UTM ikupanga gwilizano ndi DPP. Kodi Chakwera ava bwanji??
Жүктеу.....
Пікірлер: 584
@LukaAron-el5qh23 күн бұрын
Mai mawu anu ndi amphamvu ambuye awadalitse
@LysonMtalika-tb6fk23 күн бұрын
Very true Madam, we need to have strong party for alliance
@user-qq1uj7ct6n23 күн бұрын
Zipani zonsenzi zili pansi pa DPP. so lingaliro labwino kubwerera Ku DPP watching from Cape Town
@EmmyYafete23 күн бұрын
Very true mandam ,ndazikonda kwambili bwerelani kwa amai anu basi tingwetse MCP ,
@Namphuno22 күн бұрын
You have proven to have big brains than other men in UTM, you have our support
@paulkalizangoma590423 күн бұрын
This is what Malawians were waiting to hear from you. You made a right decision. Thumbs up to you all. We are fully supporting you, and we shall be behind you forever.
@EnetChiomba22 күн бұрын
Eishii koma apapa zikhala bwino bwanji ndipo zitero ndithu❤❤
@augustMag23 күн бұрын
Mau amphamvu Mai atigwira mtima Bambo wanu APM akulandilani ndi manja awiri sangalore kuti ana Ake asowe kopita iye qlipo
@LubaniLameckmbewe23 күн бұрын
I totally agree with you
@MarcosDjussa13 күн бұрын
Komatu amai awa alankhula zomanga Malawi wasopano God bless you mama
@EnriquedakazifoxZifox20 күн бұрын
Powerful massage madam and am looking forward for the mgwirizano that is coming viva 🇲🇼 🇲🇼 🇲🇼 viva DPP,,,, watching 👀 from Lusaka
Thenks utm popangangwilizano ndi dpp atiphera saulosi achoke fayaa
@SteveChapola
23 күн бұрын
Mai kaliyati libikisani anthu ife sitifuna mcp
@FocusMathews20 күн бұрын
Good watching from Joburg
@user-te4ii6sz2v19 күн бұрын
This is practical and very positive politics. Let's follow this path. I never new that in UTM there are some pipo who think like this. There is so much unnecessary noise which pipo think is politics but nope. God bless you.
@sarahnachu91418 күн бұрын
Very amazing let's unit ❤ watching from Cape Town
@VailetnyirendaShamah23 күн бұрын
Ichoke mcp please dpp my vote
@user-fi7ko7bl6f22 күн бұрын
That's good idea Ma, l salute you 💪💪 power to the people.
@BentryMwagomba23 күн бұрын
Thanks madam for the advice
@AlinafePililani23 күн бұрын
❤❤❤❤ that's beautiful idea Mai kariat
@user-vh9uk1jy7w23 күн бұрын
We're with you madam
@WilliamNhlane-fd9hi23 күн бұрын
Well spoken madam boss 🙏🙏🙏
@NumbDee22 күн бұрын
Patricia kaliat ndi makina paokha welcome back mom ur loved
@dankopland-dp3vx23 күн бұрын
UTM ngati ikufuna kuti omwe apha Chilima adzalipire akuyenera kupanga mgwirizano ndi chipani cha DPP kuti achotse MCP ndikufukula imfa ya Chakwera poyera koma ngati satero nkovuta DPP kudzagwira ntchitoyi pamene UTM imawanyoza pa kampeni
@bysongeorge324323 күн бұрын
Chomwe wamanga Mulungu wina sangachiphwasule. M'gwilizano wa Shadow wina uliwonse omwe cholinga chake ndikugwetsa MCP, ndiri nanu pambuyo....
@robinbinali843123 күн бұрын
Bravo!!! UTM welcome to DPP
@user-pv9uk6sc3w23 күн бұрын
100% mai, UTM, DPP ndi AFORD gwirizanani mugwetse MCP ndi chakwera atitopetsa, mai wa nzeru kobasi.
