Zomwe wayankhula Bon Kalindo lero pa 10 July atamupeza osalakwa pa Milandu yomwe amamuzenga

Пікірлер: 114

  • @InnocentHerrera
    @InnocentHerrera17 күн бұрын

    Concerned malawians let's gather here apule anu alakhula mbali yakuno

  • @duliaustin7179
    @duliaustin717917 күн бұрын

    Power to people malawi

  • @yuzzykamwendo3937
    @yuzzykamwendo393717 күн бұрын

    This guys, is a strong man, he hasn't any fear and all time he fights for Malawians.Lets fight hand on hand guys Dzikoli ndilathu ndithu tisaope.

  • @lualuaboyartist8868
    @lualuaboyartist886817 күн бұрын

    Kalindo I lv u I'm in studio now do your special song u de best fada 🔥🔥💪🔥💪🔥💪🔥💪💪💪

  • @Misiyusuf
    @Misiyusuf17 күн бұрын

    Proud to be Mangochi❤Welcome to Mangochi bon

  • @Legends.For.Life861
    @Legends.For.Life86117 күн бұрын

    Izo padela Koma Ife tungofuna Kuti utipelekeze Kwa sing'anga amene iwe unapita fukwa ameneyo ndikatundu ndisaname

  • @GreyJecky

    @GreyJecky

    17 күн бұрын

    😅😅😅😅

  • @user-ji2cu9xn7j
    @user-ji2cu9xn7j17 күн бұрын

    Kkk awa akuiputanso mlandi ina kķkk komabe akunena chilungamo sure inuyo soja WA mphawi mwatenga dzina la lucius

  • @NisharChirwa

    @NisharChirwa

    17 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

  • @elvisnjoka8428
    @elvisnjoka842817 күн бұрын

    Si zachilendo izi azanu a Mntambo ankatelonso tinakutulukani

  • @KimJime-d9k

    @KimJime-d9k

    17 күн бұрын

    Mtambo sanamangidweko sanamveko zowawa

  • @elvisnjoka8428

    @elvisnjoka8428

    17 күн бұрын

    @@KimJime-d9k kumangidwa ndikumeneko koma ndi anthu aja ongofuna zikawayendela basi kwinako ziiii

  • @OliviaFour-rk9ir
    @OliviaFour-rk9ir17 күн бұрын

    Umakwana ukufunka kuno kalindo uzachangamuse Ntcheu ❤

  • @Machemba-b7s
    @Machemba-b7s16 күн бұрын

    Born kalindo is my eff

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi871317 күн бұрын

    Adzafera mbendera iyi kuti? Sakugina mizimu ikumusaka.. ndndende Macbeth

  • @THE_BLESSED_SON
    @THE_BLESSED_SON17 күн бұрын

    Hahaha Kodi muputanso ina bigy milandu 😂😂😂

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk17 күн бұрын

    That's our beloved president, president for the poor always guided and protected by the living God, long live our president, we poor citizens loves you more, the Dddddd Cccccc!!!!, the senior pangolin 🔥🔥🔥🔥

  • @KimJime-d9k

    @KimJime-d9k

    17 күн бұрын

    Zoonadi ine ndi mboni kundende kuli anthu osalakwa

  • @williamdyton7498
    @williamdyton749817 күн бұрын

    Theeee DC iweyo ndi one zomwe umanena zimachitika🇲🇼✊

  • @MaryMary-dz2th
    @MaryMary-dz2th17 күн бұрын

    Akuti mademo tsopano tizipanga bwino....The DC ✊

  • @UmarMasame
    @UmarMasame17 күн бұрын

    Booooooon kalindo the comred💥💥💥🇲🇼🇲🇼🇲🇼

  • @BichahpostKasambala
    @BichahpostKasambala16 күн бұрын

    Booooooniiiiiiiiiii kaliiiiiindooooooo! Katundu osamangia unyolo koma chulungamo 😅😅😅

