BON KALINDO APA NDE WALANKHULA MOTO KUTI BUU |

Пікірлер: 135

  • @VungaQueen
    @VungaQueen15 күн бұрын

    Number Bon kalindo munthu osaopa kotse mulungu azikupatsani moyo wautali 👏👏🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f16 күн бұрын

    The DC mwana oopsa kwambiri from Njedza vg😅😅 love you more

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj16 күн бұрын

    THE DC IS THE ONE WHO TELLING PEOPLE THE TRUTH TO ANDSTAND EFFECT ON THAT'S ALL THE WAY I'M IN THE SAUTH AFRICA ESTAN CAP THANK YOU MR BON KALINDO MY ALLAH BLESS YOU ALWAYS HAVE A GREAT DAY ORROWYESS

  • @esaMoha-dm4kj

    @esaMoha-dm4kj

    15 күн бұрын

    CONGRATULATIONS TO YOUR MY BROTHER FRIEND FROM MALAWI I'M OLOSO FROM MALAWI ASHANKWELA HIS MUST LEE SINE PEOPLES OF COUNTRY 👌

  • @AshleyPhiri-m7t
    @AshleyPhiri-m7t14 күн бұрын

    The DC fire fire 🔥 your speak true papa don't be afraid, God i will protect you all the time

  • @FahadiFalaji
    @FahadiFalaji16 күн бұрын

    Watching from pmb south Africa number 1 God first❤

  • @MahallaMinistries-fv1hw
    @MahallaMinistries-fv1hw16 күн бұрын

    Thanks Bon. I deeply feel that any priest asking for citizens' silence on the Chikangawa plane accident must first silence him/herself in the Spirit. Any gracious priest must flee from the tricky temptation of deliberately misinterpreting related scriptire like Romans 13:1-7). O LORD, save the integrity of our priesthood for a godly Malawi.❤❤❤

  • @user-or7ng3fj8f
    @user-or7ng3fj8f15 күн бұрын

    Bonnnnnnnn kalindooooooooo the DC 🔥fire

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f16 күн бұрын

    Mangochi ndi district yodzuka yosagona sitimaopa ife Ayao amanyi mutimva a MCP ,ife nganganga! Pambuyo pa president wanthu the DC mwana oopsa kwambiri. Ndiponso simukwanitsa kumupha tadzuka , munantola Chilima kuchikangawa pano tonse tadzuka pa ifa ya Chilima ndipo tipanga za ku Kenya very soon.

  • @DissChikondi

    @DissChikondi

    16 күн бұрын

    Fire fire

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b15 күн бұрын

    We silute you the DC. May the almighty God continue protect you wherever uou will go♥️♥️♥️♥️

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh627614 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂your expensive mwana woopsa kwambiri eish koma Bon the DC!

  • @FlechaChipeta
    @FlechaChipeta16 күн бұрын

    Warankhura bwino kwambili kalindo ❤

  • @aggogokina8992
    @aggogokina899216 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂 azunguze anthu okubawa Boooon Kalindooo💪💪

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no16 күн бұрын

    Thanks so 🎉🎉🎉🎉🎉

  • @JosephLuna-o1d
    @JosephLuna-o1d16 күн бұрын

    Thanks for all you doing Mr kalidoo

  • @MacreaChilingulo-ob9gb
    @MacreaChilingulo-ob9gb16 күн бұрын

    The DC ! !!! MWANA WOOOOOOPSYA !!! Kwambiri , Nyama muzidya inde !; koma movutika kwambiri !

  • @MaureenMollen
    @MaureenMollen14 күн бұрын

    The DC keep the fire burning.