@marthansaliwa773223 күн бұрын
Mphechepeche mwa njobvu sapitamo kawiri. UTM iyime paokha ili ndi tsogolo kungatalike. Sitikufuna kubwereza zomwe zachitika ku MCP.
@RoyKambalame
23 күн бұрын
Ndipo zoona osabwereraso mmbuyo Maso patsogolo
@CharityMhone-uk9ym
23 күн бұрын
Koma kuima pa nonkha simungatenge boma never popanda kuphatikizana ndi chipan champhamvu 😮
@user-tk6wf2eg4z
23 күн бұрын
Imani nokha tione dpp nde ndiyamoto ndikale
@HappyKanyangala-oq1kk23 күн бұрын
Ndinu mburi zedi mulipachangu koma choononga komaso kachipani kanu kakuntha nanga ku d p p mulibepo Udani a a a si wa UTM iwe ukufuna kuononga mpunga WA UTM
@PetrusTlhokwane
23 күн бұрын
Samamva asiye adzaziona ayiwala zimene adamupangira mademo APM azabwezera zonse zija mmmn they have to learn through mistake with tose alayasi km UTM bwanji mwayamba kuti gwesa phwayi
We have to join together gentlemen and ladies indeed
@ConfusedCupcakes-ke8ql17 күн бұрын
That is point UTM ikuyenera kupanga mgwirizano DPP
@LoveHere-ki8ck23 күн бұрын
I salute you mama , good decision more 🔥🔥🔥🔥🔥
@doreenkaliati316622 күн бұрын
Mcp ikuchoka mudzina La Yehova usogoleli umene Mulungu sakondwera umene Mulungu sakondwera nawo amaugwetsa or patavuta bwanji
@JuliusAndrea-iq6xc12 күн бұрын
I totally agree with you Madam
@PetrusTlhokwane23 күн бұрын
Koma a mayi inu mutizuza kwambiri ndipo you have to learn through mistake muyambilaso tose alayasi tatopa ndi kuliratu ife Chaka chino Chigoliyati chinalephela khondo kwa David nde inu bwanji a UTM km DPP yanuyo 2020 munayipangila mademo nde mwayiwala km mukazi wa Loti adayang'ana m'mbuyo ndikusanduka chulu
@ulemukhumalo783523 күн бұрын
Osamakakamiza aliyense ali ndi ufulu ndi chisakho chake pokavota. Panopo kuigwetsa MCP nkovuta aaaa nde gwirizanowo ndi dpp?? Mayi mukunama inu kuyakhula konseko ndi mpando musatinamizepo apa.
@user-uc1pd1tc2x23 күн бұрын
Chilima akanati sanapange alliance ndi MCP ndibwenzi Chilima alipo zedi
@AbrahamTembo-z5k23 күн бұрын
Inenso ndine wa pa kanthawi ndithu MCP ndayiwona ndipo ndimaidziwa. Kungoti zangovuta kt zipani zinazi ndizazing'ono nchifukwa chake people will be FORCED to make an aliance with DPP. Koma tikawunika BWINOBWINO, DPP ndi MCP palibe kusiyana. Njauju mkulu wa ACB dafa ngati simunthu mpaka pano milandu idangozizira. UTM tsaopano payokha itha/ ndi AFORD, zitha kuchita bwino ndithu chifukwa imfa ya SKC idachita CAMPAIGN YAMPHAMVU. Makamaka ku chigawo cha ku mpoto. Kubwelera ku DPP itakhala LAST OPTION, yes mwachonchi mowawidwa mtima. Mayi ndakumvani BWINO ndithu, ndipo sindikukutsutsani kwambiri, koma DPP, ikhale last option.
