu kuti mbava zabodza zokhazokha
@dominicmphepo-jk8lk7 ай бұрын
Mwatikwana anthu inu just showing kuti you are not there to save but money hungry. Peter akagiver chipanichi chatha no one will save chipanichi. Anthu adyelanu mzanu anayiphula inu muli komweko now mukunva kuwawa mufuna muzabenso. Pano nthata za MCP zakhuta nanu munapopa zija zayamba zachepa don't worry.
@ambrozonamazemba89867 ай бұрын
Didn't have time, to watch the whole interview kma ndangovera mmene wactra differentiate PRO and Spokesperson.bac kwina koseko ndagwirzana naye bac amenei
@ireenkafatiya65687 ай бұрын
Leah nde uti were is Brian, leah is trying to be somehow kkkkk zosabeba
@roberttungande78507 ай бұрын
Alandisa chipani😊
@wayneivanmacadam7 ай бұрын
If APM dosnt stand as president DPP is finished to much childish politics nakhumwa and associates
Leah udziwe kuti mcp singalamulire DPP and zodiac ndi station ya MCP
@hendrinagama5325
7 ай бұрын
Zoona man ndkudabwa naye Mai yu
@martinkalaka2667
7 ай бұрын
Palibe radio station yachipani kambani zina inu
@martinkalaka2667
7 ай бұрын
Namalomba alibe fundo ayi akukanika kuyakha mafuso busy kukamba za mcp kupepela basi
@chikondigondwe46697 ай бұрын
Koma
@EmercianahKasiku-en6hl7 ай бұрын
Munthu uyu ndi inu nose mukuti Nankhumwa , Jeffrey,Dausi komaso Msonda ayambitse chipani chawo mulibe nzeru komaso ndinu ufunila zoipa chipanichi bcuz kuchoka kwa Chilima kunapangitsa kuti DPP iluze nde achokeso Nankhumwa nde 2025 yo muzalowa bwanji mu Bomamo?poti Nankhumwa pochoka azachokaso ndi gulu la Anthu ambiri,Chisale,Namalomba komaso Bright msaka ndi oba chimanga aja asiye kumulangiza komaso kukhala kufupi ndi president chipanichi chidzukaso kupanda apo chitha ngati UDF chizapeza mavote 250.000 basi😂😂😂😂tisaiwaleso kuti masankho ndi a 50+1 nde tichotse mamembers ena pali nzeru?
@jomochirwa7 ай бұрын
Namalomba mpakana kunena kuti ali ndi chuma kuposa a peter muthalika.pali za utsogoleli apa.izi ndichimodzimodzi ndi tonse ilipoyi
@user-frasernamaona14
7 ай бұрын
Mwamunvela bwino bwino koma? Wonelaninso sanati ali ndi chuma kuposa Mutharika wati mwinanso. Kodi mwina ndimawu oti ndi mumawasiyanisa bwanji?
@JohnstoneNkhoma-jf7qe7 ай бұрын
mawu tidaluza boma chfukwa cha nakhumwa ndi azakewo
@reltonmbawala13297 ай бұрын
Namlomba agawanitsa chipani uyu, kodi anatulukila pati
@user-qb1ef1xw5d7 ай бұрын
Dpp vuto ndiloti sichinayambile pa ground chinachita kuba chipani cha udf
@robsontyg39287 ай бұрын
Professor wa kumatako,
@lewisbonongwe8518
7 ай бұрын
Wa carlolite sopano chomwe amadziwa ndi kutukwana basi Utaphoda😂
@robsontyg3928
7 ай бұрын
@@lewisbonongwe8518 pathako pa mayi ako wava, dzitsilu dza anthu dza alhomwe
Smart man namalomba , go-ahead amalawi akudikira boma lokoma la dpp
@gladysbonongwe10387 ай бұрын
Ntola nkhaniyo apite kumudzi akadzimvere yekha
@DoYouKnow38387 ай бұрын
Ndi Brian Banda yekha angafuse Namalomba mafutso omveka bwino probably seconded by Joab Frank Chakhaza.
