Akuti MCP iwinaso 2025 Zifukwa Zake Nazi

Akuti MCP iwina 2025 opanda thandizo la Tonse

Пікірлер: 37

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b2 ай бұрын

    Chonsecho agona ndi njala anthu anthu osawona patali😩

  • @MustafaLikaomba
    @MustafaLikaomba2 ай бұрын

    Awa ndiye manyiiiiii onunkha

  • @user-ub9on7oj7l
    @user-ub9on7oj7l2 ай бұрын

    Sakuziwa chomwe akuchita

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d2 ай бұрын

    Athu ovetsa chisoni kwambili

  • @omarajibu860
    @omarajibu8602 ай бұрын

    Ndiganiza kuti pansi pa mtimapo mukuziwa kuti mukunama zomwe mukulankhulazo

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r2 ай бұрын

    Dziwani kuti tonsefe sitingakhale ndimaganizo amozi malawi ndi dziko zalazipani zambiri tosefe sitingakonde dpp aliyese ali ndi chisakho chake ndiye adpp mkuchedwa

  • @giftblack7690
    @giftblack76902 ай бұрын

    Kkkkkkkk koma munthu anakonza alibe kalikose akuvutika ndikumatamililabe ng'ona party mbava yachabe chabe chakwela kwamtele

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qh2 ай бұрын

    Azimai ovesa chisoni kwambiri pomwe kunyumba kwako kulibe chakudya

  • @ImraanJafali-dk7rg

    @ImraanJafali-dk7rg

    2 ай бұрын

    Ndiposo inu mwina adyesedwa ma2 pin

  • @user-hm9nc7lz6e

    @user-hm9nc7lz6e

    2 ай бұрын

    Zoopsatu anthu amabgidwa papango komaso asekedwA maso sakuona

  • @AdamAPhiri
    @AdamAPhiriАй бұрын

    Pa mtsonkhano wa mcp angayinyoze ndani kuti akadyedwe ndi ng'ona

  • @omarajibu860
    @omarajibu8602 ай бұрын

    Iwe ukunena kuti anthu akonzekere, ife tinakonzeka kale zochotsa masanjewa 2025.

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op2 ай бұрын

    Kumalawi kwene umo wathu tikugonela nanjala thena bwenu tikukhumba ku votelaso chakwela mmmmm sata nadi malawi wazingizga nadi eshìii koma

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn2 ай бұрын

    Awa asandichimwise odi mgone

  • @MustafaLikaomba
    @MustafaLikaomba2 ай бұрын

    Chala imapele ka usilu

  • @alexsumani6823
    @alexsumani68232 ай бұрын

    Izi izi ,muchepese ndithu ,kufuna kuutsa mkwiyo wa anthu uku mxeuii

  • @user-uv7yq1fx4r
    @user-uv7yq1fx4r2 ай бұрын

    Thawi yanu koma sangalalani komaliza malizitsani thawiyanu yatsala pang.ono

  • @stanleymollen7273
    @stanleymollen7273Ай бұрын

    Azibambo ena mzeru zero...sad

  • @omarajibu860
    @omarajibu8602 ай бұрын

    Komadi anthu opanda nzeru mulipo, zoona munthu wanzeru mpaka kumasiya kupuma kwawo kupita kunsonkhano wa izizi?

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e2 ай бұрын

    Mdalayu akudwala chakwela wapanga chan😅

  • @user-xw6rr9gm1z
    @user-xw6rr9gm1z2 ай бұрын

    Zomvesa chison ndithu mmh

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9oАй бұрын

    Kodi inu mumamufuna azinena kuti DPP izawina kodi tonse ingakhale ana agogo????

  • @binalidjeyshabahzombamalawi
    @binalidjeyshabahzombamalawi2 ай бұрын

    Mbuli za anthu

  • @MariaRajabu
    @MariaRajabu2 ай бұрын

    Munthu Ali PA Laine yokalandila zithu za mcp anganene kuti mcp iluza 2025 mukufuna asalandile kkkkkkkkkk

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi2 ай бұрын

    Anthu enawa ndi agalu awanthu

  • @mamulemathekga
    @mamulemathekga2 ай бұрын

    Ndarama sosi kwapusisa 2000 munduwamay kumanena simeneso mundu wobeleka sovesa chison asimay atu 😭🤔🤔

  • @spargomw
    @spargomw2 ай бұрын

    Nthaw mkachitsiru. Tionana 2025. Zidzakuvoteran nd Ndondocha osat anthu

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qh2 ай бұрын

    Bambo vumbe mukunena zoona inu

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem2 ай бұрын

    Kuyakhula kopusa ndithu tikumana 2025 ino

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y2 ай бұрын

    Iwe ukuyendela chigoba chimoz chachimanga komaso chigobacho chokakamisa nde kumati chakwera awina chamba eti chifukwa akupasani chitenje panyo panu anyapapi inu nanuso inu adala magalasiwo ndi mutucho pakolo pako

  • @user-gx8or3yz9u
    @user-gx8or3yz9u2 ай бұрын

    Ndalamazotu tilandila mudzipereka ndithu ife tidzilandila komasikuti tidzakuvoteraninso ai zimenezo muiwale amalawi tatopa Nanu kkkkk mudzalila chaka Cha mawa muli ku mastand tikufuna tione zina

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d2 ай бұрын

    Manyi anu

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w2 ай бұрын

    Mukunama chemwali

  • @FefieTenisha-du7ge
    @FefieTenisha-du7ge2 ай бұрын

    This is very pathetic With this kind of thinking how can we move forward as a country? I can now see clearly why this country will never develop... People are commenting on things they don't really understand.. Democracy will never work in Malawi... The masses are so idiotic that they can't even know how to elect a good leader for them

  • @user-vl8uw8mc3u
    @user-vl8uw8mc3uАй бұрын

    Anthu akufa awa komanso osapenyanso awa sorry kwabasi

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r2 ай бұрын

    Mcp bomaaaaaa❤❤