  • @CeciliaNkhoma-nz7uj
    @CeciliaNkhoma-nz7uj16 күн бұрын

    Thank you very much the DC for your work on behalf of poor Malawian

  • @ElizaSemu
    @ElizaSemu16 күн бұрын

    He feels pain of all poor Malawians Bon Kalindo mwana owopsa kwambiri the DC even angel akukuwombela mmanja good work reveals the truth while the evil hides inside the money

  • @user-mv8vy3ht3n
    @user-mv8vy3ht3n16 күн бұрын

    Watching from zimbabwe DC

  • @StevenNyozan
    @StevenNyozan15 күн бұрын

    😂😂😂😂amasulidwe basi Ana akubawa atikwanaaah

  • @user-lw9su5om5z
    @user-lw9su5om5z15 күн бұрын

    😂😂😂😂 kma bon kalindo chipongwe eee kkkkkk the Dccccccccccc

  • @SilenceSanued
    @SilenceSanued16 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂 Iputeni milandu inayo ife tiri ku msana kwanu😂😂😂😂😂 mantha njeee

  • @masmonmark84
    @masmonmark8416 күн бұрын

    Ndimawona ngati alankhula zanzeru awa tinvomereze kuti mukufunika kubwerela ku uphuzitsi kuja mukapange upgrade chifukwa chomwe mumapanga ndikunyoza koma osabweretsa solution.aaaaah

  • @masmonmark84

    @masmonmark84

    16 күн бұрын

    And Kodi mukufuna ife tizitengeka Nanu kenaka mudzatipusitse Pamawa mwayiwala kuti munanena nokhat zakuti Malawi siomufera? Ndiye musatikwanepo apa

  • @RichmondHavy
    @RichmondHavy16 күн бұрын

    The DC 🔥🔥🔥

  • @ishmaelcassim806
    @ishmaelcassim80616 күн бұрын

    The Dc mr bon kalindo you are talking true. M C P Must go Out we don't want m c p any more.Mr bon kalindo more

  • @user-ih7li3im4s
    @user-ih7li3im4s16 күн бұрын

    God always protect you, Chilungamo chako Mulungu akuziwa kufunika kwako kwa ife

  • @joneskalitsilo6556
    @joneskalitsilo655616 күн бұрын

    Akuti osampha mwanako bwanji!😂😂😂😂 Koma kalindo.. kkkkkkkkk

  • @FranklinNdovi
    @FranklinNdovi16 күн бұрын

    This nation needs causal factors that lead to the plane crash not autopsy reports.

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e16 күн бұрын

    Ambuye mutetedzereni bon kalindo ndi munthu yemwe akutitthonza pa mavuto athu

  • @lucianosamissonejose2374
    @lucianosamissonejose237416 күн бұрын

    A Bon kalindo inuyo mulungu adzikudalitsani ndine Luciano kuchokera ku Mozambique

  • @UsenLashid
    @UsenLashid16 күн бұрын

    DC woyeeeeeee katundu womanga ndi mawaya

  • @MacleanMkhalipi
    @MacleanMkhalipi16 күн бұрын

    Stand to honest Mr kalindo

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati316616 күн бұрын

    Inu ndi 1 Bon Kalindo 😂❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @nessiemfunie
    @nessiemfunie16 күн бұрын

    ,,ngakhale tili Mayiko akhunja tizabwela tizaku votelan Mr bon karindo

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza580216 күн бұрын

    Kkkkkkkkkk if you try to catch my people I will catch you 😅😅😅😅😅😅😅

  • @user-mq5vs4hn6o
    @user-mq5vs4hn6o16 күн бұрын

    Watching you from Zambia ❤❤❤❤❤❤❤

  • @PhillipLipenga
    @PhillipLipenga16 күн бұрын

    😂😂😂 aidya nyama koma azidya akulila kkkkkkk

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles234816 күн бұрын

    You are becoming bakili muluzi TV 😂❤❤❤

  • @StanlyBeza
    @StanlyBeza16 күн бұрын

    😂😂,😂😂the diiiisiiiiii

  • @GiftSaidimbewe
    @GiftSaidimbewe16 күн бұрын

    Ndimakunyadilan the DC tilinanu

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx16 күн бұрын

    Chilima anaphedwa ndi Chakwera. Aliyense akudziwa zimenezo ndipo ndikudikira mwachidwa kuti atiuze chomwe chinamupha Saulos Klaus Chilima