  • @OWENROBERTS-hf7xd
    @OWENROBERTS-hf7xd17 күн бұрын

    Salute my homie 🔥

  • @user-qy9xf4rw4e
    @user-qy9xf4rw4e17 күн бұрын

    Kkkkkkkkkkkkk koma amalume😅😅😅😅😅😅

  • @NichorusKaimira

    @NichorusKaimira

    17 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂🙌

  • @blessingschiwaya-zn8is
    @blessingschiwaya-zn8is16 күн бұрын

    Koma Kalindooo

  • @rodricklanjesi2430
    @rodricklanjesi243016 күн бұрын

    Ma background music wo akuononga zinthu fix that guys ... almost ma videos Anu got the same prob

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface428217 күн бұрын

    Live from south Africa cape town

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r17 күн бұрын

    Bon Kalindo The DC ofunika azikhala ku State House ndipo tikamuthamangitse Satana Ali kumenekoyo

  • @ChipiliroLungu
    @ChipiliroLungu17 күн бұрын

    Vuto umaphatikiza za zelu ndi zofoila zomwe nde makhala kaye ndi zofoila zakozo

  • @amonprincegenamu7203
    @amonprincegenamu720317 күн бұрын

    Booooonnn Kalindoooooo 🔥

  • @christopherpetro-pen3678
    @christopherpetro-pen367817 күн бұрын

    Apolice onse aja? Amabwelela ineyoooo🤪🤪🤪 akut pozamutenga Bon kalindo pazikhala kasinja

  • @TitusShumba
    @TitusShumba17 күн бұрын

    Kalindoooo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @pemphoashani4619
    @pemphoashani461917 күн бұрын

    Komano Kodi anthu osawukawo mukumawauza kuti azipangako chani kuti mu umphawimo adzachokemo. Chifukwatu kulimbana ndi BOMA sizingasinthe status ya osawukawo koma zitha kusintha status yanu. Mukalimbana nalo BOMA chonde tilimbikitseniso kuchita ma business chifukwa chete chete sautsa nyama

  • @Boystarpluss

    @Boystarpluss

    17 күн бұрын

    Men ma business wo mupangira kutiko?dZiko silikuyenda bhoo amayenera kumadzuzula kut amalawi wo azikhala pabwino...ngongole Zama business mutenga kut?Amati mukonze chapansi kut chapamwamba chikhale bhoo...

  • @GilbertKuchipinda
    @GilbertKuchipinda17 күн бұрын

    Pa ma china pokhapo nde wabayatu driver, operator gad zose zikugwilidwa ndi ma china lebala wawo ndi bwana wa anthu aku malawi.

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor364617 күн бұрын

    Inuyo ndi 1. More 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @johnussenu2848
    @johnussenu284817 күн бұрын

    You are welcome in mangochi bon kalindo

  • @samuelazumah1050
    @samuelazumah105017 күн бұрын

    Munyengo ya ku ng'alula

  • @TrizerDoller
    @TrizerDoller17 күн бұрын

    Number one kalindo

  • @innocentsathasteven4093
    @innocentsathasteven409317 күн бұрын

    Iwe ndi nyooo ndikukudziwa bwino bwino

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m15 күн бұрын

    Oipayo alephera yekha

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope17 күн бұрын

    Ngati Satan simumuziwa melowere ku state house Satan amakhala kumeneko pamodzi ndi Angelo ake azikhale ng'oma ,,kunkuyu ,,,mkaka ,,Monica,,chityola ,,nick amenewa nde Angelo asatana

  • @UTHMAN-WAYA
    @UTHMAN-WAYA17 күн бұрын

    T/A MABUKA 😂🔥 AND THE LAST MAN STANDING ✊🌹

  • @StanleyChirwa-d6b
    @StanleyChirwa-d6b17 күн бұрын

    Chi booooniiiiii kalindo 🤣🤣

  • @KENETHMAJASA-ud5ee
    @KENETHMAJASA-ud5ee17 күн бұрын

    Kutchaya kugwetsa, shatapuuu!

