Chilima Simtsogoleri Wabwino - Bon Kalindo

On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo says, Vice President Saulos Chilima is not presidential Material. If he was he would have show solidarity with the poor Malawians who are suffering under Tonse Alliance.
Ku Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo akuti, Vice President Saulos Chilima is not Presidential Material. Akadakhala akadawonetsa mgwirizano ndi Amalawi osauka omwe akuvutika pansi pa Tonse Alliance.

Пікірлер: 82

  • @user-qq1uj7ct6n
    @user-qq1uj7ct6nАй бұрын

    booooon kalindo Mo fayaa. keep on to give us truly updates. inu mumalankhula chilungamo chokha chokha

  • @Luxemaven8686
    @Luxemaven8686Ай бұрын

    Bon Kalindo you have gained a supporter!!!!

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3oАй бұрын

    Honest speaking Mr DC Big up

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7yАй бұрын

    Komatu a Kalindo munthu osamuipitsa choncho. Inu musamunene Chilima kuti oipa lero. Mwagwira naye ntchito limodzi. Kuipa kwa munthu amadziwa ndi Chauta basi. Inunso muli ndi zonyansa zanu.

  • @VincentNgabuhvincent

    @VincentNgabuhvincent

    Ай бұрын

    khala chete iwe

  • @HakeemJossam

    @HakeemJossam

    Ай бұрын

    aaaaah kuipa kwa munthu amakuziwa ndan? mxiew

  • @LoyidKarebe
    @LoyidKarebeАй бұрын

    Go ahead Mr kalindo we are following you

  • @ishmaeldama8906
    @ishmaeldama8906Ай бұрын

    Bon he is talking the truth, but u can see other people they talking sheet, be very careful my fellow Malawian, we must wake up guys, zinazi sizotengela kupita ku school, khalani pansi moganiza bwino, malangizo awuleletu awa,all the way from johannesburg

  • @Littlefair7

    @Littlefair7

    Ай бұрын

    Who spoke that spoke?

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321Ай бұрын

    Mukunena zoona big, koma mmalawi opusa akuona ngati chilima ndiwabwino

  • @AlastairGutt
    @AlastairGuttАй бұрын

    Kalindo is matured now

  • @devimatope9980
    @devimatope9980Ай бұрын

    man of integrate😂😂😂 Bonnnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri from Njeza village ..T/A mabuka, mulanje😊😊😊😊😊

  • @ellahmwams831
    @ellahmwams831Ай бұрын

    Mr kalindo moto 🔥 🔥🔥

  • @EagerChicken-qj6xu
    @EagerChicken-qj6xuАй бұрын

    Kodi inu mumkamuuza chilima ngati ndani? Osachita naye msanje. Pangani zanu akulu

  • @beakab2378
    @beakab2378Ай бұрын

    Zooona zokhazokha, Chilima wakhala duuuuu a Malawi tikulira, olo one day osalankhulapoyi mmene m"boma mukubedwera ndalamamu, nde atifune pano? Ine ndamitsikatu, he won't get my vote

  • @user-zm9sf2mj7u
    @user-zm9sf2mj7uАй бұрын

    Mbambande mr presdent bon kalindo kwathu kwa chulu zinthu sizilibwino tikukhalangati tili mkamwa mwa mikango

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958Ай бұрын

    Chakwera ndi Chilima wooooyeeee,muwaphe A Malawi onse mukatha mutenge mitemboyo muitafune Mukhute,popeza ndalama mwawa bera Kale,koma muziwe masiku amatha ndikugona adaku voterani wokha samaziwa zoti Chibwenzi chankhwangwa chokoma pokwera, Amalawi mukaza voteranso awa izo ndi zanu wanthuwa ndi aka Nyimbi Anunkhisa Malawi.