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus16 күн бұрын

    Tifufuza mbuziyi ikatuluka mboma...ndipo chikaferatu kundende chimfiti chimenechi.......mbuzi😮😮😮😮😮

  • @MphatsoBanda-uv4nr
    @MphatsoBanda-uv4nr16 күн бұрын

    Ati tikusendani😂😂😂😂

  • @LameckDanken-tm4rt
    @LameckDanken-tm4rt16 күн бұрын

    The DC more fire anthu admarc bwana akuvutika kooopsa bwana president wa osauka

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo144116 күн бұрын

    Asaaa koma winiko mpaka amako😂😂😂😂

  • @RASHIFORDHSK
    @RASHIFORDHSK15 күн бұрын

    My vote

  • @chifukanyo9447
    @chifukanyo944716 күн бұрын

    😂😂😂😂 ati atamangidwe ndi amako😂😂

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m16 күн бұрын

    The DC ❤❤❤❤❤

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo16 күн бұрын

    😂😂😂Akakumanga bail ilipo

  • @Zamwano
    @Zamwano16 күн бұрын

    Kd nanga ma demo aja Mesa lero pa 10 tulukan munyumba am already outside

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y16 күн бұрын

    The Dc good Messnge Mr bon kalindo ❤

  • @BensonChilundu
    @BensonChilundu16 күн бұрын

    Tikufuna Chakwera adzayankhe milandu yonse,yosakaza chuma cha boma komanso imfa ya anthu asanu ndi atatu omwe anafa ku Chikangawa ndi ena onse ngati Zikhale Ngoma,Mkaka,Chimwendo Banda mkulu wa apolisi,mkulu wa nkhondo ndi ena onse mkazi wa Chakwera komansotu mwana wake Nick

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah16 күн бұрын

    We follow

  • @LamieTiger
    @LamieTiger16 күн бұрын

    Captain kalindo dolo kwambili

  • @user-gx3xc9lk8x
    @user-gx3xc9lk8x16 күн бұрын

    The DC😂😂😂😂😂❤❤❤❤

  • @ThokozaniChadza
    @ThokozaniChadza16 күн бұрын

    Moto booo Dc tililimozi ❤❤❤

  • @ChimwemweNgwende
    @ChimwemweNgwende16 күн бұрын

    A keyala anakanika kuipeza ndege yawoyawo 24hrs ndiye pano ati akuti akufufuza chomwe chinagwesa ndege kodi achipeza? Kkkkkkkk 24hrs failed to trace ndege by using technology search ndiye achipeza chomwe chinagwesa ndege?

  • @aarongrey5620
    @aarongrey562016 күн бұрын

    Komaso Bon kalindo ndimangowona ngati tingopeza nafeso futi kujozi kuno timenyane ndiboma lachakwela ukuwona bwanji

  • @Dysonkhofi

    @Dysonkhofi

    16 күн бұрын

    Inenso ndikuona choncho Tiwachotse agaluwa

  • @LinlyNakombe
    @LinlyNakombe16 күн бұрын

    Keep fire burning

  • @williamdaka79
    @williamdaka7916 күн бұрын

    Umakwana boma lautsiru kwabasi

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili16 күн бұрын

    Kkkk boma laluza milandu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl16 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂 Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp16 күн бұрын

