A Chakwera Ndi A Chilima Ntchito Yanu Yatha - Billy Banda

On Nyasa VoiceBox, Billy Banda says that time is up for His Excellency Dr Lazarus Chakwera and his Vice President Dr Saulos Chilima becuase they have failed to govern the country.
Pa Nyasa VoiceBox, Billy Banda wati nthawi yatha kwa Olemekezeka Dr Lazarus Chakwera ndi wachiwiri wawo Dr Saulos Chilima chifukwa alephera kulamulira dziko.
#malawi

Пікірлер: 83

  • @stanleymollen7273
    @stanleymollen727313 күн бұрын

    Dzikoli likufunika ma Demo....ngini zinakwera mitengo monyasa.anthu akuvutika heavy.. Palibe chomwe tingaloze kuchiyenda.

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala13 күн бұрын

    From today, Commander atenge ulamuliro mpaka tsiku lachisankho. Chakwera out

  • @marryphili5419
    @marryphili541913 күн бұрын

    Achoke amenewa awononga Malawi wokoma uja Lero mavuto okhaokha zawavuta basi

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t13 күн бұрын

    Kumanga bakili mluzi tv Malawi azayaka moto

  • @TarPoor-ye9jx
    @TarPoor-ye9jx13 күн бұрын

    We need people like you not those people on times,zbs,mbc onse alikumbuto kwa boma lakuba ilili

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela12 күн бұрын

    Big up boss,atikwana

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z13 күн бұрын

    NO PAIN NO GAIN INSHA ALLAH WAKUVA WAVA AKUT SIYAN NCHITO MWALEPHEL PLEASE GOOOOO

  • @muhammadcassim4056
    @muhammadcassim405613 күн бұрын

    big up brother that kind of citizen needed in our country than those people the get bribe and appreciate nonsense from chakwera and chilima mulungu akupaseni mphavu ndi kuima pa chilungamo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b13 күн бұрын

    Let's put everything to our God almighty. God is watching

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce213 күн бұрын

    Rev Chakwera kms Chilima kunena zoona zinthu zawakanika ndipo achikhala athu amzeru anakasiya pansi Udindo koma pakuti ndi agalu akakamirabe ubwino wake 2025 ndipompano..

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q12 күн бұрын

    Tikulira ife a Malawi apa tithawira kuti dziko lathu lamvunda kwacha yagwaso zithu zakweraso 😢😢😢 MCP Chakwera ndi UTM Chilima vote yanga ikundimvutisaso malawi ineeeee 😢😢😢

  • @user-td6dy8mh3b
    @user-td6dy8mh3b6 күн бұрын

    We need more of you zithu zikhare bwino bwino

  • @user-un6mw5wm3x
    @user-un6mw5wm3x13 күн бұрын

    good message Mr banda

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i13 күн бұрын

    AChakwera usogoleri mwa inu mulibe kwanu ndikuononga ziko amalawi ndiwokwiya

  • @HafizahHarack-bn3bf
    @HafizahHarack-bn3bf13 күн бұрын

    Yes we are very disappointed ndi wulamuliro wathu amenewo

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x11 күн бұрын

    Mumatiimilila Mr Banda mulungu akupatsen zabwino

  • @petrosmunthali5562
    @petrosmunthali556212 күн бұрын

    2025 saiphuranso chifukwa zinthu sizilibwino, life now we struggles.

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda27813 күн бұрын

    Chakwera achoke basi enough is enough

  • @user-oe1lg4xo7w
    @user-oe1lg4xo7w13 күн бұрын

    Chakwera ndi chirima Maso ngati Kazizi nchito yanu yathaaaaa. Tulukanimoni nyumbazathu zaboma . Palibenso chifukwa chokusungirani mmaudindo choncho ngati mukufuna ntendere muzipatse ulemu Nokha popular pansi maudindo and koma ngati mukufuna kuyaluka pokakamira maudindo amalawi azakutulutsamoni ndi Manama, mateche ndi zikoti kapena chakwera ndi chirima tayesani Zidane mumuwone mmalawi akakwiya.

  • @user-rd6zo8ry2d
    @user-rd6zo8ry2d12 күн бұрын

    God message

  • @DeekeyKamanga
    @DeekeyKamanga12 күн бұрын

    Ine kumangolankhula kt tsiyan udindo sizimandpasa sense iliyonse coz olankhula ndi ambili Koma zaka zikupitabe

  • @moseskathekeni8848
    @moseskathekeni884813 күн бұрын

    Very strong message.

  • @user-xx3hs6pw5y
    @user-xx3hs6pw5y13 күн бұрын

    Munthu oipa ameneyo chakwera azipita watipha amalawi

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa12 күн бұрын

    Mbuzi zalephela zimenezo zichoke we don't want them useless president in Malawian history zitsiru zeni zeni za anthu

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c13 күн бұрын

    Zoona zache azipita basi ndithu

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j13 күн бұрын

    Ambuye lithandizeni ziko lathu la malawi tikhululukireni zochimwa zathu ngati mwatikwiira bwezani nkhwiyo wanu

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja8 күн бұрын

    Exactly these is true All it's about Allah and let's ask our Almighty Allah to guide us and to help as to take out these mbava zimene zikuonga boma lathuli kumaba ndalama zathu zamisokho

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm13 күн бұрын

    Achoke galu ameneyu

  • @user-eb7px2ex2q
    @user-eb7px2ex2q12 күн бұрын

    Tipita liti tikamupakilitse h failed us ,cement nt evn a year kukakwera kawiri eeee ai zikomo, we are nt tired

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op13 күн бұрын

    Kuyakhula kwabwino

  • @francischikaya3146
    @francischikaya314611 күн бұрын

    Anthu opanda nzeru amayankhula zopusa ngati zimenezi. Ngati akuganiza kuti DPP ilowanso m'boma ndiye bodza. Chilima sanayendetse nawo dziko. Amene akukutumani a Banda tazingodyani ndalamazo. Iwe ndiwe wapangapo chiyani?.

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma550713 күн бұрын

    👏👏👏🙏

  • @MateyoMalindi
    @MateyoMalindi12 күн бұрын

    Ndizona achoke akuba awa

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN7 күн бұрын

    My vote belongs to the dc booon kalindo

  • @homeremedys3748
    @homeremedys374813 күн бұрын

    Chakwela akufuna ataimanso koma mulungu akukana

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela12 күн бұрын

    Zoonadi ,dziko ili achoke a chakwela ndi a chilima

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp13 күн бұрын

    Apandiku ona mosi akusapota mbusi chakwera achokekumen sisilu sawandu andichilima panopa akuspota chakwera mbusiya kape

  • @aloysiusdidymus7869
    @aloysiusdidymus786913 күн бұрын

    Ndenge zikugwaso nza ku Iran zakuno ai

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y13 күн бұрын

    Good message ❤

  • @user-dv5dv8je9t
    @user-dv5dv8je9t12 күн бұрын

    One more kachasu from me, kkkk

  • @RenardYono
    @RenardYono12 күн бұрын

    Akufuna Kuti abwereyo adza pezengongore adzi dzatiso ramuka Nika apume bas

  • @LamiziIgshaan
    @LamiziIgshaan11 күн бұрын

    agalu amenewa atizuza ndithu

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m13 күн бұрын

    Dziko lamalawi likufunikila mademo akathithi ziko lapansi lidziwe

  • @alexsumani6823
    @alexsumani682313 күн бұрын

    Ndakaika ngati zingatheke kaya mwina. Ndiye zikalepheleka kuti gologolo wakakamila zitani in that scenario 9

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy11 күн бұрын

    Chakwera waononga dziko kuposa ma president onse

  • @tariroJinya
    @tariroJinya8 күн бұрын

    Brother my respect to u.inever been in any Malawi since multiparty system came in Malawi.but Chakwera is worsest and rubish president in the world

  • @ibrahmdoka7486
    @ibrahmdoka748613 күн бұрын

    Akumangani

  • @eliffagondewe8214

    @eliffagondewe8214

    13 күн бұрын

    Kkkkkkk

  • @OwenMajoni-qv3eg
    @OwenMajoni-qv3eg13 күн бұрын

    Kkkkkk Zina ndi ziwanda. Mudzionongera nazo izi ndi uchitsiru wanuwo. Nsanje ikuphani baba

  • @udkconsultancy5567

    @udkconsultancy5567

    13 күн бұрын

    True some of these ndi mademoni awa a billy bwanji ? speak peace and unity ..

  • @user-hm9nc7lz6e

    @user-hm9nc7lz6e

    13 күн бұрын

    Ndiwe opusa kwambiri mmene anthu tikuvutikira ungamaikire cakwera kumbuyo zoona

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z13 күн бұрын

    Komatu a Malawi ufulu kuchuluka aliyense kungodzuka anyozepo chakwera koma izi tipita nazo kuti kodi ana athuwa adzakhala potani ufulu umenewu boma likugona olo Bingu samkaselera zopusazi

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w13 күн бұрын

    Kkkkkkkk auzeeeee!

  • @user-xx3hs6pw5y
    @user-xx3hs6pw5y13 күн бұрын

    Munthu oipa chakwera watipha azipita

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp13 күн бұрын

    Mcp yakupa ndipo yangasa chakwera andi chilima alepela ose mbusi sawandu mbava sa kuba

  • @HopesonBuledi
    @HopesonBuledi13 күн бұрын

    😢 😂 andiliza awa

  • @OumaOuma-ge4sd
    @OumaOuma-ge4sd13 күн бұрын

    Kodi anthu amenewa mfundo zawo kampeni wachakachino angamveledwe boza zisiluzo kunama bs

  • @user-rd6zo8ry2d
    @user-rd6zo8ry2d12 күн бұрын

    Zawakanika

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o13 күн бұрын

    Kagwere iwe ndiwe ndani chitsiru usatibowe ukuti ifeyo wina kuphatikiza ndani poti ukuyankhula wekha pomwe ulipo ndi milomo ya yothethekayo galu

  • @user-jd9yz5hp7y

    @user-jd9yz5hp7y

    13 күн бұрын

    Iwenso ndi wanyawu eti? Kapena ukudyanawo a MCP kwanu ndikutiko iwe?

  • @user-st6bt5vv9c

    @user-st6bt5vv9c

    13 күн бұрын

    Chitsiru iweyo galu uyu ukunena zoona ufunse uladi pa kk kuti panali bwanji

  • @user-st6bt5vv9c

    @user-st6bt5vv9c

    13 күн бұрын

    Zulo aziona uladi musa amanyozedwa akuva pa chigumula

  • @AllanChabwela

    @AllanChabwela

    12 күн бұрын

    Ngati mwadya nawo a mcp khalani chete,anthu akuvutika

  • @user-kr1tf2tu7s
    @user-kr1tf2tu7s12 күн бұрын

    Ndiye iweyo ukati chakwera ndi chilima maso ngati kadzidzi nanga peter uja afanana ndichiyani kuphatikiza iweyo ufuse athu akuuza mene ukuonekera.kodi iwe billy banda umadziwa malamulo ?uchoke ndiwe kaya mbuzi yotheratu cadet.

  • @AllanChabwela

    @AllanChabwela

    12 күн бұрын

    Peter munthalika sungayelekezele mbuzi ziwili zikutchilidwa apazi,

  • @McNeverNjanji
    @McNeverNjanji13 күн бұрын

    Chakwela acoke sakufunika

  • @user-et3il7pi7t
    @user-et3il7pi7t12 күн бұрын

    Mademo ayambaliti

  • @tingamasi106
    @tingamasi10613 күн бұрын

    Chilima amayendetsa boma lake lambuyako? Zoti anamuimitsa ntchito for the past 2 years iwe sukudziwa? Kapena amagwira nyumba mwako? Leave chilima alone pliz wadutsa kale muzambiri

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r13 күн бұрын

    Uchisilu abillywo ali nkuchikamwa ngati adya zowawa tiyeni wauko ndinu achisilu galu amalawi ake ati chimbwe

  • @EyobeAyala

    @EyobeAyala

    13 күн бұрын

    Mbolo yako iwe

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj13 күн бұрын

    Galu wachabechabe president yuti adakwanisapo zokhumba za anthu onse

  • @danielmwatchipitsa7442

    @danielmwatchipitsa7442

    13 күн бұрын

    You are a full

  • @franciscomkwanda2525
    @franciscomkwanda25258 күн бұрын

    How can a fully grown up man Billy speak lik this ...u may have something to say but the way u present it its very poor . Go back to the drawing board

  • @user-ko1lk3br4r
    @user-ko1lk3br4r13 күн бұрын

    Judge wakumalawi akulankhula atakhuta ndalama za DPP mukuva km kkkkkkk akt sakuona magetsi kusaxima, at mukumukaniza kukateng

  • @user-ko1lk3br4r

    @user-ko1lk3br4r

    13 күн бұрын

    Mafut ku mela at sakuona HSA akulembedwa iyeyo a police akulembedwa ntchito akuvek ndithu

  • @AllanChabwela

    @AllanChabwela

    12 күн бұрын

    Magetsi anthu akumidzi samadya aise,ndipo kumaganiza poyankhula osayankha phala apa ngati munthu amadya msewu,munthu amadya magets,shame

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba13 күн бұрын

    Zazii zenzeni chitsilu chamunthu zolskhula zako zosabveka mbuzi yamunthu shupit

  • @ibrahmdoka7486

    @ibrahmdoka7486

    13 күн бұрын

    Motherless squirt

  • @danielmwatchipitsa7442

    @danielmwatchipitsa7442

    13 күн бұрын

    Mbuzi iwe

  • @Pangolinimw

    @Pangolinimw

    13 күн бұрын

    Inu achitsilu kwanu.kut .ndibwere ndikudinde

  • @AllanChabwela

    @AllanChabwela

    12 күн бұрын

    Muchoka nbomamu

  • @SynodAudit
    @SynodAudit13 күн бұрын

    Good is good: no black out but prices of 3Fs, foods, fertilizer and Fuel eshiiiiiiiiiiiiiiiiii