@viktornginde3720
7 ай бұрын
Mukadzamuchita analyze Brian Banda, n'pomwe mudzamudziwe bwino-bwino.
@SabitiChisawa-gm8ev
7 ай бұрын
Joab akhale pa number 1 bwanji?
@solutionssolutions50057 ай бұрын
Can i humbly advise all these so called DPP gurus ..Namalomba,Etc.... to currently stop from appearing to the public in issuing interviews BUT concentrate on correcting things amongs yourselves.Kakonzeni zinthu zanu kaye , zioneke kuti muli amodzi kaye then be free to appear to the public.
Пікірлер: 139
Namalomba good enough to be a DPP spokesperson ❤❤❤
Journalist ofooka..sakudziwa bwinobwino chomwe akufuna kudziwa
Achina dausi akufuna kuononga chipani ndi nankhumwa , I like this guy namalomba we are behind you
MR Namalomba zikomo kwambiri you are good spokesperson.
Good job Leah keep it up osawopa
Namalomba more fire umakwana chibwana cha kwathu ichi chosamba ichi 😅😅😅😅 2025 bomaaaaaaaa I love you Namalomba ❤❤❤❤❤
I like the way honourable Namalomba present things, we are behind you and our beloved DPP 🔥🔥🔥🔥
Nambalomba more fire 🔥
Namalomba is a smart guy, nawo anankhumwa, dausi ndi geofry ndi makape osayambisa chipani chawo bwanji
Namalomba more fire keep it up
Inutu chemwali mwadzitenga udyo akutumaniwo kuti mudzatola pakamwa
Namalomba amatha,kuyakhula and akuziwa zomwe athuwoipa wofunakusokonez chipan, ambili achinasonda ndi azizawo alowa zipani zambilimbili and mbilizawo ndikusokoneza kenako athaweko, anamalomba ndi azanu achinasaka musalolele Anawo kusokoneza
Namalomba akunena chilungamo kuti mcp ndi yomwe ikusonkhedzera
Mr namalomba ineyo ndikukulimbikisani kuti pitilizani bwana ndipo musagonje ....ineyo ndili mwanja mwa Peter mutharika ....nankhumwa ndichisilu akufuna ntchito yoti sangayikwanise ayi
Komatu apa zikuoneka kuti,mtolankhani uyu sakumvetsa zomwe a Namalomba akukamba.
This Journalist, Leah Malekano, just cuts it for me! 👏👏👏
@AndrewNtombosola-ur7vh
7 ай бұрын
Kodi pamene sakuwamvetsa a Namalombawa ndipati?
mbambande Leah 👏Good questions
Mr Namalomba good answers without hiding God bless u if u love DDP us we love it Chakwela must removed in 2025 akuononga too much our country
This guy is very smart 🎉
Ntchito ya utolikhani adona simayitanidwe anu
One step at a time Leah 🎉
Leah ndiwe dolo🔥🔥🔥🔥🔥
😂😂😂😂Namalomba 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
All the best mr
More fire Nambalomba fire 🔥 🔥
Love you namalomba
Namalombe ndi mbuli uyu saziwa zamaundindo 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@patrickmacheso5062
7 ай бұрын
Paja mbuli zilipo maguru angapo, Umbuli wa Namalomba uli better than wanuwo coz simungamufikile or pang'ono even mutatengana nonse ku family yanu.
Namalomba is a very smart guy and he deserve to be the spokes person for APM and DPP, Nankhumwa, Dausi, G Jeffrey and other empty tins that there making noise including Ken Msonda are Just making Jealous for him.
@hopeskafumbi2246
7 ай бұрын
thank you so much indeed he is wise man
@emmanuelmukondia3568
7 ай бұрын
He is good for this evil party. Nepostic
Bravo Namalomba.