@user-vf2fo1mb2c23 күн бұрын
May God please bless Malawians, Congrats from SA😂❤🎉
@MphatsoKhwengweya13 күн бұрын
I support that statement MCP should feaz out
@KondwaniBanda-j9x23 күн бұрын
Komanso chilimatu akanapanda kuchoka ku DPP bwenzii Ali president wathu moto kupita ku DPP palibe vuto
@OwenWalter-nz7uo23 күн бұрын
Omwe akusunga udaniwo tawafunsani kuti kodi wina watichosera chiyembekezo chathuyu ndi awa omwe tinasiyana nawo mwamtenderewa kwabwino kulowera nkuti? Coz pakakhala kugawanikana kwazipani MCP sichokadi u are right
@MussaHassani-zg1hm22 күн бұрын
Thanks Mai anthu mwayankhula bwino kwambiri thanks so much for ur spish
Ndipo akapanda kutuluka tiwatulutse ndiifeyo UTM,DPP, AFORD combine with UDF mcp will be defeated mai iminoyo ndi amzeru kwambiri
@WillamLawson-gk1lw23 күн бұрын
Very true mai
@user-mw8dq4is6k23 күн бұрын
Thats good idea Mai mwaganiza bho Chakwera must go .. Alliance ya Dpp, UDF, UTM ndi Afford ilii mwala Pangan zotheka bas.
@samdiverson973323 күн бұрын
Mayi mwalankhula bwino chilima was a child of apm there is no problem to go back to DPP
@allanimindozo993723 күн бұрын
Watching from Johannesburg it's good to join DPP
@user-gs7wc3nx3q23 күн бұрын
Eya mama joinani basi pangani zomwezobasi tibwerere ku dpp basi
@user-rs7vx6hc1k23 күн бұрын
Vuto lake limakhala limeneli, timakhala desperate kufuna kuchotsa chipani cholamula ndiye mapeto ake timangopanga ma plan osayang'ana kumbuyo kapena kuti kutsogoloku ziziyenda bwanji.
@user-iq5xk6ju7y23 күн бұрын
Paja DPP ndi kuchimake kwa Propaganda😂😂 Pepani a DPP the only new Malawi that as a nation we all expect is the coalition of UTM and AFORD period. We all all seek New parties in new Malawi to come. The MCP that Malawians have experienced this time NO majority can make such mistake to vote MCP again.
@user-gd6zb2bv8f20 күн бұрын
Siyani ma udani , mangani chimodzi ngati a Malawi, MCP ichoke ndipo isazapezekenso ku Malawi. Watching from JOHANNESBURG
@user-wx1jt5fd2j21 күн бұрын
Mwaganiza mokhwima maganizo abale athu a utm kupanga mgwilizano ndi DPP komanso tili ndichikhulupiliro kuti zipani mwanenazo mosogozedwa ndi Ambuye komanso anthu kulilira dziko lamalawi pamene lafikapa liphulidwe pa moto osatira azipanizo sionse angakondwere koma ambuye achite kufuna kwake pempho a DPP zichepeseninso pa anzanuwo kondanani samaliranani khululukirananipangani umodzi ochokera pansi pa mtima may God bless you
@user-te3ps3kf2t23 күн бұрын
Yes l gree with you Mai,koma ngati simungamve magnanimous a Maiyi ndiye kuti mulibe magnanimous ofuna kutumikila a Malawi koma kukhutisa mamba zanu osati kuombola aMalawi ku Bagamoyo,please paganism chtheka kugwilana manja kuombola Malawi ku mng"anjo ya moto,machine ngati achitila kuno ku south Africa kupanga boma la Malawi colution Government, osakonda anthu awo mwasiye choncho
@user-bq5ev7de1l21 күн бұрын
Kuyankhula kwabwino mai kumeneko ✊✊
@PeterNgombe-l6l23 күн бұрын
UTM, Aford, UDF and DPP maganizo abwino
@harrisbanda589122 күн бұрын
Mai MULUNGU azikudalisani chifukwa chamawu anu amphamvu ndachilimbikiso, tiyeni tigwirane manja kuti tichotse ng'onazi m"dziko muno
@miketholiwa176221 күн бұрын
Brilliant idea. Ichoke MCP
@user-fp6kh7gx9q23 күн бұрын
Good idea
@JosphineJoshua-gq1rp22 күн бұрын
Mau mau mau pachingelezi timazati so shall it be in Jesus name
Пікірлер: 584
Mai mawu anu ndi amphamvu ambuye awadalitse
Very true Madam, we need to have strong party for alliance
Zipani zonsenzi zili pansi pa DPP. so lingaliro labwino kubwerera Ku DPP watching from Cape Town
Very true mandam ,ndazikonda kwambili bwerelani kwa amai anu basi tingwetse MCP ,
You have proven to have big brains than other men in UTM, you have our support
This is what Malawians were waiting to hear from you. You made a right decision. Thumbs up to you all. We are fully supporting you, and we shall be behind you forever.
