Eeeh wachita kutembelera boma lonse andale onse Prophet Mbewe kuti awalange Mulungu

Пікірлер: 99

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e15 күн бұрын

    Ndimo mudzina la yesu mau Anu agwile ntchito pa andale okubawa mu dzina la yesu

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z10 күн бұрын

    Only Young president can do better... Coz they can do it in new model...NOT 60'S MODEL

  • @MussahIman-cw1cu
    @MussahIman-cw1cu14 күн бұрын

    U man of God continue to pray for those bad people to gate pushed from god

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda2 күн бұрын

    Amen man of God. We are tired wth that thng we call chakwera

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif955615 күн бұрын

    Mau owoona mulungu atimenyele nkhondo ameeen

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel15 күн бұрын

    Mulungu wamatembelelo kkkkk mwayamba zibwana ndimulungu ky pot ndi business yanu ndimulungu wanu

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d15 күн бұрын

    Ndipo athu atizuzuza yawa sitizaiwala m, pakana kale kale mmm ndipo asatana

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d14 күн бұрын

    Amen mau ishiii ziko lathuli ai zikomo akuluakulu kuntunda mavuto okhaokha bsi.

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo2 күн бұрын

    God bless you man of God

  • @babranzima8120
    @babranzima812015 күн бұрын

    Perfect said 👏 🙌

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje373314 күн бұрын

    Very bold.....the only Man of God that have told govt the truth

  • @TheresaKuluwemba

    @TheresaKuluwemba

    13 күн бұрын

    Koma ndipo! Koma nthawi ya APM azibusa ma prophet ansembe palipose kunali kuyakhula zoipa zaboma lija koma pano kuli ziii, palibe akukamba zoipa kapena zabwino za bomali uyuyu ekha basi, ayi zikomo

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito110914 күн бұрын

    Kodi chakwerayu tu bvuto ndi school komanso mtundu komwe akuchokera mmmmmmmm so shame walephera basi 2025 azipita !!

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne13 күн бұрын

    Tiye prophet awawa mulungu awachose 2025 zikutiwawà .

  • @AlickBaton
    @AlickBaton15 күн бұрын

    This is 2023,, but only God knows

  • @marryphili5419
    @marryphili541915 күн бұрын

    Oooh yes tatopa ndi boma ili please azibusa lowereranipo ndithu timenyereni nkhondo Kuti kumwamba kuseguke tatopa ndikulira amalawi

  • @MafunaseKamoto
    @MafunaseKamoto13 күн бұрын

    Basi man of God ndalamazo andipatsira ine tikabweze komwe zinabedwa...kkkk

  • @kennedybanda
    @kennedybanda15 күн бұрын

    Matenda ake ena mwa iwo ndi misala.

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie14 күн бұрын

    Iwe usankhepo chimodzi pakati PA ubusa ndi Der wamva osamphatikinza za mulungu ndi Zadary 😂😂😂

  • @julietmussa5103
    @julietmussa510314 күн бұрын

    Alavule ndalama zikenezo in Jesus Name

  • @PiscaDicksoni
    @PiscaDicksoni15 күн бұрын

    Amen man of God

  • @AlinafeChimoto-pp7wp

    @AlinafeChimoto-pp7wp

    15 күн бұрын

    Amen 🙏🙏 power

  • @PaulKambuzi
    @PaulKambuzi4 күн бұрын

    amen aprophert power full

  • @user-xe5il4cg5d
    @user-xe5il4cg5d15 күн бұрын

    Amen prophet

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p15 күн бұрын

    Amen mudzina la yesu

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi15 күн бұрын

    Nkhale Lili LA 2023 akuphempha ndi chimozi mozi tikuyembekezera amipingo ina tinve kunyasidwa kwanu Asilam tiye maduwa

  • @Dorah-zl9uf
    @Dorah-zl9uf15 күн бұрын

    Amen may God bunish them

  • @user-gj8td8pc4d
    @user-gj8td8pc4d14 күн бұрын

    Names nkukhala mommo mundalemo.😂😂

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande610814 күн бұрын

    May God restore our country

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji160814 күн бұрын

    Amen zikomo🙏❤️💖

  • @BrianZenengeya
    @BrianZenengeya15 күн бұрын

    Yes 100% truth

  • @michaelsakala8884
    @michaelsakala888415 күн бұрын

    100% true

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j15 күн бұрын

    Mulungu akuwonesa ukulu wake sopano mzimu wa Chilima Uli pakati pa Malawi

  • @yowasschitsosa5348
    @yowasschitsosa534814 күн бұрын

    Kkkkkk zamanyazi a prophet m'malo molalika zamulungu mwayamba ndale

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu

    @TiyanjaneMkwate-we8gu

    14 күн бұрын

    Udzimu umaenda bwino anthu akamakhala umoyo wabwino, kuvutika ndi kupemphera siziyenderan, away akuzuzula nchitidwe omwe andale athu oipawa amapanga pozunza aMalawi kuti zao ziyende, ndikupempheranso kwa Mulungu kuti ndalama akubazo zithere kugula ma kidneys, zaoneneni nkhalamba momwe zikuzunzikira kumiziku yet they were promised alot for them to win.

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie14 күн бұрын

    Koma pamenepo ine kukhosi mweee😂😂😂

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv689615 күн бұрын

    Ameeeeeeeeeeeeeeen

  • @user-po7zs9zd7u
    @user-po7zs9zd7u14 күн бұрын

    Amen amen amen amen 🙏🙏🙏❤️❤️❤️

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox286515 күн бұрын

    Gen Z is watching

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino89812 күн бұрын

    Kkkkk 2023 izi Aaaa

  • @user-hg2cw1om1p
    @user-hg2cw1om1p15 күн бұрын

    ❤❤

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v14 күн бұрын

    Osaopa mbewe chilungamo Nena boma lotopesa ili ipondeni mbewe yomweyo

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience228315 күн бұрын

    Ifenso tikupemphera mwachinsinsi ndipo mapemphero athu akutheka. MCP mthawi yanu yatha kale. Ndipo MCP yatheratu. Mark my words.

  • @user-xe5lb4uf3n
    @user-xe5lb4uf3n11 күн бұрын

    Walankhula munthu wa Mulungu

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi14 күн бұрын

    Amen

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani569715 күн бұрын

    Paja adanena zoti akantheni

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb15 күн бұрын

    Amen amen

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i15 күн бұрын

    Izizi ndizakalekale,Kodi chifukwa chani mumabweretsa zinthu zoti ndi zakale?

  • @alicechinyama4155

    @alicechinyama4155

    15 күн бұрын

    Zakale lake liti

  • @user-si7po9sd5i

    @user-si7po9sd5i

    15 күн бұрын

    @@alicechinyama4155 I saw it in 2023, but maybe you didn't see it then

  • @user-si7po9sd5i

    @user-si7po9sd5i

    15 күн бұрын

    The msg was powerful though

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw15 күн бұрын

    Ameen

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf626015 күн бұрын

    Tell dem men💯

  • @DorrahBanda
    @DorrahBanda14 күн бұрын

    Amen❤❤

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl14 күн бұрын

    Ameen 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-fb6kh2dk1y
    @user-fb6kh2dk1y14 күн бұрын

    we are after message not chaka chakacho sungani inu

  • @AminAbbass-xc4qk
    @AminAbbass-xc4qk15 күн бұрын

    🎉🎉🎉🎉🎉

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv15 күн бұрын

    May God also punish fake prophets

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r15 күн бұрын

    Anzanuso asanarowe mboma anaringat auzimu ngat inu km anasintha mawanga amarawi osangot amen zirizonse ngat simuziwa mawu bwanji munthu wowopa chauta sankhara busy ndizandare chifukwa kundare kuribe kuopa murungu baibo rimat muthange mwafuna ufumu wake ndipo zonse zizakusatani auzeni zaufumu wakumwamba osat zazikozo ayi panopa amarawi asavoteraso azibusawa ayi asibusa nomwenu ndinu amene mwawononga zikori mawonekedwe achipembezo km mphwnvu yake munaikana kare pezani njira zina zosakira ndarama akuru

  • @user-gx3xc9lk8x

    @user-gx3xc9lk8x

    14 күн бұрын

    Good point

  • @MarkManyowa
    @MarkManyowa15 күн бұрын

    Amen 😂😂😂

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel15 күн бұрын

    Iweso ndiwa bodza mulungu wake UTI

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili14 күн бұрын

    Tell them

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel15 күн бұрын

    Iweee ukubwera anthuwo ndizako

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf14 күн бұрын

    Fire abusa

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama14 күн бұрын

    Amen😂

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe744814 күн бұрын

    😮😮😮😮😂😂😂😂😂

  • @Littlefair7
    @Littlefair715 күн бұрын

    Yes boma ili ndi lolephera koma zoti uyu ndi fake prophet sizisintha.

  • @kingsleyhopematchaya5184
    @kingsleyhopematchaya518415 күн бұрын

    Simulungu mbewe ndipo tsogolo la muthu sangalidziwe ndindani amewneyu tikusauka chifukwa cha kuba kwa dpp

  • @inessmsiyambiri8517

    @inessmsiyambiri8517

    14 күн бұрын

    Uli nkati Monday zokubatu

  • @curtisewilliams8784
    @curtisewilliams878415 күн бұрын

    Cant you see that, the video was recorded in 2023? bloggers be serious

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e15 күн бұрын

    Zakale izi akulu

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula73114 күн бұрын

    Aaaa m'busa wanji olowerera zadziko?? Ufumu wamulungu siuli wadziko lapansi baba, onvera awawa palibe chomwe akutsata

  • @Musa1828-l5d

    @Musa1828-l5d

    14 күн бұрын

    Chitsiru iwe mchifukwa chake mwapha chilima

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg

    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg

    14 күн бұрын

    NDE ZOTI DZIKO LAPANSI NDI LA ANTHU OIPA ANANENA NDANI,,MULUNGU SANGAOPE KUYANKHULA ZANDALE CHIFUKWA IYEYO NDE MWINI MPHAVU

  • @isaacchiwaula731

    @isaacchiwaula731

    14 күн бұрын

    Ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi

  • @isaacchiwaula731

    @isaacchiwaula731

    14 күн бұрын

    @@CHIFUNDOCHINA-lp9lg ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi chifundo

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg

    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg

    11 күн бұрын

    ASE UTSOGOLERI WACHIPEMBEZO NDI WOYAMBA KUPOSA U PRESIDENT,,DZIKO LAPANSI LIMADUNIKA LIZIYENDERA MALAMULO AMULUNGU,,TIKAWASIRA ASATANA KUT ALAMULIRE ANTHU AMULUNGU SIYIGWIRA

  • @user-nr8oq4tr1i
    @user-nr8oq4tr1i15 күн бұрын

    Fake prophet, yang'ana za Mulungu, waisted time

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko15 күн бұрын

    Wabodzi

  • @TimothyNkhutembaChirwa
    @TimothyNkhutembaChirwa15 күн бұрын

    Amen pastor

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y14 күн бұрын

    Amen ❤

  • @ellensambo6323
    @ellensambo63233 күн бұрын

    God bless you man of God

  • @MaryJefry
    @MaryJefry15 күн бұрын

    Amen prophet

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo2 күн бұрын

    Amen

  • @user-pn6ic9yr1t
    @user-pn6ic9yr1t13 күн бұрын

    Amen amen

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah15 күн бұрын

    Ameen

  • @ellenMakoloma
    @ellenMakoloma11 күн бұрын

    Amen prophet

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef14 күн бұрын

    Amen

  • @malitajere1609
    @malitajere160914 күн бұрын

    Amen

  • @user-nv7qt1yp7g
    @user-nv7qt1yp7g14 күн бұрын

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama14 күн бұрын

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama14 күн бұрын

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama14 күн бұрын

    Amen

  • @user-no2sn1fo1h
    @user-no2sn1fo1h15 күн бұрын

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama14 күн бұрын

    Amen