Chilima Simtsogoleri Wabwino - Bon Kalindo
On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo says, Vice President Saulos Chilima is not presidential Material. If he was he would have show solidarity with the poor Malawians who are suffering under Tonse Alliance.
Ku Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo akuti, Vice President Saulos Chilima is not Presidential Material. Akadakhala akadawonetsa mgwirizano ndi Amalawi osauka omwe akuvutika pansi pa Tonse Alliance.
Пікірлер: 82
booooon kalindo Mo fayaa. keep on to give us truly updates. inu mumalankhula chilungamo chokha chokha
Bon Kalindo you have gained a supporter!!!!
Honest speaking Mr DC Big up
Komatu a Kalindo munthu osamuipitsa choncho. Inu musamunene Chilima kuti oipa lero. Mwagwira naye ntchito limodzi. Kuipa kwa munthu amadziwa ndi Chauta basi. Inunso muli ndi zonyansa zanu.
@VincentNgabuhvincent
Ай бұрын
khala chete iwe
@HakeemJossam
Ай бұрын
aaaaah kuipa kwa munthu amakuziwa ndan? mxiew
Go ahead Mr kalindo we are following you
Bon he is talking the truth, but u can see other people they talking sheet, be very careful my fellow Malawian, we must wake up guys, zinazi sizotengela kupita ku school, khalani pansi moganiza bwino, malangizo awuleletu awa,all the way from johannesburg
@Littlefair7
Ай бұрын
Who spoke that spoke?
Mukunena zoona big, koma mmalawi opusa akuona ngati chilima ndiwabwino
Kalindo is matured now
man of integrate😂😂😂 Bonnnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri from Njeza village ..T/A mabuka, mulanje😊😊😊😊😊
Mr kalindo moto 🔥 🔥🔥
Kodi inu mumkamuuza chilima ngati ndani? Osachita naye msanje. Pangani zanu akulu
Zooona zokhazokha, Chilima wakhala duuuuu a Malawi tikulira, olo one day osalankhulapoyi mmene m"boma mukubedwera ndalamamu, nde atifune pano? Ine ndamitsikatu, he won't get my vote
Mbambande mr presdent bon kalindo kwathu kwa chulu zinthu sizilibwino tikukhalangati tili mkamwa mwa mikango
Chakwera ndi Chilima wooooyeeee,muwaphe A Malawi onse mukatha mutenge mitemboyo muitafune Mukhute,popeza ndalama mwawa bera Kale,koma muziwe masiku amatha ndikugona adaku voterani wokha samaziwa zoti Chibwenzi chankhwangwa chokoma pokwera, Amalawi mukaza voteranso awa izo ndi zanu wanthuwa ndi aka Nyimbi Anunkhisa Malawi.
Koma kumanidwa udindo kulira mpakana 4 years
Bwana Born Kalindo pqjatu ndinu amene munamukakamiza Chilima kuti avomere kukhala vice president lero mukumunyozaso . Komaso inuyo mumatiuza kuti sindinu wandale koma chosecho mukuwauzaso anthu kuti akqvotere aford , udf kqpenda dpp.
Apadi akunena zoona zaka zonse takhalayi chilima ali.duuuh nde angabwele kwa ife kutiwuza chani ??
Yes you are really talking
Zoyankhula za bon kalindo zatitopetsa tsopano, katakwe ndi bakili muluzi tv
@frankiechasokoneza5802
Ай бұрын
Zakutopetsa not zatitopetsa bwana
@SamuelChauluka
Ай бұрын
Ingosiyani osamamvela bas,,,,, za ziiii
Musamuipitsile mbiri a chilima inunso simulibwino.
Bwanji adzangotiimra bon kalindo yomweyo pa u president,akuoneka ali ndi nzeru kwabasi
Zoona amasankha tsogoleri ndi mulungu. Inu musaweluze
Ndipo nkhaniyi ndioona big up DC
Chilima sanalakwise kanthu, cholinga akawukira muzimunena kuti amangowukira kulikonse? Apa pokha nde ayi, boma ili tinalivotera chifukwa cha Chilima, nde atulukeko chifukwa? Mesa kuli mavoti ake, musiyeni Chilima akhale, nthawi ikakwana ayankhula
@grandwellkatumbi4763
Ай бұрын
Aziyankhula zichani Nanu Inu chilima wanuyo
Chisilu mbuzi 😢😢😢
Ndiye tivotele ndani utiuze kalindo manyi ako
Yes DC akunena zovona
Shaaaa this was days ago
Nkhanira yakwachulu yokha mwapala. Miyambe mwazimvetsa zinthu mmene zikuchitikora. Bwerani ndi ma demo anuwo tione ngati simuyaluka
Tabalirankon aku mwera usabwere ndi mademo Ako pano pakati chita kwanuko
Dzapangeni nawo compete bwanji because it seems mukudziwa zambiritu
Ndizoona zimene akuankhula karindo chifukwa nthawi yakampeni ndiiyeyo amene amanyamula thumba la 50 kg sichakwera iyayi
Impossible ngati munthu akugwira ntchito mmboma sangayankhulepo zotsutsa boma man limenelo nde bodxa
Ipondeni Fadala........ You're a real son of Malawi........