Eishii koma apapa zikhala bwino bwanji ndipo zitero ndithu❤❤
Mau amphamvu Mai atigwira mtima Bambo wanu APM akulandilani ndi manja awiri sangalore kuti ana Ake asowe kopita iye qlipo
I totally agree with you
Komatu amai awa alankhula zomanga Malawi wasopano God bless you mama
Powerful massage madam and am looking forward for the mgwirizano that is coming viva 🇲🇼 🇲🇼 🇲🇼 viva DPP,,,, watching 👀 from Lusaka
Mau ogwila mtima kwambili 💙💙💙🔥🔥🔥
Mayi uyuyu amaganiza mwachungu ngati mwamuna 🎉❤❤❤❤❤❤❤
Mai mwayankhula za nzeru koopsya ndipo iiiiih sindikutha kukumvesesani kuti nzeru zinenezi bwanji inuyo
Good decision sitikufuna njara ku Malawi
Powerful message mama
You is best futures ❤❤ 100% that's one plan A not B ❤❤❤❤❤❤❤🎉
Good advice ,join together to remove the devil.plz.
Wake uppp UTM family, that's right decision madamm, let's forget about the past!!!
I totally agree with you madam ,,UTM must go back to its father house
Zoonadi ma tigwirizane NDI DPP,ATM,AFORD+UDF ......moto buuuuu
@JackMvura-ik2td
22 күн бұрын
Ikugwetsani MCP sizamwana😂😂😂😂😂😂😂 chakwera motoooo komaso chakwera kuwina DPP yonse tidzaponyanso Yamanja alomwe kwao sitikuyesa
@wisdomchilanga723
20 күн бұрын
Dpp, UTM,Alford, and UDF chonde phalani ziko pamoto tikudalira inu
@JackMvura-ik2td
20 күн бұрын
@@ivychithyoka1551 chakwera akupha Goliath ndi mwala umodzi 2025 gwirani yesu Adani muwaponde bwino achakwera ndikuthandizani kuponda achepa
Mai inuyo very true watching from LESOTHO ndipo ndi Mulungu amene wakunong'onezani kuti muyankhule mau amenewo
That's true Comrade there is no permanent political enemy in politics
UTM ndi DPP palibe udani if anything UTM yabadwa kuchokera ku DPP. Peter is cool ndiyemwe anamukonda SKC kuti ayambe ndale.
@isaihmagani5697
23 күн бұрын
Chabwino ndakumvani nde tinene kuti UTM itsogole ngatidi Pali kumvanadi
If we want tizivutikabe let's VOTE for MCP
Mau mau,udani wampaka muyaya mundale mulibe Tiyeni kwaADad bola Ng'onazi tizitulutse 🔥🔥
@actuarialscience2283
20 күн бұрын
MCP ndidzaida mpaka muyaya.
That's good Idea madam
Muli power speach inuyo mama🙏🙏💯💪
Powerful mama mwaganiza kuposa mwamuna ndakukondani🎉
Chakwera sakupuma bwino. Madam mumaganiza mokuya I agree and let's vote dpp utm afford udf, tigwilane manja.
Very Bravest speech Sister I salute you
Tiyeni tigwilizane ndi DPP, UDF plus Aford kungotero tagwesa
@bysongeorge3243
23 күн бұрын
@@masterchitabwino898 ndipo chomwe chizachitike ndi zija amati 'Landslide victory', m'gwilizano omwe ungachepetsenso za kugawana mitundu. Nkhani yomwe akamba Mai wo. Atsogoleri omwe akukhuzidwa asakulirane mitima, agwilizane, azichepetse atiphule a Malawi mu nyengo yowawa ngati imeneyi..eesh!!!
@user-xm3zl5cg6x
23 күн бұрын
Kwambili UTM mulungu akudalisen Ife tikufuna Malawi wa rendere osati Opana UTM thenks
@SteveChapola
23 күн бұрын
Thenks utm popangangwilizano ndi dpp atiphera saulosi achoke fayaa
@SteveChapola
23 күн бұрын
Mai kaliyati libikisani anthu ife sitifuna mcp
Good watching from Joburg
This is practical and very positive politics. Let's follow this path. I never new that in UTM there are some pipo who think like this. There is so much unnecessary noise which pipo think is politics but nope. God bless you.
Very amazing let's unit ❤ watching from Cape Town
Ichoke mcp please dpp my vote
That's good idea Ma, l salute you 💪💪 power to the people.
Thanks madam for the advice
❤❤❤❤ that's beautiful idea Mai kariat
We're with you madam
Well spoken madam boss 🙏🙏🙏
Patricia kaliat ndi makina paokha welcome back mom ur loved
UTM ngati ikufuna kuti omwe apha Chilima adzalipire akuyenera kupanga mgwirizano ndi chipani cha DPP kuti achotse MCP ndikufukula imfa ya Chakwera poyera koma ngati satero nkovuta DPP kudzagwira ntchitoyi pamene UTM imawanyoza pa kampeni
Chomwe wamanga Mulungu wina sangachiphwasule. M'gwilizano wa Shadow wina uliwonse omwe cholinga chake ndikugwetsa MCP, ndiri nanu pambuyo....
Bravo!!! UTM welcome to DPP
100% mai, UTM, DPP ndi AFORD gwirizanani mugwetse MCP ndi chakwera atitopetsa, mai wa nzeru kobasi.
Mphechepeche mwa njobvu sapitamo kawiri. UTM iyime paokha ili ndi tsogolo kungatalike. Sitikufuna kubwereza zomwe zachitika ku MCP.
@RoyKambalame
23 күн бұрын
Ndipo zoona osabwereraso mmbuyo Maso patsogolo
@CharityMhone-uk9ym
23 күн бұрын
Koma kuima pa nonkha simungatenge boma never popanda kuphatikizana ndi chipan champhamvu 😮
@user-tk6wf2eg4z
23 күн бұрын
Imani nokha tione dpp nde ndiyamoto ndikale
Ndinu mburi zedi mulipachangu koma choononga komaso kachipani kanu kakuntha nanga ku d p p mulibepo Udani a a a si wa UTM iwe ukufuna kuononga mpunga WA UTM
@PetrusTlhokwane
23 күн бұрын
Samamva asiye adzaziona ayiwala zimene adamupangira mademo APM azabwezera zonse zija mmmn they have to learn through mistake with tose alayasi km UTM bwanji mwayamba kuti gwesa phwayi
@HappyKanyangala-oq1kk
22 күн бұрын
@@PetrusTlhokwane yes edid
@selinaSingini
19 күн бұрын
Dpp yikanakhara kut yimamukonda chilima sakanachokako nde musaiware kut chilima nayo anapangira kupya mtima kulowa Ku mcp kut achose dpp mu boma mukwiyo umapangisa munthu kut asapange chinthu cholondola dekani popanga zinthu
We have to join together gentlemen and ladies indeed
That is point UTM ikuyenera kupanga mgwirizano DPP
I salute you mama , good decision more 🔥🔥🔥🔥🔥
Mcp ikuchoka mudzina La Yehova usogoleli umene Mulungu sakondwera umene Mulungu sakondwera nawo amaugwetsa or patavuta bwanji
I totally agree with you Madam
Koma a mayi inu mutizuza kwambiri ndipo you have to learn through mistake muyambilaso tose alayasi tatopa ndi kuliratu ife Chaka chino Chigoliyati chinalephela khondo kwa David nde inu bwanji a UTM km DPP yanuyo 2020 munayipangila mademo nde mwayiwala km mukazi wa Loti adayang'ana m'mbuyo ndikusanduka chulu
Osamakakamiza aliyense ali ndi ufulu ndi chisakho chake pokavota. Panopo kuigwetsa MCP nkovuta aaaa nde gwirizanowo ndi dpp?? Mayi mukunama inu kuyakhula konseko ndi mpando musatinamizepo apa.
