Zomwe Apanga A UTM Kuchoka Ku Tonse Alliance Zandisangalatsa - Manza Wa Kwa Chinsapo
On Nyasa VoiceBox, a Malawian named Manze from Chisanpo in Lilongwe shares his thoughts on UTM's decision to exit from the Tonse Alliance.
Pa Nyasa Voicebox, M'Malawi wina dzina lake Manze wa ku Chisanpo ku Lilongwe akufotokoza maganizo ake pa ganizo la UTM lotuluka mu Tonse Alliance.
Пікірлер: 20
Kumuikapo manganya chifukwa manganya ndiyemwe anapeteka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ndimkona anamuika pampando at avice president akunama manganya wangoona kutenga sambi chabe
I'm the first person to comment here I love UTM but I'm not the member of UTM
Achita bwino kuthesa ❤❤
Sanalakwise kuchoka
inenso ndikunva kukoma zedi
Nice one thanks U.T.M MORE
UTM please forge ahead. Don’t listen to any other distractive noises
Mumakwana inuyo more fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Bravo fada
Zikomo kwambiri nkulu wanga kwa mawu ako ogwira mtima. Inenso m'bale ndikanakhala mwana wa chilima mbuzi imene ija Chakwera ndikanamuthamangitsa pa maliro kuti asowepo. Amene uja si president ayi
Manze ndagwirizana nawe kwambiri pa zomwe wanenazi. Inenso Chilima akanakhala m'mbale wanga sindikanalora kuti abwere pa maliro a Chilima. Ndipo ndikanachita zoti amalawi sanaziwonepo. Kaya ndikufa nanenso ndikanafera pompo. Chakwera ndi munthu oyipa kwambiri.
❤❤❤❤❤❤
Ineyo ndinakakhala m'bale wanga ndinakati Maliro sikuika tiyeni tikamutulire chakwera akadye sured pakanavuta komanso sinakalora wina aliyense wachipani cha MCP kupedzeke pa Maliro ndithu kunakachema
Inenso ndanyadira kwambiri
Mwalakhula fundo zabwino big chakwela ndi galu yambuzi fiti
Ndipo ine ndizafunisisa anthu amenewa asazaikidwe,tizadyere nsima
Ngakhale kufa kwake kwachakwera anthu tidzavina kusangalala ndipo kaya imfa imeneyi kwaiyeyu ikuchedwa patii munthu oipa uyuu akanafa koma ndithu ambuye timenyereni mkhondo afee ndithu presedent ameneyi
Kuga mwacakwera anthu tidzakondwa komanso kuvina kuti chokupha chija chafa
Tiyeni tizavotele UTM. Kuti mzimu wachilima uzause mu mtendele
@user-qp8kh2hj9o
25 күн бұрын
Ndipo izi ndizoona satana achite manyazi