    D c wi love you 🎉

  • @Mohammed-sk1fy
    @Mohammed-sk1fy16 күн бұрын

    The DC Born

  • @Momweekly
    @Momweekly16 күн бұрын

    DC he is the voice of the voice less

  • @user-cg5ml7ym4v
    @user-cg5ml7ym4v15 күн бұрын

    Uthenga wamphavu kwambiri ife tili pambuyo

  • @thokozanisukah6448
    @thokozanisukah644816 күн бұрын

    Mfana oophya kwambili

  • @jamesgama5489
    @jamesgama548916 күн бұрын

    Unasala wekha bon anzako onse anadyesedwa ma banzi pano ali chete

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg16 күн бұрын

    Km ndodo iyandikile coz komwe tikupitak kulib kuchez

  • @LINELYBISANI
    @LINELYBISANI16 күн бұрын

    Antongwetongwe olalikira hahaha

  • @PhysicChands
    @PhysicChands16 күн бұрын

    Boni kalindo moto kuti buu umatiyimilila ❤❤

  • @FrancisDinala
    @FrancisDinala16 күн бұрын

    Watching from israel pa boma

  • @ShupeZiwa-s4y
    @ShupeZiwa-s4y16 күн бұрын

    Uyu ndi one😂

  • @fransiscopetro7491
    @fransiscopetro749116 күн бұрын

    The DC njedza Villege TA MABUKA

  • @zelliachamboto5744
    @zelliachamboto574416 күн бұрын

    Yomweyo DC😅

  • @user-rc4pf7hr9f
    @user-rc4pf7hr9f15 күн бұрын

    👌👌👌👌👌👌👌

  • @AdamSamson-gb7qz
    @AdamSamson-gb7qz16 күн бұрын

    Koma kumenekoo!!

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr16 күн бұрын

    Zikuyenera kutero, DC ndiwe President. Ukuyenera chitetezo chochuluka ndithu. Komanso achitetezowo awonjezere, azikwana 3000

  • @kayceesamuels
    @kayceesamuels16 күн бұрын

    Amve pain amenewo

  • @FreddieNkhoma
    @FreddieNkhoma16 күн бұрын

    Boni kalindo keep it up

  • @JanaAmina-iw6bf
    @JanaAmina-iw6bf16 күн бұрын

    👌

  • @TisopeChagala
    @TisopeChagala16 күн бұрын

    Enafe nde tinasiya kale kale kuonera Mbc tv

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute383916 күн бұрын

    Thanks watching from Blantyre

  • @NeverBeforeMnesa
    @NeverBeforeMnesa16 күн бұрын

    Kodi za ma demonstration pa 10 July zili Pati?

  • @user-qq1uj7ct6n

    @user-qq1uj7ct6n

    16 күн бұрын

    nane ndufuna kuziwa.. zilipati zakuyenda pa nseu lero?

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy16 күн бұрын

    Chakwera sakumvesa za kulimba mtima kwako

  • @user-zm9sf2mj7u
    @user-zm9sf2mj7u15 күн бұрын

    Thanks bon kalindo

  • @AnnieZiba
    @AnnieZiba16 күн бұрын

    Moseliwa

  • @stevejizaremu3396
    @stevejizaremu339616 күн бұрын

    Osaopa

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft16 күн бұрын

    Akalindo

  • @user-yk4by8iy8k
    @user-yk4by8iy8k16 күн бұрын

    Zoona bon kalindo mulungu alinawe

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar746816 күн бұрын

    Koma sakuyamkhulapo za manganya ku mcp

  • @davidjames679
    @davidjames67916 күн бұрын

    kod mesa mmat lelo tikathamange kod ??

  • @user-rc4pf7hr9f
    @user-rc4pf7hr9f15 күн бұрын

    🎉🎉🎉🎉🎉

  • @texonkautera
    @texonkautera15 күн бұрын

    😅😊😊😊😮

  • @PhysicChands
    @PhysicChands16 күн бұрын

    ❤❤❤

  • @MusaManati-ho4zf
    @MusaManati-ho4zf16 күн бұрын

    The dc Moseliwa mapwiya......

  • @AngolanChinga
    @AngolanChinga16 күн бұрын

    The DC ❤❤❤❤❤❤

  • @chipilirokalison1334
    @chipilirokalison133416 күн бұрын

    Mwana ooopsyaa kwambiri mulungu akudalitse

  • @Janatukaunda
    @Janatukaunda16 күн бұрын

    The DC mwana owopsa kwambiri

  • @StanleyDama

    @StanleyDama

    15 күн бұрын

    Lelo ? Wait for next

  • @JonathanChimwaza
    @JonathanChimwaza16 күн бұрын

    Chilungamo chi ma wawa chikamayakhulidwa