Ndimo mudzina la yesu mau Anu agwile ntchito pa andale okubawa mu dzina la yesu
Only Young president can do better... Coz they can do it in new model...NOT 60'S MODEL
U man of God continue to pray for those bad people to gate pushed from god
Amen man of God. We are tired wth that thng we call chakwera
Mau owoona mulungu atimenyele nkhondo ameeen
Mulungu wamatembelelo kkkkk mwayamba zibwana ndimulungu ky pot ndi business yanu ndimulungu wanu
Ndipo athu atizuzuza yawa sitizaiwala m, pakana kale kale mmm ndipo asatana
Amen mau ishiii ziko lathuli ai zikomo akuluakulu kuntunda mavuto okhaokha bsi.
God bless you man of God
Perfect said 👏 🙌
Very bold.....the only Man of God that have told govt the truth
Koma ndipo! Koma nthawi ya APM azibusa ma prophet ansembe palipose kunali kuyakhula zoipa zaboma lija koma pano kuli ziii, palibe akukamba zoipa kapena zabwino za bomali uyuyu ekha basi, ayi zikomo
Kodi chakwerayu tu bvuto ndi school komanso mtundu komwe akuchokera mmmmmmmm so shame walephera basi 2025 azipita !!
Tiye prophet awawa mulungu awachose 2025 zikutiwawà .
This is 2023,, but only God knows
Oooh yes tatopa ndi boma ili please azibusa lowereranipo ndithu timenyereni nkhondo Kuti kumwamba kuseguke tatopa ndikulira amalawi
Basi man of God ndalamazo andipatsira ine tikabweze komwe zinabedwa...kkkk
Matenda ake ena mwa iwo ndi misala.
Iwe usankhepo chimodzi pakati PA ubusa ndi Der wamva osamphatikinza za mulungu ndi Zadary 😂😂😂
Alavule ndalama zikenezo in Jesus Name
Amen man of God
Amen 🙏🙏 power
amen aprophert power full
Amen prophet
Amen mudzina la yesu
Nkhale Lili LA 2023 akuphempha ndi chimozi mozi tikuyembekezera amipingo ina tinve kunyasidwa kwanu Asilam tiye maduwa
Amen may God bunish them
Names nkukhala mommo mundalemo.😂😂
May God restore our country
Amen zikomo🙏❤️💖
Yes 100% truth
100% true
Mulungu akuwonesa ukulu wake sopano mzimu wa Chilima Uli pakati pa Malawi
Kkkkkk zamanyazi a prophet m'malo molalika zamulungu mwayamba ndale
Udzimu umaenda bwino anthu akamakhala umoyo wabwino, kuvutika ndi kupemphera siziyenderan, away akuzuzula nchitidwe omwe andale athu oipawa amapanga pozunza aMalawi kuti zao ziyende, ndikupempheranso kwa Mulungu kuti ndalama akubazo zithere kugula ma kidneys, zaoneneni nkhalamba momwe zikuzunzikira kumiziku yet they were promised alot for them to win.
Koma pamenepo ine kukhosi mweee😂😂😂
Ameeeeeeeeeeeeeeen
Amen amen amen amen 🙏🙏🙏❤️❤️❤️
Gen Z is watching
Kkkkk 2023 izi Aaaa
❤❤
Osaopa mbewe chilungamo Nena boma lotopesa ili ipondeni mbewe yomweyo
Ifenso tikupemphera mwachinsinsi ndipo mapemphero athu akutheka. MCP mthawi yanu yatha kale. Ndipo MCP yatheratu. Mark my words.
Walankhula munthu wa Mulungu
Amen
Paja adanena zoti akantheni
Amen amen
Izizi ndizakalekale,Kodi chifukwa chani mumabweretsa zinthu zoti ndi zakale?
Zakale lake liti
@@alicechinyama4155 I saw it in 2023, but maybe you didn't see it then
The msg was powerful though
Ameen
Tell dem men💯
Amen❤❤
Ameen 🙏🙏🙏🙏🙏
we are after message not chaka chakacho sungani inu
🎉🎉🎉🎉🎉
May God also punish fake prophets
Anzanuso asanarowe mboma anaringat auzimu ngat inu km anasintha mawanga amarawi osangot amen zirizonse ngat simuziwa mawu bwanji munthu wowopa chauta sankhara busy ndizandare chifukwa kundare kuribe kuopa murungu baibo rimat muthange mwafuna ufumu wake ndipo zonse zizakusatani auzeni zaufumu wakumwamba osat zazikozo ayi panopa amarawi asavoteraso azibusawa ayi asibusa nomwenu ndinu amene mwawononga zikori mawonekedwe achipembezo km mphwnvu yake munaikana kare pezani njira zina zosakira ndarama akuru
Good point
Amen 😂😂😂
Iweso ndiwa bodza mulungu wake UTI
Tell them
Iweee ukubwera anthuwo ndizako
Fire abusa
Amen😂
😮😮😮😮😂😂😂😂😂
Yes boma ili ndi lolephera koma zoti uyu ndi fake prophet sizisintha.