Chilima akanati sanapange alliance ndi MCP ndibwenzi Chilima alipo zedi
Inenso ndine wa pa kanthawi ndithu MCP ndayiwona ndipo ndimaidziwa. Kungoti zangovuta kt zipani zinazi ndizazing'ono nchifukwa chake people will be FORCED to make an aliance with DPP. Koma tikawunika BWINOBWINO, DPP ndi MCP palibe kusiyana. Njauju mkulu wa ACB dafa ngati simunthu mpaka pano milandu idangozizira. UTM tsaopano payokha itha/ ndi AFORD, zitha kuchita bwino ndithu chifukwa imfa ya SKC idachita CAMPAIGN YAMPHAMVU. Makamaka ku chigawo cha ku mpoto. Kubwelera ku DPP itakhala LAST OPTION, yes mwachonchi mowawidwa mtima. Mayi ndakumvani BWINO ndithu, ndipo sindikukutsutsani kwambiri, koma DPP, ikhale last option.
May God please bless Malawians, Congrats from SA😂❤🎉
I support that statement MCP should feaz out
Komanso chilimatu akanapanda kuchoka ku DPP bwenzii Ali president wathu moto kupita ku DPP palibe vuto
Omwe akusunga udaniwo tawafunsani kuti kodi wina watichosera chiyembekezo chathuyu ndi awa omwe tinasiyana nawo mwamtenderewa kwabwino kulowera nkuti? Coz pakakhala kugawanikana kwazipani MCP sichokadi u are right
Thanks Mai anthu mwayankhula bwino kwambiri thanks so much for ur spish
@PeterChilombo-ou2cd
21 күн бұрын
zoona koma tipange zimodzi chakwera achoke udani pambuyo pangani zomwezoo moto kuti bhuu!j
Amai munabadwa mwakuya more 🔥
UTM ingopanga alliance ndi DPP that's the only solution
Chipani cha MCP mchakupha komaso mayi inuyo mukunena zoona ndipo ang'onawo achoke.MCP adzayivotera ana a zikhaleng'oma 👋👋👋
@Hellenistic109
22 күн бұрын
Kkkkkkkkkk
@user-rx2oh3rj7p
20 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
Atsogoleri a DPP, UTM, UDF & AFORD pangani smart, strong, transparent alliance kuti tisinthe dzikoli. Amayi mwalankhula mawu a mphamvu.
Bravo madam I second you❤❤
@user-wb3us4pg4b
23 күн бұрын
kod ndindan mai akukamba zanzeru yi
Ife tili DUU (DPP, UDF, UTM) kumastand
Well done mama nkhani.imeneo ndiyabwino tiyeni ku dpp. Amene akufuna ku mcp sianthu.amenewa
Osanena Kuti ine zinandi pweteka iyai,munene Kuti m'mene adamu phera, Chilima Aliyense M'malawi zamuwawa, ndiponso nkhani imeneyi MCP tizawona Ku sogoloku Chakwera tizawona basi
UTM yavutika mokwanira. Izi zomati Bola awa tiwachotse sizithandiza. Za alliance pamapeto. Mangani Kaye chipani UTM siyaying'ono. Ku DPP chilima anavutika. Tikufuna Chitukuko ife. Cholinga sikugwetsa MCP. Tikufuna utsogoleri wothandiza.
@doreenkaliati3166
22 күн бұрын
Mau mawa Mumakwana
Zoonadi omwe a kulankhura ndi a DPP kuti UTM ipange mgwirizano ndi DPP, ndipo akuterowoso kuwa vomereza kuwauza kuti otsogola akhale wa UTM
Ine nndinatuluka ku DPP coz of UTM apaso ndibwelela chifukwa cha UTM 🔥🔥🔥🔥 SKC
Powerful tiyeni amalawi tidzuke tigwiranane manja Mcp paulendo anthu akupha inenso I wish kuti Mcp imwalire viva UTM viva DPP Rest well our hello
Live from south Africa cape town
UTM , DPP, AFORD and AFFORD make one thing with concrete agreement we were tired please with MCP regimes
God bless you mama good decision ❤
Good solution mama !!!!!
Tilowele ku DPP komweko basi,aDadi munthu womvetsa akatilandila,adadi sadziwa kupha munthu chifukwa chophangila maudindo ndi ndalama
You r the great mama
Kwambili izodi ndizoona 1 to 1 inu nokha ndi mcp kt mungamuchose mm ayi simungathe pitan ku dpp and UDF komaso afodi basi anawa azinyera ndiiithuuu
Nice and powerful decision
UTM moto🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️
Ndipo akapanda kutuluka tiwatulutse ndiifeyo UTM,DPP, AFORD combine with UDF mcp will be defeated mai iminoyo ndi amzeru kwambiri
Very true mai
Thats good idea Mai mwaganiza bho Chakwera must go .. Alliance ya Dpp, UDF, UTM ndi Afford ilii mwala Pangan zotheka bas.
Mayi mwalankhula bwino chilima was a child of apm there is no problem to go back to DPP
Watching from Johannesburg it's good to join DPP
Eya mama joinani basi pangani zomwezobasi tibwerere ku dpp basi
Vuto lake limakhala limeneli, timakhala desperate kufuna kuchotsa chipani cholamula ndiye mapeto ake timangopanga ma plan osayang'ana kumbuyo kapena kuti kutsogoloku ziziyenda bwanji.
Paja DPP ndi kuchimake kwa Propaganda😂😂 Pepani a DPP the only new Malawi that as a nation we all expect is the coalition of UTM and AFORD period. We all all seek New parties in new Malawi to come. The MCP that Malawians have experienced this time NO majority can make such mistake to vote MCP again.
Siyani ma udani , mangani chimodzi ngati a Malawi, MCP ichoke ndipo isazapezekenso ku Malawi. Watching from JOHANNESBURG
Mwaganiza mokhwima maganizo abale athu a utm kupanga mgwilizano ndi DPP komanso tili ndichikhulupiliro kuti zipani mwanenazo mosogozedwa ndi Ambuye komanso anthu kulilira dziko lamalawi pamene lafikapa liphulidwe pa moto osatira azipanizo sionse angakondwere koma ambuye achite kufuna kwake pempho a DPP zichepeseninso pa anzanuwo kondanani samaliranani khululukirananipangani umodzi ochokera pansi pa mtima may God bless you
Yes l gree with you Mai,koma ngati simungamve magnanimous a Maiyi ndiye kuti mulibe magnanimous ofuna kutumikila a Malawi koma kukhutisa mamba zanu osati kuombola aMalawi ku Bagamoyo,please paganism chtheka kugwilana manja kuombola Malawi ku mng"anjo ya moto,machine ngati achitila kuno ku south Africa kupanga boma la Malawi colution Government, osakonda anthu awo mwasiye choncho
Kuyankhula kwabwino mai kumeneko ✊✊
UTM, Aford, UDF and DPP maganizo abwino
Mai MULUNGU azikudalisani chifukwa chamawu anu amphamvu ndachilimbikiso, tiyeni tigwirane manja kuti tichotse ng'onazi m"dziko muno
Brilliant idea. Ichoke MCP
Good idea
Mau mau mau pachingelezi timazati so shall it be in Jesus name