Zomwe Apanga A UTM Kuchoka Ku Tonse Alliance Zandisangalatsa - Manza Wa Kwa Chinsapo

On Nyasa VoiceBox, a Malawian named Manze from Chisanpo in Lilongwe shares his thoughts on UTM's decision to exit from the Tonse Alliance.
Pa Nyasa Voicebox, M'Malawi wina dzina lake Manze wa ku Chisanpo ku Lilongwe akufotokoza maganizo ake pa ganizo la UTM lotuluka mu Tonse Alliance.

Пікірлер: 20

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e26 күн бұрын

    Kumuikapo manganya chifukwa manganya ndiyemwe anapeteka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ndimkona anamuika pampando at avice president akunama manganya wangoona kutenga sambi chabe

  • @Hamzamabvuto
    @Hamzamabvuto26 күн бұрын

    I'm the first person to comment here I love UTM but I'm not the member of UTM

  • @MerryWayson
    @MerryWayson26 күн бұрын

    Achita bwino kuthesa ❤❤

  • @JairoseManuel-p5p
    @JairoseManuel-p5p26 күн бұрын

    Sanalakwise kuchoka

  • @SHEREEFKanthochi-ft3dm
    @SHEREEFKanthochi-ft3dm26 күн бұрын

    inenso ndikunva kukoma zedi

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc26 күн бұрын

    Nice one thanks U.T.M MORE

  • @susantembo2076
    @susantembo207626 күн бұрын

    UTM please forge ahead. Don’t listen to any other distractive noises

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati316626 күн бұрын

    Mumakwana inuyo more fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @raffickaffick
    @raffickaffick26 күн бұрын

    Bravo fada

  • @AugustineTheu-of6nv
    @AugustineTheu-of6nv25 күн бұрын

    Zikomo kwambiri nkulu wanga kwa mawu ako ogwira mtima. Inenso m'bale ndikanakhala mwana wa chilima mbuzi imene ija Chakwera ndikanamuthamangitsa pa maliro kuti asowepo. Amene uja si president ayi

  • @VeronicaChirwa-ct4os
    @VeronicaChirwa-ct4os25 күн бұрын

    Manze ndagwirizana nawe kwambiri pa zomwe wanenazi. Inenso Chilima akanakhala m'mbale wanga sindikanalora kuti abwere pa maliro a Chilima. Ndipo ndikanachita zoti amalawi sanaziwonepo. Kaya ndikufa nanenso ndikanafera pompo. Chakwera ndi munthu oyipa kwambiri.

  • @stevenfrancism3638
    @stevenfrancism363826 күн бұрын

    ❤❤❤❤❤❤

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati316625 күн бұрын

    Ineyo ndinakakhala m'bale wanga ndinakati Maliro sikuika tiyeni tikamutulire chakwera akadye sured pakanavuta komanso sinakalora wina aliyense wachipani cha MCP kupedzeke pa Maliro ndithu kunakachema

  • @Felista-m4q
    @Felista-m4q25 күн бұрын

    Inenso ndanyadira kwambiri

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa25 күн бұрын

    Mwalakhula fundo zabwino big chakwela ndi galu yambuzi fiti

  • @MacleanKwacha
    @MacleanKwacha25 күн бұрын

    Ndipo ine ndizafunisisa anthu amenewa asazaikidwe,tizadyere nsima

  • @user-ui4ux5kc8d
    @user-ui4ux5kc8d25 күн бұрын

    Ngakhale kufa kwake kwachakwera anthu tidzavina kusangalala ndipo kaya imfa imeneyi kwaiyeyu ikuchedwa patii munthu oipa uyuu akanafa koma ndithu ambuye timenyereni mkhondo afee ndithu presedent ameneyi

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e26 күн бұрын

    Kuga mwacakwera anthu tidzakondwa komanso kuvina kuti chokupha chija chafa

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire876925 күн бұрын

    Tiyeni tizavotele UTM. Kuti mzimu wachilima uzause mu mtendele

  • @user-qp8kh2hj9o

    @user-qp8kh2hj9o

    25 күн бұрын

    Ndipo izi ndizoona satana achite manyazi