  • @macksonkalasa9668
    @macksonkalasa9668Ай бұрын

    Koma kumanidwa udindo kulira mpakana 4 years

  • @RodwellLupiya
    @RodwellLupiyaАй бұрын

    Bwana Born Kalindo pqjatu ndinu amene munamukakamiza Chilima kuti avomere kukhala vice president lero mukumunyozaso . Komaso inuyo mumatiuza kuti sindinu wandale koma chosecho mukuwauzaso anthu kuti akqvotere aford , udf kqpenda dpp.

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1qАй бұрын

    Apadi akunena zoona zaka zonse takhalayi chilima ali.duuuh nde angabwele kwa ife kutiwuza chani ??

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5oАй бұрын

    Yes you are really talking

  • @BrightKuyaka
    @BrightKuyakaАй бұрын

    Zoyankhula za bon kalindo zatitopetsa tsopano, katakwe ndi bakili muluzi tv

  • @frankiechasokoneza5802

    @frankiechasokoneza5802

    Ай бұрын

    Zakutopetsa not zatitopetsa bwana

  • @SamuelChauluka

    @SamuelChauluka

    Ай бұрын

    Ingosiyani osamamvela bas,,,,, za ziiii

  • @EagerChicken-qj6xu
    @EagerChicken-qj6xuАй бұрын

    Musamuipitsile mbiri a chilima inunso simulibwino.

  • @esternguluwe
    @esternguluweАй бұрын

    Bwanji adzangotiimra bon kalindo yomweyo pa u president,akuoneka ali ndi nzeru kwabasi

  • @MercyPhiri-nh9jy
    @MercyPhiri-nh9jyАй бұрын

    Zoona amasankha tsogoleri ndi mulungu. Inu musaweluze

  • @SibwenzaLevisoni-gm6rv
    @SibwenzaLevisoni-gm6rvАй бұрын

    Ndipo nkhaniyi ndioona big up DC

  • @PeterPadambo-kk5oh
    @PeterPadambo-kk5ohАй бұрын

    Chilima sanalakwise kanthu, cholinga akawukira muzimunena kuti amangowukira kulikonse? Apa pokha nde ayi, boma ili tinalivotera chifukwa cha Chilima, nde atulukeko chifukwa? Mesa kuli mavoti ake, musiyeni Chilima akhale, nthawi ikakwana ayankhula

  • @grandwellkatumbi4763

    @grandwellkatumbi4763

    Ай бұрын

    Aziyankhula zichani Nanu Inu chilima wanuyo

  • @user-yh3ys3qn6p
    @user-yh3ys3qn6pАй бұрын

    Chisilu mbuzi 😢😢😢

  • @KondwaniMunthali-lx5jc
    @KondwaniMunthali-lx5jcАй бұрын

    Ndiye tivotele ndani utiuze kalindo manyi ako

  • @user-ic7fq5yn6r
    @user-ic7fq5yn6rАй бұрын

    Yes DC akunena zovona

  • @georgebalala3048
    @georgebalala3048Ай бұрын

    Shaaaa this was days ago

  • @user-ep7cg9bb4m
    @user-ep7cg9bb4mАй бұрын

    Nkhanira yakwachulu yokha mwapala. Miyambe mwazimvetsa zinthu mmene zikuchitikora. Bwerani ndi ma demo anuwo tione ngati simuyaluka

  • @daveskachiphaphi
    @daveskachiphaphiАй бұрын

    Tabalirankon aku mwera usabwere ndi mademo Ako pano pakati chita kwanuko

  • @WilliamBanda-un5eg
    @WilliamBanda-un5egАй бұрын

    Dzapangeni nawo compete bwanji because it seems mukudziwa zambiritu

  • @ShukuSh-vi1hk
    @ShukuSh-vi1hkАй бұрын

    Ndizoona zimene akuankhula karindo chifukwa nthawi yakampeni ndiiyeyo amene amanyamula thumba la 50 kg sichakwera iyayi

  • @user-zs9hn3kv3e
    @user-zs9hn3kv3eАй бұрын

    Impossible ngati munthu akugwira ntchito mmboma sangayankhulepo zotsutsa boma man limenelo nde bodxa

  • @JonathanKamwetsa
    @JonathanKamwetsaАй бұрын

    Ipondeni Fadala........ You're a real son of Malawi........