  • @AuspiciousKalambula-hp7gj
    @AuspiciousKalambula-hp7gj16 күн бұрын

    Ati ine ndiye ndi "kusendendani" uyuyu sakuwopa eeesh 😂

  • @JonesMalingaMalinga-nr6jc
    @JonesMalingaMalinga-nr6jc17 күн бұрын

    Uyuyu mmmmm koma yeah

  • @SamsonMedson-oz7rq
    @SamsonMedson-oz7rq16 күн бұрын

    Cd2d❤

  • @christopherpetro-pen3678
    @christopherpetro-pen367817 күн бұрын

    Akut koma chino sichimakpa kumangidwa😜🤪🤪🤪 ochatsika siyani kuononga ndalama zathu pa nkuluyu mungoziyipisila mbili

  • @christopherpetro-pen3678

    @christopherpetro-pen3678

    17 күн бұрын

    Sichimaopa

  • @AustinBanda-wg5pw
    @AustinBanda-wg5pw17 күн бұрын

    Bon Kalindo the DC

  • @LzkayLzkay
    @LzkayLzkay17 күн бұрын

    Ife timakukonda bon Kalindo

  • @moyo77777
    @moyo7777716 күн бұрын

    Boma lopusa

  • @JonathanChimwaza
    @JonathanChimwaza16 күн бұрын

    Chilungamo sichimabisika

  • @AnabandaMasauli-rk3lg
    @AnabandaMasauli-rk3lg17 күн бұрын

    Ndalama zolipira Lawyer ndilibe ine

  • @MadalitsoJackson-ns3vu
    @MadalitsoJackson-ns3vu17 күн бұрын

    Uyuuuuuu ase ati chiboni kalindo😂😂😂😂

  • @RichardJackson-p9z
    @RichardJackson-p9z17 күн бұрын

    Zaphavu zmenez

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x17 күн бұрын

    Uyu ndi woopsaaa kwambiri ‼️🤣😂

  • @Ntchindinkhwazi
    @Ntchindinkhwazi17 күн бұрын

    Eeeeh !!! Uyuyu anatopa

  • @ozziehenderson9977
    @ozziehenderson997717 күн бұрын

    Akut atamangidwe ndamako😂😂😂

  • @FestonJuwawo-dn4lp
    @FestonJuwawo-dn4lp17 күн бұрын

    Uyuyu ndi makina😃😆😃😆😃😆

  • @VeroNica-tp5vp
    @VeroNica-tp5vp17 күн бұрын

    Eeeh kom ichi

  • @user-xg5dg7jj4d
    @user-xg5dg7jj4d17 күн бұрын

    UTM president

  • @kennedyfaraimulilo4074
    @kennedyfaraimulilo407417 күн бұрын

    Ine ndine nyooo,too much drama.

  • @PeterNamphwanya
    @PeterNamphwanya17 күн бұрын

    Chibooooon kalindooo

  • @AlickSquare
    @AlickSquare17 күн бұрын

    Koma boma muthu uyu kungomusiya basi sidzoona paka apolisi 200 kuononga misomkho ya anthu

  • @georgefungulan6648
    @georgefungulan664816 күн бұрын

    Joab tachezaniko ndi bodyguard wa kalindo bwa?

  • @ShalomShine
    @ShalomShine17 күн бұрын

    Kasunja woyeeeeeee!!!!!!

  • @awaliwilliam6472
    @awaliwilliam647217 күн бұрын

    Makosana nanu mwati mudyele ma views pa speech ya nzanu nanu yakhulan yanu mupange post bas Khan ya straight

  • @Yamikie-yamikie

    @Yamikie-yamikie

    17 күн бұрын

    😂😂😂

  • @euccotechs1744
    @euccotechs174417 күн бұрын

    Umakwana bale

  • @PempheroKachande
    @PempheroKachande17 күн бұрын

    Koma yh ,,,ichi nde Kaya😂💔🤣🤣😳

  • @marychavula698
    @marychavula69817 күн бұрын

    Inu ndi one😂

  • @Yamikie-yamikie
    @Yamikie-yamikie17 күн бұрын

    Ka instrumental kabpansiko kaksomoneza olo mukatsitse kwambiri😅

  • @user-qc1yv3zk7i
    @user-qc1yv3zk7i17 күн бұрын

    Dc nkatundu uyuuuu

  • @Humphrey265
    @Humphrey26516 күн бұрын

    😂😂😂Kalindo

  • @Fahadimalopa
    @Fahadimalopa17 күн бұрын

    this is born kalindo 😂😂😂🎉

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x17 күн бұрын

    Inu makosana stop kuika ma instrumental si nyimbo izi mixieew tonse ndi oimba?

  • @user-jr6fe2gi4b
    @user-jr6fe2gi4b16 күн бұрын

    Musatitopese

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o17 күн бұрын

    The DC mumakwana inyo

  • @AffectionateAtom-rk2kn
    @AffectionateAtom-rk2kn17 күн бұрын

    Komchi

  • @ChimwemweFredrick
    @ChimwemweFredrick17 күн бұрын

    Kom ichiii inu 😂😂😂

  • @Praise-u8f
    @Praise-u8f17 күн бұрын

    W

  • @Patgregorymanyumba
    @Patgregorymanyumba17 күн бұрын

    Kkkkkk yeah

  • @AaronMaganga-rj1pp
    @AaronMaganga-rj1pp17 күн бұрын

    Koma ichi 😂😂😂😂😂

  • @yusufdaud9663
    @yusufdaud966317 күн бұрын

    Koma ichichi eeeeh 🙌😂

  • @user-ch1jf9zk6g
    @user-ch1jf9zk6g17 күн бұрын

    Kma. Ichi🤣🤣

  • @BeautyYona-vc7jp
    @BeautyYona-vc7jp17 күн бұрын

    The DC

  • @ZiporahThiezy
    @ZiporahThiezy17 күн бұрын

    Koma ziliko 😹😹🏃

  • @lindamankhanamba7580
    @lindamankhanamba758017 күн бұрын

    Kuli zinthu ku 🇲🇼😂😂😂😂💔

  • @TamandaniGawan
    @TamandaniGawan17 күн бұрын

    kuyaka

  • @ThokiezMw
    @ThokiezMw17 күн бұрын

    Koma akulu awa

  • @Post44SunSet
    @Post44SunSet17 күн бұрын

    🫡🫡🫡🫡🫡🫡🫡🫡

  • @captainsisitomalawi1548
    @captainsisitomalawi154817 күн бұрын

    Chatokotatu ichochi ndichooopsa🤣🤣🤣

  • @ShadreckMtepuka-sj8ue
    @ShadreckMtepuka-sj8ue17 күн бұрын

    Komatu nde watokotatu

  • @user-hq5wh3pn5b
    @user-hq5wh3pn5b17 күн бұрын

    Kkkkk koma the DC

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e17 күн бұрын

    Zowonadi tikudikira za ifa zimene zija.

  • @TimothyJobe-jc1ti
    @TimothyJobe-jc1ti17 күн бұрын

    Akuti pa mdipiti okamutenga kalindo mudziikaposo kasinja😂😂😂

  • @CathyKatsokamalanda

    @CathyKatsokamalanda

    17 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h17 күн бұрын

    🤣🤣🤣🤣🤣kasinja

  • @Simayil-qx6gj
    @Simayil-qx6gj17 күн бұрын

    Wayita m,bale

  • @kha6068
    @kha606817 күн бұрын

    What's with the useless background songs ?

  • @uzacarolinakaime772
    @uzacarolinakaime77217 күн бұрын

    Inde Nyo!!!!... lol

  • @user-zp1jh9xn3d
    @user-zp1jh9xn3d17 күн бұрын

    😂😂😂😂

  • @bmbboymstyles5894
    @bmbboymstyles589417 күн бұрын

    Chiphe😆😆😆

  • @user-eh1gn1nj9d
    @user-eh1gn1nj9d17 күн бұрын

    A Kalindo mukuimira ndani bwenzi mutapita kwanu ku Mulanje muzikapanga campaign muzaimire DPP yomwe ija muzapeze chochita panopa sizikuthandizani izi muzafa osauka ndithu

  • @user-ji2cu9xn7j
    @user-ji2cu9xn7j17 күн бұрын

    Boooooooooooooooooon kalindo

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatundulo17 күн бұрын

    Kkkk

  • @MynessChirwa
    @MynessChirwa17 күн бұрын

    😂😂

Келесі