Akunena zoona kalindo
Kalindo ndiwamisala uyu
Kalindo to the people
Yaaa
Vchifukwa choti azakhala pa u president ndichifukwa achakwera amuphera..... Chifukwa chani mdziko mumalowa anthu osaziwika bwino
Bon kalindo ulemu wanu
DC ❤❤❤
Akutitenga ife uchitsilu pomwe achitsilu ndiyiwowo amalawi asukutsula ngati tinachotsa mbuyawo kamudzi chifukwa chankhadza chakwela nde ndanitso galu kwabasi
Zitsiru ndizomwe zingakhulupilire chilima opusa omwewa ndizomwe zikunamizika chilima zaupresdent alibe nazo ntchito koma iye azingodyelera mimba yakeyo
Chilima usogoleli mlibe ose ndi adyera same like chakwera 😅
Amakomadi akamwalira munthu sure
Uyu ndi wamisala chilima ndi otumidwa so sakadaima mkuyankhula mudakati ndi oukira
Kalindo akufuna atibalalise Ali ndi reason behind
Munthu amakondedwa anamwalira Pamalawi
iwe ndikumenya bwanji mulimbana ndi DC wanga
anatipwetekesa asabweleso
Ndizoona ndikugwilizana nazo
Aaaa chilima angoputsisa MCP tsingapase utsogole chifukwa chakwela akumva kukoma ndibanja lawo lotse nso dzoti chilima akudziwa chilungamo koma manyadzi uchitsilu mutayeni tiwone 2025 dzizatha bwa
Eh komatu akulu awa chilima anakulakwilani chani muja munayambila kumunenamuja mpakapano or kukuyankhani osangomusiya bwanji ndiwankulutu ameneuja amadziwa chimene akupanga nde zinazi ife mumatinyasanazo zomalimbana ndimunthu oti samakuyankhani
Uzitiuzanso za DPP ifeyo lero? Moti ukakhala umati aMalawi angamvere ndithu iweyo kkkk
Iwe sukuimirira a Malawi koma chipani china chomwe aliyense akuchidziwa. Ukulimbana ndi Chilima nthawi zonse bwanji? Kodi kwinako kulibe zofooka zawo. Usawaike a DPP ngati ndi Angelo lero. Sitinaiwale zomwe amachita padzana paja. Tikudziwa kuti mtunda wa kwanu ndi omweo. Usatinamize ife takana.
Chilungamo chimawawa,Koma DPP ayi ziko linaliko bwino mnthawi yimeneyo
Boma la Chakwera silizakhala labwino kwaiwe only if utakhala Minister. Unduna sapatsa zitsiru ngati iwe. Anthu a kwa Chulu akakuthibula bwera uzazione. Kulira 4 years kufuna udindo kkk😂😂😂😂
Chilima waonetsa kudekha ndipo sadaukire koma kalindo ndale zidakulani
@grandwellkatumbi4763
Ай бұрын
Dziko likamaonongeka mtsogoleri wabwino sadekha ....chilima akudekha zichani pamene zinthu zikufoila mdziko muno
Chilima ndi witch craft mbuzi mwana wajoka amati tizidya katatu madzi awulere magetsi awulere fetelizer wochipa. chilima ndifiti kwambili
Zoonadi zianthu zoipa kwambiri 😂😂😂😂😂😂😂
The problem with Kalindo is that he wants to be the master minder of Chilima. But he has to understand that Chilima has brains. My instincts also tells me that he is indirectly campaigning for DPP.
@user-se4cf9qp8b
Ай бұрын
This is true. Kalindo is 4 dpp
@EvanceSungani-cv9jk
Ай бұрын
In your minds but he talks vry true posatengera za ndale,,,,,and all of this akuya khula ndizoona,,,, nokha mukuziwa mene adalankhulila chilima mu campaign ya 2019 analankhula zambili mbili zokomera Ife achinyamata koma ndzt wakwanilitsapo,,,,,inuso musamangosutsa zilizonse you supposed to see the true
@Littlefair7
Ай бұрын
I fully agree with you, Kalindo is taking advantage of illiterate masses.
@GRACIOUSKENAN
Ай бұрын
Which brains dear, you talking about??? No he is bad man also,can he preform good speak today how??
Kalindo ngati ndi chamba uzavula galu iwe ukukhale wachilungamo ndiwe mulungu?? Ndiwe galu kwambiri usatibowe uziyankhulira amako ndi anthu akwanuko
@SamuelChauluka
Ай бұрын
u a big fool
Aka ndi kachilungamo
Kkkkkk
Zinthu zake
The DDCccccccccccc
Kkkkkkkkk
Izi ndi nkhani za amalawi ngakhale a president anayankha nkhani ya America mu chichewa, translate in English nonsense
It a better to dellete this video. You have cursed him
@josephchika173
Ай бұрын
Lero akuti anali tsogoleri wabwino tooo bad