Simulungu mbewe ndipo tsogolo la muthu sangalidziwe ndindani amewneyu tikusauka chifukwa cha kuba kwa dpp
Uli nkati Monday zokubatu
Cant you see that, the video was recorded in 2023? bloggers be serious
Zakale izi akulu
Aaaa m'busa wanji olowerera zadziko?? Ufumu wamulungu siuli wadziko lapansi baba, onvera awawa palibe chomwe akutsata
Chitsiru iwe mchifukwa chake mwapha chilima
NDE ZOTI DZIKO LAPANSI NDI LA ANTHU OIPA ANANENA NDANI,,MULUNGU SANGAOPE KUYANKHULA ZANDALE CHIFUKWA IYEYO NDE MWINI MPHAVU
Ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi
@@CHIFUNDOCHINA-lp9lg ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi chifundo
ASE UTSOGOLERI WACHIPEMBEZO NDI WOYAMBA KUPOSA U PRESIDENT,,DZIKO LAPANSI LIMADUNIKA LIZIYENDERA MALAMULO AMULUNGU,,TIKAWASIRA ASATANA KUT ALAMULIRE ANTHU AMULUNGU SIYIGWIRA
Fake prophet, yang'ana za Mulungu, waisted time
Wabodzi
Amen pastor
Amen ❤
Пікірлер: 99
Ndimo mudzina la yesu mau Anu agwile ntchito pa andale okubawa mu dzina la yesu
Only Young president can do better... Coz they can do it in new model...NOT 60'S MODEL
U man of God continue to pray for those bad people to gate pushed from god
Amen man of God. We are tired wth that thng we call chakwera
Mau owoona mulungu atimenyele nkhondo ameeen
Mulungu wamatembelelo kkkkk mwayamba zibwana ndimulungu ky pot ndi business yanu ndimulungu wanu
Ndipo athu atizuzuza yawa sitizaiwala m, pakana kale kale mmm ndipo asatana
Amen mau ishiii ziko lathuli ai zikomo akuluakulu kuntunda mavuto okhaokha bsi.
God bless you man of God
Perfect said 👏 🙌
Very bold.....the only Man of God that have told govt the truth
@TheresaKuluwemba
13 күн бұрын
Koma ndipo! Koma nthawi ya APM azibusa ma prophet ansembe palipose kunali kuyakhula zoipa zaboma lija koma pano kuli ziii, palibe akukamba zoipa kapena zabwino za bomali uyuyu ekha basi, ayi zikomo
Kodi chakwerayu tu bvuto ndi school komanso mtundu komwe akuchokera mmmmmmmm so shame walephera basi 2025 azipita !!
Tiye prophet awawa mulungu awachose 2025 zikutiwawà .
This is 2023,, but only God knows
Oooh yes tatopa ndi boma ili please azibusa lowereranipo ndithu timenyereni nkhondo Kuti kumwamba kuseguke tatopa ndikulira amalawi
Basi man of God ndalamazo andipatsira ine tikabweze komwe zinabedwa...kkkk
Matenda ake ena mwa iwo ndi misala.
Iwe usankhepo chimodzi pakati PA ubusa ndi Der wamva osamphatikinza za mulungu ndi Zadary 😂😂😂
Alavule ndalama zikenezo in Jesus Name
Amen man of God
@AlinafeChimoto-pp7wp
15 күн бұрын
Amen 🙏🙏 power
amen aprophert power full
Amen prophet
Amen mudzina la yesu
Nkhale Lili LA 2023 akuphempha ndi chimozi mozi tikuyembekezera amipingo ina tinve kunyasidwa kwanu Asilam tiye maduwa
Amen may God bunish them
Names nkukhala mommo mundalemo.😂😂
May God restore our country
Amen zikomo🙏❤️💖
Yes 100% truth
100% true
Mulungu akuwonesa ukulu wake sopano mzimu wa Chilima Uli pakati pa Malawi
Kkkkkk zamanyazi a prophet m'malo molalika zamulungu mwayamba ndale
@TiyanjaneMkwate-we8gu
14 күн бұрын
Udzimu umaenda bwino anthu akamakhala umoyo wabwino, kuvutika ndi kupemphera siziyenderan, away akuzuzula nchitidwe omwe andale athu oipawa amapanga pozunza aMalawi kuti zao ziyende, ndikupempheranso kwa Mulungu kuti ndalama akubazo zithere kugula ma kidneys, zaoneneni nkhalamba momwe zikuzunzikira kumiziku yet they were promised alot for them to win.