Namalomba kuchikamwa
Namalomba naye akusaka ya deya kuti azikadya ndi Ana aka palibe cha zeru apa
Nankhumwa, Dausi, Msonda komanso Jeffrey pls yambitsani chanu Chipani
Ndipo anthu amenewa akutumidwa ndi boma kuti azivuta ndicholinga aboma azapeze polowela do you think panopa tilindi a opposition nankhumwa
@user-pn7ek7wb7n
7 ай бұрын
Iwe sudziwa kalikose time ndiye ya mcp
Muthu wamkulu namalomba kuyakhula zamchere
Namalomba, a mere rift raff...Such position suit well level head persons.. always avoiding questions... deliver lacks substance... exposing the party gone to wayawaya wading in Chikangawa forest..Namalomba is the one brewing problems in the party...Unless replaced, party problems and confusion will never die until 2025 and the party will walk out again with tail tapped between the two legs...Namalomba amaopa Nankhumwa kwambiri...Analephera kumchotsa Nankhumwa as Leader of Opposition ku Parliament. Akuopa party convention...Is this not litmus to show Nankhumwa is powerful and threat to APM...Namalomba and gang are the ones forcing APM to stand stand...Zawo zaima...zosolola zija zatha..akufuna azizasololanso kumbuyo Kwa APM... These people are denting the image of APM... Shame..
Namalomba iwe ndi katswiri palibeso chipani wachigwira bwino ,ife tili pambuyo pa APM dpp woyee!
This is the caliber of politician Malawi needs onwards wadzake wolemera, full of politics. He can thoroughly present Malawi before international bodies like IMF, World Bank, bilateral donors and ably convince on behalf of Malawians...actually bomali can tap his talents....DPP please let Nankhumwa and APM amicably solve this wrangle with few reputable clergy as moderators...Nankhumwa should not be underrated has support base pa ground...reach out possible new intellectual faces who should help clear image yomwe inaonongeka in the last reign...otherwise Malawians akufuna izizi squabbles zithe! However odana ndi Namalomba akudana ndi progressive minds, he's simply the best!
Ulemu upite kwa Namalomba
Namalomba ndi machine onse otumidwa ndi Mcp ali madzi
Nthawi zina ndizofunika osamapitako uku
Thank you
Live from Kimberley Km vuto palibe no sound
Namalomba sioyenela udindo umenewu anapatdidwila kukachipinda. Leya wangoiwala kuwafusa kuti Kodi 2018 ku convention ya DPP anthu anapikisana pa udindo wa spokesperson? Nanga ena anapikisana pa udindo wa publicity secretary? Nanga ngati anapikisana mumaudindo onsewa pa convention, iwowa anatenga udindo omwe unali wandani yemwe anasakhidwa pa convention yo?
Mukuchoka ku mangoch South west
Palibe za Dausi apa Adadi Basi
😂😂😂😂😂 Namalomba ndi dolo
Mbuzi ya munthu Namalomba
Mbambande namalomba
Namalomba nthata yanjala yaku dpp ati afuna azakhale a minister of information koma maloto achumba gogo wakoyo sangawineso
Mipandoyo tayikanipo ya bwino aaaaa nanga Professor Anthur adzakhalapo bwanji Pakhale mipando ya exuctives .. Wena adzakhala ataminula apa adzakhalapo bwanji🎉 Pilizi sinthani furniture apa 😮
About time she realized she just being used these politicians for their little funny games
Iwe leya ndiwe kape usamafuse mafuso oyambanitsa anthu chomwe ungadziwe panopa amalawi akuvutika pa moyo watsiku nditsiku tikufuna mafuso opindulila amalawi kodi iweyo leya makolo ako sakuvutika kumudziko ndipo iweyo usamakhale pamenepo ngati azichimwene ako sakuvutika kodi ndiwe wa mcp. Ngati ukufuna kumva zokhudza amuthalika upite ku page house ukawafuse maganizo awo.
@patriciacraiton-sf5vu
7 ай бұрын
Kaya inu, ndikudabwa naye
@martinkalaka2667
7 ай бұрын
Leya wamufusa bwino kwambili namalomba ndipo ndamukonda
Akuti ,a spokesperson ndi amene amaitanitsa ,ma meeting,koma mopatsidwa mphamvu ,kapena kutumidwa ndi a President iiii siukumva pati?
Akuluwa ndi Solo kwambili 😂😂
Grezeda,Nankhumwa ndi osokoneza
Uyuyu ndi amene wagoneka Peter panopa madala aja ali ntulo akugona chifukwa uyuyu adawayika pa lo adzazindikila mochedwa chipani chitatha
Mbambande Namalomba
Genius shad
Kom ndiwambalumetu fira
Nankhumwa ndi wakuba...akufuna kuba chipani mgwilenj.
Awa ndiwozikonda kwambiri ndichifukwa chake anzawo amathawako musonda ali ndi nzeru awa mmmm
Leya ,bwinobwino ee
Apm boma 💙💙💙💙2025
Eish pano tapumulako za kupha alubino nde wina mkumati ndiwabwino kusaganiza kapena chani namalomba nda zake adpp amkapha alubino sitinayiwaletu agalu inu mwava😮
Anamalomba 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Osaopa lakhula
Aaaaaa yai namalomba muli ndizifukwa ndi adaus, grizeda, ndi na nkhumwa
@user-nn5ug7ul4d
7 ай бұрын
Aaaaaa choka iweee kapr
Tell them
Matchin Namalomba
Komanso a Leah mudzipanga interview anthu oti afotokoza za nzeru.please anthu akuvutika.kuti tidzimva izi zamikanganozi ayiii it's an insults.zandalezo ayii chifukwa mwini chipani chimenechi ankakana kuti iyi siwandale ayi.ndiye please mudziyika zanzeru.mbuzi zimenezi tatopa nazo
Anamalomba zoti anthu akufuna zisankho 2024 zimenezo mukudziziwa? apa ndiye mudzitibhowa ndi 2025 mukukakamila 2025 bwanji uchitsiru kapena chani usadziwa malamulo kapena kodi bwanji a opposition nonse ndiopepela munadyetsedwa chani ndiye mukati 2025 mukuganiza kuti kwacha izakhala bwanji??
Ndozitukumula chabe chilungamo mulibe umu
Who else notice kuti Namalombwa voice kufanana ndia Chilima 😊
Udindo umakukhalani kwambiri inuyo anamalomba dausi ndiye mwana ndani
Kukanganirana chipani agalu inu.mwini wake yemwe anapanga mbiri yabwino yachipaniyi.Nankhumwa akupanga chiani chanzeru pano tikuvutika ndi Chakwera ngati mtsogoleri wa opposition.Ndiye akufuna adzatsogolere ndani wakeyo.
DPP sikulowanso m Boma akuchita kuoneselatu kuti mbava zabodza zokhazokha
Mwatikwana anthu inu just showing kuti you are not there to save but money hungry. Peter akagiver chipanichi chatha no one will save chipanichi. Anthu adyelanu mzanu anayiphula inu muli komweko now mukunva kuwawa mufuna muzabenso. Pano nthata za MCP zakhuta nanu munapopa zija zayamba zachepa don't worry.
Didn't have time, to watch the whole interview kma ndangovera mmene wactra differentiate PRO and Spokesperson.bac kwina koseko ndagwirzana naye bac amenei
Leah nde uti were is Brian, leah is trying to be somehow kkkkk zosabeba
Alandisa chipani😊
If APM dosnt stand as president DPP is finished to much childish politics nakhumwa and associates
Kodi chimene mukulepherera kuitaninitsa conversion ndichichiyani
Leah udziwe kuti mcp singalamulire DPP and zodiac ndi station ya MCP
@hendrinagama5325
7 ай бұрын
Zoona man ndkudabwa naye Mai yu
@martinkalaka2667
7 ай бұрын
Palibe radio station yachipani kambani zina inu
@martinkalaka2667
7 ай бұрын
Namalomba alibe fundo ayi akukanika kuyakha mafuso busy kukamba za mcp kupepela basi
Koma
Munthu uyu ndi inu nose mukuti Nankhumwa , Jeffrey,Dausi komaso Msonda ayambitse chipani chawo mulibe nzeru komaso ndinu ufunila zoipa chipanichi bcuz kuchoka kwa Chilima kunapangitsa kuti DPP iluze nde achokeso Nankhumwa nde 2025 yo muzalowa bwanji mu Bomamo?poti Nankhumwa pochoka azachokaso ndi gulu la Anthu ambiri,Chisale,Namalomba komaso Bright msaka ndi oba chimanga aja asiye kumulangiza komaso kukhala kufupi ndi president chipanichi chidzukaso kupanda apo chitha ngati UDF chizapeza mavote 250.000 basi😂😂😂😂tisaiwaleso kuti masankho ndi a 50+1 nde tichotse mamembers ena pali nzeru?
Namalomba mpakana kunena kuti ali ndi chuma kuposa a peter muthalika.pali za utsogoleli apa.izi ndichimodzimodzi ndi tonse ilipoyi
@user-frasernamaona14
7 ай бұрын
Mwamunvela bwino bwino koma? Wonelaninso sanati ali ndi chuma kuposa Mutharika wati mwinanso. Kodi mwina ndimawu oti ndi mumawasiyanisa bwanji?
mawu tidaluza boma chfukwa cha nakhumwa ndi azakewo
Namlomba agawanitsa chipani uyu, kodi anatulukila pati
Dpp vuto ndiloti sichinayambile pa ground chinachita kuba chipani cha udf
Professor wa kumatako,
@lewisbonongwe8518
7 ай бұрын
Wa carlolite sopano chomwe amadziwa ndi kutukwana basi Utaphoda😂
@robsontyg3928
7 ай бұрын
@@lewisbonongwe8518 pathako pa mayi ako wava, dzitsilu dza anthu dza alhomwe
@lewisbonongwe8518
7 ай бұрын
Inu mulibe pathako Mr yelesa😂🤣
@robsontyg3928
7 ай бұрын
@@lewisbonongwe8518 ma refugees dzi anthu dza Mozambique 🇲🇿 msunu kanyoko palikundu penu
@randolphkazembe229
7 ай бұрын
Umazola chani kod
I wish there was a 'super like' option for this.
Anamalomba mukuopa convention bwanji?inuyo ndi gulu lanu ndi amene mukuononga chipanichi
Kunena zoonadi anthu awa atitopesa ndi nkhani zawo zopusazo
Koma ndikadakonda DPP ikadatha kuthelatu psitiii mwina tiveko Zina zanzelu zamasomphenya kukhale zipani zawanthu oganizako mwawumunthu osati zitsilu zokhazokha ziliku DPP zogawana nyama musadaphe R I P Dr bingu ndimasomphenya awo in shot zabwino zose zidapita ndia bingu bas
@SheenahMwalabu-iz3pr
7 ай бұрын
Kugawanikanatu kochititsa manyazi, why mukungokhalira kusemphana ndemutatenga boma mudzaphanatu 😂😂
Namalomba 0 pa 10
Leah wakumana nazo amawonele ena aja🤣🤣🤣
@user-mv1vp4mf7r
7 ай бұрын
Smart man namalomba , go-ahead amalawi akudikira boma lokoma la dpp
Ntola nkhaniyo apite kumudzi akadzimvere yekha
Ndi Brian Banda yekha angafuse Namalomba mafutso omveka bwino probably seconded by Joab Frank Chakhaza.
@viktornginde3720
7 ай бұрын
Mukadzamuchita analyze Brian Banda, n'pomwe mudzamudziwe bwino-bwino.
@SabitiChisawa-gm8ev
7 ай бұрын
Joab akhale pa number 1 bwanji?
Can i humbly advise all these so called DPP gurus ..Namalomba,Etc.... to currently stop from appearing to the public in issuing interviews BUT concentrate on correcting things amongs yourselves.Kakonzeni zinthu zanu kaye , zioneke kuti muli amodzi kaye then be free to appear to the public.
Very good journalist and shame to Namalomba