  • @GiftAsirKhwanya-ok2gu
    @GiftAsirKhwanya-ok2guАй бұрын

    Akunena zoona kalindo

  • @DesmondKanguwe
    @DesmondKanguweАй бұрын

    Kalindo ndiwamisala uyu

  • @SanudiJaymofred
    @SanudiJaymofredАй бұрын

    Kalindo to the people

  • @NtabaKali
    @NtabaKaliАй бұрын

    Yaaa

  • @Nomsa77
    @Nomsa77Ай бұрын

    Vchifukwa choti azakhala pa u president ndichifukwa achakwera amuphera..... Chifukwa chani mdziko mumalowa anthu osaziwika bwino

  • @PeterkinsJanuary-fv9wd
    @PeterkinsJanuary-fv9wdАй бұрын

    Bon kalindo ulemu wanu

  • @CheloyaaChikwatuu-ob2mt
    @CheloyaaChikwatuu-ob2mtАй бұрын

    DC ❤❤❤

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711Ай бұрын

    Akutitenga ife uchitsilu pomwe achitsilu ndiyiwowo amalawi asukutsula ngati tinachotsa mbuyawo kamudzi chifukwa chankhadza chakwela nde ndanitso galu kwabasi

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6wАй бұрын

    Zitsiru ndizomwe zingakhulupilire chilima opusa omwewa ndizomwe zikunamizika chilima zaupresdent alibe nazo ntchito koma iye azingodyelera mimba yakeyo

  • @vitumbikokamanga5869
    @vitumbikokamanga5869Ай бұрын

    Chilima usogoleli mlibe ose ndi adyera same like chakwera 😅

  • @josephchika173
    @josephchika173Ай бұрын

    Amakomadi akamwalira munthu sure

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vxАй бұрын

    Uyu ndi wamisala chilima ndi otumidwa so sakadaima mkuyankhula mudakati ndi oukira

  • @YohaneFoster-vq7wp
    @YohaneFoster-vq7wpАй бұрын

    Kalindo akufuna atibalalise Ali ndi reason behind

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321Ай бұрын

    Munthu amakondedwa anamwalira Pamalawi

  • @ShabanMajor
    @ShabanMajorАй бұрын

    iwe ndikumenya bwanji mulimbana ndi DC wanga

  • @HakeemJossam
    @HakeemJossamАй бұрын

    anatipwetekesa asabweleso

  • @BrianBanda-nn1gt
    @BrianBanda-nn1gtАй бұрын

    Ndizoona ndikugwilizana nazo

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711Ай бұрын

    Aaaa chilima angoputsisa MCP tsingapase utsogole chifukwa chakwela akumva kukoma ndibanja lawo lotse nso dzoti chilima akudziwa chilungamo koma manyadzi uchitsilu mutayeni tiwone 2025 dzizatha bwa

  • @SAIKINGFRIDAY
    @SAIKINGFRIDAYАй бұрын

    Eh komatu akulu awa chilima anakulakwilani chani muja munayambila kumunenamuja mpakapano or kukuyankhani osangomusiya bwanji ndiwankulutu ameneuja amadziwa chimene akupanga nde zinazi ife mumatinyasanazo zomalimbana ndimunthu oti samakuyankhani

  • @giftmingo9293
    @giftmingo9293Ай бұрын

    Uzitiuzanso za DPP ifeyo lero? Moti ukakhala umati aMalawi angamvere ndithu iweyo kkkk

  • @francischikaya3146
    @francischikaya3146Ай бұрын

    Iwe sukuimirira a Malawi koma chipani china chomwe aliyense akuchidziwa. Ukulimbana ndi Chilima nthawi zonse bwanji? Kodi kwinako kulibe zofooka zawo. Usawaike a DPP ngati ndi Angelo lero. Sitinaiwale zomwe amachita padzana paja. Tikudziwa kuti mtunda wa kwanu ndi omweo. Usatinamize ife takana.

  • @SangwaniNkosi
    @SangwaniNkosiАй бұрын

    Chilungamo chimawawa,Koma DPP ayi ziko linaliko bwino mnthawi yimeneyo

  • @giftmingo9293
    @giftmingo9293Ай бұрын

    Boma la Chakwera silizakhala labwino kwaiwe only if utakhala Minister. Unduna sapatsa zitsiru ngati iwe. Anthu a kwa Chulu akakuthibula bwera uzazione. Kulira 4 years kufuna udindo kkk😂😂😂😂

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vxАй бұрын

    Chilima waonetsa kudekha ndipo sadaukire koma kalindo ndale zidakulani

  • @grandwellkatumbi4763

    @grandwellkatumbi4763

    Ай бұрын

    Dziko likamaonongeka mtsogoleri wabwino sadekha ....chilima akudekha zichani pamene zinthu zikufoila mdziko muno

  • @MalakamMillie
    @MalakamMillieАй бұрын

    Chilima ndi witch craft mbuzi mwana wajoka amati tizidya katatu madzi awulere magetsi awulere fetelizer wochipa. chilima ndifiti kwambili

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5eАй бұрын

    Zoonadi zianthu zoipa kwambiri 😂😂😂😂😂😂😂

  • @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy
    @AnnoyedFallingLeaves-zp8dyАй бұрын

    The problem with Kalindo is that he wants to be the master minder of Chilima. But he has to understand that Chilima has brains. My instincts also tells me that he is indirectly campaigning for DPP.

  • @user-se4cf9qp8b

    @user-se4cf9qp8b

    Ай бұрын

    This is true. Kalindo is 4 dpp

  • @EvanceSungani-cv9jk

    @EvanceSungani-cv9jk

    Ай бұрын

    In your minds but he talks vry true posatengera za ndale,,,,,and all of this akuya khula ndizoona,,,, nokha mukuziwa mene adalankhulila chilima mu campaign ya 2019 analankhula zambili mbili zokomera Ife achinyamata koma ndzt wakwanilitsapo,,,,,inuso musamangosutsa zilizonse you supposed to see the true

  • @Littlefair7

    @Littlefair7

    Ай бұрын

    I fully agree with you, Kalindo is taking advantage of illiterate masses.

  • @GRACIOUSKENAN

    @GRACIOUSKENAN

    Ай бұрын

    Which brains dear, you talking about??? No he is bad man also,can he preform good speak today how??

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9oАй бұрын

    Kalindo ngati ndi chamba uzavula galu iwe ukukhale wachilungamo ndiwe mulungu?? Ndiwe galu kwambiri usatibowe uziyankhulira amako ndi anthu akwanuko

  • @SamuelChauluka

    @SamuelChauluka

    Ай бұрын

    u a big fool

  • @BazaarShaibu
    @BazaarShaibuАй бұрын

    Aka ndi kachilungamo

  • @henrykapinga1433
    @henrykapinga1433Ай бұрын

    Kkkkkk

  • @LovelyGalaxy-rb7yl
    @LovelyGalaxy-rb7ylАй бұрын

    Zinthu zake

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9dАй бұрын

    The DDCccccccccccc

  • @EmilyBakali
    @EmilyBakaliАй бұрын

    Kkkkkkkkk

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638Ай бұрын

    Izi ndi nkhani za amalawi ngakhale a president anayankha nkhani ya America mu chichewa, translate in English nonsense

  • @angelj3771
    @angelj3771Ай бұрын

    It a better to dellete this video. You have cursed him

  • @josephchika173

    @josephchika173

    Ай бұрын

    Lero akuti anali tsogoleri wabwino tooo bad