Koma pamenepo ine kukhosi mweee😂😂😂
Ameeeeeeeeeeeeeeen
Amen amen amen amen 🙏🙏🙏❤️❤️❤️
Gen Z is watching
Kkkkk 2023 izi Aaaa
❤❤
Osaopa mbewe chilungamo Nena boma lotopesa ili ipondeni mbewe yomweyo
Ifenso tikupemphera mwachinsinsi ndipo mapemphero athu akutheka. MCP mthawi yanu yatha kale. Ndipo MCP yatheratu. Mark my words.
Walankhula munthu wa Mulungu
Amen
Paja adanena zoti akantheni
Amen amen
Izizi ndizakalekale,Kodi chifukwa chani mumabweretsa zinthu zoti ndi zakale?
@alicechinyama4155
15 күн бұрын
Zakale lake liti
@user-si7po9sd5i
15 күн бұрын
@@alicechinyama4155 I saw it in 2023, but maybe you didn't see it then
@user-si7po9sd5i
15 күн бұрын
The msg was powerful though
Ameen
Tell dem men💯
Amen❤❤
Ameen 🙏🙏🙏🙏🙏
we are after message not chaka chakacho sungani inu
🎉🎉🎉🎉🎉
May God also punish fake prophets
Anzanuso asanarowe mboma anaringat auzimu ngat inu km anasintha mawanga amarawi osangot amen zirizonse ngat simuziwa mawu bwanji munthu wowopa chauta sankhara busy ndizandare chifukwa kundare kuribe kuopa murungu baibo rimat muthange mwafuna ufumu wake ndipo zonse zizakusatani auzeni zaufumu wakumwamba osat zazikozo ayi panopa amarawi asavoteraso azibusawa ayi asibusa nomwenu ndinu amene mwawononga zikori mawonekedwe achipembezo km mphwnvu yake munaikana kare pezani njira zina zosakira ndarama akuru
@user-gx3xc9lk8x
14 күн бұрын
Good point
Amen 😂😂😂
Iweso ndiwa bodza mulungu wake UTI
Tell them
Iweee ukubwera anthuwo ndizako
Fire abusa
Amen😂
😮😮😮😮😂😂😂😂😂
Yes boma ili ndi lolephera koma zoti uyu ndi fake prophet sizisintha.
Simulungu mbewe ndipo tsogolo la muthu sangalidziwe ndindani amewneyu tikusauka chifukwa cha kuba kwa dpp
@inessmsiyambiri8517
14 күн бұрын
Uli nkati Monday zokubatu
Cant you see that, the video was recorded in 2023? bloggers be serious
Zakale izi akulu
Aaaa m'busa wanji olowerera zadziko?? Ufumu wamulungu siuli wadziko lapansi baba, onvera awawa palibe chomwe akutsata
@Musa1828-l5d
14 күн бұрын
Chitsiru iwe mchifukwa chake mwapha chilima
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg
14 күн бұрын
NDE ZOTI DZIKO LAPANSI NDI LA ANTHU OIPA ANANENA NDANI,,MULUNGU SANGAOPE KUYANKHULA ZANDALE CHIFUKWA IYEYO NDE MWINI MPHAVU
@isaacchiwaula731
14 күн бұрын
Ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi
@isaacchiwaula731
14 күн бұрын
@@CHIFUNDOCHINA-lp9lg ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi chifundo
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg
11 күн бұрын
ASE UTSOGOLERI WACHIPEMBEZO NDI WOYAMBA KUPOSA U PRESIDENT,,DZIKO LAPANSI LIMADUNIKA LIZIYENDERA MALAMULO AMULUNGU,,TIKAWASIRA ASATANA KUT ALAMULIRE ANTHU AMULUNGU SIYIGWIRA
Fake prophet, yang'ana za Mulungu, waisted time
Wabodzi
Amen pastor
Amen ❤
God bless you man of God
Amen prophet
Amen
Amen amen
Ameen
Amen prophet
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen